Achakwera Akuona Ngati Chakachamawa Awinanso | Khad Wang'aluranso | Inu Mukuona Bwa

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 16. 06. 2024
  • #chilima #utm #chakwera #trending #malawi

Komentáře • 258

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 Před 9 dny +12

    This channel has to glow big....
    Its wealth watching kuwuza ntundu wa amalawi zomwe ma station ambiri will never broadcast .......
    I really support this channel sir salute....
    Machiaveli.....2pac shakur

    • @user-tk6qh9zs7h
      @user-tk6qh9zs7h Před 8 dny

      Tamangolembeni Chichewa chomwechi mutafuna mutha kumalemba Chi Lhomwe chanu chomwechi.
      Kamba kakuti English ndi Chichewa zonse zikukuvutani malembedwe

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja Před 9 dny +10

    It's true my brother these is seriously issue. MCP ndi AGalu

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z Před 9 dny +4

    Powerful message!!

  • @PetroJack
    @PetroJack Před 9 dny +21

    Chakwera akudziwa kuti waluza kale ndipo omuvotera ndi dzitsilu

    • @JamesNgwaya-vz1ox
      @JamesNgwaya-vz1ox Před 9 dny +1

      Avota afamily bas

    • @user-tk6qh9zs7h
      @user-tk6qh9zs7h Před 8 dny

      Kapena winanso uyu.
      Mbuzi yeni yeni iyi

    • @JackMvura-ik2td
      @JackMvura-ik2td Před 8 dny +1

      @@user-tk6qh9zs7h wamanyi iwe nyani wachabe DPP inatha achita Kufuna winanso afe akapangenso ndale MCP timalemekeza maliro yense osapota DPP ndiwachilomwe

    • @user-ky4ce9gb6j
      @user-ky4ce9gb6j Před 7 dny

      Ndipo zoona tu mm

    • @user-ky4ce9gb6j
      @user-ky4ce9gb6j Před 7 dny

      Anthu awawa apanga zinthu zowawa mmm

  • @sionpou2725
    @sionpou2725 Před 8 dny +1

    We need people like you in our society to tell citizens the truth

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc Před 9 dny +5

    Ma support mcp evil 😈

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 Před 7 dny

    My brother your the best and genius 💪💪🙌

  • @wittinessnkhokwe
    @wittinessnkhokwe Před 9 dny +5

    Following you sir

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 Před 9 dny +6

    My sister has been ill for days and went to St Maria Gorretti with mini - stroke and they told her to buy medication in chirani pharmacy

    • @ChristinaChimombo
      @ChristinaChimombo Před 9 dny +1

      Buy STC 30

    • @raytavares2256
      @raytavares2256 Před 8 dny

      ​@@ChristinaChimombondayamika ndikuthoza moopsya for advice mwandipatsa for my sister, I really appreciate what you have said and I don't take it light. Thank you so much for your ad and help.
      P

  • @Hellenistic109
    @Hellenistic109 Před 8 dny

    I like the way you have been articulating this Chilima Tragedy Issue...I'm a Zambian but I'm still Mourning with Malawians the Hero you lost and 8 others 😢😢.. Wish Malawians had a number of People like you who are fearless

  • @MussaJohn-gt8ep
    @MussaJohn-gt8ep Před 9 dny +4

    we here to support us. big up my brother

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 Před 3 dny

    Exactly brother mwadzi.wa munthu simasewela apenga misala onse a mcp

  • @SolomonShaibuh
    @SolomonShaibuh Před 8 dny

    Amp my vote

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d Před 9 dny +2

    Mumafotokoza zondisangalasa zonveka kwambiri

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb

    MCP and Chakwera time yawo yatha.

