WADZIDZIMUSA ANTHU UKU VP NDIKA SURPRISE VISIT ku Chikhwawa District Hospital...atutumuka😂😂😂😂

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 26. 08. 2024

Komentáře • 93

  • @Vinic-f3w
    @Vinic-f3w Před měsícem +8

    Malawi needs such heart ❤,,,, continue VP

  • @abangaabanga4677
    @abangaabanga4677 Před měsícem +6

    I commend this, this needs to be encouraged, please continue, with this kind of mentality Malawi will rise, God bless 🙏

  • @DeborahHetekere
    @DeborahHetekere Před měsícem +2

    This is good development that's the spirit that we need as malawians,,,this is exactly what Late Dr Claus Chilima wanted

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda Před měsícem +8

    Zipatala za boma mavuto aakulunso ndomweo. Ogwra ntchto amafika nthaw yomwe akufuna and sayambanso ntchto nthaw yomwe afklayo amayamba wakhala kae akut kupumula then ayambe kugwra ntchto. Imafika mpaka 9 asanayambe ai. Chomwe amadziwa nkutukwana ma patient bas

  • @giftsululu4274
    @giftsululu4274 Před měsícem +4

    Ku utm''' '' mukuona koma... Mwataya gold

  • @user-dy4gc2hr5e
    @user-dy4gc2hr5e Před měsícem +3

    Kkkkkkkkk koma vic wake kashoti

  • @veronicamalisero2671
    @veronicamalisero2671 Před měsícem +1

    A VP ndipo muyendele ma office onse aboma,,,....amakhala pa mtambasale anthu awa..keep it up, ,,,....

  • @masalinodovu1705
    @masalinodovu1705 Před měsícem +1

    Excellent Mr VP izi nde zofunikira kwambiri

  • @FloridaOssy19
    @FloridaOssy19 Před měsícem +1

    ❤❤❤❤❤❤ mwayamb bwino a manganya

  • @DinahNantchengwa
    @DinahNantchengwa Před měsícem +1

    Proud of you Mr president, zikamatele dziko lathu liziyenda bwino, anthu muzipatsla amataililadi koma akamalombikitsidwa choncho ziziyenda

  • @vanalphamphaya3518
    @vanalphamphaya3518 Před měsícem +1

    Big up the VP continue the good work you started when you were there long time.

  • @robertkalima874
    @robertkalima874 Před měsícem +1

    This is great. ife ogwira ntchito mboma tikugona kwambiri. Ngati sitifuna ntchito titsanzike

  • @Ella13400
    @Ella13400 Před měsícem +1

    Mr Usi pitilizana mwina malawi akhonzaaa.......

  • @AfickDaud
    @AfickDaud Před měsícem

    Kukhala ngat madam akunyumbatu Mr Manga kkkk mukuchta kukhalana mmene mukuendamo

  • @omarlux3434
    @omarlux3434 Před měsícem +2

    Osafuna.asye ine ndikuva kukoma ndi vp wathu

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Zama reform please a vice president yambsnipo before 2025

  • @RiaThomKata
    @RiaThomKata Před měsícem

    Well done Mr president

  • @ChifundoChikakwiya-kf1is
    @ChifundoChikakwiya-kf1is Před měsícem +1

    😂😂😂 It is promising slowly but let's hope greedy people won't disturb him

  • @elisaPhiri-k1e
    @elisaPhiri-k1e Před měsícem +1

    Ma patient kumvetsa chisoni pogona pamene ndalama zaboma zikungobedwa mmm

  • @nyasavoicebox
    @nyasavoicebox Před měsícem

    Good on the Right Honourable the Vice President for being positive. Especially when dealing with the young nurse. Samakalipa koma kulangiza kuti mavuto akunyumba aliyapo iyi ndi ntchito anthu amakudalilani muziyesesa ku bwela ku ntchito on time. Even when dealing with the DHO the conversation sinali yoti ine ndiwonke kuti ndine VP but after reprimanding her he made her feel safe to elaborate on the challenges their hospital and district are facing. Politics aside, this guy may actually care about improving Public Service Delivery in Malawi.

