Mwakasungura mariro ake ati umufuse kaye chakwera kt bwanji akumanga anthu nthawi yorira paribe zot mupusise anthu apa kenya kenya bas aporice samarani mademo awawa ndi aja anthawi ya bingu osat zoma opyezana ngat murinkanthu nanu mukuvutika masary anu onyenyekaso
Ndiye funso langa mkumati ngati tikulira maliro nanga bwanji ena mwawolilawo akumaponyedwa mundende pamene misozi yawo ikadari kutsikira mumchifuwa 😢
Uyu alibe mfundo mwakasungura iye amamuzunza ,Bingu iye amuletsa ndani asatikwiyitse akhale chete
NO PAIN NO GAIN PASEWO BASI AWONA WATUMINDWA AMENEO BWANJ CHAKWEL SAKHULILA OLILA NDIFE BASI BUZIWE
Ndipo mademo awawa atipatsa mangolomera ngatimomwe achitila anzathu achinyamata aku Kenya well done those Genz ndikawawa
Mademo achitike,iyeyo ngati akuziwa kuti tikulira maliro, bwanji anthu ena omwewo olilawo akumangidwa, komaso kwacha ikugwesedwa,
Pasewu papitidwe bas more fire
Mumuuze mwakasungulayo Kuti ndi mbuzi 😮
Amutuma
Machende ake manganya mwamulumbilisa liti musatitengele kuthako tell chakwera machende ake 😢😢😢
That galu is drunk demo yikhalepo basi mo faya 🔥🔥🔥
Mwakasungura mariro ake ati umufuse kaye chakwera kt bwanji akumanga anthu nthawi yorira paribe zot mupusise anthu apa kenya kenya bas aporice samarani mademo awawa ndi aja anthawi ya bingu osat zoma opyezana ngat murinkanthu nanu mukuvutika masary anu onyenyekaso
Tikufuna ma demostration , undule mwakasungulayu wakakamba panopa alibe mzelu
Sizikungwilinzana anthu tidalunza kale nde amene tili moyofe tife pawiri
Koma kwamangidwa anthu ena mnthawi yomweyi yolila bwanj Sanabwere poyera kudzayakhula mbwelelazi,, zopusa zimenezo
Akateroo amupasa chibazii,ma Demo sakulephereka , ngati tikulirabe maliro y anthu akumangidwa
Machende ake Galu amene apasa ndalama Galu chimunthu banda wakunamiza
Akulesamademo chamba
Mademo kulibe ndipo sachitika mademo kumalawi kuno anatha ndukuzanizi ndizoona pls tikulilaso maliro awachiwiri kwa pule ndithu sachitika ndipo ndizoona
Ndikape kwambilit ameneyoyo
Maganizo opusa kwambili ndikangati athu apita kokambilana ndipo mphindu ndichani ngati walandilla zake asatinyasepo ife iwe ndati wadananazo uzizangodya ma pwevipwevu akowo zosochelesa amalawi zithe tose tikulila iweyo wapambana chini zaziiiiiii
ifetu osamatitengera kuntoso ngati malilo anjoka iyeyo ngati akudya ndalama si onse omwe akusangalala mzipatala makhwala mulibe mwadimac chimanga sichikupezeka kwacha ikungogwa mwa uchitsilu mwatasakotu kubomako koma lafote likukwanilani agalu inu
Aaaaaaa sizikugwilizana mgati iyeyo akutele a vise president anasakhwidwa bwanji analephelanjji kuwalesa amenewo
Mbuzi yamundu
Akunama ameneyo Ife tipitatabe pasewuuu
Undule ndi wadyera wazipakula. Ine asandiyase
Uyu anapusa kale kale tinamudziwa pakanthawi
Msdemo kulibee ndukuzanizi muzisunge mademo panopa sangachike ai mwina kutsogoloku koma pano tikulila basi wina ali tiyeni kumademo apupuluma adikile kaye
Anthu mulibe nzeru Mulimbikila kuchita ma protest chifukwa chakuti kukenya kuli ma protest kwafa anthu angati ku Kenya pitani muwapangile ndalama anzanuwo
Wapatsidwa ndalama galu ameneyo
Amaneyu ndi galu kwa basi amakhalakuti tikamugende tikamuwotchele nyumba
Amupasa ndalama a Mcp chisilu ichi muthawi ya ifayi aboma akowo apanga zinthu zingati
ayi mademo achitike bwanji Boma likumanga anthu amene tikulila
Tikuvutika Ndife iwo akunjaya ndi ndalama za misonko yathu pamtumbo pako galu iweyo ukudya nawo ndalama zakuba za chakwela Galu
Adatha ameneyu musamuvele.
Tiyeni toooooooonse......pa 10...ku mademoooooooooooooo😂😂😂😂😂😂
Iweyo ndiwe ndani pamtumbo pako ku Kenya wawona azako anthu akuvutika kuno Galu iweti wakumana chakwela nonse machende anu
Pasewu bas
Galu ameneyo. Ngati watumidwa utafe ndiwe
Dont mind him. his looks have spirit of serfish akungoti bora akukhukuta alibe nao anthu ntchito anthu akuvutika dziko muno
Mumuwuze mwakasungula patumbo pake
Inde takapangeni ma demo koma phindu lake likhala chani zonsez zitsintha chifukwa Cha mademo
Mbuzi ya munthu
Uyu galu kwabasi asatinyasepo ameneyi
NGATI AMUTUMA TIKAMUTIKITIRA PANYUMBA PAKE MBUZI YAMUNTHU AMUTUMA ACHAKWERA MUFERA LIMODZI NDI MCP YAKOYO ANTHU TATOPA ZOKAMBIRANASO PALIBE ATIZOLOWERA AGALU AWA INU AMENE MUKUMUIKIRA KUMBUYO NKULUYI MWADYA CHAMBA CHOMWE AKUMADYA CHAKWERA AKAFUNA KUPHA ANTHU NDIEKUKWEZA KATUNDU
Ndichifukwa kufunika ma demo, aliyese otsutsana ndi demo,ali kazitape wa boma lamulo la demo afe ndithu.
