Musaiwale naenso anali gulu lofuna kuba chipani la kondwani nankumwa ,komanso after kuionera patali kuti sangamake pa adad basino kuthawira ku UTM KUMENEKO MPATA AKAUUPEZA ayende bwino usazabwerenso ku dpp
Dalitso was a favourite wa adad, he is the only one amene adad amamukhulupilira kuti atha kumupanga endorse. Believe me, iyiyi ndi movie ma guys wa(adad ndi Kabambe) akudziwana.
Njomba zimenezo kufuna kupusitsa a Malawi 😂, adakali ku dpp komweko koma akufuna apusise wanthu apite ku utm akatero akasankhidwa kukhala president wa utm kenako azapange n'gwirizano ndi DPP ndiye ku dppko azakhala VP wa peter akatero peter azachita resign ndiyekuti kabambe azasala nkukhala president wa DPP. Izi nzomwe amadananazo achina Nankhwa aja , peter waku Thyolo, kabambe waku thyolonso.akufuna azasiilane mpando anthuwa akuziwa chomwe akuchita
Aaaa palibe ubwino wake mnzeru za alliance ife a UTM tadzidziwa ndipo tikudzidziwa takula nazo mpaka taluza president wathu palibe angavotere izi mukunena iwalani
Ngati akufuna kupita ku UTM apite koma tione kaye performance yake Ali ku reserve bank and also ku DPP. sometimes timakhala ndi anthu oti atha kugwila ntchito bwino dziko ndikutukuka koma amalephera chifukwa sapatsidwa mpaka bwinobwino or kuwagwiritsa ntchito mosiyana ndi mbali yomwe iwowo amayiziwa and atha kupanga deliver mosavutikira if they given the necessary resources. So I believe ngati anagwirako ntchito ngati nkulu wa reserve bank nzeru zilimo, he can be useful ku dziko lathu
@@DalitsoMatope zikugwilizana bwanji usogoleri ukufunika kwa Ana chakwela so ndi wachikulire bola awa not gogo ngati Peter kabambe kuti achoke kuli vuto kumeneko uzavomereza mochedwa
Prophet liyabunya analankhula za utm Zana kuti ayigula, liyabunya is not just a prophet like others no he is Elijah of our generation, love u prophet, bless me my name is Paul kheche mvuma
Catholic zoonadi ndi church ya pamalo pose koma mulibemo choonadi, like praying for the dead, Christmas, forgiving sins like God himself,kubatiza ana,ubatizonso wabodza,kuletsa kukwatila,kumafuna kupanga control boma pomwe church and state siziyenera kuphatikizana, kusintha sabata from surtuday to sunday,tsiku kumayamba usiku kuthanso usiku mmalo moti tsiku liziyamba kulowa kwa dzuwa kuthanso kulowa kwadzuwa ndi zina zambili bible likuti turukanimo mmenemo anthu anga babulo wagwa wagwa amayi wa a chigololo wa zonyasitsa za dziko ndipo mpingo umenewu uli ndi ana ake omwe amaitsatira zochita zakezo monga sunday keeping and all things that are out side the bible these practices are from pagan the chief of all paganism is the enemy of God called satan thanks for understanding ❤❤❤❤
Akuzakhala running met wa APM MUZANDISIMIKIZA IYI N MISSION mark my wards
100%
100%
Nde runningmate azayimira chipani chanji poti ku UTM azayimira Mary Chilima
He is our president at UTM. Wachoka kuchipinda kupita pa seating room. UTM and DPP we are one.
