Za meeting yoyamba ya UTM atamwalira Chilima yemwe anali mtsogoleri wao zili motele

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 7. 07. 2024

Komentáře • 13

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Před 12 dny +7

    Chakwera kupha munthu kamba ka udindo? Ayi ndithu Mulungu akukhathe.

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Před 11 dny

    Nkhani imeneyo ndi yabwino, koma Manganya awatangwanikitsa chabe, mwamunva mzimai uja, Usi ndi wa independent, awapusitsa chabe apa.

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před 12 dny

    Ulemu wanu akaliyati team yonse ya UTM pitiliza kusunga ulemu wanu komaso ndi kukweza mbendela ya Malawi komaso mokomela amalawi chezezo la ndilakuti samalani kwambiri musagulitse chipani chanu Ku MCP Ayi foundation ya UTM chakwela sakuyidziwa Ayi, chomwe akudziwa iye tonse alayasi koma zofetsa chisoni Kuti chakwela Anantchola bridge yowolokela tonse alayasi zomwe zikutathauza Kuti chakwela sakuwelengaso Za tonse alayasi chonde chonde ndalama zimene akukoza a MCP including president Kuti akupatse inu ndikuopa mulungu wanu Musalandile Ayi chifukwa zimenezo sindalama ayi Koma ndi mwazi wa president wanu komaso Kuti Ife amalawi tipitilize kukusapotani , ndi mbili ya bwino inuso mukuona amalawi ndi Mene alusila musakhale mu gulu lonyozedwa ndi amalawi chifukwa cha ndalama mudzakhala wosowa mtendele Moyo wanu , tikumbukile Kuti silikali wa kuzomba uja Anati ine ndinali komweko Ku chikangawa ndipo tibapatsidwa ma 10,000000 Koma ine ndenkha ndikulemphela kudya ndalama iyi chifukwa cha mwazi wa chilima Muthu wosalakwa god bless UTM party including all the members

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 Před 12 dny

    UTM ikakamila chingalawa chá tonse alliance ngati m'mene anachikakamilila Cláuds Chilima , ndithudi chipani cha UTM chizathela pomwepo mu 2025 , 😊

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Před 12 dny +4

    Moto buuu akaliyati tiyeni nazo poti inu ndi omwe mumakhala pafupi ndi chilima

  • @BrunoChakukuma
    @BrunoChakukuma Před 12 dny

    Usi ndi crook musiyeni ameyo pangani zanu a utm plz

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před 12 dny

    Awa adziwona kuyipa kowombela fiti manja UTM Iithela pops asaganidze kuti .MCP yasekela aaa ngati sanalemekedze chilima awa asalawa adzingodikila kuchosedwa limodzi ndi MCP 2025 UTM adzathela popo basi dziiiii

  • @MisheckNtanbalika
    @MisheckNtanbalika Před 12 dny

    Atuluke kaye ku tonse kut fundo zawo zikhal zamphavu km akapanda kutuluka akhozelaso maplani ngt president wawo chilima tsogolo labwino la utm liyime palokha osati ndi mcp

  • @AyamMkango
    @AyamMkango Před 12 dny

    Kd mesa kuli vp kumeneko

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg Před 12 dny

    Chakwela nd fiti

  • @DalitsoMbalanje-n2p
    @DalitsoMbalanje-n2p Před 12 dny

    Osanyengela yudasi kut adye nafe imfa ija ikutiwawa.

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi Před 12 dny

    Chakwera phudzo lelo Chilima kulibe

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi Před 12 dny

    Zitakuchitikitala zimenezi ja ndizokaikisa ngati mungakhale ndi zonveka Kaya simuli ku chipani chakuphacho 😭😭😭😭😭😭😭😭😭