BON KALINDO LERO PA 16 JULY 2024 |

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 22. 08. 2024

Komentáře • 150

  • @user-lz4kc5ob1t
    @user-lz4kc5ob1t Před měsícem +2

    Ife tamupasa kale mai kaliyati president of utm

  • @user-ig9ip8jq7v
    @user-ig9ip8jq7v Před měsícem +1

    Watching from S A port Elizabeth timakunyadilani bwana pitilizani kuti imilira Mr Bon kalindo l Salute u bwana

  • @EnittaDavison
    @EnittaDavison Před měsícem +2

    Umatiymilra iweyo ulemu wako bon 🔥🔥🔥🔥👏👏👏👏👏👏

  • @justinmakiyi4189
    @justinmakiyi4189 Před měsícem +10

    As UTM and Malawi as whole country we are luck having this guy as somehow a prophet or advisor to the difference parties. The choice is in our hands to take the advise or leave them. But one day we shall remember Him. That's the free advise indeed. Regards

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před měsícem +6

    😅😅 zapana ndithu ndipo sanati and who is Manganya??? U don't know Bonnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri ndiponso mumumva, the DC mwana woyankhulira pa mchombo pa Malawi, alibe mantha ndipo saopa Unyolo kaya mfuti😅😅😅

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Před měsícem +5

    President wathu wathu amangoyima pachilungamo🎉

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Před měsícem

      @@Lazarus-qo1sl president wa zitsilu zokhazokha ndi mbuli zophumzila koma makolo awo fees anagowononga ngati mmene DPP inawonongera dzikoli

    • @VungaQueen
      @VungaQueen Před měsícem

      Mmmmmmmm inu Bon Kalindo musiye nde zitsilu tili ambili inu anthu abwino Kharani km siwani kt choyipa chitsata Mwini nadutsa sindinyoza ine

  • @christopherphiri8476
    @christopherphiri8476 Před měsícem +3

    Born kalindo will help UTM if anything engenge him to assist he is a man of action Christopher phiri from Zambia

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer Před měsícem +3

    DC born kalindo more fire 🎉

  • @SteveSamson-t9d
    @SteveSamson-t9d Před měsícem

    following kalindo Diiiiiìiiiiiiii siìiiiiiiiiiiii

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Před měsícem +3

    Awa ndiye amkamuna a UTM zili ndiinu kunyozera km Bon ndiye walangiza.

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Před měsícem +5

    The DC, Mr booooooon kalindo 🎉🎉🎉

  • @TooNajahInsideKoshah
    @TooNajahInsideKoshah Před měsícem

    Iwe ndiye president wathu wathu

  • @DalitsoTwalick
    @DalitsoTwalick Před měsícem +2

    Thanks my president for ur information

  • @user-yk5qd6sk8e
    @user-yk5qd6sk8e Před měsícem +2

    the dc 🎉🎉 mwana ooopsa kwambili

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Před měsícem +2

    Kodi a UTM mukuitana athu kwana chifukwa ninji Kodi menemo mulibeathu oti angayendese chipani ?bwinonazotu ndalama inampha mwanawamuthu zayekha ananyika sima m'mazi

  • @vincentkhunsanama584
    @vincentkhunsanama584 Před měsícem +2

    Yeah, the DC is not making mistake to advice the utm fam big up the DC

  • @JosephLemani-qq1is
    @JosephLemani-qq1is Před měsícem +3

    Mwayankhula bwino bon kalindo ena akufuna kugwetsa chipani cha UTM koma bola abwelele komwe anachokela

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Před měsícem +1

    Inetu ndimaganiza Kuti boni kalindo ndi mamuna koma ayi eti ndi wamkazi or kuganiza kwake ndimadabwa nako aaah lero ndamumvetsetsa ndi mkazi paja amavalaso ma browsers amamangaso tsitsi 😅😅😅😅😅 koma MCP yamulela bwinji because popanda MCP sibwenzi ali miss kalindo lero ayi akuyenera ponyoza MCP uku ndlama zikulowa kuchokera kwa anthu a ndale opposition 😅😅😅😅😅 uyithokoze MCP ukuchita bwino kwambili keep it up moto kuti buuu Satana akugwila ntchito yowatsogolela anthu ku moto ndi pakamwa kulankhula sosakondweretsa ambuye work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die

