Why Are police exposing the details now while the other group is not arrested? You are still investigating the matter and revealing updates just gives a chance to the other criminals Amos committed all the crimes with. You have given the chance for other robbers and nurderes to escape justice.
Zaboza inu ogwidwa agwidwabe though ayankhulapo and they’re not going in deep details zoyakhula zinalipo lkale how come they catch the dude? Mufuna Muzise ntchito a police 😅😅
Koma MALAWI 🇲🇼 POLICE MWAYIGWIRA NTCHITO. ❤❤❤❤❤❤
Why Are police exposing the details now while the other group is not arrested? You are still investigating the matter and revealing updates just gives a chance to the other criminals Amos committed all the crimes with. You have given the chance for other robbers and nurderes to escape justice.
Uyu nayeso aphedwe chimunthu chopanda nzeru zoona kupha mubale wako yemwe amakudyesa😢
Good job keep it up
Police you have been fast to talk to the public before arresting the others...you have made them run now.
Zaboza inu ogwidwa agwidwabe though ayankhulapo and they’re not going in deep details zoyakhula zinalipo lkale how come they catch the dude? Mufuna Muzise ntchito a police 😅😅
They know their job, if they have managed to find the lead they have already cracked the case.
4:36
Mmmh koma abale...your own blood
Good job
Mapazianu apolisi mukulephela kumanga anthu amene akuphesa amalawi ambiri Pano zakubuchala zilipati zakufamase zilipati zawitika zilipati lelo mwabwela poyela chifukwa Choti ndimphawi uyu mukunena Kuti simumauzidwa inu apolisi zonse zakufamase kubuchala Moti simukuziwapo khanthu site ana tsiku likubwela muzanena nokha tisanakufunseni mafunso
Uyuso aphedwe bas palibe kuchitila mwina ai ⚔️🗡️⚒️🧷🔪🐯🐆🐅🪱🦂
Congratulation Lilongwe police
Allan witika ndiye zili pat
Kodi za Njaunju zinathela pati?
Ndipo Inenso ndikadakonda nditadziwa.
Kenako tidzamva zoti wafera mu cell
Ampanga xinthu kubisa zinaxi
Kuthamangatu kumuonesa koma akapezeka wagulu la apolice azanu mubisa agalu inu mmmm
tikufuna detailed report ya Witika
Apolice athu simumachedwa kumpeza munthu aka thawa .koma mulibe chilungamo mumamtayanso after mutadya mabanzi
Nkuthekanso kuti mwina waulura kale Amosiyo Koma mwina ndiodziwika Akulephera kumubweretsa poyera
This boy Amos Is dangerous, having a sister and living with his sister for free food and secured free
Mmmm koma anaganiza bwanji uyu
Mukamaliza mlandu umenewu mumtengenso Soulosi Chilima wa ku maulanso naye
Kod mulandu wa Witika uli pat? Pot uyo sali m'boma ndy kuthamangatu kumuyalutsa eee koma apolice mmmm chinyengo
Ndipo tikudikila kuti timve watching from Lesotho
Mnyamata oyipa
We need cctv
Mtolakhani usamangoti "mlongo wawo" use also brother wa omwalirayo chichewa Cha mlongo wawo sichigwiritsidwa ntchito dziko lonse
Inu anatumidwa ndi andale ameneyo
Koma ngakhale amupeza Amos'yo amufunse bwino bwino chifukwa nkutheka alipo anamutuma
Andale anazela mwa iye
Ndipo mukunena zoona
Iiiii chimunthu chikulukulucho kumasungidwa mmmmm ndekutidi chinali chigawega kwao anachilemphera mchobvuta iiiiii koma mpaka kupha mlongo wake eeeeee
Palibeso zoti uyuyu ndi mlongo wawo ayi afunika akaphedwe
Sikusinja uyu amphedwe
Eeeeeeee 🙆🙆🙆🙆
Mu2 oipa kwambri olo umunthu osampeza
Eeeee
Km galu iwe kupha mulongo wako food for free
Anamuphelanji
sad news😡
Khondo ndanasi amakupha ndi wako
Ndipo iih chibale chinaopsya
Km zoti ndichibale ai ndithu muthu oipa uyu
Good job