My heart is totally broken due to Mr chilima's death, but I can see that this guy is lying. Uyuyu asatipusitse pano. Nthawi zina chilungamo chimadziulura chokha.
People of Malawi, greetings. How are you feeling? I know for most of you the pain of death is in your hearts, including Our President Dr Laz M Chakwela . Please let's take this time to unite and to console one another. Stop the blame game. It will not help us and our beautiful country. My fellow African brothers and sisters, I am also aMalawian citizen who loves his country deeply . Take the path of peace and stop destroying our beautiful country. The right honorable vice president will never return to earth. Just know that. Please honor his legacy by uniting your country. I am praying for the late vice president's family, our dear President and for the people of Malawi. Love is the way to go right now. I love you and will continue to pray for you . Williams Alex Mbonga
CHAKWERA, KUNKUYU, ZIKHALE NG'OMA, CHIMWENDO BANDA, MKAKA, CATHERINE HARA be careful Malawians are watching. MCP HAS ENDED; IT WILL NEVER EVER BE AGAIN!!!!
Kodi awawa akuti bwanji nawoso awa,,English yikunvuta ndiye akulankhula ngati amalankhulana ndi mabwana😂😂😂koma 😅😅😅😅kodi mukufuna mutchukilepo apa eti tamakangokumbani mbewa uko basi
Kkkkk freedom of speech...from Mulanje
Condolences to you and the family.may the Grace of GOD be with you all.amen.
Wayankhulawe yehova akukuyang'na pa khani imeneyi
Don't promote violence please
Koma akuyakhulawo siwangopeka coz mawuwo sakunveka mwa ndalama 😅😅
😂😂 Awa sanadye sizikuveka zomwe akuyankhula
The beuty of freedom of speech 😂😂
Uyuyu ndiwabodza uyu😂😂 zochita kukonza izi😂
Ineyo ndikuona kuti m c p ingothetsedwa bass
Yes ayambe chipani china zoonadi
Isadzanvekenso mcp ipite ndi ma minister ankhanza onse asadzalowenso chipani chilichonse
Kuyankhula zosamveka ,AMalawi ali ndi njala yofuna kumva zowona zosatira za imfayi .So try kubwelesa zinthu zomveka kwa anthu 😅😅😅😂😂😂
Mmmm lindani ofufuza .phuma bwanji?
Palibe Chinsinsi padziko lapansi, Mulungu amavumbulutsa zinsinsi zobisika angakhale pa nsi panyanja
Chizungu chakecho eeeee😂😂km guys mumathatu kkkk😂
Kkkkkkk komatu guys muzikhala serious
Onse akwiya apa ndi A MCP okha okha tiziona
longosola Fadah osawopa😅😅😅😅😅😅😅😅😅
Muziwe kuti mcp basi yatha mwapita ndipo tikumangani
Za boza izizi mumvere bho bho conversation yi. 😂
Wait for investigation. Don't rush.
Lankhulani chilankhulo choti muthe kukamba zomveka bambo. Nkhani yanu ndi yoti chani yomwe mwabweletsa???
🔥🔥🔥
Ndapanga subscribe,.you will update us more.
My heart is totally broken due to Mr chilima's death, but I can see that this guy is lying. Uyuyu asatipusitse pano. Nthawi zina chilungamo chimadziulura chokha.
Inu kodi mwadya chani kodi palibe chimene chikumveka apa 😢😢😢
Koma iweyo momweukuvekela ungayakhule ndi apule ine Siwa MCP Koma idzizi ndidzazi!!!!!
Aaaaaa choka iwe nawe. The way you are speaking uiungoganiza
agalu kkkkk musiyeni president
Nice greys❤
Kalikonse tikaona ,muyaluka
Mwayaluka basi, mu Chikangawa munali Mulungu si mutiuza bodzaaaaaa
Deus proverá
Mwamupha wapita basi,, kwasala muziphanano nokhanokha, ife as time goes tilimba mtima
😅😅😅😅😅😅😅😅 Nyasaland ayi zikomo
Mulungu oziwa kuweluza akupaseni madaliso ochuluka .
Mmmu Kodi ndani amenei?😮
Ndiye apa akuti bwanji. Kikikkkk
😮
Oh! No! This is serious.
Bozailo mukulephera chizungu kikkk
Mau awa angayankhulane ndi pulezidenti?
Akuyakhulayo ndindani kodi, sizochezeratu izi
Machende tazirankhura zinthu zazeru Machende ako wanva ukumuyikira kumbuyo chakwera bwanji
Ngati ndimtukwane namachende ameneyu mxxx zaziiii
Kodi can't we wait for investigation to finish first? Stop this please aaah
Palibe funds yomveka apa timawona ngati muli ndi zinthu zogwilika. Komatu izi muzitenge bwino
😅😅palibe2 chmene chikuveka mwadya koma
😅😅😅 bodza lakeso nde yayitu
Zaziii kodi mukumsowa nkhani yoti mutchukire pano???