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg Před měsícem +1

    Zikachita bwno tiziyamikilako wakulu mwayamba bwno

  • @abbasjutasi909
    @abbasjutasi909 Před měsícem +1

    Iwe nde akuphela kutulo iwe za ndege wachepa nazo
    Good job apule

  • @RotNkhoma
    @RotNkhoma Před měsícem

    Let's continue mr vp you need to go different department of government9, we need great malawi

  • @GraceGonani
    @GraceGonani Před měsícem +1

    Anthu ogwila ntchito boma amatailila kwambili mwina apa atengelapo mphutzilo😊

  • @HassanMaganizo-im6nk
    @HassanMaganizo-im6nk Před měsícem

    Kkkkk kodi limeli ndi sewero lakutiferanji kodi😂😂😂😂

  • @mayesouldphiri9889
    @mayesouldphiri9889 Před měsícem

    Iyi ndi tikuferanji ya srs 😂😂

  • @TizifaBanda-xn5tm
    @TizifaBanda-xn5tm Před měsícem +1

    Civil servant kumakhala ngati ant civil servant.worse ku chipatala it's beyond ntchito.

  • @user-ib7li8pm5h
    @user-ib7li8pm5h Před měsícem +1

    Uyu apwetekaa anthuu

  • @GiftDaftala
    @GiftDaftala Před měsícem +1

    Sizikukhala or pangono he can't even afford chilima's footsteps

  • @user-mi3fw1zg8b
    @user-mi3fw1zg8b Před měsícem

    Mr VP Usi u did it well 👏

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Před měsícem

    Anakapangaso check ku pharmacy ngati kuli mankhwala okuti odwala alandira?

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Well done VP usi. Ntchito yofunikira

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda Před měsícem +1

    Nurse kukanika kuyankha mafunso a a Usi in English Kkkķk Malawiiiii...bolakotu a DHO 🎉

    • @chigokhalid9420
      @chigokhalid9420 Před měsícem +2

      Wakwanisa komanso Mbali ina anali mantha plus I think sanaganizile Kut akumana ndi VP

  • @MtenjeHassan
    @MtenjeHassan Před měsícem

    Zayambika 😂😂 big up mr usi....

  • @fredbmazuwa8066
    @fredbmazuwa8066 Před měsícem

    VP you have got my thumb

  • @brothertonekathyole7349
    @brothertonekathyole7349 Před měsícem

    Keep it up our VP!

  • @user-nu1dj3jh7b
    @user-nu1dj3jh7b Před měsícem

    That's my VP ❤❤❤❤

  • @ChimwemweDemelo
    @ChimwemweDemelo Před měsícem

    Big up Mr vp

  • @FestoniehJim
    @FestoniehJim Před měsícem

    Izi ndie zalowa sewelo ndithu

  • @MenasKaliati
    @MenasKaliati Před měsícem

    Uyu ndiwasero basi😂😂😂

  • @BrendaJali
    @BrendaJali Před měsícem +1

    Good move

  • @user-to5rp9fu8b
    @user-to5rp9fu8b Před měsícem

    Mukawaopsezeso ku mapasport uko kuli chinyengo

  • @janemanyamba7201
    @janemanyamba7201 Před měsícem +1

    Uyu ndiye atithandizadi zoona

  • @AllanMwakalenga-wn5ib
    @AllanMwakalenga-wn5ib Před měsícem

    Yalakwa apa...mwachedwa ku vepi a nurse

  • @user-ux8qz1tg7l
    @user-ux8qz1tg7l Před měsícem

    Iwe ma nganya 10pn munthu apanganao cani 😂😂

  • @AllanMwakalenga-wn5ib
    @AllanMwakalenga-wn5ib Před měsícem +1

    Tikuferanji 😂😂

    • @EllinaBitto
      @EllinaBitto Před měsícem

      Ndendende😂😂😂😂😂😂😂

  • @Marionphuxymw
    @Marionphuxymw Před měsícem

    Kkkkkkk kma adaa changa ndichala pakamwa

  • @GustoAjasi-fl9oo
    @GustoAjasi-fl9oo Před měsícem

    😂😂😂😂 ausi anachenjela eee

  • @osmanafadi4801
    @osmanafadi4801 Před měsícem

    Wamisala anaona ndewuu

  • @user-co5yu3fs4r
    @user-co5yu3fs4r Před měsícem

    Powerful musatsiye

  • @tracybennie7783
    @tracybennie7783 Před měsícem

    Ine. Ndiye. Ndikalila. Malilo

  • @TizifaBanda-xn5tm
    @TizifaBanda-xn5tm Před měsícem

    Ndawala zikuswedwa eeee

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma4265 Před měsícem

    New sheriff in town

  • @user-tk6qh9zs7h
    @user-tk6qh9zs7h Před měsícem

    Zofunika zimenezo a VP.
    Ma Civil Servants ambiri matama komanso kumalimbikira ntchito, kukula Mtima komanso kudzikonda.
    Akuti ntchito ya m'boma imavuta polowa.
    Achangamutseni ndithu.