    • @JusticeNyirenda
      @JusticeNyirenda Před měsícem

      Thanks for the information about Jesus, but the rest is senseless

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Před měsícem

      @@JusticeNyirenda so it's better not to take part to these people we can die in sins we are in the last days all things must come to pass like economy James 5 the whole chapter famine, wars, disease all these they contribute financial crises all over the world Mathew 24 vs 5 to 8 then you will here about the national Sunday Law to combat all the crisses mentioned above by force in the name climate change and the pope will rule the world for 3 and half years but he will be overflow by all nations when they will see that no change but hypocrisy leading people to destruction and people will be against him work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die follow Jesus not politicians ndi abodza Ngati omwe akuchulikitsa machimo awo pa social media

  • @ElizaJames-by8ef
    @ElizaJames-by8ef Před měsícem +4

    African man ❤❤❤

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi Před měsícem

    Muzibwereza mau aoooooopsya kwambiri 😅😅😅 ndi iiiiiii

  • @KondwaniBilliat-t4g
    @KondwaniBilliat-t4g Před měsícem +1

    A DC tikupempha Mulungu wa kumwamba akupaseni moyo wautali ndi ntchito zanu zabwino pitilizani tilipambuyo panu nga!nga!nga!!!!!!!

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko Před měsícem

    Unayankhula zimenezo ,galu iwe!!!

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x Před měsícem +2

    Very sensible message bwana #DC♥️🔥🔥🔥

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Před měsícem +2

    Good advice Mr President

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Před měsícem +1

    The DC we are with you Mr president wa anthu osawuka ❤❤

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před měsícem +1

    Wolimbana ndi Boooo Kalindo oooo the DC atembenuke ndipo azilume kunsana more 🔥🔥🔥 Kalindooooo the DC 😅😅

  • @LuckyMhlanga-m1u
    @LuckyMhlanga-m1u Před měsícem

    Kalindo you are true

  • @HajjiSufiyani
    @HajjiSufiyani Před měsícem

    Pitilizani. Kutisogolela. Ndithu kuyakhula koveka bwana

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x Před měsícem

    Ndizona osangotenga zili zonse km a Malawi asanhhe

  • @user-wu8kp7ui5j
    @user-wu8kp7ui5j Před měsícem +3

    The DC 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @AliajoeAliajoe-vv1wo
    @AliajoeAliajoe-vv1wo Před měsícem

    Great man

  • @violetpotani
    @violetpotani Před měsícem

    Eeeish koma information mumayipeza 😅😅😅anthuwa bwenzi atangokhala coz akunyozeka

  • @Judah-zb6sl
    @Judah-zb6sl Před měsícem

    The DC ❤🎉🎉🎉🎉🎉

  • @ErickMambelera
    @ErickMambelera Před měsícem

    Umakwana kalindo

  • @WanangwaVwalika
    @WanangwaVwalika Před měsícem

    More fire!!

  • @eliaschinoko2086
    @eliaschinoko2086 Před měsícem

    The Dc Booooooooooooooooooooooooooooooooooon Kalindo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @OmrahGeraldOmrahGerald
    @OmrahGeraldOmrahGerald Před měsícem

    ❤❤❤❤ The DC kungalula

  • @davidmzee2205
    @davidmzee2205 Před měsícem

    Nde mwati Pepe Kale ?😂😂

  • @annamazingashaibuh6276
    @annamazingashaibuh6276 Před měsícem

    The DC kkkkkkkkk🔥🔥🔥🔥

  • @KingLunda-u1t
    @KingLunda-u1t Před měsícem

    Big man hooooooo

  • @Lemankais
    @Lemankais Před měsícem

    Bon ndi kampani simunthu wamba

  • @SteveZimba-e8s
    @SteveZimba-e8s Před měsícem

    Gwiritsani ntchito malangizo amene wakupatsani DC osazitaya muononga chipani chanu chabwino bwino

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb Před měsícem +1

    Ng''alula m'bale.

