Abwana president chakwela Ali ngati chidole kapena kuti katuni ena amagomungwila ntchito zaumunthu uyu mulibemo ndipo ndi khutukumve chakwela wa mwazi uyu
Let me correct you in Mzimba sugar ndi k 2495 in big mart shop ya fair price Chakwera dziko lamukanik passport anasiy kupang ndet only in lilongwe zoona zak achinyamat ntcht njee Achoke I will support that
Tikhara kuti tikungotukwana bas pa social media sizitithandiza Ife tingopanga zoti Mulungu atione ndikutivera chisoni basi Tizizivera chisoni kuti Mulungu atikhululukire
Malawi politicians are all poor minded because all of them are just after money after these ones other Gandangazi are coming ooh my beautiful country 😢😢😢
Chakwera zimene wakwanitsa kupha chilima basi palibepo chimene akupanga komaso nanga asikali Aja Amati azapanga ma video ya momwe chilima alikuti anthu Aja chonde asawaphesotu
Mangochi lake city and makanjila road and international Airport Mangochi 5star hotel palibe chimene wakwanilisapo palibepo ngakhaleso analonjeza mafuta onsika ndi fetelazer zambir
Best of the best bakili muluzi tv
Watching from Zimbabwe
Yes mwamuza zona ZIKOMO kwambili potiziwisa chikhalidwe chake
I trust bakili muluzi TV always because is talking true
I like this TV keep the fire burning dude
Ifee nga ngaa nga nga pambuyo pa ngwazi yamuyaya Dr LAZURUS CHAKWERA wathu wokendedwa 🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤❤
Galu wachabechabe iwe
Chokani apaa mwana wang'ona iwee, mwapha chilima asatana inuu 👹👺👿☻ , kunali ng'azi ina mdzaka zammbuyozo mumkaitchulanso kuti ngwazi, , lero alikuti?
Best TV station in Malawi so far.
Anthu Andale ndiabodza koma awawa eeeeeee awonjeza kwambiri
Akwanilitsa bwanji kupanga zonsezo ndalama akupatsa anthu akunja kumalemba anthu aganyu Kuti azimpha anthu ndalama zake zomphela anthu
😂😂😂 bon voyage kkk da gama emweyo wa gowelo
Aaaaa koma kunena zowona kutengela mmene analonjezela zambiri szinatheke 😢
Olo chimodzi palibe chomwe wapanga iye, 30minutes olo itakhara non stop sizingatheke ayi ,
Akutivutisadi ng'azi ameneyu 🐬🐊🐊🐊🐬
We really appreciate for this channel
Kkkkkkkkkkkk koma brother mumatha Inu mudzangokhala president ndinuyo chaka chikubwerachi
Kunkuyu umve zimene ndikunenazi,, iweyo ndi amene akumuuza zabodza chakwera wakoyo. Achakwera mumve Mau angawa,, kunkuyu akukunamizan ndi mfundo zake zopeperazi. Chifukwa iyeyu akukulimbikisan kukuuzan zabodza zomwe amalawi Eni ake sakukondwera. Muzafa ifa yowawa.
Best TV ever..may God continue protecting you Bakili Muluzi TV
Mr Kamwendonjira okudya Matako agaluwa sangawine Chisankho in the Next Polls
Boss mwaiwalatu chitukuko China chomwe MCP yapanga kupha Ralph ndi Chilima
Best tv bakili muluzi
❤❤❤timakunyadila man kwambiri tione ku lsrael ndi ku Russia zikuti bwanji kumeneku
Chakwela ndi mfiti kwabasi
Ine n'saname Chakwera amandinyasa
Kkkķķ😅
Chilichonse chamoyo chikàmaphedwa sichilephela kuphupha chikamafa , umu ndimomwe chikuphuphila chipani cha magazi cha mcp killing party
kumkuyu ma chende abambo ake chakwera ndi mcp ndizigawenga za kupha anamupha chilima mcp ndi chipani chazigawenga zitsiru zokha zokha
Chakwela mumuone khope yakeyo chigawenga cheni cheni akakhaka mkaka ngati wagwa kotamba
Chitumbili chingwile pangali mbwaa in 2025😂
Powerful long live bakili muluzi TV
😅😅😅😅koma anthu.inu musandisekese akut akaziwo mimba nguuu ngat mbuzi yakhuta mphale yokuba
Koma ada awa amatha kwambiri, kuwelenga mwachifase ndimodekha
Ali Maso rwaa! Ngati Nazikambe kkkkkkk koma Manganya😂😂😂
Chakwera waononga dziko la Malawi .angongwetsa kwacha mosanganizira anthu osauka
Abwana president chakwela Ali ngati chidole kapena kuti katuni ena amagomungwila ntchito zaumunthu uyu mulibemo ndipo ndi khutukumve chakwela wa mwazi uyu
Kunkuyu mapwala ake ndithu
Keep it up brother man!!
