Beating individuals in full view of the police is similar to what DPP used to do while in power. They used to beat people while the police watched. These two political parties have similar colours: whether MCP or DPP palibe wabwino. DPP looks angelic now that they are out of government. Inuso munali amwano kwambiri muli M'boma you are not a necessary evil. However mnthawi yanu the economy inaliko bwino. Ndinu madolo you could see to it that a common man shouldn't suffer in the village, apo pokha nditha kukuvulirani chipewa, though munali ndi zofooka zanu
Amalawi tiyeni tipange analyse the actions of Mcp led government against the rule of law. Are you serious to say that Nankhumwa is eligible to be leader of opposition despite being mcp or dpp or utm? Guys tikamapanga comment be sober minded for mmawa zinthu zimasintha. Let's sustain our democracy.
Dpp you have failed us with your greed. Mikangano yakuchipani pano iyo yayamba kusokoneza parliament. We can all read and understand what is happening. So what about the injunction? Should the speaker be in contempt of court deliberately because of the immunity given to parliamentarians during their sitting? Or just to make dpp happy? You failed in government and you have failed in opposition. Inu amene mkulimbikira APM mkuononga DPP.
Munatinamiza university ku mzimba andale mutipha amalawi
Yes they had their own weaknesses palibe mngelo apa
Mwakhuta kachasu kkkkkk opposition yimawawa myiwona
Apm my vote
Ifeso tikuphempha mseu waku mzimba eswazini mzalangwe road, contractor anachokaso kumseu umenewu, please chonde tithandizeni kuwakumbutsa a president awa akuwudziwa mseu umenewu, mseu umenewu ukudutsa kafukule mpaka kufika ku ekwendeni. Mayendedwe akuvuta kwambiri kumseu umenewu.
Akulu akulu musaope mcp, tisabwerere ku one party system. Sitilola zimezo. Mavuto achuluka ku Malawi. Lichoke boma ili.
Pano ndiyanu muyiwona dwambadzi a DPP munatasa kwambiri mudzikolo
Dzitsilu inu adpp
Inuyo mwayiwalira zomwe mudayichitira utm ku Mangochi ndi Machinga?
Separation of Government arms meaning what? Inuyo munazichita?
Bozi iwe
Akuphedwa anthu ku mzuzu siinali nthawi yanu?
Miyakupa yophatikiza ndi nyekhwe ku dpp. Kkkkkkkk ku opposition si zinthu
Why can't you go to court sort out your issues. Vacate the injunction remove Nankhumwa from the leader of opposition position, start afresh basi
😂😂😂😂 inuyo guys mutenga Boma
Inu mukulankhula ngati wamsembe munali kuti dpp zigawenga achina japi akuzunza amalawi???
Walephela kulamulila ameneyu osamuvela chisoni achoke busa wakhaza ngati ameneyu sindinamuwoneko ine ayi ati Phela ana athu uyu
Ineyo lero ndinapita ndi mwana ku chipatala Cha Dedza central ,mwayo anathyoka m'kono dzana koma ndagula ndekha chikhakha olo mankhwala sanampatse komanso pomwepo mkutiuza kuti basi dzipitani . Zinthu kumalawi sizikuyenda .
Dedza Central hospital nde yakuti? But very unfortunate if it happened
DPP be careful mcp ndiaanthu oipa kwambiri, even nanu mupanga zanu zopusa zomwe zinakutulusani boma koma mcp chenjera nayoni ikuongerani chipani,,
Mwaiwala zimene mumapanga ndi adzanu ndipang,Ono simunathe anthu angat mwavuta anthu a DPP
Beating individuals in full view of the police is similar to what DPP used to do while in power. They used to beat people while the police watched. These two political parties have similar colours: whether MCP or DPP palibe wabwino. DPP looks angelic now that they are out of government. Inuso munali amwano kwambiri muli M'boma you are not a necessary evil. However mnthawi yanu the economy inaliko bwino. Ndinu madolo you could see to it that a common man shouldn't suffer in the village, apo pokha nditha kukuvulirani chipewa, though munali ndi zofooka zanu
APM anatuluka anthu ake omwewa
Anthu akulu akulu ngati inuyo mavuto mukuwadziwa bwanji osapanga chiganizo koma anthu awa kugona amaonjeza
😂
Muyeso uja mumayesa nawo anzanu dzana lija ndi umenenso akukuyesa nawo inu lerowu
Amalawi tiyeni tipange analyse the actions of Mcp led government against the rule of law. Are you serious to say that Nankhumwa is eligible to be leader of opposition despite being mcp or dpp or utm? Guys tikamapanga comment be sober minded for mmawa zinthu zimasintha. Let's sustain our democracy.
A Mhango muzingozivutha musaganize kuti mwina azakupasani u vice president was dziko,Mayazi
Zakukhoti tichedwa nazo
Osatinamiza ife ayi. Munachita opusa kunatha basi.
Chitsilu ndi chakwera wosalimbana ndi dpp cz muzalila 2025 mukuiwona ikulamulira
Mukapitiliza kugona a DPP mupitilila kugona nyekhwe mukuenela kudzuka
Karma 😂😂😂😂
Opusa anthu onsewa zimene amachita ali mboma ndizimene amachita.
Waboza iwe
DPP rise up again. DPP hungry lion now
Agalu awa alibe manyazi zedi, akuti chani zokhapidwa??
Dpp you have failed us with your greed. Mikangano yakuchipani pano iyo yayamba kusokoneza parliament. We can all read and understand what is happening. So what about the injunction? Should the speaker be in contempt of court deliberately because of the immunity given to parliamentarians during their sitting? Or just to make dpp happy?
You failed in government and you have failed in opposition. Inu amene mkulimbikira APM mkuononga DPP.
Kodi Inu lero zikukuwawani kuti anthu a chipani akumenya a chipani chitsutsa?
Mwayiwala zomwe anyamata Anu amachitila muli mboma ?
Inu mwaonetseratu kuti muli desperate kuti mukapitilize kuba kuja munkachita kuja.
Munyopoka... Chakwera will continue.. Inu takhalani kaye ku opposition...
This useless party.
Kkk😂
Corrupt mcp
A Mhango muzingozivutha musaganize kuti mwina azakupasani u vice president was dziko,Mayazi
Too much weak wene futseki