Yambitsani chipani chanu adausi,,,bingu wa muthalika atawona kuti akupangana over take ndi muluzi anapanga chipani chake ,,,ine zavotera adad ❤❤❤ ,,,dausi akufuna kufa atsanalape
This is Democracy chipani sichikhala Cha munthu mmodzi or banja ai zinathetsa chipani changa UDF zokakamiza chipani kukhala zakubanja meeting ya chipani kupangira ku Page house munyumba ya munthu kkkk go go Nankhumwa umatha iweyo
Iyi si AGC meeting ndipo zimene mukukambilana si za chipani Cha DPP koma inuyo mukungogalukila chipani cha original DPP tsogoleri wake ndi ownable Peter Mutharika. Ndipo pemphelo lanu ndi lopanda ntchito ndipo Mulungu sangavomeleze pemphelo ili ndipo Dausi ndi wakupha olo Mulungu akudziwa za Dausi wapha anthu ambili ali ku Mcp ndipo musamamunvele ndi chokupha chimunthu ichi
@@Littlefair7 Kodi mukamnvatu kuti ku Malawi kulimbuli,amatanthauzati zimenezi, ndipo, ukamziona ngati zinalowa mkalasi koma zinabwelako mmutu muli zimamina thooooo! Kikkkkk ma form form okhaokha kikkkkkkkk!!!!
These people are patrotic to the party, they are the ones who are willing to preserve the party not Za NAmalomba ndi APM za misala basi. big up people mwachititsa manyazi a ku page hausiii
Chinthu chomwe chikundidabwitsa ndi chakuti misonkhano ya gulu ili zikumaulutsidwa ndi ma TV station wodziwika bwino Zodiak, Times MBC. Pamene misonkhano ya ADAD yikumakhala pa Bakili Muluzi Tv kapena pa Ngaliba TV.
I know what am talking about and God is withstand for everyone so why you are feeling pain with that word heaven is expensive and wait for the outcomes
Koma nde kuyalukatu, komatu iwe Nankhumwa, route yomwe watenga iwe wasochela ndipo sizikuthandiza Kodi unaganiza kuti anthu angakusankhe iwe kukhala mtsogoleri wa dziko?
@@eliffagondewe8214 Ndalama za chinaso tsopano? Kodi you think MCP can be so low like your DPP? Sponsoring what? Hahahaha! Shame on you, by the way,this is normal when you are in opposition! Tangokhalani kaye choncho and wait the next level your division muthawa nokha
Daus Ndi wa mcp siwa dpp ndalama zikucokera kwa chakwera iwe daus ndi nakhumwa yambitsa chisoni chanu Osati ndi d pp prezdent ndi Peter bas daus ufune usafune
Iwe kadausi ukuima ngati mndani ku NGC, yet you're mcp member, and that party is not mcp party but DPP ,,,,,,,,koma ya! Mcp ilowadi m'boma mogulidwa azipani Zina,koma Mulungu si munthu mudziwaso ukulu wa Mulungu,, ........bodza ndalama apatsidwa ndi mcp
Jeffrey ndiwe hule loputsa kwabansi msonkhano umenewo ndiwanu ndi ma boyfriend ako ngati Ken msonda nankhomwa ndiwe mbuli sungakhare president wa dziko agalu inu,
Matsoka a DPP anayamba poyamba kumusala SKC...Bingu anladziwa kuti chipani ichi chinkafunika new minds....
Anthu awa alibe mzimu kkkk
This is Democracy country. Others are in Dpp to affect rights and freedom. We are Dpp we will never allow as blood party.
Tell your people to form their own party not this nonsense, DPP is belongs to APM not Nkhumbwa, Dausi and other useless people.
Mukanangolemba chichewa boss, chingerezi chanuchi eeeee olo graduate akhoza kulira.
@@Littlefair7 mwatero Kodi? Midziwa bwanji olembawo si a graduate?
@@kaitanokagalu
Koma chingerezi chomwe chalembedwa apa ngati amakakamizidwatu, tiyeni tizilemba language yathu momasuka basi.
@@Littlefair7 kikkkkkk ndiye anthu oterowo amakhala amakanitu osati masewela hahahahahahah!
Yambitsani chipani chanu adausi,,,bingu wa muthalika atawona kuti akupangana over take ndi muluzi anapanga chipani chake ,,,ine zavotera adad ❤❤❤ ,,,dausi akufuna kufa atsanalape
This NGC meeting has been sponsored by MCP gurus, and atola nkhani ogulidwanu tikukuziwani
MCP ilibe nthawi ya zopusazo m'phwanga ilibe Ndalama zogula anthu a DPP,kuti adzitani anthuwo?
