Eeeh uyu ogwila ntchito ndi ku Malawi First watumiza uthenga wake wa mphamvu, othokoza ndikudzudzula

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 9. 07. 2024

Komentáře • 40

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa Před 20 dny +4

    Zowona zowona zowona mawu oyanjanisa amenewo more fire 🔥🔥🔥🔥 🔥🔥🔥

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Před 20 dny +2

    Viva Malawi First 🇲🇼🔥 Big up Brother Salo nthawi zonse mumayima pa chilungamo

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Před 20 dny

    U have said it loud & clear Big up Brother men

  • @user-dy5bj9ck5e
    @user-dy5bj9ck5e Před 20 dny +1

    Well done Mr chidzukulu

  • @bernardnambwe7753
    @bernardnambwe7753 Před 20 dny +1

    more fire mumatha

  • @constancemkandawire7378

    United we stand divided we fall tufuna anthu ngati inu ku malawi indeed opposition party Itati imeme ma activists to join forces ku mademo aaaaaaa this ruling party can't stand the heat,enough is enough we are sick and tired of this government. VIva comrades viva

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 Před 20 dny +1

    Malawi first❤

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg Před 20 dny +1

    💥💥💥💥

  • @WilliamBanda-o5r
    @WilliamBanda-o5r Před 20 dny

    Mwanena chilungamo opposition kugona kwambiri yet akufuna kuzalamulira

  • @MustapherLino
    @MustapherLino Před 20 dny +2

    Chakwera ndi mbava

  • @user-vx5kv8dz3d
    @user-vx5kv8dz3d Před 20 dny +2

    Zoona zoona

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx Před 13 dny

    Ndipo ankaona azawo mene amamangira ma demo a chakwera ndi mtambo mpaka anawina

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v Před 20 dny +1

    💪💪

  • @user-mi3fw1zg8b
    @user-mi3fw1zg8b Před 20 dny +1

    Fire mabomba

  • @douglaskamanga7679
    @douglaskamanga7679 Před 19 dny

    A brother Salo, Kodi aliyense azi Nena za mtundu wake? Ndipamene timalakwitsila zinthu a Malawi. But Malawi first better not mutundu. Mukuona bwanji? Zapa mtundu ndekuti sizatonsetu

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Před 20 dny

    😂😂kung'aluratu 🔥 🔥 🔥.

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 Před 20 dny

    Mwang,alura bwana wachi yao

  • @Yussuf-b1p
    @Yussuf-b1p Před 20 dny

    Zoo Zoonad auzeni

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Před 20 dny

    Wasaalile kwereko wachiyao wangalusa😂😂

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Před 20 dny +1

    Zoona tinayika manyaka muboma

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 Před 20 dny

    Kkkkkkk amalawi akutizolesa manyi chakwela kkkkk zonvesati chotson

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 20 dny +2

    Wachiyao samapanga zatulo more 🔥 Mr kumeneko

  • @shepherdkingston
    @shepherdkingston Před 20 dny +1

    Umakwana

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 Před 20 dny

    Step down chakwela and anthu ako

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire Před 12 dny

    Kupha anthu kuba ndrama

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Před 20 dny

    Lets fight together 💪

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před 20 dny

    Zikomo malawi ukufuna anthu olimba mtima ngati inu MCP yatikwana zedi awa ndagalu kwabasi

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h Před 20 dny

    Koma nkaz naye wa chakwela ndimbuzi kwabasi sawiza mamuna wake kuti ayi musamuphe chilima

  • @GiftNasila
    @GiftNasila Před 20 dny +1

    ❤❤❤❤❤❤❤😅

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Před 20 dny

    Brother salo zoona ena amangotokota koma akuopanso

  • @OsmanPatrick
    @OsmanPatrick Před 20 dny +1

    Kkkkkk kmtu kulu unyoro baba

    • @CatherineMbela
      @CatherineMbela Před 20 dny

      Unyolo sichopyesela Koma ndi chiyambi cha Moyo wasopano osamangoopa amalawi zilizonse

  • @MerryWayson
    @MerryWayson Před 20 dny

    Kuswakuswa chilingamo palibe kumuvoteraso chakwera

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 Před 20 dny

    Chilungamo chokha choka

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Před 20 dny

    Chonde uyu ayenera kumangidwa ayi sikumenyera ufuru uku koma kutukwana munthu sichoncho nde ama khot aziti alibe umbon mene munthu akutukwana president wa ziko kut ndi wakupha nde muziti alibe umboni

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw Před 19 dny

      Mangochi bro imapampadsa makovi or apolice amasiwa kut Mangochi 🙌🙌🙌🙌

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Před 20 dny

    Ichi ndi chitsiru cheni cheni nde uganiza kut president wa ziko angalephere kumanga kanyumba r u serious koma ngat ndi jealous zikomo ,anthu inu akumwera muli ndi nkwiyo waukulu mene anzanu akuyendesera ziko ndipo ngat Pali anthu amene awononga zikoli ndi inuyo anthu akumwera ndi ma president anu ,kamuzu zikoli analisiya pa bwino koma ndi uchitsiru wanu ,munagulisa ma kampani onse a boma pano mukuvutika mwayamba kulila ndipo mulila zenizeni sitingakuvoteleni kut muzabwelelenso ayi takana

  • @isaacchiwaula731
    @isaacchiwaula731 Před 20 dny

    Zimenezi ndiye anthu nkumayamikira? Zili ndi phindu lanji? Awawa angayendetse dziko? Basi comment, kuma-commentar zopusa ngat izi? Shame on u. Nokha mukuyankhula kut mumayenda pansi mutavala silipansi while president-yo ali ndi ulemerero, ndie onunkha kukhwapa ndindani 😂😂😂😂😂😂 ndiwe munthu onvetsa chisoni aise

    • @ThomasPeter-zt2ju
      @ThomasPeter-zt2ju Před 12 dny

      U don't know what ur talking mutu wako mwazaza mamina okha oka