Zaululuka kuti Chakwera wapha Chilima

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 17. 06. 2024

Komentáře • 178

  • @Mpikamezo20-nt5dv
    @Mpikamezo20-nt5dv Před 17 dny +1

    Kkkkk freedom of speech...from Mulanje

  • @MumbaPlayson
    @MumbaPlayson Před 17 dny +2

    Condolences to you and the family.may the Grace of GOD be with you all.amen.

  • @BridjetFrank
    @BridjetFrank Před 17 dny +9

    Wayankhulawe yehova akukuyang'na pa khani imeneyi

  • @user-tg3bl5ey9v
    @user-tg3bl5ey9v Před 17 dny +3

    Koma akuyakhulawo siwangopeka coz mawuwo sakunveka mwa ndalama 😅😅

  • @user-zf9xs3zj9b
    @user-zf9xs3zj9b Před 17 dny +2

    😂😂 Awa sanadye sizikuveka zomwe akuyankhula

  • @thondoyaenterprise3795
    @thondoyaenterprise3795 Před 17 dny +1

    The beuty of freedom of speech 😂😂

  • @Wittie0505
    @Wittie0505 Před 17 dny +1

    Uyuyu ndiwabodza uyu😂😂 zochita kukonza izi😂

  • @DevidsamZikacha
    @DevidsamZikacha Před 17 dny +5

    Ineyo ndikuona kuti m c p ingothetsedwa bass

    • @acklaschintowe
      @acklaschintowe Před 17 dny

      Yes ayambe chipani china zoonadi

    • @jackiemayanika
      @jackiemayanika Před 17 dny +1

      Isadzanvekenso mcp ipite ndi ma minister ankhanza onse asadzalowenso chipani chilichonse

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Před 17 dny

    Kuyankhula zosamveka ,AMalawi ali ndi njala yofuna kumva zowona zosatira za imfayi .So try kubwelesa zinthu zomveka kwa anthu 😅😅😅😂😂😂

  • @ElizabethMaononga
    @ElizabethMaononga Před 17 dny

    Mmmm lindani ofufuza .phuma bwanji?

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Před dnem

    Palibe Chinsinsi padziko lapansi, Mulungu amavumbulutsa zinsinsi zobisika angakhale pa nsi panyanja

  • @Donvaga
    @Donvaga Před 17 dny

    Chizungu chakecho eeeee😂😂km guys mumathatu kkkk😂

  • @JustinLipipa
    @JustinLipipa Před 17 dny

    Kkkkkkk komatu guys muzikhala serious

  • @mafukenimasangwi5487
    @mafukenimasangwi5487 Před 17 dny +1

    Onse akwiya apa ndi A MCP okha okha tiziona

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Před 17 dny +1

    longosola Fadah osawopa😅😅😅😅😅😅😅😅😅

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d Před 17 dny +2

    Muziwe kuti mcp basi yatha mwapita ndipo tikumangani

  • @AngungaThatcherNgoma
    @AngungaThatcherNgoma Před 17 dny

    Za boza izizi mumvere bho bho conversation yi. 😂

  • @johnkambala692
    @johnkambala692 Před 17 dny

    Wait for investigation. Don't rush.

  • @rholingssambale8274
    @rholingssambale8274 Před 17 dny +1

    Lankhulani chilankhulo choti muthe kukamba zomveka bambo. Nkhani yanu ndi yoti chani yomwe mwabweletsa???

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v Před 17 dny

    🔥🔥🔥

  • @wilbroadm
    @wilbroadm Před 17 dny

    Ndapanga subscribe,.you will update us more.

  • @user-ty5wq9js8f
    @user-ty5wq9js8f Před 17 dny

    My heart is totally broken due to Mr chilima's death, but I can see that this guy is lying. Uyuyu asatipusitse pano. Nthawi zina chilungamo chimadziulura chokha.

  • @user-or7ng3fj8f
    @user-or7ng3fj8f Před 17 dny

    Inu kodi mwadya chani kodi palibe chimene chikumveka apa 😢😢😢

  • @FrancisStima-sc7zs
    @FrancisStima-sc7zs Před 17 dny

    Koma iweyo momweukuvekela ungayakhule ndi apule ine Siwa MCP Koma idzizi ndidzazi!!!!!

