Zomwe wayankhula Waxy Kay pa Maliro a Bambo ake a Bishop Kapenga ku Robins Park in Blantyre

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 1. 07. 2024

Komentáře • 83

  • @JOHNOlesmasCosmas
    @JOHNOlesmasCosmas Před 5 dny +21

    imfa ya munthu olungama pamaso pa Yehova pamakhara chimwemwe zilibwino indeed
    waxy mzimu wa Yehova ukuyankhura iye wangokhara chotengera chake
    may His soul rest in internal peace 😭😭😭

  • @ListerMunthali
    @ListerMunthali Před 5 dny +10

    Ndikukumbuka mu ulaliki wina wake bishop kapenga ananena kuti ngati situation ndiyoti sungayisithe no matter what, osalira just say zikomo ambuye.
    Pachifukwa ichi nane ndikuti zili bwino ndi mzimu wawo for God has relieved him from all his pains🙏

  • @WellosMphonde-wd2cx
    @WellosMphonde-wd2cx Před 5 dny +5

    Munthu akamwalira kulira kumatanthauza kusowa chiyembekezo pamene mau ake a Mulengi amati tisalire pakuti mu zonse tidziti zilibwino nde mukati speech yolakwika nde kuti chani. Lolani akulimbika mtima akhale akulimbika mtima pakuti ndi mawu ndipo mwa mawu tidzachuta mwa mawu. Say Amen/Ameen

  • @ALINAFEMKOMERA-cm1md
    @ALINAFEMKOMERA-cm1md Před 5 dny +4

    He got broken... He wrote a status he was comforted that he should be strong since the father is in a better place
    Now he is strong anthu muyakhulisaso
    Mumtima akuliratu munthuyu

  • @user-pn7cj9hb3t
    @user-pn7cj9hb3t Před 5 dny +9

    Chomwe walakwitsa Waxy Kay ndi chani anthu inu? Kapena simudziwa mau simudawelenge?

  • @user-uo3lm5wl5j
    @user-uo3lm5wl5j Před 5 dny +6

    Ifa ya wamuthu olungama kumwamba kuli chimwemwe mwAna wazelu kwabassi ndiwochepa agazindikile mawu wayakhula mwanayu Kwa amene amakhululupila mulungu wava tathsuzo lake amen

    • @MaeCuinhane-gq7ub
      @MaeCuinhane-gq7ub Před 5 dny

      Ndipo imfa ya munthu oyera mtima imakhala yokoma chifukwa amakhala akudziwa za komwe akupita

  • @user-pq7hj9jl6i
    @user-pq7hj9jl6i Před dnem

    I personally support waxy. All is well indeed. It reminded me of my late mum. She said all is well and the future is so bright. Kwa okhulupirirafe zilibwino ndithu. Chauta salakwitsa. The lapture is here and Go's is taking his righteous ones. Go well bishop .

  • @AnthonyChibwe-bf4de
    @AnthonyChibwe-bf4de Před 5 dny +5

    He has to say so,, there is no way kut azikhala akudandaula yet zinthunzo zachitika kale komaso sangathe kuzibweza pat. Mmalo moti azingodandaula wasankha kusangalala that's a good choice or adakayankhula zodandaula zidakasintha chan? Umenewo nde umunawo mesa,

  • @snowkybeats
    @snowkybeats Před dnem

    Beautiful speech for a believer. Celebrating a life well lived.

