phuzitsi wina wa school yosula aphuzitsi wapeza nkazi emwenso ndi phuzitsi akupanga zadama.

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 11. 08. 2022

Komentáře • 65

  • @zainabchikakuda8764
    @zainabchikakuda8764 Před rokem +2

    Komatu. Kulakwa chommenyera mwamuna wako nchiyani nzimayi oipa ukupha mwana waeni 😭😭😭

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri Před měsícem

    Akacheza amamwa eti kkkkk

  • @fineenemy2045
    @fineenemy2045 Před rokem +3

    Language is clear komano zudabwisa mainawo koma mwat ndiku malawi uku?

  • @kelvinskada5619
    @kelvinskada5619 Před 5 měsíci +1

    Two bad, watching from malawi

  • @AndrewPilliotmw
    @AndrewPilliotmw Před 2 lety +3

    Vuto ndi mamunayo........ Anyway watching from Maputo (koma ndine mmalawi ndithu)

  • @PaulokossimasiPaulo
    @PaulokossimasiPaulo Před měsícem

    😂 hulem nkayo

  • @Envanceabwinobamusieli-sf9tt

    Koma atolakhan ku Mozambique mukugwira ntchito yotamandika mpaka kutiwonesa stadium 😂😂😂😂

  • @user-ez7th2rv7g
    @user-ez7th2rv7g Před 7 měsíci +1

    Thanks for the update

  • @confidencebanda109
    @confidencebanda109 Před 2 lety +1

    Mayi uyo ndiwolakwa bola akanathesa banja za uhule wake akanapangila pa nkhomo pa makolo ake fro malawi

  • @LimitedMolotali
    @LimitedMolotali Před 3 měsíci

    Nkaziyo ndihule aphesa amuna

  • @Xtar_deadlol1
    @Xtar_deadlol1 Před 2 měsíci

    Za ziii kusowa zotola nkhani Chan

  • @chippiephiri4505
    @chippiephiri4505 Před 2 lety +3

    Mamunayi ndiwopoyila

  • @westonnsulupi4056
    @westonnsulupi4056 Před 2 lety +2

    From Malawi

  • @ernestbwanalisauteni3483

    Kkkkkkkkkk zosokonezeka kkkk

  • @mayeserokaponya5196
    @mayeserokaponya5196 Před rokem +1

    Man banja losagwirizira ili nawenso ndiwachibwezi basi zatherana Malo ndi awana

  • @chicco2294
    @chicco2294 Před rokem +1

    Mainawa akuti bwanji?? I didnt know ku mosco mumalankhula Chichewa choncho

  • @lamackbanda6869
    @lamackbanda6869 Před 2 lety +1

    Olakwitsa ndi mamunayi zinthu zonsezo zimachitikazo opanda action kuonesa. Nkhani yamalilo inaliso yayikulu olo sanayithambasule. Komaso zimayiyu sanatenge ndalama ku bank koma zimuna akewo ndi amene amamanga nyumbayo. Naye mamunayo ofafusa kuti ndalama akuzithenga kuti zomangila nyumba kumangoyang'ana zimamutsangalasa

  • @grantmachira9668
    @grantmachira9668 Před 2 lety +1

    Mayiyo ndiwosalakwa amadzilimbikira ekha abambowa angothetsa banja basi but it seems mkaziyo ndi bread winner mkazi malo anagula yekha

  • @victorsmbewe4816
    @victorsmbewe4816 Před 2 lety +4

    Emotional damage 🤕🥴😜

  • @ndazionaanastasiaannaphiri4843

    Palibe chabwino zonse zolakwika mkazi yo nde worsen

  • @josuahkachali1489
    @josuahkachali1489 Před 2 lety +1

    From Malawi but am stay in Kuwait

  • @lamackbanda6869
    @lamackbanda6869 Před 2 lety

    Ntchito yapamwamba guys mumayitha♨♨♨♨

  • @zakeyophiri4308
    @zakeyophiri4308 Před rokem +1

    Pls inuyo nkhani zina muziysa Kubisa nkhope kapena azalankhula atayang.ana kumbali chitsazo nkhani ya mnyamata akuti anapeleka mimba kwa mtsikana kapena mtsikana uja amene chifukwa media imapita patali tidzalephela kumufusila kapena kukwatiwa adzati ena anampatsa kale mimba