Mbolo yamake galu ameneyo ndikanakhala ku Malawi ko ndikananthana naye chisilu chamunthu ichi mademo wooooooooye
tilira pa masiku 21
A choke amenewo zausilu
Km iye sadave kt nthawi yomwe tikulilayi kwacha idagwaso ndiye tizingosekelela zimenezo tikamatche panseu basi
Mwakasungula machende ako iweyo anthu akumudzi akuvutika kwambiri kumanena zoti anthu aspange mademo mowa umenewo wamwa kuti 3:01
Km iye sadave kt nthawi yomwe tikulilayi kwacha idagwaso ndiye tizingosekelela zimenezo tikamatche panseu basi 3:01
Tiyeni tiyeni 🔥 ameneyo ngati wamutuma chakwera zake zmenezo
Zopusa watumidwa uyu Ife osauka ndiamene tikukumana ndizowawa tipita pansewu basi nanga Ngati tikadalila malilo ndifukwa chani a boma akumanga anthu nde iwo sakuwona Kuti tikulila malilo
Mwadya banzi uyu
Ndiwe galu kwabasi ngati warandira ndarama ka gwere wuko nyani
Efe tipita bas pa musewu
Mademo akhaleko msamuvere ameneyo komano akhale a peaceful osakhala ngati aku Kenya unless apolisiwo ngati angapange za ukape then take them on
IWE NDIWE OPUSA OKUBA IWE WAPASIDWA NDALAMA UGALUWAKO WALILA AMAKOO
Akunamatu ameneyu
❤
tiyeni pa sewu osasekelela dzompusa
Watumidwa ameneyo galu ameneyo palibe zokambilana apa
Ndichisiru akumanga abwanji athu ndiwe osaganiza bwino umadya bwinotu iwe athu akuzuzika mbolo yako wadya chibazi😅
Akuphasa chidadzi uphusa iweyo
Mbuzi ya mcp iyi chitsiru cheni cheni cha munthu
Amakhala mbali ya boma akulu amenewa
Musiyeni umphawi wamuswa ameneyu
Enawo akukwanisa bwanji kumanga andu kapena kugwesa kwacha ife tilikoko
Mkati molira momwemo mzika zili mkati mofinyidwa mopanda chifundo, ndiye zikusiyana pati?
Adindo akuyenera kukhala osamalitsa posaonjezera mikwiyo kwa a Malawi.
Mademo achitikile kunyumba kwa ameneyu
Ma demo alipo whether he likes it or not...
Ndi galu ameneyo wapasidwa chi banz
Napanyelo amei Galu vuto lake chakwela ndi osamva za anthu amei kumunyala mademo azione ruto ku Kenya
Ngati amalawi akulila makiro nanga anthu akumangidwa bwanji?
Funso mkumatero
Mumuuzekuti asatiphuzitse kutukwana enafe tinazolowela kupeleka ulemu
Ife kuno ku lilongwe tinamaliza mademo mwina kimwera kwanuko
Akufuna akawadyetse bans ma representatives wo basi end of story
Tiyeni Tiyeni Tiyeni pa sewu musamumvele wamisalayo
Walandila Ndalama ku MCP AkusakupusaniMbuzi Yamunthu
Galu ameneyo siyen palib akuziwa
Ma Coward remember JB
Akudya limozi ndi chakwe lol a
Amupasa ndalama zambiri ndichisiru ameneyo
Ndiopusa ameneyo
Akunama ameneyu
Angophedwa basi munthu olesa mademo
Mboliyake iyeyo anthu akulila ndeno bwanji kwacha ikungogwa daily
Uyu anagulidwa kale ndi aroma and there is nothing chanzeru chomwe amalankhula
No sitimva zimenezo takwiyatakwiya bas..kumanga president wathu Bon Kalindo ife tikuona..no sorry 😢😢
Pajatu abambo awa ndiopanda phindu kuyambila kale za ziiii
Malilo talila kwakwana sangadzukeso Basi tiyeni ku mademo
Give me his name
Ma demo ndiye kulirako
Vilekeke
Ndi galu ameneyu anthu asamvere galu uyu
Pantumbo pake pamakeso ife pa 10th July tipita pansewu bas
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Bwanji ena akumangidwa ena akulira??
Ndichitsiru ameneyo wadya bazi let's go guy's apa ndi Kenya Kenya fire all idiots
Akati mpala ngati?? Chende zako
Ndigalu kwambiri akuletsa mademo yoo.
21 days yolira ikhala itatha podzafika pa 10 July.
Akumanga bwanji ngati akudziwa zoti akulira.
Asatichimwitse mayankhulidwe
Amutuma ameneyo mbuzi yamunthu.. Bwanji Ngati tikulira maliro why akumanga anthu osalakwa .why akugwetsa Kwacha nthawi yorila .Mr kasungula kagwere uku mukupita Ku mademo siinuyo mwadya baz