😂😂😂😂😂ati kagowero kkk km naseka bwanji
Akunamizana akuti awina ndipo sawina anthu ameneyo ndipo azafa ndi mtima ndithuu my vote for Dpp hoyee
Abwana bwanji mzakhale president zikuwoneka kut muli ndi nzeru zoti mngasinthire znthu
Afune asafune 2025 azaluza akumkuyu akumpusitsa kape wawoyo
Onse ndi amagazi mmanja kumkuyu sakudziwa comwe akuyakhula
Let me correct you in Mzimba sugar ndi k 2495 in big mart shop ya fair price
Chakwera dziko lamukanik passport anasiy kupang ndet only in lilongwe zoona zak achinyamat ntcht njee
Achoke I will support that
Koma pa udindo wa upulezidenti uja umafunika kukhala okhwima nzeru.😂😂😂akt amakajambulitsa zithunzi ku china akazawo Ali pompo ..
Chakwera chomwe wa kwanitsa ndi Mabokosi AMALIRO osati chitukuko Chitsiru cha munthu .
Kkkk 😂😂 khaniyo ndiyowona amange gowelo bs zachamba bs
Akapume atisautsa mokwana agalu amenewa
l,m watching from .am angry with Britain .mcp never win
Best TV in Malawi keep
Bakili TV number one ❤
Kumukuyu alibe ku immigration anthu akuvutika kwambiri komaso kuba passport amati yikhala k50,000,pano ndi k500,000
Mosses ndi mmodzi mwa afiti mmalawi muno.
Inu ndinu heroe bwana ,MCP isazabwelere muboma kufikila titafa chifukwa muwaru,gadama,solobala ,chilima,chisiza anaphedwa ndi MCP komanso amatenje
Tamulimbikiseni nkhani yomanga gowelo Ku airport komwekoyo😂😂😂
Akadzi Ake kamimba ngu Ngati mbudzi yakhuta mphare yakuba 🤣🤣🤣
Kkkkk akuti umange gowero Garu iwe
tafufuzani za ku Burkina Faso kuli president wazeru kwambili mutibweletse mbili yake bg man
Yes plz
Kkkk ati kamuyenda njila anadya matako agalu.nde ndi nkazake ngt otupa mutu uja😂
Komanso Mzuzu airport Ngati airport ya witchcraft kkkkkk
He has forgotten about the boolet train your just reminding him now poor Malawi that used to be a milky and honey country shame on us 😂😂😂😂
Ndiana sakuziwa kathu auze mwina aiwala. 😅😅😅
Chakwera tatopa nayo bolani afe basi anthufe tatopa naye kwambiri
Tikhara kuti tikungotukwana bas pa social media sizitithandiza
Ife tingopanga zoti Mulungu atione ndikutivera chisoni basi
Tizizivera chisoni kuti Mulungu atikhululukire
Kkk koma ndaseka yandibaya yomanga kagowero ku ku airport
Tell tell my favorite bro Lai malawi ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Mcp izalila maliro onyamula wina azathawa malawi akufuna
President uyu ndi pa nja penipeni munthu osadziwa chimene akuchita ndi munthu wanji
Sindikudziwanso Kuti ndiophunziladi uyuuu
Kunachita kuyiwala zomwe alankhula dzulo zimayenda Koma mkalasi munthu ameneyu
Iwe aise video iyi ndiyakale wamva galuso iwe eti uzingoponya ma videos akale kale
Best TV ever
Malawi politicians are all poor minded because all of them are just after money after these ones other Gandangazi are coming ooh my beautiful country 😢😢😢
Apm my vote
Ndaonadi nkhope yamfitidi
Enainutu mukutukwanira ameneyu mukuziwa kut 2025 muyaluka amanena chilungamo maka mphava za MCP zimadananaye ndipo anamachende achakwera ndiguluranu tikumana 2025 minyeromwanu nonse😊
Chakwera Kodi sigaru ameneyu
Kkkkk khani ndiyomanga gowero ,
Best TV in Malawi 🇲🇼
😂😂.😂 Chilichonse chakwera ndichakwera adatelo APM
😅
Yakwia ndi mizimu
Zoonadi amange Gowero ku Airport komweko.
