BAMBO NDI MWANA APHEDWA NDI ANTHU POWAGINIZILA KUTI NDI FITI By gova

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 5. 09. 2024

Komentáře • 59

  • @Liki-Likiladies
    @Liki-Likiladies Před rokem +7

    Zinazi pena umazaona ngati ukulotatu....tisamatengere malamuro mmanja mwathu chonde government must wake up and shield her innocent souls.

  • @TiagoManuelBanhaBanha
    @TiagoManuelBanhaBanha Před měsícem +1

    Heee angonia é outro nível 😢😢

  • @joegibsonzulu2599
    @joegibsonzulu2599 Před rokem +5

    Nkhani yoziziritsa nkhongono. Zambirizi zikuchitika chifukwa cha mangawa,umbuli ndinso kaduka. Izi zipangitsa kuti anthu adzingophana ngati nkhuku chifukwa cha nkhani ngati zimenezi.

  • @josuahkachali1489
    @josuahkachali1489 Před rokem +2

    Very sad watching live from Kuwait

  • @jvpondan4332
    @jvpondan4332 Před rokem +3

    😭😭😭😭😭komatu sibwino abale tapempherani iiii

  • @osamabinraden9391
    @osamabinraden9391 Před rokem +1

    Keep up bansosamana👏👍

  • @sergiopauloposse7610
    @sergiopauloposse7610 Před rokem +1

    Balanço Semanal está melhorando cada vez muito mais obrigado pela informação. E muito triste.

  • @austinvincent773
    @austinvincent773 Před rokem +2

    Proud of you barancol

  • @mavuschitseko7757
    @mavuschitseko7757 Před rokem +3

    Mmmmmm tili mmatsiku otsiliza zedi😭

  • @RuthMvula-kq2dd
    @RuthMvula-kq2dd Před rokem +2

    Ambuye atithandize

  • @EdwardGeorgeKasabola
    @EdwardGeorgeKasabola Před 7 dny +1

    Koma zosayenda

  • @pililanibuliyani7684
    @pililanibuliyani7684 Před rokem +1

    Za ufiti ziripo koma sibwino kutengela malamulo manja mwako boma lirowelerepo zikomo Agova

  • @promise3693
    @promise3693 Před rokem +1

    Anthuwo akanadikira ndipo choonadi chilamaululika ... ndiye iwowo apha ndiye wakufa winayo apezeka bwanji

  • @ririvilla1423
    @ririvilla1423 Před rokem +2

    Apolisi sakugwila ntchito yawo anthu apha anthuwa aphedwenso

  • @martaarauio1347
    @martaarauio1347 Před rokem +2

    Afela zawo amenewo kumoto Basi

  • @halimahussein6571
    @halimahussein6571 Před rokem +1

    Chilungamo ndichakuti anthu aku Mozambique sagawa kamba ndi ankhadza nkhondo yinawalowa mmitima

  • @lazarusziyaya3997
    @lazarusziyaya3997 Před rokem +1

    Kodi ku Mozambique malamulo a ufiti amati bwanji ?

  • @frankmaluwa5120
    @frankmaluwa5120 Před rokem +1

    Aaaaaaa this is out of hand now ngati zinthu zikutere tsopano ndiye Kuti apolice kapena Kuti achitetedzo sakugwira ntchito yawo, Koma zikomo kwambiri Inu anyamata a balaco semanao mukugwira ntchito yotamandika

  • @louiskk100
    @louiskk100 Před rokem +2

    Umbuli wachuluka...Mukatero muyambe kumenyana,nkhondo sinakukwaneni eti?

  • @lucysimbani3971
    @lucysimbani3971 Před rokem +1

    Zosayenda ayi anakangowamenya mkuwasiya mwina osati kumphelatu ayi mwina akanasiya ufitiwo

  • @rabeccagama4067
    @rabeccagama4067 Před rokem +1

    Boma linayenera kutengapo gawo sizoona amalawi umunthu tinausiya kuti Nkhani zogopeka plus maudani aaaaaa amalawi pliz tiyeni tikondane ndithu komaso pena zimaonesa umbuli nanga mene awaphamo chisithe chani mudzimo maliro asiya kumwalira ana awo a malemu mwapasa picture yotani nakakonda atamagidwa anthu amenewa aaaaa munthu kumumpha ngati galu

  • @aleksawilliams710
    @aleksawilliams710 Před rokem +1

    🤔🤔Mozambique nkhani izi zikuchulukiratu

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Před rokem +3

    This is completely out of ignorance , civic education is greatly needed in these areas . Innocent souls are being killed.