  • @ThokohKalonga
    @ThokohKalonga Před 9 dny +5

    Zosatheka kuvotera chakwera mm no🤔

  • @BishoppeterChanza
    @BishoppeterChanza Před dnem

    Yes zeni zen zimenezo

  • @chippyfelium5064
    @chippyfelium5064 Před 9 dny +2

    Big Up 🔥🔥

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q Před 9 dny +3

    Zophana zinari zakare pano nithawi yoti nizigwira chito tizipanga mabizinesi tizipeza ndarama.osati kuphana ayi chakwera ni sataniki

  • @CharlesGwape
    @CharlesGwape Před 8 dny +1

    Ndipo ife tinadziwa kale kuti dpp ndiyonyasa ndipo sizidzathekaso kutenga boma ili

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 Před 9 dny +5

    Who will arrest CHAKWERA poti he has killed chili and Ralph kasambala?

    • @Tenjklvtcy
      @Tenjklvtcy Před 9 dny +1

      Unamatu iwe😅😂

    • @Creslevison-vj2sl
      @Creslevison-vj2sl Před 8 dny +1

      Kulankhula kopanda umunthu ,am a chewa too koma akupanga zopusa ndipo sindingapange zopusa ngat akupanga chakwera nda nzakezi ai

    • @raytavares2256
      @raytavares2256 Před 8 dny

      ​@@Tenjklvtcy ndanama pati kuti mundiweluze bwino bwino kuti ndisadzalakwenso?

    • @Tenjklvtcy
      @Tenjklvtcy Před 8 dny

      @@raytavares2256 osamaperekera umboni wonama iweyo unamuona chakwera akupha anthuwo zoverazo

  • @hamissimdoka9665
    @hamissimdoka9665 Před 9 dny +7

    Zoona big mumakwana koma keep it up

    • @user-tk6qh9zs7h
      @user-tk6qh9zs7h Před 8 dny

      Zitsilu kuyamikirana pa Zopusa

    • @user-pn7cj9hb3t
      @user-pn7cj9hb3t Před 8 dny

      Iweyo khala ndi udolo wakowo ukuyankha comment ya chitsilu bwanji?

    • @user-tk6qh9zs7h
      @user-tk6qh9zs7h Před 8 dny

      @@user-pn7cj9hb3t kagwere uko Munthu okhulupilira zonama iwe

  • @eltonchimlambe2860
    @eltonchimlambe2860 Před 9 dny +3

    genius

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr

    Big up brada

  • @mosleykandiero3042
    @mosleykandiero3042 Před 8 dny

    Yes , read it as well he was a great diplomat he discovered about people,land and authority

  • @futurekanjanga1290
    @futurekanjanga1290 Před 8 dny

    Mumatipatsa hope.... God bless you

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 Před 8 dny

    Big up Bravo keep it up

  • @Laesanayatullahritchielumanzah

    The real citizen

  • @user-xj7xx2qo3g
    @user-xj7xx2qo3g Před 8 dny

    Keep it up tithane ndimakapa a mcp malawi poison party

  • @user-ex7jn2fh1g
    @user-ex7jn2fh1g Před 6 dny

    I support you bro

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 Před 9 dny +2

    And after stealing they make sure that all stolen money is in a format of assets or forgiven exactly the same way late Kamuzu did. Now Malawi I becoming a mafia Elchapo state if not Hushpu in Dubai.

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před 8 dny

    Yes that's true sadzapeza mtendere chifukwa mizimu ya anthu onse amene aphedwa pangoziyi idzakhala ikufuula mpaka kalekale

  • @VincentKamwendo-kh3hi
    @VincentKamwendo-kh3hi Před 9 dny +2

    Thats true bro

  • @user-bl5fd9ff8i
    @user-bl5fd9ff8i Před 8 dny

    Our own Snoop Dog ,I love your sense of humor

  • @user-yv3jp3it2t
    @user-yv3jp3it2t Před 9 dny +2

    Athu amene akuyikila chakwela kumbuyu ndi wa mcp and ndiwakuba as for me l can't support chakwela why u people u hate the Truth chakwela and his cabinet apha chilima that is truly evidence ok

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo8006 Před 9 dny +3

    Good work brother

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d Před 9 dny +3

    Brother ukunena zoona anthu ochitabwino sakonda ziko lawo ati mmene anadusa iwo enaso aduse momwemo zoti Mulungu waika pamenepo kuti ena apulumukilepo alibe nazo kungomulora satana akule mmiyoyo yao bsi zosaenda.