  • @enockdaisi1306
    @enockdaisi1306 Před 17 dny

    Aaaaaa choka iwe nawe. The way you are speaking uiungoganiza

  • @BrownMainje-sh7hj
    @BrownMainje-sh7hj Před 17 dny

    agalu kkkkk musiyeni president

  • @HalistarStreet
    @HalistarStreet Před 17 dny

    Nice greys❤

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu Před 18 dny

    Kalikonse tikaona ,muyaluka

  • @marypatriciamakuru226
    @marypatriciamakuru226 Před 17 dny

    Mwayaluka basi, mu Chikangawa munali Mulungu si mutiuza bodzaaaaaa

  • @fidelixdezembro4599
    @fidelixdezembro4599 Před 17 dny

    Deus proverá

  • @LinessdorisScot
    @LinessdorisScot Před 17 dny

    Mwamupha wapita basi,, kwasala muziphanano nokhanokha, ife as time goes tilimba mtima

  • @MustaphaImuran
    @MustaphaImuran Před 17 dny

    😅😅😅😅😅😅😅😅 Nyasaland ayi zikomo

  • @NellxXebo
    @NellxXebo Před 17 dny

    Mulungu oziwa kuweluza akupaseni madaliso ochuluka .

  • @sfelanchirwa4190
    @sfelanchirwa4190 Před 17 dny

    Mmmu Kodi ndani amenei?😮

  • @user-rz6xh8qg5r
    @user-rz6xh8qg5r Před 17 dny

    Ndiye apa akuti bwanji. Kikikkkk

  • @BensonChizenga
    @BensonChizenga Před 17 dny

    😮

  • @noahmshanga-rb1xc
    @noahmshanga-rb1xc Před 17 dny

    Oh! No! This is serious.

  • @user-ry9ql9jv3y
    @user-ry9ql9jv3y Před 17 dny

    Bozailo mukulephera chizungu kikkk

  • @fxmw
    @fxmw Před 17 dny

    Mau awa angayankhulane ndi pulezidenti?

  • @WilliamKawaza
    @WilliamKawaza Před 17 dny

    Akuyakhulayo ndindani kodi, sizochezeratu izi

  • @SmartJumbe
    @SmartJumbe Před 17 dny

    Machende tazirankhura zinthu zazeru Machende ako wanva ukumuyikira kumbuyo chakwera bwanji

  • @GwejeNundwe
    @GwejeNundwe Před 17 dny

    Ngati ndimtukwane namachende ameneyu mxxx zaziiii

  • @sylviachitseko397
    @sylviachitseko397 Před 17 dny

    Kodi can't we wait for investigation to finish first? Stop this please aaah

  • @FelixMhango
    @FelixMhango Před 17 dny

    Palibe funds yomveka apa timawona ngati muli ndi zinthu zogwilika. Komatu izi muzitenge bwino

  • @efkayshaun890
    @efkayshaun890 Před 17 dny +2

    😅😅palibe2 chmene chikuveka mwadya koma

  • @knacktricky8521
    @knacktricky8521 Před 17 dny

    😅😅😅 bodza lakeso nde yayitu

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Před 17 dny

    Zaziii kodi mukumsowa nkhani yoti mutchukire pano???

  • @YamzyAmos
    @YamzyAmos Před 17 dny

    Koma 😂iweyo amene wapanga audio iyiyi anakupanga

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z Před 17 dny

    Mukufuna mudziwe mau ake eni eni kut mumuphenso wadya koma akuopa kufa mcp kkkkkk

  • @VioletMaseko-ys4cu
    @VioletMaseko-ys4cu Před 17 dny

    Koma bodza lakelo😊

  • @AllanaChiphazi
    @AllanaChiphazi Před 17 dny

    Mwayambira pakati nkhaniyo bwanji?? Komanso Mulungu akuone ndi bodza lakolo and chilungamo akuchidziwa ndi Mulungu

  • @MacBanda-df5zk
    @MacBanda-df5zk Před 17 dny

    Kafukufuku ameneyo akhala opanda chilungamo ,this is Malawi ndikafukufuku uti unaphulapo kanthu kanzeru?wait and see.