  • @HarryUmarih
    @HarryUmarih Před rokem +1

    Mumakwana

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Před rokem +2

    Nsanje and kaduka

  • @chifunirogoliat4630
    @chifunirogoliat4630 Před rokem

    Sopano ngat mukut ufit kulibe mfiti zina zimafika poulura kunena zokha kut zimatamba ndikupha anthu muufiti..zimakhala kut ndichan

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Před rokem

    Umbuli akapolo umphawi Majerouse
    Sukulu ndiyofunika. Kupha anthu ngat nkhuku akapolo otembereredwa...

  • @fatimahluis6450
    @fatimahluis6450 Před rokem +1

    Koma kumeneko mkuti

  • @MarcelinoManquena-ws8nd
    @MarcelinoManquena-ws8nd Před rokem +1

    Oooo pepani kwambili

  • @majendauzananilimitedi2049

    Pitilizani kumatipatsa actualizações ❤

  • @user-qs2do1jc3f
    @user-qs2do1jc3f Před 7 měsíci +1

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @JosephBanda-fl5ss
    @JosephBanda-fl5ss Před rokem +1

    Please pitiliza ni kutipasila

  • @iangama35
    @iangama35 Před rokem +1

    enanu mukut zalakwika km muzazindikila ufitiwo mukazakumana nawo.....ufiti ulipo guys wake up.......ine ndalhulupilira nkhaniyi...

  • @user-rs9fx5uj7z
    @user-rs9fx5uj7z Před rokem

    Anakumana ndi zukwa

  • @peterbanda7003
    @peterbanda7003 Před rokem +2

    School anthu awa ikufunika kwambili

  • @aliciabanda3656
    @aliciabanda3656 Před rokem +1

    Mmmmm koma abare inu sambi

  • @lydiaamos4214
    @lydiaamos4214 Před rokem +1

    Danger in the Last days

  • @bonifaciosimao8620
    @bonifaciosimao8620 Před rokem +1

    Zovetsa chisoni kwambiri 🥲

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 Před rokem +1

    Komano afiti awonjeza serious anthu amafika potopa abale osati anthuwa olakwa chifukwa even ukapita ku police uva zilibe umboni ndiye anthu atani kutopa ngati amfumu akuyankhula chocho afiti polani moto chifukwa anthu atopa

  • @jazakalemani3127
    @jazakalemani3127 Před rokem +1

    A balaco mwasowatu bwanji mwasiya kutipasira nkhani?

  • @jvpondan4332
    @jvpondan4332 Před rokem +1

    Komatu ndikanakonda ndikadakhala mudzi umenewu

  • @sulaimanabanda9605
    @sulaimanabanda9605 Před rokem +1

    Apolsi akulephera ntchito yawo

  • @jvpondan4332
    @jvpondan4332 Před rokem +1

    Koma simukufunikira mudziranga anzanu choncho

  • @promixphotography8056

    Ndikuti uku mwati

  • @mariamhalid9185
    @mariamhalid9185 Před rokem +1

    Eeeee abale ndi chian kwenikwen...tili mmasiku omaliza

  • @marianyirenda
    @marianyirenda Před rokem +1

    This area is too much primitive ,these people they must go to school they are still living old fashion ways they believe in witchcraft

  • @miloslundu6366
    @miloslundu6366 Před rokem +1

    a police sanathandize sanapeleke mau oteteza banjali

  • @zainabchikakuda6297
    @zainabchikakuda6297 Před rokem +1

    Boma lichitepo kanthu anthu tikutha ,

  • @victorbanda7546
    @victorbanda7546 Před rokem +1

    This is very bad izi ndi nkhani zopanda umboni kodi munthu wakufa amalakhula?apa mwapha anthu osalakwa kunali bwanji kuwatengera ku police kusiyana ndikuwapanga khaza ngati zimenezi,boma likuyenera kuchitapo kanthu

  • @armandojohn7641
    @armandojohn7641 Před rokem +1

    ,,,,

  • @dakasaul3111
    @dakasaul3111 Před rokem +1

    Mmmmmmmm mavuto aakulu zedi zikomo balaçio