I'm very proud with this man and I love him so much ,samadzipanga proud ku ma social media moyo wake za family yake ayi ,komanso ngati muthu woti wagwira ntchito m'boma simudzamva any speach ina iriyonseyo ayi , amachita kukhala ngatinso ku Malawiko anachoka koma ayi ,amawonetsa kuti ziii ameneyo amakhala busy kumasamalira zopanga tsogolo la ana ake ,ndi momwe mwamvera apapa za mamphunziro awana ake ,uhule ngati anthu woyimbawa momwe timamvera iyeyu ayi ndithu ,ndimamumva kukoma mkati mwangamu koopsya ada awawa
Ati ku ndale sikoti kuli ndalama zoti ukhoza kuphunzisila ana aaaah ndie kuti zimveke bwanji? Iweyo billy anthu ambili amakuziwila mu music and umaimba bwino and kuimba uku kunapeleka chidwi kwa anthu ovutika kukuika mu m'boma ndi maganizo oti ukhoza kusintha ziko, koma anakaziwa kuti umapanga za moyo wake ndi family koma pa chilungamo ndiwe munthu oipisisa kwambili pa ndale ziko lako sumalikonda wadyela sangatukule ziko.
Ndietu ukayankhula amati ndiwe wa nsanje aaah zichani umakhala umakhala kuti pena ukunena chilungamo. Uyu anthu samamuziwa bwino bwino coz sanakhale nae , amamuziwila mu nyimbo and kwa ine ku nyimbo amaimba bwino mumakhala nfundo , koma kumuonesesa amapanga za family not ziko ndi munthu oipa kwambili
I'm very proud with this man and I love him so much ,samadzipanga proud ku ma social media moyo wake za family yake ayi ,komanso ngati muthu woti wagwira ntchito m'boma simudzamva any speach ina iriyonseyo ayi , amachita kukhala ngatinso ku Malawiko anachoka koma ayi ,amawonetsa kuti ziii ameneyo amakhala busy kumasamalira zopanga tsogolo la ana ake ,ndi momwe mwamvera apapa za mamphunziro awana ake ,uhule ngati anthu woyimbawa momwe timamvera iyeyu ayi ndithu ,ndimamumva kukoma mkati mwangamu koopsya ada awawa
Munthu wamkulu kwambiri , A bwana ozichepesa kwambiri . Inuyo big ,God bless you .
kuphudzitsa Ana mopereka chidwi kwa anthu omvera ndikutha kuona kuti palibe mphwepwa mwa Ana onse
Ulemu wanu Mr billy ndimakunyadirani kwambir ❤❤❤
I like Billy Kaunda mainly the number NALIYERA
I thank God I was part of your generation as well as your music, we are blessed by your art
Ndine emweuja,my favorite song
BK my legend... We love you honourable here in Zambia. Your music is so classic.
My favorite artist n the role model himself
Opanda mbiri yoipa Billy kaunda pitilizani kukhala munthu wa bwino achimwene ❤❤❤❤❤ from Capetown
Ndiye emwe uja… watching in the States.
Eeee iwe phe ameneyu timadziwa kuti ndinu biggy Inu🔥
onabo bile mkaunda voice very nice ❤❤ Mr. nkhumani
My favourite musician Bill Kaunda
The old legend still lives on.
Munthu wodzichepetsa kwambli ndiyamba kumvela nyimbo za billy kaunda mucha 1999
Big respect to Billy kaunda 💚🇲🇼💪
A classmate timakunyalani
May God bless you all the time
Mwacheza ndi Munthu wa bwino uyu kwambiri
Billy u stil young boy lv ur music
Well done Mr BK, we love you more
Few seconds into the interview and yep. Great voice from the host
Ndangosilila maphudzisidwe a ana ooo God bless you big and humble man
two
❤❤❤watching from south Africa sand
Oyimba opanda matukutuku God bless you
Ndi big man pophunzitsa Ana ake sukulu
Zikomo kwambiri oyimba yemwe sanavekepo ndi nkhani zanyasi ndi Billy kaunda ndipo ndioyimba okhazikira pa luso lake timakunyadirani malume k
Munthu odekha ndi dzeru zache ,I really like him, with his songs too
I like your songs MR
I like that guy so much
Ulemu wanu Mr presidente 🙏🙏🙏🙏
THIS MAN IS CALM.
Very inspired ❤
Cool man yoh ilove the personality
Mawu a billy kaunda takumbuka amalawitonse
Bless you Bro
Very humble man ❤
Our new MP
I remeimber when I was a kid pa chiwembe
The best
A humble Man
Legend
Ati ku ndale sikoti kuli ndalama zoti ukhoza kuphunzisila ana aaaah ndie kuti zimveke bwanji? Iweyo billy anthu ambili amakuziwila mu music and umaimba bwino and kuimba uku kunapeleka chidwi kwa anthu ovutika kukuika mu m'boma ndi maganizo oti ukhoza kusintha ziko, koma anakaziwa kuti umapanga za moyo wake ndi family koma pa chilungamo ndiwe munthu oipisisa kwambili pa ndale ziko lako sumalikonda wadyela sangatukule ziko.
Aaaa nde kachepatu ka inteviewko
How can i access the book "Hills and Valleys"'?
Uli boh bily
Humble mn ❤❤❤❤❤
Abily timakunyadirani mwasinthisa zambiri mziko muno
Ndi oimba yemwe sayangana pansi pa nyimbo zake ,.. amatha
Amandidalisa kwambili wakwanthu kupoto ndine symon phetera munthu imozi amandisangalatsa
Ahhhh mwakafupikisatu abale
Cool man
Awawa kungowataya basi palibe angamasule zingwe Nsapato zawo
Nice 🔥
Timati Mzimba osati Nzimba😮
Humble man
My man.
Zazelu basi
50+ koma looking fresh...
Wa akulu tsopano timakunyadirani mumatha.
Master
mwimbanga makola akulu tingateta yayi
Ana sachuluka man🔥
It is his music career not carrier.
Komatud makolo anu anabeleka mpaka ana 11,,ayi ntchito anaigwira
Nthawi inachepa koma.
Munthu ozichepesa kwambiri komaso wanzelu
Oh koma wabeleka
Sikefa chimoto
Billy uli ndi Ana 7 ine ndiri ndi 8 ndichitsomo cha namalenga
In politics ku Blantyre palibe chomwe tingaloze chomwe amapanga chothandiza
Ndietu ukayankhula amati ndiwe wa nsanje aaah zichani umakhala umakhala kuti pena ukunena chilungamo. Uyu anthu samamuziwa bwino bwino coz sanakhale nae , amamuziwila mu nyimbo and kwa ine ku nyimbo amaimba bwino mumakhala nfundo , koma kumuonesesa amapanga za family not ziko ndi munthu oipa kwambili
Kwabac
Koma nde unasosolatu man, ana 7 alone?, kkkkkkk
Amavuta kuphunzira ndi kulela osati kubeleka kkk