Welcome to our beloved party UTM osaopa, osafooka osatopa SKC ndi ineyo ndi iweyo ndi ifeyo
Akabambe amafuna uprezdent ndiye mmene inangocitika ngodzi ya kuchikagawa achilima mkutisiya mumtima mwawo.amakondwa kuti atenga uprezdent ku utm akuluwa musavutike nawo asiyeni akaimire ku utm
Musaiwale naenso anali gulu lofuna kuba chipani la kondwani nankumwa ,komanso after kuionera patali kuti sangamake pa adad basino kuthawira ku UTM KUMENEKO MPATA AKAUUPEZA ayende bwino usazabwerenso ku dpp
Dalitso was a favourite wa adad, he is the only one amene adad amamukhulupilira kuti atha kumupanga endorse. Believe me, iyiyi ndi movie ma guys wa(adad ndi Kabambe) akudziwana.
Mwana amalira ninkodzo wake asiyeni ayende bwino both him and others are not settled kutha kwamunthu kumeneko
Komano movie imenei zitengera kuti akupitako akakhaladi president
Ngati watuluka muchipani cha dpp pali ndjira ziwiri zokha zimene ndingamuwuze 1 kuyambisa chipani chake. 2 asalowe chipani chilichose mumalawi.
Chifukwa pali njira imozi imene ndawona kuti kumalawi kuli vuto loti anthu wosiya zipani zao ndikumalowa kwina amakhala osokoneza kwambiri komaso amakala anthu okula mutima palipose safuna kukhala opanda udindo
Akuwoneka upule akufuna ndithu maganizo anga nduwona ngat Dpp itat yapanga alliance uyuyu afuna cholinga azakhale running mate
Kumalawi kuyenelaso kukhala lamulo loti ngati munthu ali muchipani asatuluke ndikulowa chipani China ngati watuluka basi a siye ndale.
2025 tikupempha ku parliament kuti akachose lamulo loti 50+1 aliyese apite ndichipani chake 2025. No alliance ( mugwirizano )
Zikupangisa phokoso ziko silikuyenda bwino
Ndi running mate wa peter uyu from aliance ya utm ndi dpp kuti anthu aku dpp asadzayankhure zambiri iyi ndi plan
Ikhoza kukhala good move , tiona zambiri sitinati. Ku DPP kuli vuto komabe izi sizintha chikoka chomwe chilipo pakati pa anthu ngati tisaonenso ena akuchoka..
Guys apa pagona ndale zazikulu iye uja akatenga president ku utm azapanga alliance ndi dpp
Ayende bwino bola ngati machoka mwamtendele
It is mission not kunyanyala mungopusapo
Zitseko ndi zotseku ku utm
We love DPP and we love UTM as well, the decision is very good and powerful than joining MCP ❤❤❤
Bola ngati abwelera utsogoleri weniweni osati kupusisa anthu patsogolo kutembenuka hmmm
Musapusitsike inu izi ndiye amati ndale zenizeni akungofuna kutipusitsa awa ,iyi ndi plan yoti dpp yonse idakhalilana pansi kuti ipangidwe ndicholinga choti utm ija ijoyiniletu ku dpp ndiye kabambe watumidwa ngati nthumwi kuchokela ku dpp kulowa utm.woooo!
Pitani ku UTM.We want energetic leaders in UTM
Pamene zafikapa sip
Njomba zimenezo kufuna kupusitsa a Malawi 😂, adakali ku dpp komweko koma akufuna apusise wanthu apite ku utm akatero akasankhidwa kukhala president wa utm kenako azapange n'gwirizano ndi DPP ndiye ku dppko azakhala VP wa peter akatero peter azachita resign ndiyekuti kabambe azasala nkukhala president wa DPP. Izi nzomwe amadananazo achina Nankhwa aja , peter waku Thyolo, kabambe waku thyolonso.akufuna azasiilane mpando anthuwa akuziwa chomwe akuchita
Apa mwaganizo mozama bro,zitha kukhaladi chomcho
Aaaa palibe ubwino wake mnzeru za alliance ife a UTM tadzidziwa ndipo tikudzidziwa takula nazo mpaka taluza president wathu palibe angavotere izi mukunena iwalani
Pitani mmtendere anthu adyera inu.
