Boma Latha - Samuel Lwara

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 11. 07. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara asserts that due to UTM's withdrawal from the Tonse Alliance, Malawi theoretically lacks a government. The Alliance has been dissolved.
    Ku Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wanenetsa kuti chifukwa UTM idatuluka mumgwirizano wa Tonse, dziko la Malawi lilibe boma. Alliance yathetsedwa.
    #malawi

Komentáře • 37

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Před 24 dny +1

    Boma palibe and we got no president now

  • @alickkachepa3801
    @alickkachepa3801 Před 24 dny +1

    Chakwela sakonda zikoli

  • @BertharrySecurity
    @BertharrySecurity Před 24 dny +2

    Boma latha, MCP yikazawina ndiyekuti Abela zisankho

  • @tasmania527
    @tasmania527 Před 19 dny

    Awa a Lwara awa sazatha bwino. Ali ndi chimtima chovutika kwambiri. Kaya ndi kukhwima kaya ndi chani koma mathero awo ali pafupi.

  • @LoveHere-ki8ck
    @LoveHere-ki8ck Před 24 dny

    Yagawana zida band 😂😂😂😂

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Před 24 dny

    Ma corner onse obela ma vote mcp mwatulukilidwa kale

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Před 19 dny

    Thako limozi 😅😅😅

  • @thomasphiri7799
    @thomasphiri7799 Před 24 dny +1

    😂😂😂😂

  • @LucianoKapepuza-sy9wx
    @LucianoKapepuza-sy9wx Před 24 dny +1

    Chakwera achoke Ku state house

  • @maxwellchilima5440
    @maxwellchilima5440 Před 24 dny

    🎉 judiciary it's your role now. Apa honestly boma lathapo

    • @rexnyalugwe4910
      @rexnyalugwe4910 Před 24 dny

      Law society of Malawi. UTM yachotsa vote yake, Kodi otsalawo mandate to govern Ali nayo?

  • @OssmanAbubaker-t3n
    @OssmanAbubaker-t3n Před 24 dny

    Zoonadi Mr Lwara simukunama apa palibetso chanzeru MCP athako

  • @user-um6yo6nc3e
    @user-um6yo6nc3e Před 24 dny

    Awabwezele a Dad aja basi...

  • @OliverNkhoma
    @OliverNkhoma Před 24 dny

    Boma latha palibepo

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Před 24 dny

    Latha boma kumalawi kulibe boma 😂 achakwera agalu chimunduchopa ndamanyasi

  • @BertharrySecurity
    @BertharrySecurity Před 24 dny

    Ndipo zakhalabwino kwambiiiiiri

  • @grayakuzikemanda3114
    @grayakuzikemanda3114 Před 24 dny

    Mphamvuyo ma MP 4 basi boma latha?

  • @user-wb9ji3oe5o
    @user-wb9ji3oe5o Před 24 dny

    Latha boma limenelo ndipo mcp iri mmadzi ndipo achita manyazi

  • @brendachiwamira
    @brendachiwamira Před 24 dny

    Apule atilankhule chifukwa sadalowe kunyumba ya chifumu ndi chipani,km akupezeka kumeneko chifukwa Cha tonse alliance.ndiye alliance ndiyomwe yatha.

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x Před 24 dny

      Yaaah ndiokuti a Malawi tipange action kaah Kuti tipange referendum

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Před 24 dny

    Boma rathadi basi

  • @MikeChingala
    @MikeChingala Před 24 dny +2

    Silingathe Ai chifukwa utm inali just a small part of mcp

  • @user-jc5tf8jl1m
    @user-jc5tf8jl1m Před 24 dny

    Mcp yabisala pa chipande in 2025

  • @YaqoobStandwell
    @YaqoobStandwell Před 24 dny

    Mcp yantha kungot yawina ndiye kut yabela palibe wina aliyese akuifuna ndipo or atabela sitizalola kutilamulila ngat akufuna kulamulila azikalamulila nyumba mwake amalawi sakumufuna or akakamile amalawi sakufuna enan or akupatsen kena kake koma nokha mukuziwa chilungamo mukuchiziwa kut palibe wina aliyese akuchifuna chipan cha mcp and achoka or atabela tizachotsa ndimakofi

  • @joaquegerman2250
    @joaquegerman2250 Před 24 dny

    Vinyo watcha tibalalike

  • @BrightPhiri-bt6ev
    @BrightPhiri-bt6ev Před 24 dny

    Chakwera simbuli ngati iweyo samuel lwara.chakwela salankhula akalankhule chifukwa cha iweyo ndiwe ndati kapolo wadziko iwe kumangokhalira kuchikamwa.alliance siyinachite kutha koma utm yachita kutuluka yokha ndiye boma litha chifukwa chan? Dikila uwone ngati boma lithe.zifukwa zomwe ulinazo ndi mcp ndizaiwe wekha.mesa unkadya komweko ku state house? Siumatisokosela nthawi imene umadyayo bwanji? Panopa anakuthamangisa ndiye uzitipangila phokoso fotsek zako ndithu.

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Před 24 dny

      Hehehe muona kuti mutani Boma latha basi mixeeeeee

    • @BrightPhiri-bt6ev
      @BrightPhiri-bt6ev Před 24 dny

      Uko ndiye timati kuzikwata ndi chala maloto a chumba.funso ndiloti kodi president ndani ku malawi? Ngati president alipo ndiye kuti boma lilipo.utm siingathese boma.ufune usafune chakwela ndi president wa boma kkkkkkk

    • @Eric-gb9ms
      @Eric-gb9ms Před 24 dny

      Ndiwe wakuba ngati chakwera wakoyo mwantha muziwona

    • @BrightPhiri-bt6ev
      @BrightPhiri-bt6ev Před 24 dny

      Ndinaba pa khomo pa pako ?? Iwe ndiwe galu eti ndiponso mbuli yamunthu anthunu mmadana ndi reality.akanakhala kuti dzulo muja watula pasi udindo ndi chakwela bwezi panopa kuli chipwilikiti.koma kutuluka kwa utm ndi kaliati sikungasinthe chilichose mufune musafune chakwela 2025 wooooooo ndiponso ndachepesa chakwela 2030 woooooo.msegula mumimba chaka chake ndichino.kulakalaka mutasamuka mmalawi muno.as long muli panthaka ya malawi president ndi chakwela.

    • @Eric-gb9ms
      @Eric-gb9ms Před 24 dny

      @@BrightPhiri-bt6ev mbuli ndiwe because you don't know what you talking about

  • @mzondinkosi1151
    @mzondinkosi1151 Před 21 dnem

    Problem is that you think you are very intelligent. NO. Latha bwanji? Tione ngati latha.