Video není dostupné.
Omlouváme se.

A Michael Usi Alibe Impact Inaliyonse Ku UTM Olo Ukhansala Sangawine - UTM Member

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 28. 08. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, A UTM member says that Vice President Michael Usi has no real impact in UTM, he cannot even contest as a councillor and win.
    Pa Nyasa VoiceBox, membala wa UTM wati Vice President Michael Usi alibe chikoka mu UTM, sangapikisane nawo ngati khansala ndikupambana.
    #malawi

Komentáře • 62

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy Před měsícem +14

    And munthu otan oti nd mtsogoleri km ma meeting amwambo wamaliro osapanga attend kmnso akapanga attend osayankhulapo chonsecho nd mtsogoleri amathanthauza chan???

  • @josephinemisomali6840
    @josephinemisomali6840 Před měsícem +7

    Funso mkumati Kodi nsalu zikugawidwa lerozi Kaya ndingongole zomwe zikufuna kuperekedwa lerozi nthawi yonse zinali kt amadikila Chilima amwalire Kaye UTM gwilanani manja Zambiri zichitika Koma osafooka

  • @LamieTiger
    @LamieTiger Před měsícem +5

    Mbili ya usi amakhala president straight tithakuona khadza Za John Tembo

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Před měsícem +4

    Rest in peace SKC , we shall always remember you, 2025 ndipafupi apa

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 Před měsícem +4

    Well spoken

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Před měsícem +3

    Osamaphweketsa Bon Kalindo. Bon Kalindo analosera za imfa ya Chilima. Ndipo ananena pa 6th June 2024 kuti Chakwera wakonza plan yakupha Chilima ndi ndege. Ndipo anamuuza Chilima asakwere ndege. Pa 10 June ndege ya Chilima inagwetsedwa. Pa 15 June, MCP inamanga Bon Kalindo kamba ka ma audio.

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Před měsícem +3

    Tidzadandaula akadzatuluka kaliati chifukwa ndi chipilala cha chipani

  • @SamuelMthengo
    @SamuelMthengo Před měsícem

    Very powerful message.

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt Před měsícem +3

    Zoona Mau abwino kwambili maso kusongolo

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em Před měsícem +1

    Viva UTM viva

  • @thomasphiri-zr3xs
    @thomasphiri-zr3xs Před měsícem

    Very true comrade le take on Nyalonje has no political impact indeed in her last constituency b4 her lost her seat pipo in the constituency booted her out bcos of her characters manners...........my plea to UTM G.members mama kaliati do a better research on mps to stand in 2025 elections don't just hand pick the rejects from other parties now are paying back what we sow in 2019.

  • @alinafesalima5597
    @alinafesalima5597 Před měsícem +2

    A Michael Usi ndi munthudi owumila koopsa ine ndagwirizana nanu ndipo sapasa munthu ndalama yake

  • @thomasphiri-zr3xs
    @thomasphiri-zr3xs Před měsícem

    Lets allow new members why pipo r flocking to UTM now.....there is potential to win elections though reqiures proper partners.
    However let's give chance to madam Mary Chilima if so she can accept to compete any position now or later but God shows that in the years to come Shaun Chilima will bounce back into politics same UTM with powerful change and will rule the country.
    What late VP Chilima was doing hasn't been fulfilled so spiritually power is coming back to complete where left.

  • @Marymahendra
    @Marymahendra Před měsícem

    Thanks to god you have come out from the lion side completely different between evil people xx

  • @khumalonyirenda4437
    @khumalonyirenda4437 Před měsícem

    Morefire Dr, micheal usi

  • @VincentMtambo
    @VincentMtambo Před měsícem

    Kaliati is Very loyal. Ndinaona nthawi ya Bingu sanathawe

  • @beakab2378
    @beakab2378 Před měsícem

    Good message, 👏👏👏

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz Před měsícem +1

    Uku ndiye akuyakhula was wondering kuti guys how can u trust Micheal usiiiii???

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn Před měsícem

    UTM siinagawanike koma tsopano tingodziwa kuti ma utm members enieni ndi atiwo
    Ife till nganganga pa UTM

  • @daviskamonde4882
    @daviskamonde4882 Před měsícem

    Reality!!

  • @suzenzulu9412
    @suzenzulu9412 Před měsícem

    UTM should support Kaliyati for presidency.

  • @AbrahamTembo-z5k
    @AbrahamTembo-z5k Před měsícem

    Zikuwoneka kt alibe impact ku chipani, koma ku Dziko, alinayo. PENYETSETSANI KWAMBIRI OSANGOCHITA ZINTHU ZA PHUMA ndi MKWIYO. S.K.C. pomusankha, adawonamo NZERU ndipo ambiri tinakhutira. Dr Michael Usi, ali ndi popularity across the country. Mwina poti ife tikuziwonera patali mwina.

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 Před měsícem

    Usi si wa UTM ndipo kalikonse tikaonana pa 19 Friday li

  • @user-yv8hc3fd7f
    @user-yv8hc3fd7f Před měsícem

    We want Kabambe

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p Před měsícem

    This is good

  • @JamesIngeni-ku3qj
    @JamesIngeni-ku3qj Před měsícem

    Manganya is a betrayer and I can believe kut munthuyu ndi oipa nchochi

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Vuto ku Malawi ndi kukoza or kiyanjanisa ayi ndithu koma kupasula ndi kibwelesa chidani pakati pa anthu or chipani UTM be careful mawa sikutali chilima anasankha usi chilipo chomwe anawona mwayiye

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem

    Zoona abwana amene mukuyankhula,,pitilizani kulangiza anthu a UTM,,Bon Kalindo akufunila DPP iwine

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda Před měsícem

    Utn kuyaghayika

  • @eliasmgala8469
    @eliasmgala8469 Před měsícem

    Micheal Usi mukumunenayotu Chilima dolo amene timamunenayo, anamusankha iye kt akhale Vice wake enanu kukusiyani uko. And I think amaganizadi bwino munthu uja. Imagine akanasankha wina like this one or ena aja!

