Velikost videa: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Zobrazit ovladače přehrávání
Automatické přehrávání
Přehrát
Zoona kalindo awuuze mbuzi za chakwera ife ahlomwe sianthu opusa tu uziona.
Koma amalawi, munapanga ma demo nkhani zazing’ono, mademo mukulephera pano zinthu zitayipiratu. Mwagonanso amalawi, mademo akufunika
Zokha tikuchita dziko lamalawi mulungu alekelera'zoon lelo UDF lelo yakhalaso yazelu lelo DPP lelo yakhalaso yazelu chomwe tikufuna amalawi ndichan mfziko mwathu momo ndiuzen
We're behind you the DC
The DC mwana owoopsa kwambiri,we are behind you
Zinthu zake dziko muno nsaname zafika poti munthu ukumazifusa kuti koma anthu opanda ma lawyer fe tili ndikoti tikasume????
Chinthu chikafa ndieno chizikhara chazelu kapena boma likatuluka ndipomwe lizikhara lazelu
Booon kalindo usasochelese amalawi
Kkkkkkkkkkkkk inuyo mukuti Malawi Ali bwino et ????
When This Chakwela is out of power him and his whole cabinet minister they must be arrested and all state money they stolen they must pay back
Iweyo udzafera anako osati amalawi aliyense pano wadziwa kt iweyo ukupanga business pabuyo pamalawi uzisochelesa machota omwewa
Iweulindi boza
Vuto takutulukilan kut siinu omenyera ufulu koma cadet wa dpp kkkk vote ndmutima ukunama iwe
Kwambiri kwake iyee ndiwandale chabe uyoo
Munthuyu kumutengera ndiekut wasatira Misara yake palimbepo chazelu akuuza amalawi
Wamisala ndi iweyo ife tiri pa mbuyo pa DC.
Ife palibepo tikuchiwona chovuta inumukudya ndrama zaku opposition ndinu mukunjoya
@@user-bn8ci6vx5c DC waboma lanji'?
Osati ife uziti iwe
uli mgulu lofuna kuononga malawi nde unyatu Born kalindo akunyeletsani mukalaka kulowa pansi
Azathuwa akupangatu business mwina simukudziwa munthuyu akudya ndrama za opposition mwina simudziwa mukupanga ma moment azanu zikulowa Inu mulichete ndinakholowa kumudz
Zoona kalindo awuuze mbuzi za chakwera ife ahlomwe sianthu opusa tu uziona.
Koma amalawi, munapanga ma demo nkhani zazing’ono, mademo mukulephera pano zinthu zitayipiratu. Mwagonanso amalawi, mademo akufunika
Zokha tikuchita dziko lamalawi mulungu alekelera'zoon lelo UDF lelo yakhalaso yazelu lelo DPP lelo yakhalaso yazelu chomwe tikufuna amalawi ndichan mfziko mwathu momo ndiuzen
We're behind you the DC
The DC mwana owoopsa kwambiri,we are behind you
Zinthu zake dziko muno nsaname zafika poti munthu ukumazifusa kuti koma anthu opanda ma lawyer fe tili ndikoti tikasume????
Chinthu chikafa ndieno chizikhara chazelu kapena boma likatuluka ndipomwe lizikhara lazelu
Booon kalindo usasochelese amalawi
Kkkkkkkkkkkkk inuyo mukuti Malawi Ali bwino et ????
When This Chakwela is out of power him and his whole cabinet minister they must be arrested and all state money they stolen they must pay back
Iweyo udzafera anako osati amalawi aliyense pano wadziwa kt iweyo ukupanga business pabuyo pamalawi uzisochelesa machota omwewa
Iweulindi boza
Vuto takutulukilan kut siinu omenyera ufulu koma cadet wa dpp kkkk vote ndmutima ukunama iwe
Kwambiri kwake iyee ndiwandale chabe uyoo
Munthuyu kumutengera ndiekut wasatira Misara yake palimbepo chazelu akuuza amalawi
Wamisala ndi iweyo ife tiri pa mbuyo pa DC.
Ife palibepo tikuchiwona chovuta inumukudya ndrama zaku opposition ndinu mukunjoya
@@user-bn8ci6vx5c DC waboma lanji'?
Osati ife uziti iwe
uli mgulu lofuna kuononga malawi nde unyatu Born kalindo akunyeletsani mukalaka kulowa pansi
Azathuwa akupangatu business mwina simukudziwa munthuyu akudya ndrama za opposition mwina simudziwa mukupanga ma moment azanu zikulowa Inu mulichete ndinakholowa kumudz