Tsono wamenyedwanso mkazi ali wake kumenyedwa ndi mkazi aaaah this is not true guys😂😂😂😂nde mkazi amamangitsa nyumba inu osapezekako olo amfumu sakukudziwani zovutatu izi
In a true sense the man is wrong, because he was never be involved with the woman if it is true where was the men the time when the woman started to build the house?
So you people the way you speak the language don't you like each other like Malawian people? Aren't you the same people, tell me what is the different there between you and Malawian?
It's true that the language that is being spoken in this video is exactly the same that is spoken in Malawi.We are one people, with one language, one culture , same values and similar traditions.We were only divided by colonial boundaries.Its a great pity that sometimes we seem to perpetuate these colonial divisions.
Komatu. Kulakwa chommenyera mwamuna wako nchiyani nzimayi oipa ukupha mwana waeni 😭😭😭
Akacheza amamwa eti kkkkk
Language is clear komano zudabwisa mainawo koma mwat ndiku malawi uku?
Akuti Mozambique osati malawiyi
Two bad, watching from malawi
Vuto ndi mamunayo........ Anyway watching from Maputo (koma ndine mmalawi ndithu)
Me too
😂 hulem nkayo
Koma atolakhan ku Mozambique mukugwira ntchito yotamandika mpaka kutiwonesa stadium 😂😂😂😂
Thanks for the update
Mayi uyo ndiwolakwa bola akanathesa banja za uhule wake akanapangila pa nkhomo pa makolo ake fro malawi
Nkaziyo ndihule aphesa amuna
Za ziii kusowa zotola nkhani Chan
Mamunayi ndiwopoyila
From Malawi
Kkkkkkkkkk zosokonezeka kkkk
Man banja losagwirizira ili nawenso ndiwachibwezi basi zatherana Malo ndi awana
Mainawa akuti bwanji?? I didnt know ku mosco mumalankhula Chichewa choncho
Olakwitsa ndi mamunayi zinthu zonsezo zimachitikazo opanda action kuonesa. Nkhani yamalilo inaliso yayikulu olo sanayithambasule. Komaso zimayiyu sanatenge ndalama ku bank koma zimuna akewo ndi amene amamanga nyumbayo. Naye mamunayo ofafusa kuti ndalama akuzithenga kuti zomangila nyumba kumangoyang'ana zimamutsangalasa
Mayiyo ndiwosalakwa amadzilimbikira ekha abambowa angothetsa banja basi but it seems mkaziyo ndi bread winner mkazi malo anagula yekha
Emotional damage 🤕🥴😜
Palibe chabwino zonse zolakwika mkazi yo nde worsen
From Malawi but am stay in Kuwait
Oky
Ntchito yapamwamba guys mumayitha♨♨♨♨
Pls inuyo nkhani zina muziysa Kubisa nkhope kapena azalankhula atayang.ana kumbali chitsazo nkhani ya mnyamata akuti anapeleka mimba kwa mtsikana kapena mtsikana uja amene chifukwa media imapita patali tidzalephela kumufusila kapena kukwatiwa adzati ena anampatsa kale mimba
Osamusiya bwanji
Tsono wamenyedwanso mkazi ali wake kumenyedwa ndi mkazi aaaah this is not true guys😂😂😂😂nde mkazi amamangitsa nyumba inu osapezekako olo amfumu sakukudziwani zovutatu izi
bambo inu ndi inu opoyira zedi.
Koma ma statement akusiyana mwamunayu akuyankhula mosiyana ndiazimayi aja
May someone assist me Kodi zikuchitika ku dziko lanji izii komanso nchiyankhulo chanji
It's chichewa in Mozambique 🙄
In a true sense the man is wrong, because he was never be involved with the woman if it is true where was the men the time when the woman started to build the house?
of cause
Mozambique
Kom nkhaniyo mamunai zikuoneka kut malo sanagule nao.Komaso zimaiyo ndi uhule lothelatu zochitisa manyanzi zed
Kom saname nkhaniyi kadakonda mukanamuonesa mzimai wa chigololo yo timuone kkkkkkk
Mahule ,
Mabanja oyambila mvitsamba
Kulakwa🤔
👀 from malawi
Malowo ngakhale atakhala kuti nyumbayo anagula ndi iwowo komabe ali pa banja nyumbayo ndiyawose basi
Kodi akulankhula chilankhulo chanji guys
It's Mozambique
Yes
Nkazio ntanbuali
Zovuta izi
Mabanja akenso ndendi achi'chainatu
Mchifukwa chake timanena kuti akaziwa tikawamphunzitsa amachuluca mzelu zovetsa chisoni kwambiri
Zosankhala bwino ayi
Ati agulitse malo ndalama agawane?? Zosakhala bho
Where exactly is this sad news happened
Mozambique iyi
Ndemwati ndinu amalawi? I really wish to visit and learn more about this place
Samalawi this is angonia
Koma ndi ku Malawi kapena Mozambique?
Mozambique
So you people the way you speak the language don't you like each other like Malawian people? Aren't you the same people, tell me what is the different there between you and Malawian?
It's true that the language that is being spoken in this video is exactly the same that is spoken in Malawi.We are one people, with one language, one culture , same values and similar traditions.We were only divided by colonial boundaries.Its a great pity that sometimes we seem to perpetuate these colonial divisions.
Kodi mayina akuchulidawa ndi ku malawi ?
ayi, koma kalipentalayo
Mozambique
Mozambique
Penço nr d BS de Whatsapp
865112269