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Před 8 dny

    Never thought 💭 this he gonna win again never

  • @FELIXCHIWATU
    @FELIXCHIWATU Před 8 dny

    Imvaaa!!!!

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu Před 8 dny

    Good one

  • @danielsulani8689
    @danielsulani8689 Před 9 dny +1

    ❤❤❤

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v Před 9 dny +2

    Ndipo

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b Před 8 dny

    Bwana

  • @Malambia
    @Malambia Před 8 dny

    Fuso langa ndili nalo ndi Ili Black box inali kuti same day Malawi munalowa ndege almost 10 komano ndege ya Chilima yokhayo siinapezeke coz kanthu kaja kamaonetsa or isowe bwanji

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b Před 8 dny

    Anthh omwe tikuwafuna ndi awa osati Ben longwe kubakira chigawenga chakwera

  • @Jetada-ph9tq
    @Jetada-ph9tq Před 9 dny +2

    Mibado yawo yonse idzaona zowawa 😢 mcp chipani chotembeleredwa

  • @PatrickTembo-lm1ih
    @PatrickTembo-lm1ih Před 8 dny

    Biggy mmakwana malawi vutolidakalipo coz mmene mwanenela atsogoleri amafuna azioneka iwowokha osati ena komatso ambili Ali ndintima woti ndiziyitanidwa ndekha ma milionea

  • @KondwaniChikwawe
    @KondwaniChikwawe Před 8 dny

    Your crazy just leav it

  • @dondamissonchdziwe3958

    Anthu a menewa amwene aziyenda bwino, komanso ndimati ndi pemphe Asirikari aku Malawi asapitirize kumu yang'anira, Chifukwa Ku South Africa a dziwa Kuti ma Israel akumanga misasa Ku Malawi, Kuti achitire Chiwembu Dziko la south Africa,ndiye Africa yonse iku ya ng'ana kumeneko,Ndiye muone m'mene iyenso aphedwere Ndipo zakonzedwa kale.

  • @user-jm8kw9gw2d
    @user-jm8kw9gw2d Před 8 dny

    There will be pressure in MCP, azayamba kuyambana okhaokha ndi kuwululana, mwazi wa a chilima si mwazi wa nkuku, may God cause confusions in the camp of the enemies

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p Před 9 dny +16

    Never vote MCP 2025

    • @sheila5812
      @sheila5812 Před 9 dny

      Olo councilor or Mp ayi

    • @Tenjklvtcy
      @Tenjklvtcy Před 9 dny +5

      My vote my choice MCP woyeee🎉

    • @user-kc1ij6on5k
      @user-kc1ij6on5k Před 9 dny

      You don't know how to talk to people,

    • @JackMvura-ik2td
      @JackMvura-ik2td Před 9 dny

      Azipita kwao uyu kuzimbabwe nyani tilibe ntundu umeneu Kuno Omani mphonozo guys

    • @LaxAllison
      @LaxAllison Před 8 dny

      Ovotera chakwera ndiopusa opandanzerunso

  • @HussainSwaffie
    @HussainSwaffie Před 7 dny +1

    Dpp ikulowanso m'boma 2025❤❤

  • @SaulosMbuna
    @SaulosMbuna Před 9 dny +1

    Akafula akanatha kutipatsa governance yabwino. #monarchy

  • @kasupeowenpaul
    @kasupeowenpaul Před 9 dny +2

    Akamuna😂

  • @AnnieBanda-rb2dk
    @AnnieBanda-rb2dk Před 3 dny

    zoona achakwera amaona ngat awina osaziwa kut akuononga, osaziwa kut akuzionongera zinthu ekha apa ndipomwe azaziwe kut pokoza zina zinaso zimaonongeka, 2025 ndipomwe azaziwe kut khobwe sinyemba no vote awo magazi a chilima akumuyenda pa mphumi pake uyo

