Boma Latha - Samuel Lwara
Vložit
- čas přidán 11. 07. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara asserts that due to UTM's withdrawal from the Tonse Alliance, Malawi theoretically lacks a government. The Alliance has been dissolved.
Ku Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wanenetsa kuti chifukwa UTM idatuluka mumgwirizano wa Tonse, dziko la Malawi lilibe boma. Alliance yathetsedwa.
#malawi
Boma palibe and we got no president now
Chakwela sakonda zikoli
Boma latha, MCP yikazawina ndiyekuti Abela zisankho
Awa a Lwara awa sazatha bwino. Ali ndi chimtima chovutika kwambiri. Kaya ndi kukhwima kaya ndi chani koma mathero awo ali pafupi.
Yagawana zida band 😂😂😂😂
Ma corner onse obela ma vote mcp mwatulukilidwa kale
Thako limozi 😅😅😅
😂😂😂😂
Chakwera achoke Ku state house
Kwambiri big azipita
🎉 judiciary it's your role now. Apa honestly boma lathapo
Law society of Malawi. UTM yachotsa vote yake, Kodi otsalawo mandate to govern Ali nayo?
Zoonadi Mr Lwara simukunama apa palibetso chanzeru MCP athako
Awabwezele a Dad aja basi...
Boma latha palibepo
Latha boma kumalawi kulibe boma 😂 achakwera agalu chimunduchopa ndamanyasi
Ndipo zakhalabwino kwambiiiiiri
Mphamvuyo ma MP 4 basi boma latha?
Latha boma limenelo ndipo mcp iri mmadzi ndipo achita manyazi
Apule atilankhule chifukwa sadalowe kunyumba ya chifumu ndi chipani,km akupezeka kumeneko chifukwa Cha tonse alliance.ndiye alliance ndiyomwe yatha.
Yaaah ndiokuti a Malawi tipange action kaah Kuti tipange referendum
Boma rathadi basi
Silingathe Ai chifukwa utm inali just a small part of mcp
You are a liar
Mcp yabisala pa chipande in 2025
Mcp yantha kungot yawina ndiye kut yabela palibe wina aliyese akuifuna ndipo or atabela sitizalola kutilamulila ngat akufuna kulamulila azikalamulila nyumba mwake amalawi sakumufuna or akakamile amalawi sakufuna enan or akupatsen kena kake koma nokha mukuziwa chilungamo mukuchiziwa kut palibe wina aliyese akuchifuna chipan cha mcp and achoka or atabela tizachotsa ndimakofi
Vinyo watcha tibalalike
Chakwera simbuli ngati iweyo samuel lwara.chakwela salankhula akalankhule chifukwa cha iweyo ndiwe ndati kapolo wadziko iwe kumangokhalira kuchikamwa.alliance siyinachite kutha koma utm yachita kutuluka yokha ndiye boma litha chifukwa chan? Dikila uwone ngati boma lithe.zifukwa zomwe ulinazo ndi mcp ndizaiwe wekha.mesa unkadya komweko ku state house? Siumatisokosela nthawi imene umadyayo bwanji? Panopa anakuthamangisa ndiye uzitipangila phokoso fotsek zako ndithu.
Hehehe muona kuti mutani Boma latha basi mixeeeeee
Uko ndiye timati kuzikwata ndi chala maloto a chumba.funso ndiloti kodi president ndani ku malawi? Ngati president alipo ndiye kuti boma lilipo.utm siingathese boma.ufune usafune chakwela ndi president wa boma kkkkkkk
Ndiwe wakuba ngati chakwera wakoyo mwantha muziwona
Ndinaba pa khomo pa pako ?? Iwe ndiwe galu eti ndiponso mbuli yamunthu anthunu mmadana ndi reality.akanakhala kuti dzulo muja watula pasi udindo ndi chakwela bwezi panopa kuli chipwilikiti.koma kutuluka kwa utm ndi kaliati sikungasinthe chilichose mufune musafune chakwela 2025 wooooooo ndiponso ndachepesa chakwela 2030 woooooo.msegula mumimba chaka chake ndichino.kulakalaka mutasamuka mmalawi muno.as long muli panthaka ya malawi president ndi chakwela.
@@BrightPhiri-bt6ev mbuli ndiwe because you don't know what you talking about
Problem is that you think you are very intelligent. NO. Latha bwanji? Tione ngati latha.