Kususukira upresident nkana mwatuluka mtawona kuti ku utm sck wamwalira
Samapita ku UTM SKC alimoyo🤣
Kkkkkk
Let's meet on our alliance
Apa nde akufunadi kuimaliza UTm cholinga akasakhidwe kudzakhala Vice president kuti UTM itheretu iyi ndi plan
Welcome Mr kabambe to utm
Welcome to UTM monga ngati member chabe osati President
Welcome to UTM Mr
Ngati akufuna kupita ku UTM apite koma tione kaye performance yake Ali ku reserve bank and also ku DPP. sometimes timakhala ndi anthu oti atha kugwila ntchito bwino dziko ndikutukuka koma amalephera chifukwa sapatsidwa mpaka bwinobwino or kuwagwiritsa ntchito mosiyana ndi mbali yomwe iwowo amayiziwa and atha kupanga deliver mosavutikira if they given the necessary resources. So I believe ngati anagwirako ntchito ngati nkulu wa reserve bank nzeru zilimo, he can be useful ku dziko lathu
Wayiwonera patali sangamake pa Apm
Osapusisika inu uyu ndi Cousin wa APM pachi bale chawo
Mwapusa mr mukanangokhara komweko bwezi trem inayo akanakupatsani kuti mudzaimire km apa palibe mwachita
wachita bwino kusiya chipani cha kubanja
Muuzeni akalowe Ku MCP asati nyatsa
A UTM musanyadire,woteroyo ngwa dyera
Wachita bwino akalowe UTM . Vote yanga azaipeza
Wadabwitsa ndani munthu olo chipani alibe
Aaaaakabambe kabambe
Munalibe impact iliyonse mwainu yen Danish bwino
Welcome to UTM
Go well
DPP 2025 boma muzakumbuka
Kabambe akuthawa chani ku DPP? Kapena Biden wa Malawi?
Kkkkkkkl😂😂
Akuthawa chipani cha family watopa nacho
Zakhara bwino chipan cha banja ichi
Pitani ku aford basi
Ku Dpp usogoleri kulibeko koma dyela kukakamila udindo gogo imeneija osapasako mpata achinyamata
Achinyamata ngati inu alepheratu
Chakwera wapasa ndani mpata?? Mesa nae wakakamira 😅
@@MzadziWangaakufuna amalizitse kudya misokho ya malawi
@@DalitsoMatope zikugwilizana bwanji usogoleri ukufunika kwa Ana chakwela so ndi wachikulire bola awa not gogo ngati Peter kabambe kuti achoke kuli vuto kumeneko uzavomereza mochedwa
Ali ndi tsoka ameneyo
Peter Mutharika sangasiye mpando once voted into power unless death takes him. So l salute that decision Kabambe has made
Ndipo zoona Peter Munthalika sangasiye mpando wa chipani cha achimwene ake zoona
Prophet liyabunya analankhula za utm Zana kuti ayigula, liyabunya is not just a prophet like others no he is Elijah of our generation, love u prophet, bless me my name is Paul kheche mvuma
😂😂😂😂
Wachita bwino alowe chipani chapamaloponse ngati catolica
Catholic zoonadi ndi church ya pamalo pose koma mulibemo choonadi, like praying for the dead, Christmas, forgiving sins like God himself,kubatiza ana,ubatizonso wabodza,kuletsa kukwatila,kumafuna kupanga control boma pomwe church and state siziyenera kuphatikizana, kusintha sabata from surtuday to sunday,tsiku kumayamba usiku kuthanso usiku mmalo moti tsiku liziyamba kulowa kwa dzuwa kuthanso kulowa kwadzuwa ndi zina zambili bible likuti turukanimo mmenemo anthu anga babulo wagwa wagwa amayi wa a chigololo wa zonyasitsa za dziko ndipo mpingo umenewu uli ndi ana ake omwe amaitsatira zochita zakezo monga sunday keeping and all things that are out side the bible these practices are from pagan the chief of all paganism is the enemy of God called satan thanks for understanding ❤❤❤❤