[Delayed Premier] Bon Kalindo - Dziko Lasokonekela Chifukwa Yona Anathawa Ku Nineve

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 11. 09. 2024
  • Ladies and Gentlemen, welcome back to Nyasa VoiceBox Today we have brought an Audio from One of our contributors here on Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo, Titled “Dziko Lisokonekela Chifukwa Yona Anathawa Ku Nineve”. In this audio Bon Kalindo touches on various topics and issues including but not limited to the ongoing corruption case against the Right Honorable Vice President of Malawi Saulos Klaus Chilima as well as the road to the 2025 general elections.
    Amayi ndi Amuna, talandiraninso ku Nyasa VoiceBox Lero tabweretsa Audio kuchokera kwa mmodzi wa omwe atithandizira pano pa Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo, Mutu wakuti “Dziko Lisokonekela Chifukwa Yona Anathawa Ku Nineve”. Mu audio iyi a Bon Kalindo akukamba nkhani zosiyanasiyana kuphatikizapo nkhani ya mulandu wa katangale omwe ukuchitika kwa wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko la Malawi a Saulos Klaus Chilima komanso za chisankho cha 2025.
    For Context Please refer to teh links below: | Kuti Mudziwe Zambiri Chonde Onana Ma Linki A M'muswa:
    malawi24.com/2...
    www.malawivoic....
    This audio was supposed to be released on Nyasa VoiceBox yesterdays but we. encountered technical difficulties that resulted in the delayed released of the audio clip on our channel. Thank you for your patience. We hope you will enjoy it.
    #malawi

Komentáře • 18