Chisawawa | Maliro Achilima | Timva Zinthu | Tiyeni Tidekhe Kaye Amalawi.

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 11. 06. 2024
  • #malawi #trending #viral

Komentáře • 73

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před 3 dny +1

    This should mark the begining of a great revolution in malawi. Panunkhe mphila basi sitidikiranso za 2025.

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Před 6 dny +6

    Koma chakwera 🙌🙌 mupaka kumpha muzanu ngati galu mulungu akukathe ndithu kulimba mtima ngati fiti yayikazi Koma wayaluka kulibe kuwina 2025 wukazawina ndiye Kuti wabera Koma sikuzakhara mtendere

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim Před 6 dny +7

    Sadiki mia ,chiwaya kasambala lero chilima amalawi tidzaputsa pakana liti chakwera ndipitanaye

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Před 6 dny +7

    Udindowo saupeza Chakwera. Chakwera ndiwe otembereredwa.

  • @abdullalajabu5871
    @abdullalajabu5871 Před 4 dny

    timawonedwa kupusa amalawi chifukwa choti ndefe odeka komaso sitikuyiziwa nkhondo fuso ndikumati tizapange bwanji kuti nafeso tizakale osawopa😭😭😭😭

  • @IsaacTsinde
    @IsaacTsinde Před 6 dny +4

    Sichinakawinina chimenechi kupanda Chilima amuphayo

  • @johnlameck8366
    @johnlameck8366 Před 6 dny +5

    Koma chilima yenkha anamulakwira bwanji

  • @user-lq4bc2dr2n
    @user-lq4bc2dr2n Před 6 dny +1

    Palikundu pake ndipo galu ameneyo achite kuyipa khope ngat utsiku 4😭😭😭

  • @SandraIssa-lo8il
    @SandraIssa-lo8il Před 4 dny

    Komatu Chilima mwamulakwira kwambiri. Anakumenyerani campaign kuti muwine in 2020, lero mwapha munthu amene adakumenyerani nkhondo, inuyo mmadziwa bwino kwambiri kuti ku north and Southern region without chilima simukadawina. Ndipo this tine around forget it

  • @janetchinga695
    @janetchinga695 Před 6 dny +4

    Chalakwika kwambiri kupha anthu Ena chifukwa cha munthu mozi 😢😢😢

  • @BlessingsFranklinWadson
    @BlessingsFranklinWadson Před 6 dny +3

    Pwanya pake chakwera pamtumbo

  • @user-lf6qf2tw5o
    @user-lf6qf2tw5o Před 6 dny +3

    Zonse ndikulakwitsa nanga ndindan amafuna kufa pa onsewa

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn

    Ngati a Malawi apapa sitipangapo kanthu palibenso tsogolo la dziko

  • @MaureenMchenga
    @MaureenMchenga Před 3 dny

    Zosakhala bwino kwambri😢😢😢😢

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před 6 dny +2

    Ambuye atichitile chifundo ku Malawi ndikutukhululukila pazimwe sitinachite bwino pamaso pake😭😭😭

  • @AgnesChikonje
    @AgnesChikonje Před 6 dny +3

    Komanso munthu modziyo amupheranji poti democracy ndiyawina aliyense

  • @pepichikako7122
    @pepichikako7122 Před 5 dny

    Koma Amalawi atopa. You know our people can be ruthless. Ine if I were him I would seek asylum. He looks like people want to take revenge on him and his family members.
    My prayers to the Chilima and all our fall Malawi government crew.

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před 3 dny

    Chitsiru chinanso ndi army commander valentino, osanyengerera, asowe.

