Komentáře •

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb

    Tisiye nsanje,,nkukhala okondana.

  • @CliveWhitman-rr9ew
    @CliveWhitman-rr9ew Před 2 dny

    I have been touched from his first album till today ,he has been and he will be my only BEST in Malawi when it comes to music...
    MHSRIEP

    • @GoodmanBashir
      @GoodmanBashir Před dnem

      @@CliveWhitman-rr9ew and he was an icon indeed

  • @franciskaphwiti6271
    @franciskaphwiti6271 Před dnem +1

    Uthenga sukumveka accordingly as it is being poorly disturbed by the audiobackground..

  • @EnetChiomba
    @EnetChiomba Před 2 dny +1

    😢😢 rip sordier mulungu afungatire mzimu wanu mwalimbana nako kulimbana kwabwino

  • @WilfredYekha
    @WilfredYekha Před dnem

    May the soul of Soldier Lucius Banda RIP,One word Which We Suppose to Remember is To Keep on Knowing That We Are Here As Vistors, Any Time From Now Something Can Happen On Our lives.

  • @user-hx2nq4pq3l
    @user-hx2nq4pq3l Před 2 dny

    Mzimu wanu Lucious uuse mumtendere mwatisira nyimbo zanu zophunzitsa munalidi munthu okonda anthu ena

  • @user-hx2nq4pq3l
    @user-hx2nq4pq3l Před 2 dny

    Lulu kuyankhula mokhwima munzeru kwambiri , mzimu wa soldier Lucious Banda uuuse mumtendere

  • @AbdulAzeezChapita
    @AbdulAzeezChapita Před dnem +1

    It means he was controlling lots of people

  • @Twanguuser-ub7mb9ru6g

    Mulungu awadalise kumwambako soldier

  • @AlexMthunziChimpeni

    Lulu wandiyankhulira bwino kwambiri mtima umeneu usausiye.mzimu wa soja uuse mtendere

  • @SusanMunguambe
    @SusanMunguambe Před 2 dny

    Ambuye atichitile chifundo😭

  • @GoodmanBashir
    @GoodmanBashir Před 2 dny +1

    Bad eeeeeish

  • @PhilimonMbewe-m1q
    @PhilimonMbewe-m1q Před dnem

    Ambiri tamvutika mzimu wake uwutse mumtendele

  • @user-tr1xz4sy1w
    @user-tr1xz4sy1w Před dnem

    Rest in peace soldier

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb

    Anali ozichepesa kwambiri watimenyera ufulu.

  • @khalilugiftmasala3982

    Popeza kunalembedwa kut cha moyo chilichonse chizalawa imfa ndipo aliyense adzafa ndithu ine ndingoti zimu wawo a soldier uwuse muntendele kufikila tsiku lachiweluzo lomwe tizaonane nawo abale onse amene atisiya munthawi imeneyi tiyeni tilire koma mwachiyembekezo

  • @user-cu9jq2zn4t
    @user-cu9jq2zn4t Před 2 dny

    So sad

  • @pemphero3jere344
    @pemphero3jere344 Před 2 dny

    Nyimbo zamatathauzo tizisowa

  • @RitaDickson-ls7ol
    @RitaDickson-ls7ol Před 2 dny

    Rest in peace

  • @user-xc1gk6bw6m
    @user-xc1gk6bw6m Před 2 dny

    REST IN PEACE MY DAD SOLDIER 😭😭😭😭😭😭

  • @MarinaSakala-u5d
    @MarinaSakala-u5d Před dnem

    M😂ay he rest in peace

  • @MemoryMlotha
    @MemoryMlotha Před 2 dny

    R I P😂

  • @liundejaffali
    @liundejaffali Před 2 dny

    RlP

  • @jackmakanjira2046
    @jackmakanjira2046 Před dnem

    The song in the background title please 🙏🏾

  • @ledsonsunday336
    @ledsonsunday336 Před 2 dny

    Musazaneni zanzeru zanga,masazanene zakuchuka kwanga...ngati mufuna kunena zinthu mukanene kuti ndinali soldier kwa amphawi...muzimu wasoja uzagona..... Please respect his wish stop praising him in death as he wished

  • @FrankBanda-f5e
    @FrankBanda-f5e Před 2 dny

    Komawamwarirayo ndikatundu

  • @GracianSomola
    @GracianSomola Před 2 dny

    Koma ma jacket okupsya waa