  • @MDAmir-ku4lf
    @MDAmir-ku4lf Před 4 dny +1

    Waxy akunena zoona, mau a munthu okhulupilira ndi oti zilibwino. Abale amzanga munthu akamwalira sinthawi yoti ife tizilira ndi nthawi yosangalala chifukwa chani ndikuyankhula choncho, chisanzo munthu akamagwira ntchito kaya ndi pa company kaya m'boma amayembekezera kuti mwezi ukatha akuyenera kukalandira salary, ndiye funso nali, ndindani amene amapita kokalandira salary akulira tipeza kuti palibe wina aliyense amakhala osangalara kuti lero tikadyera nyama, ndi chimozimozi inu ndi ine mulungu anatisankha ndikutisiya pano pa dziko lampasi cholinga chimene anatisiila pa dziko la pansi ndi chani tizimugwadira nthawi ndi nthawi, ndiye tamugwadira mulungu, mwini wake emweyo yemwe timamutumikira uja watiitana tamwalira ndicholinga choti akatipase malipiro pa ntchito yomwe iye anatipasa takhala tikumugwilira tidakali ndi moyo abale amzanga sinthawi yomalira imene ija ayi ndinthawi yotchulusa kupempha kwa mulungu kumupemphelera m'bale wathu kuti ngati anali ochita ntchito zabwino mulungu amuonjezere zabwino zochuluka pa ntchito yomwe iye anali kugwira adakali ndi moyo komanso ngati anali ochita ntchito pena zoipa mulungu asachulukise kuyang'ana zoipa zake Ameen

  • @LeahNundwe-wh6vz
    @LeahNundwe-wh6vz Před 3 dny +1

    Today's children at their parents funeral leaves alot of questions really

  • @thokozanisukah6448
    @thokozanisukah6448 Před 5 dny +1

    Indeed zili bwino aliyese azafa komano kuluza munthu sichithu chophweka nde kumankhala makolo ako

  • @FlorahBanda-fl4vf
    @FlorahBanda-fl4vf Před 5 dny +7

    Speech iyi ndiyofunika azungu koma ife tiziti mwatilawula😢

  • @RedKoffii-gl2vx
    @RedKoffii-gl2vx Před 5 dny +6

    Mwana ulimba mtima

  • @ZaffboyYellows
    @ZaffboyYellows Před 5 dny

    I'm very sorry 😢Your highness young king. If you want to talk ' I'm here at any time

  • @WakisaPhiri-e1e
    @WakisaPhiri-e1e Před 5 dny

    RIP Pastor 😭 Anthu awa amkavana

  • @mikheykaunda3540
    @mikheykaunda3540 Před 3 dny

    RIP Munthu wakulu Kapenga we shall miss u

  • @samuelkapasula-mn6es
    @samuelkapasula-mn6es Před 4 dny

    Zoonadi.....Zili bwino mwa Yesu khristu.....

  • @user-ly4ug6wm9k
    @user-ly4ug6wm9k Před 3 dny

    My grandma said when someone passed away within two days ,,,,,,, umawona ngat zocheza koma dikila pathe masiku nde akut zilibwino ??? Pamenepa😢

  • @nkosikhonasiphiwemdlalose227

    Some of the tribes in Zim they celebrate when they lose someone zili bwino akapumule ali ndi Yesu wao

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Před 5 dny

    Owooo chabwino

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu Před 5 dny +1

    Osamamuchemerera mfanayu ndikape chisiru paumunthu speech umatulusa malingana ndimaro ache awa anali bambo ake osati ngt kanali kushow koziwonesera kt kaya akazi akafire zachamba

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano Před 4 dny

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤
    0:11

  • @unarinematshomo2841
    @unarinematshomo2841 Před 4 dny

    Muthu akamwarila, timarila pa nthawi imeneyoyo, ndee waxy kay sanalakwitse moti speech yake ili bho ndithu.

  • @jamesbowman-cw8ts
    @jamesbowman-cw8ts Před 4 dny

    Koma ndiye Kuli mixed bag of comments,... Waxy this Waxy that,... aMalawi musiyeni mwana, walimba mtima ndi chiyembekezo kuti bambo ake ali malo abwino opumula ndi Yesu wawo ndipo palibe chodandaula,... Ndiye mukuti chani anthu "abwino" komanso osunga "chikhalidwe" chachiMalawi inu??
    Pena ngati ndinene kuti dikirani abambo anu akazamwalira muzayankhule speech yanu yabwinoyo,....koma poti imfa si yabwinonso. So whatever,
    Rest well Bishop Kapenga. We knew as man of God and we're sure to God your soul has returned. Rest Bishop rest🕊️🕊️

  • @OwenTembo-xq6ug
    @OwenTembo-xq6ug Před 5 dny

    Sizilibwino ndizolilitsa kwambili 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @GetrudeGama-gu5rb
    @GetrudeGama-gu5rb Před 5 dny +1

    Zowonadi ziribwino kwaiwo kwantha kwatsara kwaife

  • @chemapa
    @chemapa Před 4 dny

    zabodzazo zosamvekazo Mulunguyo anamuuzira kuti? pamaliro sitchukira. tisamaseweretse dzina la Mulungu. kulowetsa chibwana pamaliro a mtumiki wamulungu.