  • @GracePendame
    @GracePendame Před měsícem

    Ndiwakabudura uyu usi simunthu wabwino ndi yudasi uyu osamusekerera

  • @EliasKawuwa
    @EliasKawuwa Před měsícem

    Anthu a UTM mwadzadza ndi nkhwidzi pa wina ndi zake, mmalo mongwirizana chifukwa chopititsa patsongolo chipani chanu,mmalo mwatsongoza kuika patsongolo zofuna zanu,choncho mwaononga chipani Cha mwini wake Malemu SKC ,ndipo zimene mukuchitazi,anakakhara kuti SKC Ali moyo,nonse SKC anakakukwapulani kwambiri pazimene mukuchitazi,ngati mmene ambuye Yesu anachitira ataona anthu akungwiritsa tchalitchi kugulitsira malonda, the problem is,nonse mumafuna ma udindou Boma,nde mmalo mwake mwafuna kuuikira azanu ama udindo Boma, that's very bad, just feeling sorry for all UTM members kuti atsongoleri anu onse ndi adyera,ndipo chipani Cha UTM chitha movetsa Chisomo,chifukwa Cha dyera, that's why zipani zambiri Malawi muno ndi family parties,at least zimayendako, koma zinazi nde Kaya ndithu,dyera lakula mu UTM,mwaononga chipani chifukwa Cha Nsanje

  • @AMONINICHOLAS-g2m
    @AMONINICHOLAS-g2m Před měsícem

    Masophenya andari ndi Chilima Inu aye Mp mikuyakhulani mulibe vision

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o Před měsícem

    Yudas 😢

  • @amosnyirenda-pl1ss
    @amosnyirenda-pl1ss Před měsícem

    wasanje ise nikaliyati wako musiyeni usi alamulile

  • @BellaMandala
    @BellaMandala Před měsícem

    Uncle shortawo bas angokhala ku MCP komko bas

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Před měsícem

    anthu ofuna kugulisa utm aja ena ndakuluwa

  • @JustusSNkhata
    @JustusSNkhata Před měsícem

    Komanso kuchoka mu mgwirizano chisalhale chifukwa kuti anthu a UTM asiye kutumikila a Makawi

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh Před měsícem

    Ndipo sidzawaonaso,apa mwayankhula bwino mwandilumbitsa mtima,anandinyasatu short one ameneyu

  • @LivaneMsyamboza
    @LivaneMsyamboza Před měsícem

    Ndipo mwayakhula bwino

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Před měsícem

    Onse ankayamba chonchi ndi pang'ono pang'ono uzakhumudwa atakhala nsogoleli wa ziko enanu muli ndi nkhwizi chabe ndi mzanu musiyeni ,gulu la kaliat likufuna kubwerera kwao paja ndi a dpp

  • @IsaacChapotera
    @IsaacChapotera Před měsícem

    Mau a mphamvu

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před měsícem

    Akaliayati ndi nkhalidwe lawo atamwalila abingu anachita chi.mozi mozi kunyoza mai j b ndiye amene akuziwa mai kaliyati sakudabwa ayi

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem

    Anthu akonda ndrama ndi galimoto za Boma,,anthu Albie chikondi

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před měsícem +1

    Inu ndi adpp msatisokose ife ayi adyela ndinuyo mmene anamzuzila adpp lelo adpp bdiabwino kwachilima poti wamwamwalila ayi kaya msanyoze ausi ayi i u ndiamene mkufuna kugulisa chipani kwa adani

    • @user-wd9yd1bg9n
      @user-wd9yd1bg9n Před měsícem

      Muziti poti mcp ysmupha nanga mukubisa chani

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

      Ana anjoka inu mukhalira yomweyo

    • @beakab2378
      @beakab2378 Před měsícem

      DPP mukuinyozayo inamusiya Chilima apite wamoyo, iye nkumainyoza nkupita ku ng'ona zokupha. Phunziranipo phunziro.

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e Před měsícem

    Mau omveka bwino micheal utsi pomwe anaoneketa kuti si wa utm ndi nthawi ya maliro achilimA osayakhula chili conse kungofziwiratu kuti ndiyemwe anapereka chilima manja mwa chakwera ndiye manganya si wautm koma mcp

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu Před měsícem +1

    Tisankhe Patricia Kaliati kukhala president .Ndipo ndi munthu olimbikira ,opanda mantha komanso ochuluka mmalawi muno timamudziwa ndi kumukonda

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

      Zoona Patricia Kaliati mpando omwe Ali akhale omweo

  • @user-hr6dj4xc8l
    @user-hr6dj4xc8l Před měsícem

    😂😂😂😂 uko kunali kulira kwa anamalra

  • @hissimajohn965
    @hissimajohn965 Před měsícem

    Za ziii

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica Před měsícem +1

    Alindi impact mudziko lamalawj kuyambira kelekale. Sagawa masweet.

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Před měsícem

    Say NO to Kabambe (utm presidency)

  • @user-er7ub4ug7y
    @user-er7ub4ug7y Před měsícem

    Atumidwa ndi MCP awa

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Před měsícem

    Awalandire alendo ofuna kulowa UTM koma osati zogulisa chipani kumpasa obwera (mlendo) kumpatsa u president kodi nkatimwanu mulibe angaimire u president? Mene mwavutikira basi mukagulisa chipani iyo ndi trick
    Say NO to Kabambe (UTM presidency) pls