Koma 😂iweyo amene wapanga audio iyiyi anakupanga
Mukufuna mudziwe mau ake eni eni kut mumuphenso wadya koma akuopa kufa mcp kkkkkk
Koma bodza lakelo😊
Mwayambira pakati nkhaniyo bwanji?? Komanso Mulungu akuone ndi bodza lakolo and chilungamo akuchidziwa ndi Mulungu
Kafukufuku ameneyo akhala opanda chilungamo ,this is Malawi ndikafukufuku uti unaphulapo kanthu kanzeru?wait and see.
Osamaoneka kuchenjera pa gulu dekhani
Mcp khalidwe lonyasa sangasiye awa dzigawenga zawanthu izi Mulungu akukantheni nonse amene mwachotsa miyoyo yabale athu asanu ndi anayi
Mau a maluzi sasowa kmb edit yo mwaesesa ndithu
Amamvera za anthu. Iye ubongo alibe?
Kkkkk zoyenda eshiii
😂😂😂 hahaha km guys et
Mukuti chiyani kodi?
Pepani,God is with Malawi.U are trying to who?
Nde UTM mchita chiyani ndi chakwela???????
Kodi ukuti chani iwenso ??? Tayankhula zonveka apa asah !! Ngat ulibe zonena osangokhala bwanji ..
Zimenezi sizinanveke?
Waboza uyu
Munthuyutu sakuuza inu alipo amene amamuuza nde angotibenthulira
Chitsilu iwe iweyo ndi ndani? Watani Kodi? Sakunveka😮
Ife tikumva amene sanave zake zimenezo
Za ziii.mungoliubwa lubwatu apa
Amwen ife sikut tili pano umawononga data ndi nkhan zake ngat izi plz ifa ndi ifa ndpo ikachitika imakhala kut yachitik basi
Ayi tamva nawo zakuchipinda .. Ife tili chete kutchela nkhutu. Iponde fadaaaaa
Iwee wasowa zochita eti .....kagone !! Palibe chomwe chikumveka zomwe ukulankhula....ndiwe Cadet takudziwa iiiiiiya ....ungoti kukamba Ichi kusiya kukamba Ichi kusiya kagwere uko shatapu !!!!!
Umbuli at its best,,,,you want to hear what you think,,,,,,,
A government of national unity is possible but it will simply be to ransack the economy and go home.
Koma ndiye zawo Zada basi panopa aliyese waziwa Kuti MCP ndi ya kumpha ndipo yizakhara history mupaka kalekale
😂😂😂😂 Koma abale....
Ayise unadya chani?
Mudziona simunati aphwanga mfiti Inu akapolo inu
MCP mudziwaso 😂😂
Foolishness at it's best. Tiyeni tikalime kuminda uku andale asiyeni sugar anapanga kale
People of Malawi, greetings. How are you feeling? I know for most of you the pain of death is in your hearts, including Our President Dr Laz M Chakwela . Please let's take this time to unite and to console one another. Stop the blame game. It will not help us and our beautiful country. My fellow African brothers and sisters, I am also aMalawian citizen who loves his country deeply . Take the path of peace and stop destroying our beautiful country. The right honorable vice president will never return to earth. Just know that. Please honor his legacy by uniting your country. I am praying for the late vice president's family, our dear President and for the people of Malawi. Love is the way to go right now. I love you and will continue to pray for you . Williams Alex Mbonga
Sirent
Senseless
Komatu tikuva zithu pano aliyese ndi wa nzeru kuti ukhale wa nzeru unyoze chakera basi
Tayakhulani zomveka man mukuti chani kodi
Akuyankhura ndani izi??
Chitsilu cha munthu iwe ambuye akuone ndipo akuyendere ndithu
Kodi wamwa ambuye ntengeni akuyankhula apayutu
Koma chizungu chavutapo apa
Zosaveka izo kubwebweta nenani zoona apa
Iwe ndi kape fada wayaluka.
Mawu ake amenewo ungayankhulane ndi bwana ake ati?😅😅
😂😂😂😂
Koma bodza ili simudalikonze bwino tsopano mwayamba kunyozetsa za chisonizi.wosamatelo ife tili ndi chisoni esh.
Who is speaking here? How do we know this is genuine?
Za ziii ngat izi. Ma tittle kungoika just to attract anthu basi.
Za boza izi comfused cump ndi yomwe yikukoledzera moto
😢😢😢😢
Chizungu chimenecho ungakumane ndi president...?😂😂
😅😅
Washoke chakwel please matogo yake
Iwe kasambe Kaye palibe chomwe chikuveka apa
CHAKWERA, KUNKUYU, ZIKHALE NG'OMA, CHIMWENDO BANDA, MKAKA, CATHERINE HARA be careful Malawians are watching. MCP HAS ENDED; IT WILL NEVER EVER BE AGAIN!!!!
Musokosa chabe apa
Kodi awawa akuti bwanji nawoso awa,,English yikunvuta ndiye akulankhula ngati amalankhulana ndi mabwana😂😂😂koma 😅😅😅😅kodi mukufuna mutchukilepo apa eti tamakangokumbani mbewa uko basi
Kape iwe
Khalani komweko musathawe nanunso mudyedwe
Voice of poor person iyi
Iwe
😂😂😂 musamale kwambiri chifukwa ma activists amene alipo panopawa ndioopsa, ndima aliens so be careful you'll die without anything touching you