Game zikwanje tsopano poti mwawadziwa osaiwala yanu ija tili kuma stand
This is Democracy chipani sichikhala Cha munthu mmodzi or banja ai zinathetsa chipani changa UDF zokakamiza chipani kukhala zakubanja meeting ya chipani kupangira ku Page house munyumba ya munthu kkkk go go Nankhumwa umatha iweyo
Iyi si AGC meeting ndipo zimene mukukambilana si za chipani Cha DPP koma inuyo mukungogalukila chipani cha original DPP tsogoleri wake ndi ownable Peter Mutharika. Ndipo pemphelo lanu ndi lopanda ntchito ndipo Mulungu sangavomeleze pemphelo ili ndipo Dausi ndi wakupha olo Mulungu akudziwa za Dausi wapha anthu ambili ali ku Mcp ndipo musamamunvele ndi chokupha chimunthu ichi
Bravo nakumwa ndi Jeff wa feff. Ana a chabe osafuna kusekerera zopusa. Ana inuyo musazafe
Dausi pepan ngat unayamwa belelamako choonde mwayes mwana wa mulungu akuyendere ndith zomwe mwakonza tazimva kale sizomwe uku fotokozazo ayiiiii booza ambuye ambuye talila ameen
Uku ndiye kuyankhula kopusa, mwana wa Mulungu akulowa pati pamenepa? Kupusa bwanji kodi?
Dawus ndiwosokoneza Kodi osangoyambitsa chipanichanu bwanji iyi ndi DPP yakhothi
Koma Inu ndalama mwadyazo musanza ndithu anthu achabe inu
Ma Court akulamulidwa ndi MCP ndiye nzachidziwikile kuti akumuopa APM and akufuna Nankhumwa kuti akhale President cholinga adzadutse moyera.
MCP pamenepa ikulowa pati? Umbuli bwanji kodi?
@@Littlefair7 Kodi mukamnvatu kuti ku Malawi kulimbuli,amatanthauzati zimenezi, ndipo, ukamziona ngati zinalowa mkalasi koma zinabwelako mmutu muli zimamina thooooo! Kikkkkk ma form form okhaokha kikkkkkkkk!!!!
Pungwe pungwe uwu bwezi akulandila Ali bomawa Koma mukupangana Nokha Nokha anakhumwa Ku paliamenti mumangogonako kod amalawi minyama yathu yatunduwanji 😢😢😢😢😢
So sad can't believe it 🙌🙌🙌
These people are patrotic to the party, they are the ones who are willing to preserve the party not Za NAmalomba ndi APM za misala basi. big up people mwachititsa manyazi a ku page hausiii
All blame to Nankhumwa. He will never be president
Nankhumwa mbuzi ya munthu and akuona ngati angalamulire dziko la Malawi, kukhala President si ntchito yophweka amufunse Chakwera mmene akulephelera.
MCP iyi.Onse amene asankhidwawa ndi a MCP in DPP uniform.
That's why mu comment section mu mwadzadza a MCP
😂😂😂😂 chisakho chakunyumba Kwanu chani😅😅
Amene wakhala akusatila khaniyi bwino bwino kuchokela pa chiyambi akuziwa kuti Anthu awa akupanga zolondola
Ndizoona mukunenazi koma eni ake a DPP sakuzilondola ndipo ndi anthu onvetsa chisoni,I think they are ignorant by nature
This is absolutely not a DPP I used to know and like.
Koma ziliko ndalama I apha yesu koma usanza sure🔥🔥🔥
Chinthu chomwe chikundidabwitsa ndi chakuti misonkhano ya gulu ili zikumaulutsidwa ndi ma TV station wodziwika bwino Zodiak, Times MBC. Pamene misonkhano ya ADAD yikumakhala pa Bakili Muluzi Tv kapena pa Ngaliba TV.
Amachita capture mwaulere?
Useless immature politicians
Anthu opanda nzelu inu simungaone 😢momwe anthu akuvutikira mdziko muno??? ....zitsiru kwambiri
Mungoyamba Chan ndye tiwone Kut mufkanazo pat Koma DPP singawono ngeke Nd makape ngat inu
Ambuye ake ati amene akudaliseni lusifala dausi ndinu munthu wakulu muzikhala ndi zeru zofuna kuthandiza amalawi simuzawina
Akuwona ngati kulanda chipani ndi izee akulephela kumupha penter mapeto ake abalalika akugwilisa tchito makhothi sopano mukuzinamiza tikuwonelani kuti mukafika kuti
They're doing in accordance to Court orde 😅😅😅😅
Shame on you guys eesh
Dpp yeni yeni ndi iyiyi. Osati zankharamba yakumangochiyi
We ignore all your plans and secrets but just wait for the response from heaven mark my. Words. You are cheating yourself.