  • @user-vs5lk2hj3k
    @user-vs5lk2hj3k Před 8 dny

    The problem is omwe azavote next year alibe ma phone oti atha kumanvela kapena kuwelenga za pa social media

    • @Okalekale
      @Okalekale Před 8 dny

      Zoona,itakhala radio station,chifukwanso or atakhala nawo ma phone wo,ndi umphawi unabweretsedwa ndi democracy Wu ambiri sangaveko uphungu wina ndi winawu.Koma ine monga nzika yokonda dziko langa ndimadana ndi democracy kwambiri.Inatigawa ndipo ndikuooa kuti tikupitaku ndi nkhondo basi.Malawi itabwera pamodzi ndikukhala ndi chipani chimodzi momwe mudzakhale oyimila dera lililonse kuchoka ku Nsanje mpaka ku Chitipa ingatukuke.
      Zosintha-sintha zipanizi sizitithandiza,chifukwa ma plan azachuma sangakwanilitsidwe mu zaka four or five,never! chifukwa akaluza ndikulowapo ena,ena aja amabweranso ndi ma policy awo osiyana ndi amene anayambako aja,mwinanso nawo adzaluza kudzabwera ena ndi ma policy awoawonso ndiye kuti palibe kupita patsogolotu pamenepo,oluza ndi a Malawi amene amavotawo,dziko layima.Chitukuko sikumanga kokha,chitukuko cheni-cheni ndichoti moyo usakhale owawa,katundu asamadule,njala ithe koma ndi democracy sizotheka ayi.Bingu akanakhala anali ndi Moyo ndi amene anafunika kupitiliza chifukwa amene aja anali ndi masomphenya komanso okonda dziko lake,koma malamulo a democracy sakanamulora chifukwa democracy ndi,"awo adyako nafenso tikadyeko" rubbish yokha-yokha.

  • @HajjiPrinceHassan
    @HajjiPrinceHassan Před 8 dny

    Big up brother

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli Před 9 dny

    Mxiiii Lord have mercy

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 Před 9 dny +1

    It's a curse for selling fellow black people in South Africa and they do it today with Israel.

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g Před 7 dny

    Mcp is the party full of blood from the beginning

  • @hagayichiluwe
    @hagayichiluwe Před 8 dny

    Even mutachita sanje bwanji koma chakwela adzamwalila akudya money ,kukamwa kopotokako galu

  • @fannyzimba149
    @fannyzimba149 Před 9 dny +4

    😭😭😭😭😭

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh Před 9 dny +1

    Amalawi akuti ukuwawuza iwe kape osakawuza kazi wako zopusazo bwanji

  • @GeorgeAjida
    @GeorgeAjida Před 9 dny

    That's true brada

  • @user-vf9bs9vz2g
    @user-vf9bs9vz2g Před 8 dny

    Uzinamiza mbuli zinzako zomwezi if you have evidence come and provide it ndiwe kape kwambili ndi macadet anzako onse akupanga support

  • @user-ot6lt8iy8f
    @user-ot6lt8iy8f Před 8 dny

    🔥

  • @user-fy5lw8vk9k
    @user-fy5lw8vk9k Před 9 dny +4

    Thus pro found bro..keep up a good work

  • @SteveBanda-wf8uq
    @SteveBanda-wf8uq Před 9 dny +2

    Tiwakwapula akamapanga misokhano

  • @NedLouisNed
    @NedLouisNed Před 8 dny

    Walankhula ngamo bro zophana nzakale

  • @clojistix_g
    @clojistix_g Před 9 dny +1

    Guide book yawo ndi zitsamba mwa aSing'anga

  • @sylvesteralfred8355
    @sylvesteralfred8355 Před 9 dny +1

    Zoonadi man mumakwana ndipo mukulitsegula maso dziko komanso Malawi wa lero siwakale uja

  • @AmujeMwamad
    @AmujeMwamad Před 6 dny

    fotsek apa, kumene kuja pali kutukua ,bcz ose amene mmapanga ndale ndiovutika ngt ine.Mulibe zochita zina zotsatira zake mmaba ma tax athu.