  • @ElizabethMaononga
    @ElizabethMaononga Před 17 dny

    Osamaoneka kuchenjera pa gulu dekhani

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y Před 17 dny

    Mcp khalidwe lonyasa sangasiye awa dzigawenga zawanthu izi Mulungu akukantheni nonse amene mwachotsa miyoyo yabale athu asanu ndi anayi

  • @user-tw9nl6ks9d
    @user-tw9nl6ks9d Před 17 dny

    Mau a maluzi sasowa kmb edit yo mwaesesa ndithu

  • @listonnantapo1670
    @listonnantapo1670 Před 17 dny

    Amamvera za anthu. Iye ubongo alibe?

  • @sokojane4015
    @sokojane4015 Před 17 dny

    Kkkkk zoyenda eshiii

  • @Donvaga
    @Donvaga Před 17 dny

    😂😂😂 hahaha km guys et

  • @robertkalima874
    @robertkalima874 Před 17 dny

    Mukuti chiyani kodi?

  • @FOSTERLUPIYA-zc1xv
    @FOSTERLUPIYA-zc1xv Před 17 dny

    Pepani,God is with Malawi.U are trying to who?

  • @stevenghambi3471
    @stevenghambi3471 Před 17 dny

    Nde UTM mchita chiyani ndi chakwela???????

  • @burtonjere-wn3qu
    @burtonjere-wn3qu Před 18 dny +11

    Kodi ukuti chani iwenso ??? Tayankhula zonveka apa asah !! Ngat ulibe zonena osangokhala bwanji ..

  • @ElizabethMaononga
    @ElizabethMaononga Před 17 dny

    Za ziii.mungoliubwa lubwatu apa

  • @user-gh7zg5dd7l
    @user-gh7zg5dd7l Před 17 dny

    Amwen ife sikut tili pano umawononga data ndi nkhan zake ngat izi plz ifa ndi ifa ndpo ikachitika imakhala kut yachitik basi

  • @ReginaMhango-zn2iy
    @ReginaMhango-zn2iy Před 17 dny

    Ayi tamva nawo zakuchipinda .. Ife tili chete kutchela nkhutu. Iponde fadaaaaa

  • @tendaimakamabviko5916
    @tendaimakamabviko5916 Před 17 dny

    Iwee wasowa zochita eti .....kagone !! Palibe chomwe chikumveka zomwe ukulankhula....ndiwe Cadet takudziwa iiiiiiya ....ungoti kukamba Ichi kusiya kukamba Ichi kusiya kagwere uko shatapu !!!!!

  • @ivymakiyi
    @ivymakiyi Před 17 dny

    Umbuli at its best,,,,you want to hear what you think,,,,,,,

  • @Royhauya-uw2kr
    @Royhauya-uw2kr Před 17 dny

    A government of national unity is possible but it will simply be to ransack the economy and go home.

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Před 17 dny

    Koma ndiye zawo Zada basi panopa aliyese waziwa Kuti MCP ndi ya kumpha ndipo yizakhara history mupaka kalekale

  • @user-ty4pq5ub3q
    @user-ty4pq5ub3q Před 17 dny

    😂😂😂😂 Koma abale....

  • @nyanguoipa6996
    @nyanguoipa6996 Před 17 dny

    Ayise unadya chani?

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn Před 17 dny

    Mudziona simunati aphwanga mfiti Inu akapolo inu

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 Před 18 dny

    MCP mudziwaso 😂😂

  • @PaulMalemba-pp8hk
    @PaulMalemba-pp8hk Před 17 dny

    Foolishness at it's best. Tiyeni tikalime kuminda uku andale asiyeni sugar anapanga kale

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga Před 17 dny +2

    People of Malawi, greetings. How are you feeling? I know for most of you the pain of death is in your hearts, including Our President Dr Laz M Chakwela . Please let's take this time to unite and to console one another. Stop the blame game. It will not help us and our beautiful country. My fellow African brothers and sisters, I am also aMalawian citizen who loves his country deeply . Take the path of peace and stop destroying our beautiful country. The right honorable vice president will never return to earth. Just know that. Please honor his legacy by uniting your country. I am praying for the late vice president's family, our dear President and for the people of Malawi. Love is the way to go right now. I love you and will continue to pray for you . Williams Alex Mbonga