Please you cannot mention heaven so cheaply, heaven is not a weapon of threatening others. Withdraw your nonsense please.
I know what am talking about and God is withstand for everyone so why you are feeling pain with that word heaven is expensive and wait for the outcomes
@@SolomonNjolomole
Stop your holier than thou mentality, God is not a politician, stop mentioning God so cheaply.
Peter or ataima independent azawina
Adzawina ku Thyolotu kkkkk. Keep dreaming
@@tasmania527 kikkkkkk hahahahahahaha koma abale ku Thyolo kokha Kodi? Ayesle kuima payekhapo aone dziko mmene limakhalira.
Koma nde kuyalukatu, komatu iwe Nankhumwa, route yomwe watenga iwe wasochela ndipo sizikuthandiza Kodi unaganiza kuti anthu angakusankhe iwe kukhala mtsogoleri wa dziko?
Tiona zithu 😂 dpp once a mighty party now in shambles.
MCP is hiding behinde these gungstars
Proofs please!
For sure ndalama azitenga kuti akulephera kulongosola
@@eliffagondewe8214 Ndalama za chinaso tsopano? Kodi you think MCP can be so low like your DPP? Sponsoring what? Hahahaha! Shame on you, by the way,this is normal when you are in opposition! Tangokhalani kaye choncho and wait the next level your division muthawa nokha
Zabodza
Ajefu osadanda muchila
Mesa adausi analowa muchipani mcp?
Daus Ndi wa mcp siwa dpp ndalama zikucokera kwa chakwera iwe daus ndi nakhumwa yambitsa chisoni chanu Osati ndi d pp prezdent ndi Peter bas daus ufune usafune
Zindikirani kuti ,ndinu aNGC, koma okuba ndithu zandinyatsa.Mukufuna kugulitsa chipani,ku MCP.
Malawian the can't vote for Nankhumwa forget it serious
Parties shouldn't be owned as an estate...case study ya UDF is pathetic versus MCP owned by people
But those families support the parties financially
Zaugalu zimnezo mwasowa zochita
Nankhumwayo ndiye ayitu masanje enieni
Koma akuluakulu nankhumwa ali mchimutu eeeee simwangodzadza mamina mmenemu
Zanu izo,nthawi ikakwana mulapa.
Ndikuona kuti iyi ndi mcp Reserve not DPP party awa akabwedza ndalama zonse zomwe apasidwa
A DPP menyani nkhondo yolowa boma
Mukawina zathane nawoni adani anuwa.
Kutereku amenewa ndi osaukanso kwambiri kumalawiko ofuna kudya nawo kuchokera ku MCP
Iwe kadausi ukuima ngati mndani ku NGC, yet you're mcp member, and that party is not mcp party but DPP ,,,,,,,,koma ya! Mcp ilowadi m'boma mogulidwa azipani Zina,koma Mulungu si munthu mudziwaso ukulu wa Mulungu,, ........bodza ndalama apatsidwa ndi mcp
Maina onse apa ndiongoeserera zaziiiii
Dausi chonde usamati amalawi amalawi ake atiwo aaaaa kkkkk
Thi is the buttle,Who can seiz the fire
Mbamva izii muwoneni dausi mayakhudwe ake ayenera kuziwa kuti mulungu simunthu
Nankhumwa woyeeeeee
Nanu a Dausa, tadzinenani chilungamo.ndiye a Presidentiwo anakuchitani ok?Ndiye mmene mwatelo mukawauza chani,a Peter.KuBA uku
Akuononga dziko akufunaso awononge chipani cha ddp, akathidwaso ndi mulili winatu? Kkkk
Inu kd ndinu upusa eeeti inu mukuona gt angavotele nakhomwa ndi ndani koma inu mukupusa bwanji nakhomwa angakhale president mwapenga
Uyoyo lafu jumayo zaka zosezi wakhara aliboma wapangako chiyani akumanga ma ronge kwawo kuno kumachita kusowa mseu anthu woipa nokha nokha wopanda chisoni ndiamalawi womvutika simungavomereze kuti mwakura agalu inu
Muyaluka inu mulungu akukathani ndithu athu osokemeza inu
Anthu awa ndi anthu oyipa
Ndipo sakumva chisoni ndi amalawi ndipo mulungu akuona
A dausi uzimu unawachokera,zaumphawi wa a malawi alibe nazo ntchito
Machende ako iwe dausi mulungu akulanga
Jeffrey ndiwe hule loputsa kwabansi msonkhano umenewo ndiwanu ndi ma boyfriend ako ngati Ken msonda nankhomwa ndiwe mbuli sungakhare president wa dziko agalu inu,
NANYONGO WAMAKO GREZDA JEFRY
Anthu omwe akupanga dzinthu koma osaziwa chobwera mawa
Anthu awa sakumva chisoni kunena kuti ndi afiti sitikulakwitsa
Anthu oukira inu mulibe NZERU serious
Powerful asogoleli
Kodi Nankhumwa wanuyo angamuvotere ndani kkkkk inu dzitsilu za ana?
