Msika Wa Ziwalo part 2...

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 11. 02. 2023

Komentáře • 56

  • @lawrencemsefula5108
    @lawrencemsefula5108 Před 5 měsíci +1

    Great work Abel God bless you..

  • @burnnetsikwese
    @burnnetsikwese Před 5 dny

    Mulungu ndi mwini chuma

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 Před 9 měsíci +1

    Mwanayinso ndi opusa bwanji samakana

  • @aleksawilliams710
    @aleksawilliams710 Před rokem +2

    Tikuyisatatu nkhaniyi,,,momwe amkakambilana ndi Mr manjolo ndi Enest yo timazimva ndipo akut wakhala business akupanga wagwidwa nayeyu ndiwanambala 5,,,ntchito yake ndi yomweyo koma samagwidwa ,makolowo akungodandaula Poti kubeleka koma nanga akanakhala kut wagwidwa Mathews yo atamupaha kale zikanakhala bwanji? Tiunikepo pamenepo a Abel,from Balaka thank u

    • @victoriawilliam4490
      @victoriawilliam4490 Před rokem

      Ine kuona kwanga ndikuona ngati mkulu waku Thyoloyi ndiamene amamukocha mwanayi kuti azilankhula zimenezi cholinga ogulawo amukhulupilire msanga

  • @abdulkatopola3612
    @abdulkatopola3612 Před rokem +3

    Tapezani camera yabwino pls ndinu wailesi yaikulu pls

  • @bobchola5083
    @bobchola5083 Před rokem +1

    Nice one Mr Abel

  • @user-eo7om7vj8e
    @user-eo7om7vj8e Před rokem

    Big up manjolo God bless you

  • @arnoldtem4
    @arnoldtem4 Před rokem +1

    Mr well done

  • @graceelias7381
    @graceelias7381 Před rokem +1

    Good work Abel

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 Před rokem +2

    Mwana okongola Mathews

  • @janemvubu7750
    @janemvubu7750 Před rokem

    Good work mr Abel

  • @maxwellmustafa3078
    @maxwellmustafa3078 Před rokem

    God bless you Mr Abel

  • @medsonkapondera5836
    @medsonkapondera5836 Před rokem

    Zandikhuza bravo kwa a TA ndi majolo

  • @standykuchaga5355
    @standykuchaga5355 Před rokem

    Nice continue Abel

  • @user-fe6pp9gc6u
    @user-fe6pp9gc6u Před 7 měsíci

    Good job Mr Aber

  • @alexgweje8610
    @alexgweje8610 Před rokem +1

    Anthu amene mumachita mchitidwe uwu wonyansawu Mulungu azikukanthani ndithu

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 Před rokem

    Makolo amwanawo asabakile mwana wawo..ndipo mwana ameneyo a langidwe basi ..iyeyo analora bwanji nanga anthu four aja ..alangidwe basi

  • @user-sl6ty4dv6n
    @user-sl6ty4dv6n Před 7 měsíci

    Good boi, God is with us all, be well my boi

  • @BdhfbHdhe-pd7nh
    @BdhfbHdhe-pd7nh Před rokem +1

    Grory to be God

  • @user-eg5zi2jk7p
    @user-eg5zi2jk7p Před 9 měsíci

    😢😢😢😢nkhondodi ndianasi kuti muivetsetse nkhaniyi anthu wa ndpachibare kufuna kugulitsa mwana wa m'bare wawo

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 Před rokem

    AMalawi mphada amene mukupangayo muzitenga anu ana..mudzafa manja ali kumbuyo...

  • @chifunirosaka9077
    @chifunirosaka9077 Před rokem

    Achinyamata osamatengeka ndizinthu zachabe chabe zopandatsogolo taonani mnyamata uyu akufela zaeni chifukwa pakhomo pake pakuoneka povetsa chisoni kwambili

  • @mathewsscotch2105
    @mathewsscotch2105 Před rokem

    Aaaa ndimadabwatu kuti ithera pompaja

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 Před rokem

    The boy is genius than Chakwera wa monika ..Akadakhala chakwera bwez akungot sindikudziwa ... kufuso lililose

