Yohane kuchokela Ku thyolo Maganizo anga ndi oti ziko la Malawi silizatheka chifukwa andalewa ukungopanga za mimba zawo osakhala kutumikila anthu plus dyela yawachulukila
Kunena zoona chakwera uyu sakufunikira, komaso ngati iyeyo ali ndi nzeru akanangosiya osaimaso watizuza mokwanira ife amalawi apite uko mwana wa satana mbusa waboza,ine Doreen kuchokera kuno ku South Africa krugersdrop
So sad that the student from university could not express herself in English. What example are we giving to those who aspire that one day they can go to the place of high education in Malawi.
Akulu inu ndinu oipa mtima msanje sipindula yeserani Zanu tikuoneni Malawi is open for everyone chakwera anayesa zake zidayenda kwatsala iwe wa msanje we Moyo kuwawa tisatero tichedwa adaaaa voterani adad musiyeni chakwera zake zinayera kale
Program iyi ilibwino kwambil 100%, pitilizan ndthu kutisangalasako🎉🎉
Ithink mutamupangaso include Mr bon kalindo ma program ngat awa zitha kukhala bwino
Asogoleri bakili kuba, peter kuba, joyce banda kuba and Chakwera kuba... Vuto ndi kuba basi
Mr Banda number one
Kuyakhula ❤❤kwabwino
Komanso maakitivisiti akutengapo mbali poononga dziko monga anthu awa ntambo Ben longwe munlo layitoni akumabwera ndi zina loti oyimira wanthu koma lero onse akubakira boma chifukwa chadyera maakitivisitinso nkhati awa akutengapo mbali poononga dziko .
Kuyankhula kwa bwino ❤
Ilibwino program Mr pitilidzani
Umoyo wamunthu simasewera zimafunika kulimbikira paiye yekha koma idzi zoti boma aziyenda ndi matisheti ndi kaufa nkamagawa ndizosathandizika chomwe chikufunika kusegula makhomo omwe asekeka andalama ziseguke mabizinesi awanthu aziyenda aliyense azitha kuzipangira paiye yekha
Yohane kuchokela Ku thyolo Maganizo anga ndi oti ziko la Malawi silizatheka chifukwa andalewa ukungopanga za mimba zawo osakhala kutumikila anthu plus dyela yawachulukila
Where was this
Kod ku Lilongwe tipanga liti program iyi ndi 100% ndithu
Brain your a great dada
University graduates you’re looking for other people to employ you instead of you to be the change that you need by creating those opportunities
Kom yah
Kom Mumbai's inayi kkkk ndaiposa kkkkkk kuchita represent kkkk
ing`ambeni bg
mzofunika mwayambazi zikanakhala bwino kupanga madela ambiri ndi mchimidzi
Programu ili shrp
Takuthokozani kuti mukufufuza maganizo awanthu mupitiĺize
Koma molaro omangopanga paliposewo ndie kusokonezako ngati program ili ya for good izi ofundika muziunikilepo
Shaya
Best TV
Kunena zoona chakwera uyu sakufunikira, komaso ngati iyeyo ali ndi nzeru akanangosiya osaimaso watizuza mokwanira ife amalawi apite uko mwana wa satana mbusa waboza,ine Doreen kuchokera kuno ku South Africa krugersdrop
Koma a brayn mwayamba ndale?
Ash
Ku poly chidzungu chikuwadzungulira eti eish
Not ku poly but some anali maperi amangonama kut ndi akupoly
Koma kulemba ntchito anthu opuma kale koma chakwela
So sad that the student from university could not express herself in English. What example are we giving to those who aspire that one day they can go to the place of high education in Malawi.
I observed that and I was just scared to mention it.
Hy
Gonjetsani adani athu, njala,nthenda, nsanje
Program ipitilire ilibho kwambili
Muuzene chakwela yo wamamina mmutuyo choopanda mzeru choongolamulidwa ndimwanawakwe
😂😂😂😂😂
Akulu inu ndinu oipa mtima msanje sipindula yeserani Zanu tikuoneni Malawi is open for everyone chakwera anayesa zake zidayenda kwatsala iwe wa msanje we Moyo kuwawa tisatero tichedwa adaaaa voterani adad musiyeni chakwera zake zinayera kale
Kuti uku
Ine yohane bobo kuchokela zinda uno wa Durban maganizo anga ndioti bwana brayan zinthu sizikuyenda pa Malawi vuto ndi usogoleli womwe tili nawo kmaso chondidabwisa kuti avomeleze kuti zinthu zawavuta ndipanene akufunaso kuti ayime dye zosatila zake mavuto azipitililabe