You have spoken wisely and positively to all the audience that's true kuti this government of Chakwera and his tonse alliance have totally failed and destroyed Malawian economy and it will be difficult for the next government to restore it
Church silimakhala ndi anthu a opposition okha, mliso a m boma, ukulalika mosasamala utha kuyambanitsa anthu m MPINGO. Maka nthawi ya campaign tilimoyi.
Kudzudzula kulipamenepo koma inunso atsogoleri athu achikatolika mulindivuto. Timakonda kuloza chala anzathu koma ndichani timapangapo polithandiza bomalo. Tikati tiyang'anitsitse kumpingo kwathu inuyo atsogoleri a ntchito anunso simumawasala molongosoka mumalipiro. Mwachitsanzo a Gulupa samapatsidwa malipiro abwino komanso a ntchito ena. Ifenso tikonze gawo lanthu mpamene tidzizuzula enawa. You should also set good example in leadership. Zisakomere mbuzi kugunda galu.
Popeza mwati ndi munthu wa Mulungu bola tamva koma sanafike kukhala mwana wa Mulungu popeza nayeso ndi wochimwa koma ndi wa bodza uyu Ngati kumpingo kwawo walephera ndiye alonze chala wina angoyesetsa nayeso kutukula dzikolino ndizofunika kugwilana manja koma mukalowetsa ndale ndi mu mpingo momwe ndiye Kuti tigwa tonse ndi nkhosa zomwe or iye sungayendetse dziko ife a DPP zinatikanika kale 😅😅😅
Iweso ukulalika zopusa, economics yakuti unaphunzira iwe, you do not compare zinthu zosiyana,, Mozambique ukuchita compare ndi Malawi, kapena Tanzania .... Just chinthu chimodzi like DOOKO,LA PA NYANJA ..... what it earns cannot compare ndi Malawi.Ukawauzenso nawe omwe akutumawo.
That's a very greatful speech we need such type of people who can't fear but they stand for the right thing keep it up pastor/bishop
I LIKE YOU FATHER AWUZIDWE ZOONA NGAKHALE ALI OSAMVA KOMA TIDZAWONANA PA 2025
You have spoken wisely and positively to all the audience that's true kuti this government of Chakwera and his tonse alliance have totally failed and destroyed Malawian economy and it will be difficult for the next government to restore it
Muli nzeru umu this audio shud reach to the state 🏠
Ndipo zimafunika kutii uthengawu uwafikire ndithu ukulu amenewa munthu osamva ngati ameneyi sindinamuonepo inee maulendo mbwee mbwee
A patriot.....kuphunzitsa economics momveka bwino...economics 101
True and lovely words
Akulu mulungu adzikusogolelani mukuyankhula chilungamo ngati munthu wamulungu
Patakhala kuvota mau anu ndavotera kale,u r a good preacher
That's true i do respect your massage father keep it up i like the ward's you taling as
Zikumveka bwino ndithu kuchokera pa mawu amenewa boma la abusa a Chakwera lalepheradi. Zikufunika kusankha moyenera.
Thanks very much God bless you. Your talking the truth
Your talking the truth God bless you thanks very muh
A Malawi kususuka zithu zoti sizitithandiza kukopeke nditu k500
Chilungamo chilibe zoti wochimwa ali momwemo ayi. Truth will remain and the wise will choose the right way to go. The foolish will blame the advice.
God bless you pastor don't fear for that you know is no clear but to talk people to know
Thank you man of God
Good advice thanks
What an intelligent gentleman
Well said......👏👏👏👏👏👏👏👏
Kodi abishop mawuwo basi antha siinu mikuyankhula ndimulungu wakutumani. Tikudikila titsegulenni maso ndi chilungamo
Boma anachita kulilira ili that's y vamunyera chakwera pls anthu apa central region musamuvoterenso uyuyu atipha
This pastor should not get arrested 🔥🔥🔥💯
Zochezatu mukauze
Tatopa ndimbuz izi
Mpaka anthu aMulungu kuyamba kuwayankhulisa zandale chifkwa chakuononga ndalama mopusa
Good speech ❤❤❤❤
Akanakhala wins chakwera akanangoimika manja chifukwa zinthu sizilibwino muno mu Malawi walephera yekha anthu chance anamupatsa
Our next Bishop of blantyre archdiocese
Very true man of God
Bg amenewo ndiye mau amphav zinthuzi zimafunika kuganiza mozama tisanasankhe otilamulira
Well said
Oro muthalika a lowe mudzavutika chimodzimodzi musaone kuti akalowa Mutalika ndiye zinthu zisintha ayi mukuzinamiza kwambiri tiyeni tiziwelenga mau aMulungu atiuza zoona awatu ndi masiku otsiliza Buku lopatulika linanana kale kuti masikuotsiliza mudzaona nkhondo kukangana mu maiko osiyanasiya and munthu afzakonda ndalama not munthu nzake ndipo zinthu zambiri zidzakhala zokwera mtengo kwambiri ine ndakambako zokomo abale mwabuye
That's true pastor we need to use the brain life now is expensive
Anthu Ngati awa ndi amene timawacuna
Ine ndinauza koma sakuva
It's true that they failed
Strong man of God
Samuel told Saul kuti umfumu wanu wakanidwa. Ndiye abusa azingoti zakumwamba?? Kulowa kumwamba ndi umphawi aaaaah
Powerful
It is very true that they have failed
Ndiponso achepesanso mauwo
Church silimakhala ndi anthu a opposition okha, mliso a m boma, ukulalika mosasamala utha kuyambanitsa anthu m MPINGO. Maka nthawi ya campaign tilimoyi.