  • @user-oy6dl1pv9e
    @user-oy6dl1pv9e Před měsícem +1

    Following kwa Diiiiiiiiiiiisiiiiiiiiiiiiiiiiii

  • @SanidaChirwa
    @SanidaChirwa Před měsícem

    Ing'alilen fada ,osaopa ay Malawi ndiwathu uyu

  • @FelixKazembe-wi5zb
    @FelixKazembe-wi5zb Před měsícem

    Ndizosantheka kutuluka anthu onse chipani" choti mudziwe chipani cha UTM chamwazikana! Pepho langa ndiloti osalawo asachuluke zomwe zitapangise chipani kuchepa mphavu...manganizo anga.😢

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 Před měsícem

    Thanks for the advice Mr kalindo

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma Před měsícem

    Akunamizana kwambili athu amenewa mcp ikutula udindo pasi

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v Před měsícem

    Utm samalani ndi kabambe ndi brocko yati musabwerere Ku DPP matchera chenjerani mafana

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Před měsícem +11

    The DC 🎉🎉🎉🎉🎉

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Před měsícem

    Ur right the DC akapusa kulowa mikangano

  • @user-sk3ld2ss7s
    @user-sk3ld2ss7s Před měsícem

    Boni kalindo ndi chilata chopanda kanthu, chomangosokosera...

  • @Maliko-bp1xn
    @Maliko-bp1xn Před měsícem

    Mukulankhula zooonadi

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Před měsícem +1

    Ndinzoonadi asangotora munthu

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Před měsícem

    The DC mwana wowopsya kwambiri Bon kalindo

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 Před měsícem

    The DC mnyamata oopya kwambiri 😅😅

  • @EmmanuelMalata-r4j
    @EmmanuelMalata-r4j Před měsícem

    Mumatiyimilira bwana❤

  • @YolliyajeerasYeeras
    @YolliyajeerasYeeras Před měsícem

    Mwana ooooooooooopsa kwambili

  • @RuthMoto
    @RuthMoto Před měsícem

    Mukhalise comrade Bon kalindo

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před měsícem +2

    Amp alibe nawe nthito kambwe iwe chisilu

  • @user-pb6wb3iz7z
    @user-pb6wb3iz7z Před měsícem

    Well narrated

  • @BrightNkhoma-xz4bg
    @BrightNkhoma-xz4bg Před měsícem

    Athu opusa kwambiiri akuona ngat tikugona......... Our president Bon Kalindo 🇲🇼🇲🇼🇲🇼 😂😂😂😂 pepekale

  • @user-mk4ju6iw7c
    @user-mk4ju6iw7c Před měsícem +1

    Mwathandidxa akafunakunyodxela anyodxele okha

  • @SHABBASELEMANI-o8d
    @SHABBASELEMANI-o8d Před měsícem

    Ati PEPE KALE... koma DC

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma Před měsícem

    We folow

  • @jacksonmaster2288
    @jacksonmaster2288 Před měsícem

    Kalindo UTM amaikonda kwambili

  • @EstherBailoni
    @EstherBailoni Před měsícem

    DC , tiye Nazo usaope

  • @DICODIDICODI
    @DICODIDICODI Před měsícem

    No☝️THE DC

  • @richardjumah198
    @richardjumah198 Před měsícem

    UTM malangizo a ulele awa please

  • @user-rr7je1zi8t
    @user-rr7je1zi8t Před měsícem

    Kuti nkhaaaa wabwela bon kalindo

  • @KondwaniBilliat-t4g
    @KondwaniBilliat-t4g Před měsícem

    Backward never forward ever ❤

  • @PeterNamphwanya
    @PeterNamphwanya Před měsícem

    Chi booooon kalindooooooo🎉🎉🎉🎉🎉

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo Před měsícem

    The DC

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Před měsícem

    Sakumudziwa Boooon Kaliindo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před měsícem

