CRUISE 5 WITH GEORGE THINDWA

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 15. 07. 2019
  • George Thindwa is a curious man. He is the Executive Director of the Association for Secular Humanism in Malawi and a confessed atheist. He says he has not set his foot in church, and doesn't see any need to. He does not believe in the existence of God or even the Devil. He is a well-accomplished Economist and once headed the Economics Association of Malawi - ECAMA.
    Follow this program and hear more about his background, family and his arguments on how he thinks the world came into being.

Komentáře • 75

  • @mosessemuh9681
    @mosessemuh9681 Před 16 dny +1

    Nthidwa ndi Genious, His brain is superpower.....! You're not alone Mr.

  • @blessingsnkhwazi273
    @blessingsnkhwazi273 Před 5 lety +10

    Well educated man koma omvetsa chison eeeeeee ayi, anthu anga akuonongeka chifukwa cha kusadziwa.

  • @ThumbikoChipofya-gq7sd
    @ThumbikoChipofya-gq7sd Před rokem +3

    Ndiyambe ndikuthokoza aChakhaza pocheza ndi mkuluyu, poyamba background yake ( childhood development ) Ku mbali ya chipempedzo sinali bwino .Chinanso nchakut sakufunika kumuweruza koma kumupemphelera kuti apulumutsidwe ndi Ambuye Yesu khristu pot malemba akut mu nthawi yakusadziwa Mulungu analekelera ,nkhan siyongopita Ku mpingo koma kumdziwa womtumikira monga zinachitikira pa machitidwe atumwi9 ( nkhan ya mayitanidwe amtumwi Paulo).Kuonjezera apo Mr Thindwa choti mudziwenso nchakuti maphunziro ngakhale Ali ofunika simayankho amavuto onse amoyo uno ndikupatsani chitsanzo cha nkhani ya m' bible mu buku LA machitdwe atumwi chapter16:16-40 pa nkhani yomwe anamangitsa Paulo ndi Sila.Mutha kuona kut chayambi cha matenda awobwebwetuka uja monga luka ( wolemba bukuli) akufotokozera sichimene adotolo amatenda amisala angafotokoze .Akatswiri azachuma sangafotokozenso out chinsinsi cha kuchita bwino kwa omwe amapindula ndi zimezi ndi chiyan? Komanso gwero lakuvutika kwa wodwala uja? Palinso nkhani zawomenyera ufulu anthu kuyambira wodwalayo,Atumwi aja ngakhale amene anabesa chuma chawo kudzera mzomwe zimachitikazi palibe chomwe angachite munyengo ngati izi.Akupatsan funso mwadwala chipatala chalephera wina atakupempheleran nkuchira mu dzina LA Yesu Khristu mwayankha mododomatu? Mwinanso titakamba za Vuto la uhule anthu alangizidwa kuyipa kwa vutoli kupasidwa ndalama out apeze zochita koma osasintha enanso ndalamazo nkukhala Nazi koma osasintha Alonso ophunzira taonani pano Dziko likupereka ufulu kwa achinyamata kutenga njira zolera chikhalirecho zambiri sizawateteza kumatenda opatsirananapogonan KO'd akuchuluka otenga matendawa mdzina LA ufulu tinene kut zikuyenda ?mutha kuona kut Chifukwa chakuti chiwanda chili mkat mwa munthu uja sichinachotsedwe vuto lizingozungulira Muli ndi maphunziro abwino pezan zochita zabwino moyo wanu uli mdzanja la Yehova yang'aniran mathero ake Hebrews9:27 komanso Ku Genesis 3 akut unapangidwa Ku nthaka komwekonso udzabwelera bwanji maphunziro alibe yankho Ku vuto la imfa? Ndibwelenso Ku machitidwe 16 chimene chinapangitsa Paulo kuzindikira gwero la vuto lija ndiye mphamvu ya mzimu woyera( Mzimu wa chidziwitso ) Yemwe mungampeze mutalapa ndikuvomereza Khristu Yesu ngat mpulumutsi wa moyo wanu ( machitidwe2:38) nkhoswe imene Ambuye Yesu anawauza ophunzira akekudzawatumizira ndikuwatsogolera mu choonadi komanso kuvumbulutsa zinsinsi zochekera kwa Mulungu kudzera mwa mwana wake Yesu Khristu.Chiuta wawe namwe zuwa liweme.