  • @patriciagondwe2934
    @patriciagondwe2934 Před 6 dny +2

    Mulungu dalisani malawi

  • @user-ic2xk6kg9z
    @user-ic2xk6kg9z Před hodinou

    😭😭😭😭

  • @Justman34_dislike
    @Justman34_dislike Před 4 dny

    Chilima walakwanji abale😭😭😭

  • @benzobanda-ed8tp
    @benzobanda-ed8tp Před 4 dny

    Good

  • @benzobanda-ed8tp
    @benzobanda-ed8tp Před 4 dny

    Good wayankhula bwino bola akanafa ndiyeyo chichakwelacho

  • @jamesbanda1730
    @jamesbanda1730 Před 4 dny

    Mr president what happening in Malawi ha our home hear of Malawi our country is finishing with politicians Malawians are know going tru problems of end of Malawians financial Mr president must step don Malawi this movement of Kamuzu Banda know in Malawi Malawians the are back old movement with some people of Kamuzu Banda Gov.

  • @user-mf8fi8wt5d
    @user-mf8fi8wt5d Před 4 dny

    Anthu akwiya kumene this is not the 1970s anymore

  • @AbdullahaziziAmoswalala
    @AbdullahaziziAmoswalala Před 6 dny +2

    😢😢😢

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Před 6 dny +1

    Awuzeni ndithu mwina anva tikulira ife😢😢😢😢

  • @ElliottBelon
    @ElliottBelon Před 5 dny

    Mulungu akudziwa 😭😭😭😭

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v Před 6 dny +3

    Chakwera Chakwera Chakwera wapha Chilima why

  • @kolslongs2740
    @kolslongs2740 Před 6 dny +2

    So sad

  • @Short1212-ny4ng
    @Short1212-ny4ng Před 6 dny +1

    Tikupeza tikupanga

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim Před 6 dny +1

    Malawi poison party mmmm chakwera imfa yomwe yagwika lero chilima mawa idzakupeza .

  • @joaojoao1983
    @joaojoao1983 Před 6 dny +1

    Munamusanka ndinu.

  • @TressLuka
    @TressLuka Před 6 dny

    Malòdzatuuu 😢😢😢😢

  • @JacksonMoyo-tm8dv
    @JacksonMoyo-tm8dv Před 6 dny

    Achakwera, zikhale ng'oma ndi kunkuyu atule pansi udindo atiphweteka kwabasi

  • @Justman34_dislike
    @Justman34_dislike Před 4 dny

    Sikusinja Gwenembe

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq Před 6 dny +1

    Amalawi dzofuna tingoyamba khondo basi

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Před 6 dny

    Kodi anthu amenewa akulira onsewa ntendere mukupeza komaaa???😢😢😢😢😢😢

  • @IsaacTsinde
    @IsaacTsinde Před 6 dny +2

    Afiti opemphera a chakwera

  • @fumbomumba5016
    @fumbomumba5016 Před 4 dny

    Chakweka ndi mbuzi kwabasi

  • @EnelessLundu-sn8om
    @EnelessLundu-sn8om Před 6 dny

    Kuntcheu kokhako osakamupatsa mpando kt akhale gwape ameneyo

  • @KasimuMaulana-mu8we
    @KasimuMaulana-mu8we Před 6 dny +1

    Kwamtele ndi chimadala

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i Před 5 dny

    98% says a ........ ndi omwe apha a .......😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt Před 6 dny

    Koma ife amalawi tilibe nzelu ndithu tinamusankha tokha gulu uyu chakwela Kodi tingaskhe munthu woti alibe kalikonse ndikumusankha kuti akhale president zowoona zimenez andiso munthu woti akuthawa mulungu ndikusata satana ndiye ife nkumati ndiwabwino alongosola zinthu zoona tiyeni tiphuzilepo kanthu ife amalawi tiyeni tiseguke matso

  • @user-vf2fo1mb2c
    @user-vf2fo1mb2c Před 6 dny +1

    Devils kupha no good

  • @JosephChatama
    @JosephChatama Před 6 dny +1

    Mbudzi yamano kusi ikufuna umboni wina

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e Před 6 dny

      Chisiru iwe kwabasi mbuzi anamno ako ndi amako iwenso ndi wamagazi mmmm munya muona asatanic inu

