A Police Ndi A Army Ntchito Yanu Siyoopsyeza A Malawi - Bon Kalindo

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 11. 05. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo want to speak with Malawi Security Agencies, telling them that their job is not to terrorise Malawians but to keep Malawi and Malawians safe and secure.
    Pa Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo akufuna kulankhula ndi Nthambi za chitetezo ku Malawi, kuwauza kuti ntchito yawo si kuopseza Amalawi koma kuteteza Malawi ndi Malawi.
    #malawi

Komentáře • 28

  • @custommantchombe-rn1oo

    Kalindo umatha..big up

  • @user-gs7qk6lk7z
    @user-gs7qk6lk7z Před 18 dny +1

    The DC

  • @BethsiderTavares-ug4sv

    Osati dzikwi za anthu? Times hot currents said it was filled with a lot of people.

  • @user-wq9ex2sf3b
    @user-wq9ex2sf3b Před 18 dny

    I love you bwana bon kalindo

  • @BethsiderTavares-ug4sv
    @BethsiderTavares-ug4sv Před 18 dny +1

    The picture was designed by Junta club

  • @edsonkamba3170
    @edsonkamba3170 Před 18 dny

    I love the DC

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Před 18 dny

    The D.C. ❤❤

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m Před 18 dny

    The DC ❤❤❤

  • @ChaibishuSwadck
    @ChaibishuSwadck Před 18 dny

    Dc❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤🎉

  • @user-fp5qn5ci2v
    @user-fp5qn5ci2v Před 18 dny +1

    Kumbayani zikuvuta kupeza ma ID

  • @user-wq9ex2sf3b
    @user-wq9ex2sf3b Před 18 dny

    Bon kalindo angalamule ziko kupamba chakwela ndi chilima

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s Před 18 dny

    Achalume

  • @user-fp5qn5ci2v
    @user-fp5qn5ci2v Před 18 dny

    Ku Namiwawanso zikuvuta kwambiri kupeza ID

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn

    Malawi is one of the country that is still poor because of politics

  • @uchizJoelMumba
    @uchizJoelMumba Před 18 dny

    Akalindo ndionga Palibe chomwe angatiuze chazelu or misala inachuluka mmutu

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před 19 dny

    Osangolowa dppyo bwanji kalindo

  • @ChiyembekezoPhiri-sv8nw

    The DC iiiiiiiiiiiiii mumaitha

  • @user-lw4hw9ce4w
    @user-lw4hw9ce4w Před 18 dny

    The dc asiye achitetezowo aziona pasogolopa boma limasintha asaiwale

  • @JamesMalango
    @JamesMalango Před 18 dny

    Army anzawo akulanda maiko uko, Malawi yomvetsa chisoni kwmbr ndi asilikali omwe tonse tulo lokhalokha

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před 19 dny

    Ndi wandale siwomenyela ufulu ayi kambweee galu masa unali kale mdpp

  • @BethsiderTavares-ug4sv

    It's called the abuse of power and intimidation just to oppress loyal descent citizens. Here at home the Bobby metropolitan police including the community police they protect us and arrest criminals not the other way around. Here we love our police and you feel secured and warmth around them, you can actually tell them anything very fast thus if you saw someone committing crimes.

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp

    Kumachinjili anthu alumapita 3aam ukapanda kulawla form suinumkha ATI anthu 250 ATI patsoko

  • @mauricetayali8041
    @mauricetayali8041 Před 18 dny

    The DC boni kalindo, kawawa

  • @patassonelucaszovuta3431

    Nyamata omenyela ufulu alomue

    • @BethsiderTavares-ug4sv
      @BethsiderTavares-ug4sv Před 18 dny +1

      Osasankha mtundu DC ifenso anthu aku mpoto timawakonda a DC athu not only for alomwe.

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před 18 dny

    KALINDO udziwe kuti mcp ndiyoyipa dzedi Abitsa ndalama ziko cholinga anthu adzitsauka iwowo adzigula dzinthu adzigawa mene akugawala Ufa kaya ndalama ndidzina dzotelo malo kodza chuma chadziko kuti anthuwo adzigula okha asaaa koma a mcp inu ndi agalu kwabasi

  • @user-ef7lq1zj9n
    @user-ef7lq1zj9n Před 19 dny

    The DC ❤❤❤