LIMPOPO FM WITH COMRADE NTANYIWA USIKU wathawu

Sdílet
Vložit

Komentáře • 83

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Před 22 dny +3

    Mr Chikangawa Chakwera Bp yakwera kale kuti muulura chani 😅😅😅😂😂😂😂yomweyo galu iwe

  • @MikeKanyaza-bm5tp
    @MikeKanyaza-bm5tp Před 22 dny +3

    Osamasowa antanyiwa please 😊

  • @JosephHill-fy1bb
    @JosephHill-fy1bb Před 22 dny +6

    We are here already comrade ✌️

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm Před 22 dny

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Před 22 dny +1

    ose amene ankufunna kuphedwa mulungu salolla mashall Allah bless you always

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli Před 19 dny +1

    Loud n clear from Johannesburg

  • @meganabigail-ye7fw
    @meganabigail-ye7fw Před 22 dny +1

    Sitiopa wokupha thupi koma timaopa mulungu amene amapha thupi ndi mzimu.
    Ondikumbila dzenje agwelamo yekha.
    Mulungu wa Daniel, shadreck, mishel and abdenego will protect onse amene mayina awo Ali pa list.

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Před 22 dny +1

    Good morning, welcome back tinakusowani tinayamba kudandaura

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Před 22 dny

    The best Radio station in the world. Big up Comrade

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana Před 22 dny +3

    Koma ndaseka ngati zabwino 😂😂😂 athu onsewo akaphedwa nde iwo adzawina zisakho Kom hahahaaaaa chakwera akunama kwambiri kumwamba kukanena kuti kwatha ndi kwatha basi paribeso zoti apha muthu wina a ntanyiwa dzikoli silachakwera ndalama sizingamupindulire komaso paribe zoti anga gure chipani paribe yemwe afuna achoke komaso akaliyati sangalore mudzina layesu ndikuti patibe zoti muthu anga gure chipani awo akalandira ndalama ndizawo za kunyumba kwao and olo apatse ndalama kakiyati olo adzalandira koma chilungamo chisitha chimakhalabe chilungamo ndinaonera esau ndi abere choipa chitsata mwini MLUNGU WATHU SALEPHERA

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl Před 22 dny +2

    Ndikamava kanyimboko ndiye ndimasangarara ndimazdziwa kuti chirungamo chirimunjira

  • @DaitonKabila
    @DaitonKabila Před 22 dny

    Comrade am 100% support u always ing'alure fadah

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 Před 22 dny +1

    I ❤ this program

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o Před 22 dny

    I salute Comrade ntanyiwa,, ndiye titani Comrade amalawi tiyen titengen gawo tipemphere kwambiri

  • @AnusaNkhoma
    @AnusaNkhoma Před 22 dny +1

    Waying'alura kuno mtanyiwa

  • @VaseleMsiska
    @VaseleMsiska Před 22 dny +2

    Koma kukhala anthu Ku Malawi. Koma chakwelà azatha ngati ma curtain.

  • @modestamhango7737
    @modestamhango7737 Před 22 dny +1

    Angozinamiza anthu onsewa Mulungu sangalore kuti aphedwe.

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Před 22 dny +1

    Ntanyiwa wadzuka bwanji kumeneko ifetu tilibwino ndithu tiye nazoni

  • @AbdullahBnp-l8m
    @AbdullahBnp-l8m Před 22 dny

    long live Mtanyiwa here in capetown i support you❤

  • @SydneySibande-z6k
    @SydneySibande-z6k Před 22 dny +1

    Long liveNtanyiwa

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o Před 22 dny +1

    Muzina la yesu christu achakwera kungopha modzi muziona ndithuuu😭😭😭😭

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg Před 22 dny

    Oh Lord have mercy on us Malawians
    Tipulumutseni ambuyeeeee ............Mbuzi ikakondwa kwambiriiii amalonda alipafupi la 40 likudzaaaaaaaa list mwayikayo ikhala yanuuuuu anthu akupha amagazi m'manja inu

  • @user-pl2lj6mh1z
    @user-pl2lj6mh1z Před 22 dny +1

    Koma dziko lathu tinalozedwa bas zoona kumuopa chakwela kamuthu kamodzi tiyen tipange ngat ku Kenya please zausilu zikuchitikazi

  • @JamesDaud-jz7uq
    @JamesDaud-jz7uq Před 22 dny

    You are our head lamp Mr Mntanyinya tipempha mayiko ena atithandize kuchotsa president okuphayu

