Mwa Atupele Muli Utsogoleri - Concerned Citizen
Vložit
- čas přidán 7. 09. 2024
- On Nyasa VoiceBox, one concerned citizen says that Atupele Muluzi, has the ability to be a good leader as President of the Republic of Malawi due to his academic qualifications and professional experience.
Pa Nyasa VoiceBox, mzika ina yokhudzidwa yati Atupele Muluzi, ali ndi kuthekera kokhala mtsogoleri wabwino ngati Purezidenti wa Republic of Malawi chifukwa cha maphunziro ake komanso luso lake.
#malawi
Kod atupele sizingathele abambo anuo ukuthandizen kampen? Inetu ndikuona chomcho madalawo atithandize bwanji
Atupele is the only hope Malawians have now. This is the reason: He stops practising politics after general elections. This means he will start developing the country after elections. Please, let's try this.
Good msg
Excellent news
Well saying im with you 100%
Atupele muli usogoleli wabwino koma short temper koma ndi oganiza bhoo
Voice 🔥
❤❤ that's good idea 💡🎉
Koma Atupele sizingagwire Guys dziko si la achina Muluzi ndi Achina Muthalikas
Akulu mukuyakhula zoona. Tikufuna anthu anzelu ngati inu. Pitilizani kupeleka upangili ngati uwu mpaka zithu zizasitha
Chikangwawa bisy kugwesa ndege ya vice president
Akulu mwanena zoona kwambiri.vuto ndi umbuli kwambiri ku Malawi.
Guys tiyeseni atupele pls amalawi
💯
Kumeneku ndiye kupusa ngati mmalawi muno zipani zikumatha chifukwa chake ndi choti zimakhala za mabanja basi munthu wazelu uli bze kusapota dpp kapena udf ?
I have 💯 of this speech
100❤
Good Message Mr
,,💯zoona
Ndipo zoona
Well said
Mwayakhula bwino kwambiri amalawi ndi athu onvuta
MWA bubu mungakhale utsogoleri wanji , maphunziro sinkhani ,za ziiiiiiii
Amenewo ndiye mawu braz
Kodi apapa iweyo ukukamba zobera Mavoti or chani ? APM 2025 🇲🇼🗳
Koma he should have gone ku mbaluku to campaign for his councllor. Koma kuopa kukapereka ndalama pa ground kuumila akuluwa.
Ine sindingasapote chipani chabanja ai
Koma abale kodi tidzingomva zandale daily? Taonjezatu manyasa, tikukhala ngati timadya ndale tsopano.
Zoonadi Brother zikumveka ndithudi.
Not Muluzi family, kusolola awa
Zoona ndithu munthu oti anaphunzira za economics amayendetsa bwino dziko
Atcheya ndi wama jokes
Ok timuvotela
Nkhan pa ground wakumva wamva
Atupele he can't make it as a leader,he fails at his own constituency as MP in machinga.
Chikangawa kkkkkk
Azisiyana ma twins zochitika.
Sober minded man...
M pretty sure kut Atupele ndiekhao amene angaliphule dziko La Malawi pamoto
Koma Atupele sizingagwire Guys dziko si la achina Muluzi ndi Achina Muthalikas
Vuto lake ndilimenero amalawi inu