Zoona zak ineso ndikudabwa
Pofikana kupasa undindo daus mu chipani chafelanthu bas🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Jefure hure uzitenge bwino tikoza kuyendesa ma video ako orawura wava
Ku DPP mwayamba zopusa kwambiri, udindo sitikakamila amakusankha ndi Mulungu.
I can't understand
Anamalomba diwoipa, pamozi ndi peter wawoyo. Kodi chilima kaliat ndi ena aja anachokelanji ku dpp ?
Onsewo ndi amcp so app mukumana
Anyani inu
Anthu awa aphana sure 😂😂😂
Nankhumwa ndi a scam 😂😂😂😂😂
Osangoyambisa chipani chanu bwanji zisilu inu
Pa anthu 71 abwelako ndi 23
Zikumgooneka kuti ndiinubuzi
Bwanji anthunu muyambitse chipani chanu than kumabisalira kumbuyo kwa Chipani cha Dpp mukufuna kusokoneza chipanichi ifetu tikufuna Peter Munthalika osati izi mmene tikuvutikiramo
Koma chomanamizira MCP ndichiyani kwenikweni??? Aaaaaa kungokhala kamtundu kokonda nkhani zopeka
Choka dawusi machendiwako
Zitsilu zokha zokha zonse zimene zinali kumeneko mbuz za mcp zimenez daus ndi chitsilu
Kkkkkkkkkkk koma y inu mukupanga ngt scpan cmoz aaaaa akuvotelen ndmbwyanu bx
Mbuzi za anthu izi...agalu
Amayi amenewa azatha katani believe me am giving her 4 months
Nankhumwa ndi galu ,panyopako
ufiti uwu
Ufiti ndiooopsadi,
Njila ikachepa salinbilana zimafunika wina kupatuka ngt ndare ndi zabwino yambisani chipani chanu
Anthu adyela 🚮
Kupanda kutere dpp ikatha 90 days atha kuithetsa
Mwatumidwa ndi Mcp anyapapi inu
Agalu
Mai uyu akapanga zausir azaona zomwe anaona Jen jefureyu basi pooooo9 dausi ndi was mcp ndith muzaziona ndithuuuuu yes mbon yakumwamba
Otsilu za anthu inu
Kwavuta ndale ndizachabechabe
This is mcp kkkkkk
Aaaaaaa MCP itiso tsopano? Kikkkkkkk Kodi DPP imathasonkukhalaso MCP chitani manyazi. Ndipo zikukhudzeni
Mcp 2 iyiiii hummm
@@eliffagondewe8214 palibepo MCP,tikuuzeni ndife ndipo muzinva, ku Opposition ndi mmene kumakhalira ndipo simunati. Kuteloko mwangoyamba apapa, nanga mukaluzaso ulendo uwu kikkkkkkkk hahahahahaha ambiri muthawa sure
Anthu akulu akulu opanda mzelu mudziti chipani cha mcp dpp yakutiko ubwino wake amalawi pano maso anayela simungawapusitse mpakana pemphelo hhhhhh
Ukali wa usilu uwuuuu
Kodi adausi anankhumwa ndi azanu simungayambitse chipani chanu before zisankho kuchitika mukufuna chani ku dpp tayambitsani chipani chanu ndipo anthu akusatani koma zoti muzingopa against sizikuthandizani ndipo simungawine chomwe mungachite tulukani dpp ndikuyamba chipani china kapena mu joine zipani zina komanso mudziwe kuti anthu akukuonani sangakulupilileni chimodzimodzi ngati saulosi chilima