  • @user-ht7vs3dp2u
    @user-ht7vs3dp2u Před 22 dny +1

    Pemphelo rathu ndichida chomwe timangonjesera adani zenje akuwakumbira athu onseo agweramo onse akupereka mayina awathu osarakwa imfa akunenayo atamwalire ndiwo 2025 isanafike mulungu akuona

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 Před 22 dny +1

    Lord have Mercy

  • @louismagongwa
    @louismagongwa Před 22 dny +2

    😂😂😂😂😂 nde mcp itsala yokhatu nanga anthu osewo akawapha ku opposition kudzakhala ndan mcp muzitenge bwino zithuzi vuto mwakhalitsa padzuwa muli kotsutsa😅😅😅😅😅😅😅😅

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 Před 22 dny +1

    Atchela kumawa nkhangazaona anyanayo

  • @user-iv4dj1pi3b
    @user-iv4dj1pi3b Před 22 dny

    Comrade ntanyiwa ..great man ft kalindooooo

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x Před 22 dny

    We're always with you buddy Ntanyiwa.♥️🔥🔥

  • @LouisKanje
    @LouisKanje Před 22 dny

    Okhesa mwazi yehova sakondwera naye olo nyama ikatero
    Mulungu amapereka Chicano paizo

  • @Nelsonmatenda
    @Nelsonmatenda Před 22 dny

    We love you comrade ..tell us more

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Před 22 dny

    Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu adalise wina aliyese astaguffllal yha Allah thallah brother

  • @augustinechibbalazi8897

    My gracious heavenly Father have mercy on Malawians

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s Před 22 dny

    GOD bress u Mr mtanyiwahhh!!

  • @user-hg5oj3ko1o
    @user-hg5oj3ko1o Před 22 dny +1

    Iiiii ndiye atipha tonsetu

  • @MustafaAbdullah-pb5zv
    @MustafaAbdullah-pb5zv Před 22 dny +1

    Amalawi kumudziko tadzukani mumchotse chakwelayo......dziko silake

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Před 22 dny +1

    Antanyiwa nlipo abale osamasowa chonchi

  • @kondwaniwhite2871
    @kondwaniwhite2871 Před 22 dny

    Nice 👍 nndinakusowani

  • @CharlesmakveliNyirenda
    @CharlesmakveliNyirenda Před 22 dny +1

    Iwe chakwela Mano kuyipa ngati nyemba ya pa nyini ya Monica wako uyo usatibowe ife

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Před 22 dny

    Am just a Malawian but my president is Traore..on my DP😅😅😅

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja Před 22 dny +1

    Achakwera ku state house atawako posachedwapa

  • @mathewsmdzanja3276
    @mathewsmdzanja3276 Před 22 dny

    I salute you comrade!

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali Před 22 dny

    Ndipo galu ameneyo siomuchula kuti mr iyayi chakwera akufuna amalawi atani 😂😂😂

  • @HusseinMoffatt-mi1fl
    @HusseinMoffatt-mi1fl Před 22 dny

    Amtanyiwa bwanji Kodi odio sikumveka bwinotu

  • @MerryWayson
    @MerryWayson Před 22 dny

    Timakunyadilani Mr Mtanyiwa koma za anthu ogwidwa pa Bedbrig Ili pat naosotu akanapita Maliro kwao kumalawi iya

  • @leonardjika2100
    @leonardjika2100 Před 22 dny

    WHEN YOU ARE PLAYING THE MUSIC OR OTHER VOICES WE CAN NOT HEAR CLEAR PLS TELL YOUR TEACHINIAN

  • @user-ny3it3jp9l
    @user-ny3it3jp9l Před 22 dny

    Lipopo support ❤ 💙

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Před 19 dny

    Koma mulipo a Ntanyiwa, mulibwanji kumeneko

  • @AminahMussah
    @AminahMussah Před 22 dny

    anthu onsewo awakwanitsa koma Mulungu wake waliyenseyu aaaa

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d Před 22 dny

    Mr Chakwera pamtumbo panu ndinthu

  • @originalblack100
    @originalblack100 Před 22 dny

    aziwombere yekha lazalo wa ku kasiya ndi a zinzake onse, kuyambila zikhale, chimwendo kukunyu ndi agututu a thakati onse a congress. BRR brrrrr pha pha pha, comarde mumakwana boss.🤣🤣🤣🤣🤣🤣