  • @POker_On1.
    @POker_On1. Před 4 dny +1

    Zibwíno 🙏🏾

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano Před 4 dny

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano Před 4 dny

    Mau abwino kwa munthu olungam

  • @SinyoroMoyo
    @SinyoroMoyo Před 4 dny

    Chitsiru chamwana ,nde chojowera-jowera ndichani .ngati zili bwino osangoyankhula bwino bwino kupereka ulemu kwa anthu ena bwanji.kufuna kutchuka ndi uchitsiru udzazindikira bwino patsogolo

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 Před 5 dny

    Wavala mzimuwamji mwanau

  • @kondwanibuleya-br9gr
    @kondwanibuleya-br9gr Před 5 dny

    😢 what a man up

  • @Choicemlw
    @Choicemlw Před 4 dny

    Yesu analira pa maliro a Lazaro

  • @maxyfreeman9691
    @maxyfreeman9691 Před 3 dny

    Kaya mwanayu sanasute koma

  • @jelblinds2017
    @jelblinds2017 Před 4 dny

    There is nothing wrong jst that we as malawians have poor and shallow minds

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm

    Mwana wamuna azikhara olimba mtima choncho waxy mbiri yako yabwno umakhara bwno ndi bambo ako ambuye akuze malire amoyo wako ndi abale ako😢

  • @Mphatsolikotima
    @Mphatsolikotima Před 5 dny

    Rip bishop kapenga 😢

  • @CatherineKumwendaCatherine

    Kwa munthu oti amaziwa za kumwamba mwana wayakhura zomwe Mulungu amatilimbikisa pamavuto or pa Mtender tiziti zili bwno

  • @JosephJosab
    @JosephJosab Před 5 dny

    Ku show kapena maliro

  • @Mazexifeyoh
    @Mazexifeyoh Před dnem

    Powerful

  • @billykamwendo6517
    @billykamwendo6517 Před 5 dny +1

    Ife ndi a Malawi, izi nzachizungu ndipo naaa ine sindingayankhule chonchi ali oti ndi bambo anga.

    • @TadalaChithope-yg9fo
      @TadalaChithope-yg9fo Před 5 dny

      Azibambo nthawi zambili amakhala olimba mtim and uyuso panja mean oyamba ayenela kukhala strong komas tiyamike kut bambo ake amwalila waxy atatembenuka mtima komas kwaimayife zovuta kom kwa mamun ngt uyu akudziwa chomwe akuchita komas mwa okhulipilila izi zosavuta ngt munawon live yadzulo mayi ake okhala akaz awo anayimba nyimbo xa phamvuso coz ndi anthu okhulupilila and akudziwa kut akuyakhula mulungu wawo

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa Před 5 dny

    Sitinazolowele spech ngati izi kuno kwathu

  • @Queen-m6f
    @Queen-m6f Před 3 dny

    May His Soul Rest in Peace 😢

  • @user-wz1jy3uj8p
    @user-wz1jy3uj8p Před 5 dny

    ❤❤❤❤❤❤

  • @user-jn2oc3cn3q
    @user-jn2oc3cn3q Před 4 dny

    Km ine kaya ndi chimodzichi km speech yi sinandivekere mwaumunthu

  • @BestMtawali
    @BestMtawali Před 5 dny

    Ndalama unadya zacosoma zja nyimbo zake ndizit unaimba?????😩😩😩😩

  • @marryrobert7092
    @marryrobert7092 Před 5 dny

    A malawi uziwa kurangiza mwana warakwa chani kod simuziwa kuti muthu akafa sibwino kurira mokweza ndemumatu iyi azirira

  • @eltonnankhwere3284
    @eltonnankhwere3284 Před 5 dny

    Of course am satisfied with the speech it seems unakonzeka ngati ukupita
    ku show.i remember you wrote kuti tiyeni mawa tikakumane pa Robins Park ndikaimba nyimbo in other way its not fitting