Chakwera mbole yamake anthu akutinena kuno maina osiyana siyana akuti ndiife chikangawa😢
In fact chakwera nd mbuzi
Chakwera zimene wakwanitsa kupha chilima basi palibepo chimene akupanga komaso nanga asikali Aja Amati azapanga ma video ya momwe chilima alikuti anthu Aja chonde asawaphesotu
Bakili mulizi❤❤❤❤
Awuzeni agaluwa apange zoti kumwelako anthu onse akhale okhozekera kukaponya ma vote awo powapasa chaudzika in time cz ngati izi sizitheka obviously mcp izabela ma vote komanso kuchepa kwa anthu ovota kumwelako zizathandizira kuti mcp iwineso ndiye chonde yesesani kuti anthu kumwelako axavote ndithu
Thanks brother for news
Akadzi akenso sanatchene Childress cha kumidzicho mpaka China sure bwanji manyazi chimodzi chokhachokha
Kkķkkk koma iwe akuthyola kholingo chakwela ndi satana
Zikomo Bakili TV Pamozi ndi aulusi ena ndi ena pomatiziwisa
Kunkuyu ndi mfiti otheratu
Gautrain from Pretoria to OR Tambo international it takes 1, 30minutes is only 45kilometers
😅😅😅 at bola Vasco da gama 😅😅
Ameneyudi ndi kamwendo njira akudya matako agalu 🐕🐕🐕😂😂😂😂, mbwaa ya munthu 😂😂😂😂
Dziko la Malawi silidzasithaso ngt atsogoleli anthu sadzasintha
They will be no one who will fix this Malawi let's just be honest the one who can take over will be worse than this
Hello sir morning's ❤❤❤
Mwati vasco dagama eti😅😅😅😅😅😅
Bwana kumanena kuti mwamaliza 🙄😫
Amangokhala chateee😂😂😂😂
Kumkuyu ndi Mr nonsense
Zoonad MCP singawineyi, thanks bro for informing us
Iwe osamaba za bakili muluzi tv
Mangochi lake city and makanjila road and international Airport Mangochi 5star hotel palibe chimene wakwanilisapo palibepo ngakhaleso analonjeza mafuta onsika ndi fetelazer zambir
Nthawi Yakamuzu Timagula packet ya Sugar k1 , nyama 1kg 20 tambala, thumba lafeteleza lili pa k2 koma boma ili zonse zafika mma sousande, what a shame
Mwammodzi ndine anandimana ngongole kunifu kuwapatsa achipani
Aaa uyu chakwela ndi MCP yakeyi wawononga dzinthu kukwela passport ndiyi akupanga katon KWACHA YASALANO CHIDZUDE CHA NDALAMA PANO KUMANGA ANTHU PA DZIFUKA ZAZIIII dzotsedzo ndikuphatso chilima aaaa awa ayende bwino adzazabweletso boma MCP ndi agalu kwabasi
Ndipo Mcp sizalowaso mu boma