Kodi umafuna anene kuti zithu zilibwino zisali bwino? Taganizani kae bwinobwino amwene osathamanga poyakhula taonani kwa nthawi yoyamba anthu a Mulungu kuyankhulapo m'mene dziko likuyendera ndipo ndi ambiri zedi moti mukwanitsa kuwaletsa onsewo? Tadekhani inuyo ngati simukuona manvutowa khala phee muzingodyelera apa sakunena za campaign ayi koma kutsegula maso anthu amene akunvutika, ndipo idakakhala campaign in church bwezi pakunveka ena kumutsutsa pompo koma ngati akumuombera m'manja choncho ndekuti anthuwo akunvomerezana nazo zomwe munthu wa nzeruyu akuyankhula ku mpingo wa Mulungu. Dziwani kuti mudziko Mulungu adalenga anthu anzeru kuposa azitsogoleri anthuwa koma kuzichepetsa kokha kumapambanitsa so you better watch your mouth.
Unenesko uli papa
🙏🙏🙏🙏
🙏🙏🙏🙏🙏
Osati zocheza
Mbambande Father
Mumakwanila fr 😂😂
Kudzudzula kulipamenepo koma inunso atsogoleri athu achikatolika mulindivuto. Timakonda kuloza chala anzathu koma ndichani timapangapo polithandiza bomalo.
Tikati tiyang'anitsitse kumpingo kwathu inuyo atsogoleri a ntchito anunso simumawasala molongosoka mumalipiro. Mwachitsanzo a Gulupa samapatsidwa malipiro abwino komanso a ntchito ena. Ifenso tikonze gawo lanthu mpamene tidzizuzula enawa. You should also set good example in leadership. Zisakomere mbuzi kugunda galu.
Zamphanvu 🙏
Kukhala ngati kachilungamo
Udatani umuwuza peter wakoyo mbuli ya mbusa iwelenge yohane 10 mbusa wakuba iwe
Takumvani Abusa
Zochezatu😂😂😂😂😂 chilungamo
Chakwera ndi Tambala Wakuda anabwera kuzaononga Dziko lino
Mau
Sizocheza
Ku bandura osaopa osafooka kkkk
Palibe chomwe amaziwa chipani chosaziwa economy chipani chomvesa chisoni
Akumanganitu
Dont fear everything akulu
Uyu ndi wabodza anthu malo poti awauze anthuwa mau achipulumutso akupanga kampeni yandani inu mungafanizile dziko lamalawi la Mozambique or zambiya zambia ndi dzikolimene limagulitsa miyala ya mtengo wapatali komanso muli Ma boulder ambili amatolera ndalama zochuluka komanso kumalawi timabalana kwambiri sizigwiliza ndikuchepa kwadzikolo Mozambique kuli ma madoko awili amene ama bweletsa ndalama plus mogodi anthu amulungu ngati awa ndi amene amapangitsa kuti dziko lisamayende bwino chifukwa amaiwala mau aMulungu amayamba kulalikira ndale mudziko simungakhale m'dalitso ayi toyeni tizipemphera kuti mulungu afalitse Malawi zikomo
Akunenatu chipulumutso kupulumutsa miyoyo ya anthu apulumuke kunjala kuumphawi kukukwera mitengo ya zinthu Kodi mau oti kupulumukawa amakamba zakumwamba kokha pepani ngati ndakulakwirani koma sitingamakambe zaulemelero ukudzawo pamene apapa anthu tikuvutika
Popeza mwati ndi munthu wa Mulungu bola tamva koma sanafike kukhala mwana wa Mulungu popeza nayeso ndi wochimwa koma ndi wa bodza uyu Ngati kumpingo kwawo walephera ndiye alonze chala wina angoyesetsa nayeso kutukula dzikolino ndizofunika kugwilana manja koma mukalowetsa ndale ndi mu mpingo momwe ndiye Kuti tigwa tonse ndi nkhosa zomwe or iye sungayendetse dziko ife a DPP zinatikanika kale 😅😅😅
Ameen Ameen tikuvutika abale mulungu atikhululukile achakwela chonde mwachose ndithu
Alomwe awa tazilarikilani za ufumu wa Mulungu
Mu church mumakhala anthu azipani zasiyasyana sibwino kukamba za ndale mufzagawanittsa church as a pastor keep your opinion to yourself
These are part of Malawi disaster
Zoona zake
Uyu ndiwabodza zambia nayo ili pamavuto azachuma munthu wa mulunguyu ndiwabodza kwambiri
Wabodxa ndi iweyo
This is a proof that MCP will reign again
Simudayankhule bwino bispo. Munthu wamulungu sanayenera kutero
Inuyo ndinu munthu wandani malume
Opusa ameneyi zikugwilizana bwanji ndiulaliki
Iweso ukulalika zopusa, economics yakuti unaphunzira iwe, you do not compare zinthu zosiyana,, Mozambique ukuchita compare ndi Malawi, kapena Tanzania .... Just chinthu chimodzi like DOOKO,LA PA NYANJA ..... what it earns cannot compare ndi Malawi.Ukawauzenso nawe omwe akutumawo.
Ngati ndiwe wa MCP wuzipase wulemu amalawi tilipa moto sitimasekesekerere ndi mbamva zimenezi
Ndiwe opusa kwambiri ndi MCP yakoyo
Umva pheni wa MCP ulendo uno
Point ndiyonena kuti, zinthu zochepa zomwe tili nazo tizigwirisa ntchito bwino.
Anthu oipa inu ndi inu nomwe munali pastogolo kulemba ma kalata kuuza anthu kuti avotele agule wa
Akulu mulungu adzikusogolelani mukuyankhula chilungamo ngati munthu wamulungu