  • @martiusgeorge6514
    @martiusgeorge6514 Před 5 lety +6

    Powerful God always with him that's why he like Rabecca Malope songs because in doing that he is praying

    • @andreamillar9896
      @andreamillar9896 Před 5 lety +1

      Kuyipa kwa Makolo athu potsatengera Ana athu ku Church ndizimenezo a Bambo awu Satanic. Teach a child to know God while he is still young.

  • @alfredkhogolo1715
    @alfredkhogolo1715 Před 16 dny +1

    These are nothing but the facts

  • @mayababy1877
    @mayababy1877 Před 5 lety +6

    Uphawi umapangitsa uchimo.izi akupanga pofuna ndalama.the songs he likes are highly spiritual. God loves you mumbuli wanuwo

  • @SimeonKamwana
    @SimeonKamwana Před 10 dny

    Kodi National Anthem ija amayimba nawo kapena amaiwona kuti ndiyolakwika?

  • @kunsichilazarus9212
    @kunsichilazarus9212 Před 5 lety +2

    And chimene chidakusangalatsani kuti muzikonda nyimbo za Rabecca ndi umulunguwo please musabisale bambo

  • @aishachisale4267
    @aishachisale4267 Před 3 lety +1

    Koma zikomo🙌🙌 eeee

  • @aishachisale4267
    @aishachisale4267 Před 3 lety +2

    Akuluwa a Eliya aposatu😆😆

  • @blessingskakusa7836
    @blessingskakusa7836 Před 10 měsíci

    Long live George

  • @glorydelezah9629
    @glorydelezah9629 Před 5 lety +2

    Thanks for the enlightenment, this is absolutely awesome

  • @Omwale
    @Omwale Před 13 dny

    this guy

  • @gloriakamanga7329
    @gloriakamanga7329 Před 5 lety

    A Thindwa Rabecca amaimba gospel nde mumapempheranso.

  • @joelmkandawire954
    @joelmkandawire954 Před 5 lety +9

    That is according to him, (he doesn't believe in God) not you and me, so leave him alone. It's not up to us to judge him.

  • @edwardbanda5469
    @edwardbanda5469 Před 5 lety +5

    God is calling him, that is why he loves Rabecca malope. God Himself will make way to bring this man to Himself. He is God of mercy.

  • @stephenlupanga1970
    @stephenlupanga1970 Před 5 lety +1

    Joab ndi #1 kkkkk wampanikizatu munthuyu

  • @kassimjuma8822
    @kassimjuma8822 Před 3 lety +1

    Dzimene mukuyankhula madala ndizopanda nzelu

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před 4 lety +1

    Titha kuphunzira kwambiri koma nkukhalabe opanda nzeru ngati akuluwa, ndi Mulungu Amene amapereka mphepoyo kutidziwitsa kuti mmadzi simuli bwino ndiye wina kupanga ignore that plain warning.

  • @kingstonchawinga3869
    @kingstonchawinga3869 Před 5 lety +2

    Eiiiish ambuye akukhululukireni

  • @DivineSyntaxMw
    @DivineSyntaxMw Před 2 lety +1

    Ati Mulungu kulibe, kuyankhula kwa zitsiru.😏

  • @nchessie
    @nchessie Před 4 lety

    Adzakumane ndi wa njoka ujaface to face adzakambilane bwino

  • @DennnisGogoda
    @DennnisGogoda Před 6 měsíci

    Bible limati, “ Chisilu chimati kulibe Mulungu “ I guess the man so just so ……Let me save my word.

  • @redsonrichard1364
    @redsonrichard1364 Před 15 dny

    Nanu munyanya mwakumana ndi wen wen Satanists

  • @christopherchimbetete2196

    Chamba

  • @aubreywallo1987
    @aubreywallo1987 Před 5 lety +2

    God forgive him!

  • @chesterphiri7523
    @chesterphiri7523 Před 5 lety +1

    Poor soul, just being intelligent as he is explaining it's God's blessing.

