Orton Chirwa anali founder wa chipani cha Malawi congress Party komanso anali Mmalitiri amene anamenyera nawo ufulu wa dziko la Malawi kuchoka mmanja mwa atsamunda.
Kamuzu Banda is responsible for poverty in Malawi by killing people who could have contributed to the economic development of the country.....May the souls of Orton and Vera Chirwa Rest in peace.
you are good on history but the problem is umadana ndi MCP,ukamapanga ma stories ako just do it osati kuonetsa mbali,remember that was one party and ndizoonekeratu kut nkhaza zinaliko koma osamakolezera moto,,,,
@@rossbank7248 ife tili kunja kuno chifukwa makolo athu analandidwa malo ndi kamuzu. Bullshit president amene uja akanakhalapo lero ndikanathana naye ndekha with my bare hands
@@neliyachambakata8523 not this video. Some videos before this one. There is a clear portrayal of innocence of other regimes... and the conclusion of John Chilembwe saga is unfounded since his body was never found
Mulandile ulemu wanu ndikutha kuidziwa bwino mcp kudzela ku Bakili tv,keep it up God bless you big.
Best tv ever next time mutiuzeko yemwe anapha sidic mia mwana wa kwathu ku chikwawa😢
Rest in peace Orton Chirwa Kamuzu Banda will never get peace in his grave including people who are supporting his MCP party guys
Kuva history ya MCP ine sizavotaso mu Dziko la Malawi basi thanks
Kamuzu Banda is responsible for poverty in Malawi by killing people who could have contributed to the economic development of the country.....May the souls of Orton and Vera Chirwa Rest in peace.
True
Thanks my brother for shading light to us
this is the real history that we should put in our education system in Malawi
i appreciate this channel.very unique content
Yoooo thanks brother for your information ❤
He was genius
Malawi has such a sad history .Thanks for the content
thank so much, very enlightening
Rest in peace Orton chirwa it's a very very sad story
Mutiwuza liti yemwe anapha Evison Matafale
Ilipo kale
Zikomo milandu yoopsa iyi. Ambiri ali ndi magazi m'manja ndipo chowonadi chiyenera kuuzidwa. Dzikoli silidzachira popanda chilungamo.
Koma dzimandiwawa kamuzu kumene uliko mapwala ako😢😢😢
MCP will never change
MCP ingothesedwa 🤦🏿♂️
😢😢😢 kamuzu banda mulungu amukanthe ndinthu asamukhululukire coz anali devi
Thank u for lovely history
Pls tifufuziren mbiri ya Amnesty International
Umaitha keep it up bro
Kamuzu ana pasa phavu ndichirwa akayazana alekeni ku mapeto kwa che ndaziona
Channel ilbwino👍
God bless you my Bro.
You are indeed a historian
That's very sad story. RIP.
Very stupid MCP the then Government,,Tembo and Kadzamira are heavily responsible for apology to the family victims
😢😢😢 Kamuzu ndi sadzakupeze
you are good on history but the problem is umadana ndi MCP,ukamapanga ma stories ako just do it osati kuonetsa mbali,remember that was one party and ndizoonekeratu kut nkhaza zinaliko koma osamakolezera moto,,,,
No question, Orton Chirwa is the founder of Malawi.
Tell us who kill Dr chilima?
Mcp were heartless and real devil. 😢😢😢
Munthu woyipa kamuzu obelayu
Wasn't there a political party called "Nyasaland African National Congress " party in Malawi?
Koma ya nkhazatu
Sindinkadziwa kuti chikamuzu chinali choipa chonchi
You will never become who you were meant to be if you keep blaming everyone else for who you are
but its important as well to know history of where we are coming from
Kamuzu and MCP worst Government ever in Malawi kuposa asamunda
Channel cha chibwana.time yonseyi mudali kutiko cadet uchira
Mcp nd yamagadzi mpaka kale
That was far too much
Akulu mumatikonza kwamiri
Amalawi ambili amachita zinthu chifukwa cha kusadziwa.
Muma kwana amweni mutsatsiye kufukura nkhani
Kamuzu was a devilish mind
Kafukufuku wana penapake niwabodza
Rest in peace Orton chirwa.
Mcp was more than evil. Kamuzu hell fire
Very nice story
Keep it up
@@rossbank7248 bodza lake la kuthako kwakoko? asakudziwa ndani ku Malawi kuno kuti Orton chirwa anaona zoopsa komanso kuphedwa ndi chipani cha mcp?
@@rossbank7248 ndipo iweyo ndiwe chitsiru kwambiri. Zoona ungamayikire kumbuyo mcp mmene idathera anthu mdziko muno?
Pamntumbo pamako wamva galu iwe
@@rossbank7248 ife tili kunja kuno chifukwa makolo athu analandidwa malo ndi kamuzu. Bullshit president amene uja akanakhalapo lero ndikanathana naye ndekha with my bare hands
I will never get tired
Mcp ndiyimeneyi koma mulungu anatiyankha koma muluzi bingu peter joyce a mbola malawi sazasinthapo zivute zitani
Can you please exclude Bingu monga simmaona Zabwino zonwe anapangila amalawi?
This is new MCP not the old one, do not mix these two. Wamva author?
Whatever but this mcp logo is very ugly in the minds of people who suffered with this cruel kamuzu
Regardless of the new mcp the damage they did is unforgivable and i will never be on their side
Please make the channel as objective and independent as possible. It has great content. Don't favour sides please
But I think they are not taking side. They are just talking of what happened during that time.
@@neliyachambakata8523 not this video. Some videos before this one. There is a clear portrayal of innocence of other regimes... and the conclusion of John Chilembwe saga is unfounded since his body was never found
@@Justman34_dislike koma zimene akunenazo ndi zabodza? Sizinachitike? Let us be serious guys chifukwa zomwe akunena munthuyu tonse tikuzidziwa kale, palibepo zabodza apa. Mukuzitenga ngati zandale chifukwa choti akutchula mcp, komano mcp inapangadi zimenezo
Iwe zimenezo amakuuza ndani mbuzi iwe
Kape iwe sudziwa history ya Malawi!! Kamuzu chimunthu choipa kwabasi