  • @felixmagombo520
    @felixmagombo520 Před 9 dny

    Aga khan is a private hospital, owned by people with so much wealth. Talking of the mess we are in now, abambo ako a Peter Mutharika ndi inu nonse a DPP ndi omwe munasakaza chuma cha boma and left this country in serious debts. Palibeso wa MCP amene angayende mwa mantha, for what?

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp

    Hahahahaha sawina lazalas

  • @chiletsokazembe-ri4ic

    mmmm mukuona ngati dpp ikhoza kuwinaso? kkkk ngati kulioimira kumeneko kkkk

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne Před 8 dny

    Sitivota kwa munthu wàmagàzi

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f Před 8 dny

    Nchimo kuzunza😢

  • @chiletsokazembe-ri4ic

    Kkkk wasowa zofotokoza iwe wayamba kupenga kkk

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Před 9 dny +1

    Mbiri ya ndionyasa

  • @RicardoManuelEstivin
    @RicardoManuelEstivin Před 2 dny

    Zona chakwera Ndi nfiti, a Muluzi ankanena zoona

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v Před 8 dny

    Chakwera plan yomwe anayipanga kupha Chilima basi azichosera mavoti okha agalu amenewa

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj Před 8 dny

    Mbambande big ulemu wanu

  • @yamikanifischer
    @yamikanifischer Před 9 dny +1

    Which evidence you looking for

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba Před 9 dny +1

    Anthu amapenga misala ndi ma drug .kumayenda maliseche

  • @BisalomuMgwagwa
    @BisalomuMgwagwa Před 9 dny

    Simukunama boss

  • @natashaevans6953
    @natashaevans6953 Před 9 dny +1

    Mumativesa kukoma inuyo

  • @FauziaMwamadi
    @FauziaMwamadi Před 9 dny +1

    Chilungamo chikwabayatu a mcp

  • @user-nj4pn8gx7y
    @user-nj4pn8gx7y Před 9 dny

    ❤❤❤❤❤❤❤❤DPP

  • @tendaimakamabviko5916

    Musanamunamizile Chakwera ndipo Mulungu akukhululukileni mukunena zinthu zomwe mulibe nazo umboni .....nomwenu ndamene mwapha Chilima Kuti muononge mgwirizano wathu

  • @LaxAllison
    @LaxAllison Před 7 dny

    Wanzeru ndiwe ukukonda anthu okuphawe

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Před 8 dny

    Ifeyo kuno ku Ntcheu Central BAWI pankhumba tagwilizana zodzavotera APM 2025 ndipo MCP ndi Chipani chakumpha

  • @yohanezimba8329
    @yohanezimba8329 Před 9 dny

    Don't bother only God knows the truth

  • @user-dd1qq5xq1k
    @user-dd1qq5xq1k Před 8 dny

    MCP , never never again watikwana,

  • @VeronicaGrecian
    @VeronicaGrecian Před 9 dny

    Adani aku UK 😂😂

  • @user-mv1er5zr7e
    @user-mv1er5zr7e Před 8 dny

    Adzabera mavoti ndi zomwe akundalira

  • @LaxAllison
    @LaxAllison Před 7 dny

    Iwe ndi kape unakakhala uli ndi zochita sibwenzi ukumayankhula kunyela Kodi ukuyankhulila kuchiphisi kapena kuti ngati uli ndinzeru usandiyankhulenso

  • @FabianMhango-zk6nv
    @FabianMhango-zk6nv Před 8 dny

    MCP will never change 😢

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Před 9 dny

    Ndipo sindiziwa kt kapen azapanga bwaji? Koman ifa sithawik pano thawi yamuthera

  • @HENDRIXNKHOMA-pw2jq
    @HENDRIXNKHOMA-pw2jq Před 8 dny

    Zazi bwerani pa ground

  • @MatthewsNgulube-er3hz
    @MatthewsNgulube-er3hz Před 9 dny +1

    Muli nd I vuto