  • @user-hj5oq5jm9v
    @user-hj5oq5jm9v Před 22 dny

    Ing'alureni fadah

  • @user-ny3it3jp9l
    @user-ny3it3jp9l Před 22 dny

    Lipopo ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤ ❤❤❤❤

  • @PatrickMtira
    @PatrickMtira Před 22 dny

    Tinakusowani Boss

  • @edmorswalley6663
    @edmorswalley6663 Před 22 dny

    Mulungu sichejemu auzeni

  • @user-mv8vy3ht3n
    @user-mv8vy3ht3n Před 22 dny

    God is able

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk Před 22 dny

    Mmmmmmm ayi zagawana ku mitunduzo ayi....usatinamize ingonena zoooyenera kunenazo....timakutsat Ra mwachidwi...km zotigawanisazo sitilora...tonse nda Malawi ndipo palibe adzatigawanisa

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk Před 22 dny

    Apa bet bridge aja awafinye especially waku MALAWI athane naye ndi opusa

  • @user-wo2kh4xe8q
    @user-wo2kh4xe8q Před 22 dny

    futi yomwe akufuna aphere azawo apita ndi iwoo mulungu simunthu

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember Před 22 dny

    Mukamachedwa kupanga post timakhala ndi nkhawa
    Kut chachitika chan

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Před 22 dny

    👍👍👍👍🤝🤝🤝🤝👍

  • @kamwazabonomali825
    @kamwazabonomali825 Před 22 dny

    Komatu kulimbana ndi aNtanyiwa kuzipusisa ndithu. Awa ndi akatundu omangidwa ndizitsulo. Mbambande.

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg Před 22 dny

    💥💥💥💥

  • @AminAbbass-xc4qk
    @AminAbbass-xc4qk Před 22 dny

    🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @user-lj7lm6ly7z
    @user-lj7lm6ly7z Před 22 dny

    Palibe so kuphedwa apa Inu ambuye akukutetezerani a ntanyiwa ndi azinzanu onse timakuikizani mmapephero

  •  Před 22 dny

    Okupha nayeso azafa... palibe kuopa mcp ndi azitsogoreli ikagwere

  • @user-bw2cv9sd7x
    @user-bw2cv9sd7x Před 22 dny

    a comrade yobu 13;13 yakhulani mosaopa

  • @user-yu4np2wq4s
    @user-yu4np2wq4s Před 22 dny

    Zosatheka athu APHA Aja sanakwane BaiBulo Linati okumba zenje agwelemo yekha ndiiiiiiithu amene watenga gawo lokupha athu amenewa agweramo okhaaaaa ambuye invani simunawalenge athu Kuti azuzike paziko pano inu mukule Ife tichepe

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Před 22 dny

    Nsembe yomwe inapelekedwa zaka zapitazo ya ufulu chakwera waipangisa expire akufuna mwazi wina otchuluka

  • @ArnoldBinali
    @ArnoldBinali Před 22 dny

    Koma chakwela eeee

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Před 22 dny

    Muwamve Mai kaliyati mmene anayankhulira kumaliro a LUCIUS BANDA kumuyamikira president kut ankamuthandiza Lucius,pomwe Lucius wavutika kwambiri mmoyowu.i will never trust politicians.kulira konsekuja,lero akufuna alemerere pa imfa ya chilima.Amai awawa apapa ndiye azionongera mbiri .Akufuna awanamize aMalawi.

  • @VanessaGwangwa
    @VanessaGwangwa Před 22 dny

    ❤❤

  • @LouisKanje
    @LouisKanje Před 22 dny

    Chilango

  • @user-oq5rg5mz7q
    @user-oq5rg5mz7q Před 22 dny

    Zosatheka osewo kafu olo atalimbikila bwanji

  • @ChiefJustin-cl8jl
    @ChiefJustin-cl8jl Před 22 dny

    Nthatha za njaladi

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember Před 22 dny +1

    Koma Chakwera zoti kuli Court la ICC lomwe limathana ndi ma President aku Africa akuziziwa
    Mr President becareful kunali ma President a mphavu kunjaku koma anaphedwa enaso anali okondedwa ndi anthu awo osati inu

  • @Uncle_B265
    @Uncle_B265 Před 22 dny

    Komatuu tili pa ululu eeeeee

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před 22 dny

    MCP or chakwela si mulungu agalu amenewa atikwana dzene 2025 kwatalika dzedi asanephe anthu ofunika MOTI PAKANGOFA MUNTHU WINATSO CHILIMA NDI ANTHU 8 AJA AKWANA chifukwa ife amalawi sitimakhulupila kuti MCP yokupha timati yakele yija iyi ya wong"ono ung'onu KOMA PANO ALIYETSE WAWONA YEKHA KUTI MCP YAMAGADZI NDINTHU

  • @mipeacemakermw9501
    @mipeacemakermw9501 Před 22 dny

    Wina watukwana chakwera uku 😂😂czcams.com/video/WRDkQ8s_34k/video.htmlsi=r_3Qm9tNpQwXfR0D