  • @johnsong2118
    @johnsong2118 Před 5 lety

    komadi madala awa sangangokhalakhala,akuyenela amadya chamba

  • @ellenfumuyiliko1390
    @ellenfumuyiliko1390 Před rokem

    Bola a Eliya aja amadziwa kuti Mulungu aliko osati phwephwa izi

  • @Chikomukomu
    @Chikomukomu Před 5 lety +1

    All am seeing is confusion from this guy. He was contradicting himself during the chat

  • @joechimba742
    @joechimba742 Před 2 lety

    Inde mdala

  • @user-hc6rc7yr8y
    @user-hc6rc7yr8y Před 25 dny

    Satana uja ndamuona ndi maso lero😮

  • @frankmaluwa2749
    @frankmaluwa2749 Před 5 lety

    Humble man friendly person, I'm very sorry for that papa about being arrested for the mcp government by Dr Banda

  • @kassimjuma8822
    @kassimjuma8822 Před 3 lety +1

    Mulungu adzikukhululukilani madala

  • @geee7672
    @geee7672 Před 5 lety

    But Rebecca Malope is a Gospel artist

    • @ralphhenderson5312
      @ralphhenderson5312 Před 5 lety +1

      Nchifukwa chake tikuti ndimbuli sakudziwa chomwe akupanga Mulungu amukhudze

  • @yankhomtonga6325
    @yankhomtonga6325 Před 5 lety +3

    Looking at the comments it clearly shows how ignorant the so called christians are: Calling the non believer osazindikira. you guys need enlightment for sure dont just believe for the sake of believing

    • @georgesiwale8127
      @georgesiwale8127 Před 17 dny

      Yes, I am wondering too. We need to wise up

    • @simonabraham7241
      @simonabraham7241 Před 17 dny

      For sure, these so-called christians are something else 😂😂😂

  • @CatherinePhiri-bw7wm
    @CatherinePhiri-bw7wm Před 16 dny

    Bible linanenakale kuti the fool say there is no God, ndiye mukamawona anthu atelewa wosamadwabwayi p

  • @duncanchizizi6543
    @duncanchizizi6543 Před 3 lety

    Kkkkkkkkkkkkkk

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g Před 16 dny

    Drange kwambir kapen fodya
    Wa chamba😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @medsonboti1984
    @medsonboti1984 Před 4 lety +3

    The holy spirit gives one the ability to sense the presence of God. If the spirit is not in you then there is no sense.

    • @youmad9087
      @youmad9087 Před 3 lety

      What spirit is that?

    • @aminbwanali3954
      @aminbwanali3954 Před 2 lety

      This man is the brother of falawo he deserved to be panished

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před 4 lety +3

    Ndi omvetsa chisoni, infact he is worse than the devil himself. The devil doesn't dispute the existence of God, according to the book of Isaiah and Ezekiel, the devil wants to be like God the most high. This old man is totally out of his mind.

  • @peterbanda5425
    @peterbanda5425 Před 5 lety +1

    Akuluwa mutu ukugwila koma

  • @basharkhan8933
    @basharkhan8933 Před 5 lety

    Ngati chili chamba chikugwira ntchito

  • @rashidjackson7085
    @rashidjackson7085 Před 3 lety

    Mkuluyu wangokura koma nzeru mulibemo. Google mwini wache ndi muthu osati mulungu ndipo nthawi zina siigwira network

  • @manzykawika8988
    @manzykawika8988 Před 5 lety +1

    Muziwerenga Bible Mr thindwa

    • @apatsamuula4676
      @apatsamuula4676 Před 2 lety

      Alibe thawi yowerenga bake akuyakhula xoduka mutu

  • @mussahswallehchimisa5348
    @mussahswallehchimisa5348 Před 5 lety +1

    koma abale mmmmm zodabwisa kwabasi munthu wankulu ngati ameneyu?? 😯😯😯

  • @weruzanicustom4954
    @weruzanicustom4954 Před 2 lety

    This atheist akungofunika maumboni amachilitso. Funso lakuchipatala lamuyimitsa mutu mpaka wavomera kuti akhoza kukhulupilira kkkkkkkkkkkkkk

  • @kunsichilazarus9212
    @kunsichilazarus9212 Před 5 lety

    Kkkkkkkk koma Joab umakumana nazo inetu abambo awo komwe akulowa sindikudziwako.

  • @ellengwazanga6350
    @ellengwazanga6350 Před 5 lety

    Bambowa ndi chiwanda, akufunika mapephero.

  • @ndipo1
    @ndipo1 Před 5 lety +2

    aaaah kumvets chisoni you dont believe in God- you missing out on a lot hey.

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před 4 lety +1

    According to the Bible Mr. George Thindwa ndi achitsiru, that's it and i can prove it and he has proven it himself kuti, he is a fool.

  • @ellenfumuyiliko1390
    @ellenfumuyiliko1390 Před rokem

    Anangokula nzeru alibe🚮