  • @Tryness-wb6dj
    @Tryness-wb6dj Před 5 dny

    Rest well Bishop Kapenga

  • @ShyreenKwisongole
    @ShyreenKwisongole Před 3 dny

    Emen

  • @mikemakamo7360
    @mikemakamo7360 Před 5 dny

    Koma mwana wakondwelatu 😂😂😂
    Zotindipamalilo wayiwala yoh mphamvu ziko likulowa bola

  • @AneesaMoosa-nv6bq
    @AneesaMoosa-nv6bq Před 5 dny

    Rest in peace bishop kapenga

  • @HussainGaffarOlaiza-hy9sg

    💔🕊

  • @DJcliffBandakhudzanga

    Waxy ndi nfana olimba mwana wamamuna adzitelo

  • @rabeccadytone8772
    @rabeccadytone8772 Před 4 dny

    Wakhutu la uximu wanva

  • @daziana2023
    @daziana2023 Před 5 dny

    Zilibwino

  • @FranckieDambah
    @FranckieDambah Před 5 dny

    Eeeeee waxy umatha kuyankhura

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu Před 5 dny +1

    Iyi ndi lmfa osapanga zibwana kawonesa picture yanji kwa azukulu amipingo pamwambo wamaliro kakuti sharp wachani zachamba

  • @TadalaChithope-yg9fo
    @TadalaChithope-yg9fo Před 5 dny

    😭

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo8006 Před 5 dny +1

    Guys mwanai watani kodi
    Paribe muthu amasangalala pa ifa ai .
    Uyu wandikaikisa chabwino R.I.P pastor kapenga

    • @HannahChingwalu
      @HannahChingwalu Před 5 dny +1

      Chakaikitsa pamenepo ndichani?? Akuyenera kutero kumene chifukwaso zili mmalemba Mulungu ananena kuti kwaikika kwamunthu kufa,,chamoyo chilichonse chikuyembekeza imfa Ambuye alemekezeke chifukwa wakwanilitsa mau ake,,osati zanuzo apa

  • @MarthaMfulusa-vj3xe
    @MarthaMfulusa-vj3xe Před 3 dny

    Strange

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 Před 5 dny

    Muzidyatu bwino ganjayo

  • @BudaEarth
    @BudaEarth Před dnem

    Dadas

  • @EmmanuelNgamuti
    @EmmanuelNgamuti Před 5 dny

    Young man where hv u taken the energy to make this non African speech on a day like this?

  • @DavieChangoima
    @DavieChangoima Před 5 dny

    Sorry rnp

  • @YellowmanExen-nw1hy
    @YellowmanExen-nw1hy Před 2 dny

    I think this man waxy mutu wako sumakoka,ngati chili chamba mmmm.are sure bambo ako apita you can say this nonsense sure?

  • @Ampambachulu
    @Ampambachulu Před 5 dny

    Bro thought he killed

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 Před 5 dny

    Waxy akanakhala ngati chija chinthubidwa cha chilima chija akanag'alura

  • @SamsonChiwera
    @SamsonChiwera Před 5 dny

    Mmmm waxy Kay Kuno ndi kumalawi ndye yaaa kumbali Ina it's ok kuti zilibwino koma another side this speech is useless to me when you grow up that's when you will realize that l made silly speech RIP Mr kapenga

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Před 5 dny

    Kuyankhula kotani uku, mwana wachibwana

  • @BlessingsMangwaya-mk4fi
    @BlessingsMangwaya-mk4fi Před 5 dny +9

    This is not a fitting speech for the day your father passed away 😪😪

    • @lindamyaba
      @lindamyaba Před 4 dny

      Be serious man, waxy mwaonetsa maturity, zili bwino

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 Před 4 dny

      Sonotu anthu odziwa mawu zimaaiyana ndi osadziwa mau zili bwino basi ambuye walora

  • @Melinavituhs-tc8ys
    @Melinavituhs-tc8ys Před 5 dny

    Komatu for sure now irealize rhst crying during someone's daeth is for us poor imagine what is this speech 😭😭😭😭😭💔💔end with sure
    Anyway rest well pastor kapenga