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 Před měsícem

    I remember achilima anayambaso chonchi kenako nae alowa mu system...... Hope this will no stop

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo Před měsícem

    😂😂😂 Km manganya

  • @HappinessMilanzi-b2m
    @HappinessMilanzi-b2m Před měsícem

    Zikuoneka kuti mutithandiza

  • @user-cm3pl3pb9u
    @user-cm3pl3pb9u Před měsícem

    Kkkkk ine ndimaona ngati sewelotu😂😂😂😂🎉🎉

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Před měsícem +1

    Ngati zenizenitu, nkana unampeleka Bhiyeni umafuna zimenezi.

    • @EllinaBitto
      @EllinaBitto Před měsícem

      😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @emmanuelkenneth4768
    @emmanuelkenneth4768 Před měsícem

    😅😅😅😅 well planned

  • @Uncle_B265
    @Uncle_B265 Před měsícem

    Ngati azimaliza ndiyen tione

  • @ruthkaoloka4772
    @ruthkaoloka4772 Před měsícem

    ndi drama kodi?

  • @EmmReece
    @EmmReece Před měsícem

    mcp iwinaso bad

  • @AlinafeSolomoni
    @AlinafeSolomoni Před měsícem

    Koma akuoneka ngati afika movuta koma ndimunthu ochezeka

  • @EvanceSteven-u5g
    @EvanceSteven-u5g Před měsícem

    Nice

  • @jonathanmbewe4246
    @jonathanmbewe4246 Před měsícem

    Mupitenso ku immigration mukawonekeleko bwana

  • @user-xe5lb4uf3n
    @user-xe5lb4uf3n Před měsícem

    Bola zipipitirire

  • @Choicemlw
    @Choicemlw Před měsícem

    Mu manifesto a Tonse alliance anati ankadzalowa m'boma anthu azipita ku ntchito 8:30
    Aiwala nthawi yomweyi kodi?

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo Před měsícem

    Akuyankhula ngt akupanga tikuferanji

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 Před měsícem

    Ukuoatenga anthu ngati zitsiru USI government ukuti kulibe ndalama koma zomwe akumagawa kumusonkhano akuzitenga kuti?

  • @user-xx4yi4mq5m
    @user-xx4yi4mq5m Před měsícem

    ipase moto usi bola osazasitha mukazapasidwa mwayi.......try hard this year 2025 boma....

  • @user-mm3es3ph7h
    @user-mm3es3ph7h Před měsícem

    Malume mukukwana

  • @StellaErias
    @StellaErias Před měsícem

    Pitilizani bwana azimayi oyembekezela timavutika zipatalamu agalu amenewa amazimva ubwana zipatalamu

  • @user-qs3vs8kz6n
    @user-qs3vs8kz6n Před měsícem

    Mulunguakupatseni phamvu

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 Před měsícem

    ❤❤

  • @willieBillschiumbuzo
    @willieBillschiumbuzo Před měsícem

    Ipatseni moto a vice ama 10:41 wonjeza kubwera mochedwa kutchito ma nurse akafika ayambe kaye aseweretsa 4n then aziyamba cha ma 9 kugwira tchito

  • @danielkhinguirossejuliasse6106

    ndiye wapanga sewero lamphamvu

  • @EmmReece
    @EmmReece Před měsícem

    mcp iwinaso

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Před měsícem

    Zandale ziduse uko nawo anthu ogwira ntchito chipatala za boma amapanga matama muzapanadi

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda Před měsícem

    Ma nurse ku malawi osadziwa English Kkkķk km zlko. Usi wayesetsatu

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma4265 Před měsícem

    Ananena kuti asenda aliyense waulesi

  • @FlorenceBillyGama
    @FlorenceBillyGama Před měsícem

    Ubwana syndrome inavulaza a malawi ambiri

  • @AishaUthman-mg7db
    @AishaUthman-mg7db Před měsícem

    😂😂😂😂

  • @user-eu3qz2so4n
    @user-eu3qz2so4n Před měsícem

    Zapamwamba