    Bola mwachenjez ali ndi khutu ambve

  • @Momweekly
    @Momweekly Před měsícem

    Well spoken

  • @MecyMalothi
    @MecyMalothi Před měsícem

    The D C our pangolin

  • @jumahgeorge
    @jumahgeorge Před měsícem

    Following

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon Před měsícem

    Born kalindo the deceeee

  • @user-rr5nq2uo6i
    @user-rr5nq2uo6i Před měsícem

    Big up the DC

  • @AnyumbaJulias
    @AnyumbaJulias Před měsícem

    Ulemu wako iweyo bon kalindo

  • @user-zl5wv8ix8u
    @user-zl5wv8ix8u Před měsícem

    Kalindoo akunena dzoona

  • @jumahgeorge
    @jumahgeorge Před měsícem

    The DC more 🔥

  • @JohnWindford-jv8ls
    @JohnWindford-jv8ls Před měsícem

    Kma azipumako Tizimvako zina.

  • @marcelolemos1484
    @marcelolemos1484 Před měsícem

    THE DC

  • @ClementJosephy
    @ClementJosephy Před měsícem

    Inuyo munavaya patali ana achepa,... Eeeeee

  • @BrightonKamwendo-db1ci
    @BrightonKamwendo-db1ci Před měsícem

    Mau onveka zeeed mbuyanga

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev Před měsícem

    Kabambe simunthu ..

  • @MaxwellKananji-r5d
    @MaxwellKananji-r5d Před měsícem

    Makamaka pamene wanena kut pakufunika mery chilima amutenge kut agwile naye ntchito pamenepo Mr DC mwanena zoona ndipo mzimu wa SKC utha kuusa mumtendele

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Před měsícem

      Chifukwa chamkazi wakeyo?
      Mukunama ....za Mulungu amaweruza yekha ndipo sapanga pangano ndimunthu...Za dziko lapansi musaphatikize Mulungu

    • @FelixKazembe-wi5zb
      @FelixKazembe-wi5zb Před měsícem

      Ndichaka amalawi dale zimativuta chifukwa mumafuna anthu omwewo azipanga dale. banja lonse abambo akakhala president mwanaso akufunaso wu president omweyo ayi😂😂😂😂 dale sichoncho.

  • @user-hq6dq7zr1e
    @user-hq6dq7zr1e Před měsícem

    Auzeni a utm azinyozela wokha

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah Před měsícem

    We follow

  • @lydiagadama4887
    @lydiagadama4887 Před měsícem

    The Dc

  • @YusufIbrahim-w1g
    @YusufIbrahim-w1g Před měsícem

    Boooon kalindo is not sepro man is big man chizulo chat ambawi Allah bless him

  • @RhodaNombo
    @RhodaNombo Před měsícem

    Mmatiimilila the dç

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar7468 Před měsícem

    Aaaaaaaaaa awa amaopa manganya ndamzawo

    • @Raph-kayRaph-kay-g5v
      @Raph-kayRaph-kay-g5v Před měsícem

      Manganya nkanyama kanji? Phwala lako wamva

    • @oskidooscar7468
      @oskidooscar7468 Před měsícem

      @@Raph-kayRaph-kay-g5v manganya olo nda bambo ako angafanane iwenso chisilu et
      Manganya is a vp of malawi
      You like it or not

  • @TemwaKabisa
    @TemwaKabisa Před měsícem

    The DC 🎉🎉🎉🎉🎉❤❤

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn Před měsícem

    Pepekale ameneyo wakumalawi?kapenawaku ithiopia

  • @JosephyMagombo-t7d
    @JosephyMagombo-t7d Před měsícem

    The DC ✊️

  • @stormchatepa134
    @stormchatepa134 Před měsícem

    bwana nyo

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 Před měsícem

    ❤❤❤