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z Před 17 dny

    Komatu tikuva zithu pano aliyese ndi wa nzeru kuti ukhale wa nzeru unyoze chakera basi

  • @Christopher-xc2ey
    @Christopher-xc2ey Před 17 dny

    Tayakhulani zomveka man mukuti chani kodi

  • @user-ty4pq5ub3q
    @user-ty4pq5ub3q Před 17 dny

    Akuyankhura ndani izi??

  • @user-cj1nw7bi1k
    @user-cj1nw7bi1k Před 17 dny

    Chitsilu cha munthu iwe ambuye akuone ndipo akuyendere ndithu

  • @user-lb8xz9lt3z
    @user-lb8xz9lt3z Před 17 dny

    Kodi wamwa ambuye ntengeni akuyankhula apayutu

  • @jackmuhura1797
    @jackmuhura1797 Před 17 dny

    Koma chizungu chavutapo apa

  • @AlexSymon-he1vt
    @AlexSymon-he1vt Před 17 dny

    Zosaveka izo kubwebweta nenani zoona apa

  • @user-us5hw4uy3t
    @user-us5hw4uy3t Před 17 dny

    Iwe ndi kape fada wayaluka.

  • @Abigail-fh1rm
    @Abigail-fh1rm Před 17 dny

    Mawu ake amenewo ungayankhulane ndi bwana ake ati?😅😅

  • @jomochirwa
    @jomochirwa Před 17 dny

    Koma bodza ili simudalikonze bwino tsopano mwayamba kunyozetsa za chisonizi.wosamatelo ife tili ndi chisoni esh.

  • @user-gr5zt6kw3s
    @user-gr5zt6kw3s Před 17 dny

    Who is speaking here? How do we know this is genuine?

  • @amourvido8027
    @amourvido8027 Před 17 dny

    Za ziii ngat izi. Ma tittle kungoika just to attract anthu basi.

  • @festusmhango
    @festusmhango Před 17 dny

    Za boza izi comfused cump ndi yomwe yikukoledzera moto

  • @OFG-th3st
    @OFG-th3st Před 17 dny +1

    😢😢😢😢

  • @franciscoduartie5762
    @franciscoduartie5762 Před 17 dny

    Chizungu chimenecho ungakumane ndi president...?😂😂

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet Před 17 dny

    Washoke chakwel please matogo yake

  • @chissanobanda5004
    @chissanobanda5004 Před 17 dny

    Iwe kasambe Kaye palibe chomwe chikuveka apa

  • @NEBERTMVULA
    @NEBERTMVULA Před 17 dny

    CHAKWERA, KUNKUYU, ZIKHALE NG'OMA, CHIMWENDO BANDA, MKAKA, CATHERINE HARA be careful Malawians are watching. MCP HAS ENDED; IT WILL NEVER EVER BE AGAIN!!!!

  • @andrewchiusiwa3487
    @andrewchiusiwa3487 Před 17 dny

    Musokosa chabe apa

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p Před 17 dny

    Kodi awawa akuti bwanji nawoso awa,,English yikunvuta ndiye akulankhula ngati amalankhulana ndi mabwana😂😂😂koma 😅😅😅😅kodi mukufuna mutchukilepo apa eti tamakangokumbani mbewa uko basi

  • @noelchitimbe
    @noelchitimbe Před 17 dny

    Kape iwe

  • @IsaacTsinde
    @IsaacTsinde Před 18 dny

    Khalani komweko musathawe nanunso mudyedwe

  • @laureenshaibu
    @laureenshaibu Před 17 dny

    Voice of poor person iyi

  • @user-dp4lv6lo2o
    @user-dp4lv6lo2o Před 17 dny

    Iwe

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn

    😂😂😂 musamale kwambiri chifukwa ma activists amene alipo panopawa ndioopsa, ndima aliens so be careful you'll die without anything touching you