  • @peterbanda7003
    @peterbanda7003 Před 2 lety +2

    Osamusiya bwanji

  • @chembachilemba7623
    @chembachilemba7623 Před 2 lety +1

    Tsono wamenyedwanso mkazi ali wake kumenyedwa ndi mkazi aaaah this is not true guys😂😂😂😂nde mkazi amamangitsa nyumba inu osapezekako olo amfumu sakukudziwani zovutatu izi

  • @ngendahayososthene1398
    @ngendahayososthene1398 Před rokem +1

    bambo inu ndi inu opoyira zedi.

  • @floramtiwa211
    @floramtiwa211 Před 2 lety +1

    Koma ma statement akusiyana mwamunayu akuyankhula mosiyana ndiazimayi aja

  • @chancyutekakayala2445
    @chancyutekakayala2445 Před rokem +1

    May someone assist me Kodi zikuchitika ku dziko lanji izii komanso nchiyankhulo chanji

  • @joebrown1158
    @joebrown1158 Před 2 lety +2

    In a true sense the man is wrong, because he was never be involved with the woman if it is true where was the men the time when the woman started to build the house?

  • @zaithwachiwaya8885
    @zaithwachiwaya8885 Před 2 lety +1

    Kom nkhaniyo mamunai zikuoneka kut malo sanagule nao.Komaso zimaiyo ndi uhule lothelatu zochitisa manyanzi zed

  • @promise3693
    @promise3693 Před 2 lety +2

    Kulakwa🤔

  • @smithelectro-plumb2994
    @smithelectro-plumb2994 Před 2 lety +1

    Kodi akulankhula chilankhulo chanji guys

  • @luciajames604
    @luciajames604 Před rokem +1

    It's Mozambique

  • @DelcidioDiogoPedro-ir9ni

    Nkazio ntanbuali

  • @paulmgombebanda-mr19sate

    Zovuta izi

  • @osamabinraden9391
    @osamabinraden9391 Před 2 lety

    Mabanja akenso ndendi achi'chainatu

    • @eliasfaunteni6849
      @eliasfaunteni6849 Před 2 lety

      Mchifukwa chake timanena kuti akaziwa tikawamphunzitsa amachuluca mzelu zovetsa chisoni kwambiri

  • @lucysimbani3971
    @lucysimbani3971 Před 2 lety +1

    Zosankhala bwino ayi

    • @nemamoleni3041
      @nemamoleni3041 Před rokem

      Ati agulitse malo ndalama agawane?? Zosakhala bho

  • @memorymalikita3628
    @memorymalikita3628 Před 2 lety +1

    Where exactly is this sad news happened

  • @tadalaimwa394
    @tadalaimwa394 Před rokem +1

    Ndemwati ndinu amalawi? I really wish to visit and learn more about this place

  • @jessienkhoma2492
    @jessienkhoma2492 Před rokem

    Koma ndi ku Malawi kapena Mozambique?

  • @joebrown1158
    @joebrown1158 Před 2 lety +1

    So you people the way you speak the language don't you like each other like Malawian people? Aren't you the same people, tell me what is the different there between you and Malawian?

    • @joegibsonzulu2599
      @joegibsonzulu2599 Před rokem

      It's true that the language that is being spoken in this video is exactly the same that is spoken in Malawi.We are one people, with one language, one culture , same values and similar traditions.We were only divided by colonial boundaries.Its a great pity that sometimes we seem to perpetuate these colonial divisions.

  • @shariffalick796
    @shariffalick796 Před 2 lety +1

    Kodi mayina akuchulidawa ndi ku malawi ?

  • @user-gu4kk2bt4h
    @user-gu4kk2bt4h Před 10 měsíci +1

    Penço nr d BS de Whatsapp