Mwa Atupele Muli Utsogoleri - Concerned Citizen

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 7. 09. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, one concerned citizen says that Atupele Muluzi, has the ability to be a good leader as President of the Republic of Malawi due to his academic qualifications and professional experience.
    Pa Nyasa VoiceBox, mzika ina yokhudzidwa yati Atupele Muluzi, ali ndi kuthekera kokhala mtsogoleri wabwino ngati Purezidenti wa Republic of Malawi chifukwa cha maphunziro ake komanso luso lake.
    #malawi

Komentáře • 41

  • @ClementsKamanga
    @ClementsKamanga Před měsícem +2

    Kod atupele sizingathele abambo anuo ukuthandizen kampen? Inetu ndikuona chomcho madalawo atithandize bwanji

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Před měsícem

    Atupele is the only hope Malawians have now. This is the reason: He stops practising politics after general elections. This means he will start developing the country after elections. Please, let's try this.

  • @MzondiKaunga
    @MzondiKaunga Před měsícem +1

    Good msg

  • @Lingstone-r3z
    @Lingstone-r3z Před měsícem +1

    Excellent news

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa Před měsícem +1

    Well saying im with you 100%

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Před měsícem

    Atupele muli usogoleli wabwino koma short temper koma ndi oganiza bhoo

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 Před měsícem

    Voice 🔥

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Před měsícem

    ❤❤ that's good idea 💡🎉

  • @edenbelievemseteka5197
    @edenbelievemseteka5197 Před měsícem

    Koma Atupele sizingagwire Guys dziko si la achina Muluzi ndi Achina Muthalikas

  • @user-fl7br3dw4h
    @user-fl7br3dw4h Před měsícem

    Akulu mukuyakhula zoona. Tikufuna anthu anzelu ngati inu. Pitilizani kupeleka upangili ngati uwu mpaka zithu zizasitha

  • @EssaSimon-qw8cl
    @EssaSimon-qw8cl Před měsícem

    Chikangwawa bisy kugwesa ndege ya vice president

  • @WilliamBanda-o5r
    @WilliamBanda-o5r Před měsícem

    Akulu mwanena zoona kwambiri.vuto ndi umbuli kwambiri ku Malawi.

  • @ThomasMaxwell-ks7yi
    @ThomasMaxwell-ks7yi Před měsícem

    Guys tiyeseni atupele pls amalawi

  • @Anafinyambi
    @Anafinyambi Před měsícem

    💯

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Před měsícem

    Kumeneku ndiye kupusa ngati mmalawi muno zipani zikumatha chifukwa chake ndi choti zimakhala za mabanja basi munthu wazelu uli bze kusapota dpp kapena udf ?

  • @YusufuKaifa-fr4wt
    @YusufuKaifa-fr4wt Před měsícem

    I have 💯 of this speech

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt Před měsícem

    100❤

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před měsícem

    Good Message Mr

  • @starneckkulemero7548
    @starneckkulemero7548 Před měsícem

    ,,💯zoona

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 Před měsícem

    Ndipo zoona

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 Před měsícem

    Well said

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo Před měsícem

    Mwayakhula bwino kwambiri amalawi ndi athu onvuta

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu Před měsícem

    MWA bubu mungakhale utsogoleri wanji , maphunziro sinkhani ,za ziiiiiiii

  • @MustapherLino
    @MustapherLino Před měsícem

    Amenewo ndiye mawu braz

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga Před měsícem

    Kodi apapa iweyo ukukamba zobera Mavoti or chani ? APM 2025 🇲🇼🗳

  • @mzeewandembonyirongo2972
    @mzeewandembonyirongo2972 Před měsícem

    Koma he should have gone ku mbaluku to campaign for his councllor. Koma kuopa kukapereka ndalama pa ground kuumila akuluwa.

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Před měsícem

    Ine sindingasapote chipani chabanja ai

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před měsícem

    Koma abale kodi tidzingomva zandale daily? Taonjezatu manyasa, tikukhala ngati timadya ndale tsopano.

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p Před měsícem

    Zoonadi Brother zikumveka ndithudi.

  • @johnkambala692
    @johnkambala692 Před měsícem

    Not Muluzi family, kusolola awa

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před měsícem

    Zoona ndithu munthu oti anaphunzira za economics amayendetsa bwino dziko

  • @kennedybanda
    @kennedybanda Před měsícem

    Atcheya ndi wama jokes

  • @HypeGallery-ur9xd
    @HypeGallery-ur9xd Před měsícem

    Ok timuvotela

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo Před měsícem

    Nkhan pa ground wakumva wamva

  • @ahmedmsume1489
    @ahmedmsume1489 Před měsícem

    Atupele he can't make it as a leader,he fails at his own constituency as MP in machinga.

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před měsícem

    Chikangawa kkkkkk

  • @kennedybanda
    @kennedybanda Před měsícem

    Azisiyana ma twins zochitika.

  • @GeorgeMwale-ce8eb
    @GeorgeMwale-ce8eb Před měsícem

    Sober minded man...

  • @HamzaLiya
    @HamzaLiya Před měsícem

    M pretty sure kut Atupele ndiekhao amene angaliphule dziko La Malawi pamoto

  • @edenbelievemseteka5197
    @edenbelievemseteka5197 Před měsícem

    Koma Atupele sizingagwire Guys dziko si la achina Muluzi ndi Achina Muthalikas