    • @cliftonmsowoya
      @cliftonmsowoya Před rokem

      Ndipo sukunama aise chakwela chilichonse samachidziwa 😂😂😂😂😂😂

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 Před rokem

    Akanakhla majolo kunena kuti abwere munthu wamoyo Kodi Elosoni akanatha kumupha mwanayo ndikupitisa ziwalo??? Nkhani yovuta iyi

  • @josephybenjamin3877
    @josephybenjamin3877 Před rokem

    Tendai Mezzan akuti2 mwana wa afiniyasih

  • @isaacmussa2942
    @isaacmussa2942 Před rokem

    Umphawi okha okha chosecho mukupanga business yoopsa achita bwino kukumangani agaru

  • @ambuyampundubanda9419

    Good job, but when you say that hidden part do so. We can see the gentleman. Edit the video.

  • @tshepangmatebele7822
    @tshepangmatebele7822 Před rokem

    Nkhani yomvetsa chisoni komanso yoopsa

  • @elizabethziba1652
    @elizabethziba1652 Před rokem

    Eshiiiii koma the trauma amupatsa mwanayi eeee God have mercy on us

  • @lilianchikondi195
    @lilianchikondi195 Před rokem

    Bomanso limaziwapo kanthu zazimenezi, that's why sapanga kanthu akamvesedwa zaizi,we thank mibawa tv potulusa poyera nkhani zi

    • @cliftonmsowoya
      @cliftonmsowoya Před rokem

      Kunakakhala kuti ndiku south zitha kale kale izi

  • @gracechiumia7103
    @gracechiumia7103 Před rokem

    Munthu ameneyo chilango chikharepo basi nanga akanati apitise ziwalo simwanayo akanampha basi?chilango chikharepo kuti anthu ena atolepo mphuzilo

  • @rabisonpias5131
    @rabisonpias5131 Před rokem

    Nkhnai Zomvuta, Mwanayu Kodi ali ndi Dzaka zingati..!?
    I mean mwana emwe adatenga mwana mzakeyuu..!?

  • @geniuskamwanje
    @geniuskamwanje Před rokem

    Manjolo thank you

  • @tingamasi106
    @tingamasi106 Před rokem +1

    Tikudikira part 3 yaku police

  • @victorauwana7258
    @victorauwana7258 Před rokem +2

    Handsome kid

  • @TheVizionet
    @TheVizionet Před rokem

    Manjolo ndi a TA ndiofunika kuwafufuza

  • @mbawabuliyan9704
    @mbawabuliyan9704 Před rokem

    Zachisoni kwambiri Mwana wa bwino bwino

  • @aleksawilliams710
    @aleksawilliams710 Před rokem +2

    Tikudikilirabe part 3 ngati mkotheka Mr Abel🤗

  • @cliftonmsowoya
    @cliftonmsowoya Před rokem

    Komanthu eeeeeee

  • @pauldaka7966
    @pauldaka7966 Před rokem

    Tikusatira mwachidwi

  • @user-vx4gu4fs9s
    @user-vx4gu4fs9s Před rokem

    Mulungu nd wamkulu basi

  • @omarlux3434
    @omarlux3434 Před rokem

    Zachisoni

  • @ellenjulius-jk3jb
    @ellenjulius-jk3jb Před rokem

    A mfumu kuyakhula kwake kumeneko angaweluze khani bwinobwino koma

    • @rosebanda3613
      @rosebanda3613 Před rokem

      😂😅😂😅😂

    • @thokokawaza
      @thokokawaza Před 5 měsíci

      Amfumu wopusa awa, seems akudziwapo kenakake! Akuikira kumbuyo chigawenga

  • @janetmanda6412
    @janetmanda6412 Před rokem +1

    Umphawi wasanduka nyambo pamalawi ya anthu achuma, someone big behind the scene

  • @pauldaka7966
    @pauldaka7966 Před rokem +1

    Tikudikirabe zakukhoti zinayenda motani?

  • @Malani41
    @Malani41 Před rokem +4

    Thanks for continuing this story! I feel it for the poor boy! I’m glad that he is saved. His fate was about to be gruesome!!! Kudos to the two people who saved this kid. It hurts to even imagine how traumatizing this is going to be for this kid for the rest of his life. We all need to be following up on him. Just sad. Wish the perpetrators got the death penalty for this.