  • @EliasBanda-qj4bn
    @EliasBanda-qj4bn Před 4 dny

    Chakwera nigalu kwambiri

  • @mostermostz5895
    @mostermostz5895 Před 6 dny +2

    Simikizilan ngat chakwera waphad chilima. Osamasokoneza maganizo azanu. Ngat pali umbon okwanira ufotokozen tikusaten

    • @FosterChilumba
      @FosterChilumba Před 6 dny

      Kamanyi wakudambwe iwe ukuti chiyani

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e Před 6 dny

      Ufuna unoni wanji cakwera ndi wakupha wasatanic mbusa wakumidima wapha chilima ndi anthu ena munthu oipitsitsa mdziko lamalawi osava chisoni ladzalo cakwera

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j Před 6 dny

      Chakwela ndi okupha kumene ndipo aka sikoyamba ,wakhala akupha kuyambila ku church pofuna utsogoleri. Koma apa ndie walakwila dziko lonse pakupha chilima.

    • @ElliottBelon
      @ElliottBelon Před 5 dny

      Mboli yako

    • @user-wd9yd1bg9n
      @user-wd9yd1bg9n Před 5 dny

      Olo iweyo umboni oti chakwera ndiyemwe wapha ulinawo koma ukufunsa chinyezi mbafa galu iwe.

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem Před 6 dny +1

    Tibweze bas

  • @PatriciaMbewe-xn7ke
    @PatriciaMbewe-xn7ke Před 6 dny

    Zowawatu koma

  • @ChosenChirwa
    @ChosenChirwa Před 6 dny +3

    Ndipo angodikira tiyike maliro awonasotu chakwera

  • @michaelamon9691
    @michaelamon9691 Před 6 dny +2

    Nkhani yolowetsa ndale pa maliro.

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 Před 6 dny +2

      Ngati mwapha Chilima ndiye mukalowanso mudzapha angati? Afiti otembereredwa inu.

    • @spargomw
      @spargomw Před 6 dny +3

      Zitakhala zachitikira m'bale wako ungayankhule zopusazo? Misozi ya a Malawi ikhala ikumkumbutsa Mulungu dairy ndipo Mulungu aika chirichonse pa Mbalambanda

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e Před 6 dny +1

      Ukati palowa ndale ukutathaudza chani iwe ndi opusa amalawi tikudziwa kuti cakwera wapha chilima mcp chipani ca magazi

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 Před 6 dny

      @@user-hm9nc7lz6e Mkazi wanzeru kwambiri. Chauta akudalitse umaganiza mwanzeru.

  • @ulemujumbe8501
    @ulemujumbe8501 Před 6 dny

    Komanso mfiti imeneyi isakapezekeko Ku maliroko

  • @robertkalima874
    @robertkalima874 Před 6 dny +3

    Akuwuze ndani? Pita kafufuze sinanga uli ndi nzeru kwambiri. Kuyankhula mopusa uku

  • @jamesbanda1730
    @jamesbanda1730 Před 4 dny

    No no no as pastor

  • @georgeraphael8198
    @georgeraphael8198 Před 6 dny +1

    Ndi ngozi basi,a Malawi kupusa bwanji,muzachangamuka liti kodi? Kodi oyamba kufa pa ngozi ndi Chilima ekhayu?
    Musachuluse kulankhula zopusa, chifukwa anali munthu omveka za ziii 😂😂😂😂😂😂

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e Před 6 dny

      Udzinena zimenezo ndi amako wamva cakwera wasatanic wapha chilima

    • @EnelessLundu-sn8om
      @EnelessLundu-sn8om Před 6 dny

      Muuzeni chakwera kt akubanja akt usapezeke kumaliro kt adziwe kt anthu takwiya naye opusa ameneyu

    • @KestonNGUBO
      @KestonNGUBO Před 4 dny

      Pa manyo Ako wav iwe

  • @user-kj6qj1md5e
    @user-kj6qj1md5e Před 6 dny

    Tikaonana kumaliloko ndiwathu ku ntcheu wina akatsala ine zachamba sifuna