DR KABAMBE ATULUKA DPP | NKHANI MADZULO |

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 25. 08. 2024

Komentáře • 45

  • @chisomokawotcha1766
    @chisomokawotcha1766 Před měsícem +6

    Ayi ndi pamene mudzadziwe kuti ndale ndi zovuta kuti amusankhe kabambe running mate ku dpp bdi zovuta cause kueme kuja kuli mikhala kale nde apite ku utm cholinga akazapanga alliance kabambe azamutwnga ngati running mate wake fro m utm nde ndale zimenezo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před měsícem +5

    Akabambe olo atachoka dpp iwinabe

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d Před měsícem

      Kabambe alibe chikoka alingati Mangacha sete zawo onse

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Před měsícem +2

    Chipani cha dpp chilibe vuto.zipani zambiri zilibe vuto koma vuto ndi anthu wofuna mawudindo sakufuna kulolelana kuti wina alamulire ndiye anthu wotuluka zipani musawalole azipani zina kulowa muzipani zanu ndiwomweo amazesa zisokonezo. Pali wina wayakhula kuti mcp yinawina zisakho ameneyo akunama tonse alliance ndiyimene yinawina. Koma chidukwa chaumbuli ndi kuzikonda ndichifukwa mcp yikuona ngati inawina. Kopanda alliance bwezi mcp ili kunja.

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Před měsícem

    Achina khwangwala kadyera😊😊😊

  • @user-og4oe5yp4w
    @user-og4oe5yp4w Před měsícem +1

    Ku UTM kulibe munthu angakhale president ndiye akabambe awona kuti mwina ndi mwayi wake

  • @jomochirwa
    @jomochirwa Před měsícem +3

    Adalitso kupupulumatu uku.mwina amayembekezela kuti utm ichoke kaye ku tonse.

  • @user-pk6vq1cr1b
    @user-pk6vq1cr1b Před měsícem

    Amenewo ndima setting andale muzazindikila pasogolo

  • @BrianJoe-z7u
    @BrianJoe-z7u Před měsícem +2

    Zoonadi kupupulumadi akuona ngati akatenga u prezidet koma kabambe zachisoni

  • @ShabaniKuswere
    @ShabaniKuswere Před měsícem +1

    Dyera kabambe koma akuluakulu anthu andale dyera kuteroku waona kuti ku DPP mpando wautsogoleri saupeza ndeapapa mpungwepungwe omwe uli Ku utm ndi Dr Usi iye watengerapo mwai ofuna kukatenga utsogoleri. Koma chipani cha DPP sikuti chipangidwa affect chifukwa kabambe tsogolo lake la ndale silinayambe kuoneka

  • @user-kc7sd3te3d
    @user-kc7sd3te3d Před měsícem

    Musiyeni kabambe apite but still more DPP yiwinabe whether you like it or not

  • @user-og4oe5yp4w
    @user-og4oe5yp4w Před měsícem

    Akabambe akufuna upulesidenti ku UTM

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb Před měsícem

    Mbava zokha zokha.

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před měsícem

    Munapha mesa Chilima nde a UTM atuluka musanamalize koma akusiyilani Kamanganya ka yudas😅

  • @AndrewSimakweli
    @AndrewSimakweli Před měsícem +1

    Boma lilibe masompsenya

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 Před měsícem

    Iweyo Ndiye wasalira mu tonse alayansi, Nonse amene mwasala mu tonse alayansi musama lire,muphesanso a Malawi ena

  • @user-xo8ms5wh2s
    @user-xo8ms5wh2s Před měsícem +1

    Kabambe akuthamangira ku UTM akufunako akakhale President sakudziwa kuti President wa dziko lino ndi Mutharika

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

      Aaaaa iwe usavutike ndi ankhalamba yakoyo kagwere

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před měsícem +1

    MCP ndi Chakwela ndi yakupha

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d Před měsícem

    Ife a UTM tatuluka chifukwa Chakwera anapha Chilima

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před měsícem

    Anthu akutuluka mwa alliance chifukwa chakwela akutenga ngati mpandowu anawupeza mwa iye yekha 2 alliance sakupeza mmphindu la alliance chakwela wangopanila yenkha zabwino zonse ndichifukwa UTM yatuluka yawona kuti wina wake wa phangila zose

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d Před měsícem

    Kabambe alibe chikoka

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 Před měsícem +1

    Phuma koma silabwino.

  • @JamesIngeni-ku3qj
    @JamesIngeni-ku3qj Před měsícem

    Kod anali a dpp sindimaziwa ine

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb Před měsícem

    Musiyeni atuluke akuuza anthu chifukwa chiyani??

  • @ChristianMtambalika
    @ChristianMtambalika Před měsícem

    Akanakhara chaponda tikanadandaula km munthu oti sungatipindulire ulibenso ntchito tikangokusunga monga osowa chochita

  • @MagaLassi-tg7lj
    @MagaLassi-tg7lj Před měsícem

    Asatiphe mutu uyoyo akapume Ife nganga APM

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Před měsícem

    Achoke basi siofunikila

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 Před měsícem

    Mumasuleni Nkasa

  • @PeterKasakula
    @PeterKasakula Před měsícem

    Nkhalamba ija akuthawa kambakokakamila udindo chipan chachibanja ngatiufumu😂😂😂😂😂😂😅😅😅😅😅😅😅😅

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g Před měsícem +1

    DPP yatha bas😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @Yanjanani
    @Yanjanani Před měsícem

    Oipa athawa yekha popanda omuthamangitsa

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt Před měsícem

    Zabhobho

  • @user-rz9rm4cb8x
    @user-rz9rm4cb8x Před měsícem

    Awa a umozi ndi achitsilu .mcp sinatengepo boma

  • @nellikkmwenda7087
    @nellikkmwenda7087 Před měsícem

    Amutalika.amutuma kabambe kuti apite ku utm

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y Před měsícem

    Farewell

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m Před měsícem +1

    Asiyeni akabambe analindicholinga

  • @user-xu9rh1lm8o
    @user-xu9rh1lm8o Před měsícem

    Kodi anali ndi udindo wanji ku Dpp

  • @user-kc7sd3te3d
    @user-kc7sd3te3d Před měsícem

    Musiyeni kabambe apite but still more DPP yiwinabe whether you like it or not

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před měsícem

    Anthu akutuluka mwa alliance chifukwa chakwela akutenga ngati mpandowu anawupeza mwa iye yekha 2 alliance sakupeza mmphindu la alliance chakwela wangopanila yenkha zabwino zonse ndichifukwa UTM yatuluka yawona kuti wina wake wa phangila zose

  • @user-kc7sd3te3d
    @user-kc7sd3te3d Před měsícem

    Musiyeni kabambe apite but still more DPP yiwinabe whether you like it or not

  • @user-kc7sd3te3d
    @user-kc7sd3te3d Před měsícem

    Musiyeni kabambe apite but still more DPP yiwinabe whether you like it or not