Dalitso Kabambe watuluka monyanyala ku DPP ndipo statement yasonyeza kale ku Chipani chomwe akupita

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 20. 08. 2024

Komentáře • 68

  • @user-lw4hw9ce4w
    @user-lw4hw9ce4w Před měsícem +6

    Akuzakhala running met wa APM MUZANDISIMIKIZA IYI N MISSION mark my wards

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Před měsícem +2

    He is our president at UTM. Wachoka kuchipinda kupita pa seating room. UTM and DPP we are one.

  • @hamischikalimba6626
    @hamischikalimba6626 Před měsícem +2

    Welcome to our beloved party UTM osaopa, osafooka osatopa SKC ndi ineyo ndi iweyo ndi ifeyo

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e Před měsícem

      Akabambe amafuna uprezdent ndiye mmene inangocitika ngodzi ya kuchikagawa achilima mkutisiya mumtima mwawo.amakondwa kuti atenga uprezdent ku utm akuluwa musavutike nawo asiyeni akaimire ku utm

  • @thokojames5231
    @thokojames5231 Před měsícem +4

    Musaiwale naenso anali gulu lofuna kuba chipani la kondwani nankumwa ,komanso after kuionera patali kuti sangamake pa adad basino kuthawira ku UTM KUMENEKO MPATA AKAUUPEZA ayende bwino usazabwerenso ku dpp

    • @jeremiahmalikebu2393
      @jeremiahmalikebu2393 Před měsícem

      Dalitso was a favourite wa adad, he is the only one amene adad amamukhulupilira kuti atha kumupanga endorse. Believe me, iyiyi ndi movie ma guys wa(adad ndi Kabambe) akudziwana.

    • @user-st6bt5vv9c
      @user-st6bt5vv9c Před měsícem

      Mwana amalira ninkodzo wake asiyeni ayende bwino both him and others are not settled kutha kwamunthu kumeneko

    • @thokojames5231
      @thokojames5231 Před měsícem

      Komano movie imenei zitengera kuti akupitako akakhaladi president

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Před měsícem

    Ngati watuluka muchipani cha dpp pali ndjira ziwiri zokha zimene ndingamuwuze 1 kuyambisa chipani chake. 2 asalowe chipani chilichose mumalawi.
    Chifukwa pali njira imozi imene ndawona kuti kumalawi kuli vuto loti anthu wosiya zipani zao ndikumalowa kwina amakhala osokoneza kwambiri komaso amakala anthu okula mutima palipose safuna kukhala opanda udindo

  • @SueWahna
    @SueWahna Před měsícem

    Akuwoneka upule akufuna ndithu maganizo anga nduwona ngat Dpp itat yapanga alliance uyuyu afuna cholinga azakhale running mate

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Před měsícem

    Kumalawi kuyenelaso kukhala lamulo loti ngati munthu ali muchipani asatuluke ndikulowa chipani China ngati watuluka basi a siye ndale.
    2025 tikupempha ku parliament kuti akachose lamulo loti 50+1 aliyese apite ndichipani chake 2025. No alliance ( mugwirizano )
    Zikupangisa phokoso ziko silikuyenda bwino

  • @chisomokawotcha1766
    @chisomokawotcha1766 Před měsícem +2

    Ndi running mate wa peter uyu from aliance ya utm ndi dpp kuti anthu aku dpp asadzayankhure zambiri iyi ndi plan

    • @bysongeorge3243
      @bysongeorge3243 Před měsícem

      Ikhoza kukhala good move , tiona zambiri sitinati. Ku DPP kuli vuto komabe izi sizintha chikoka chomwe chilipo pakati pa anthu ngati tisaonenso ena akuchoka..

  • @PharrohmagawaZimba230
    @PharrohmagawaZimba230 Před měsícem

    Guys apa pagona ndale zazikulu iye uja akatenga president ku utm azapanga alliance ndi dpp

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e Před měsícem

    Ayende bwino bola ngati machoka mwamtendele

  • @user-ln7ff4su2r
    @user-ln7ff4su2r Před měsícem +1

    It is mission not kunyanyala mungopusapo

  • @TimothyPalira
    @TimothyPalira Před měsícem

    Zitseko ndi zotseku ku utm

  • @lyiemax
    @lyiemax Před měsícem

    We love DPP and we love UTM as well, the decision is very good and powerful than joining MCP ❤❤❤

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Před měsícem +1

    Bola ngati abwelera utsogoleri weniweni osati kupusisa anthu patsogolo kutembenuka hmmm

  • @jomochirwa
    @jomochirwa Před měsícem

    Musapusitsike inu izi ndiye amati ndale zenizeni akungofuna kutipusitsa awa ,iyi ndi plan yoti dpp yonse idakhalilana pansi kuti ipangidwe ndicholinga choti utm ija ijoyiniletu ku dpp ndiye kabambe watumidwa ngati nthumwi kuchokela ku dpp kulowa utm.woooo!

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Před měsícem

    Pitani ku UTM.We want energetic leaders in UTM

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 Před měsícem

    Pamene zafikapa sip

  • @user-nu1dj3jh7b
    @user-nu1dj3jh7b Před měsícem +1

    Njomba zimenezo kufuna kupusitsa a Malawi 😂, adakali ku dpp komweko koma akufuna apusise wanthu apite ku utm akatero akasankhidwa kukhala president wa utm kenako azapange n'gwirizano ndi DPP ndiye ku dppko azakhala VP wa peter akatero peter azachita resign ndiyekuti kabambe azasala nkukhala president wa DPP. Izi nzomwe amadananazo achina Nankhwa aja , peter waku Thyolo, kabambe waku thyolonso.akufuna azasiilane mpando anthuwa akuziwa chomwe akuchita

    • @user-gp10.10
      @user-gp10.10 Před měsícem

      Apa mwaganizo mozama bro,zitha kukhaladi chomcho

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

      Aaaa palibe ubwino wake mnzeru za alliance ife a UTM tadzidziwa ndipo tikudzidziwa takula nazo mpaka taluza president wathu palibe angavotere izi mukunena iwalani

  • @JamaniNyirongo
    @JamaniNyirongo Před měsícem

    Pitani mmtendere anthu adyera inu.
    Kususukira upresident nkana mwatuluka mtawona kuti ku utm sck wamwalira

  • @user-pu1fy9rs3h
    @user-pu1fy9rs3h Před měsícem +1

    Samapita ku UTM SKC alimoyo🤣

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y Před měsícem

    Let's meet on our alliance

  • @Aminayaumi.in8tn
    @Aminayaumi.in8tn Před měsícem

    Apa nde akufunadi kuimaliza UTm cholinga akasakhidwe kudzakhala Vice president kuti UTM itheretu iyi ndi plan

  • @FarookStambuli
    @FarookStambuli Před měsícem

    Welcome Mr kabambe to utm

    • @isaihmagani5697
      @isaihmagani5697 Před měsícem

      Welcome to UTM monga ngati member chabe osati President

  • @paularason
    @paularason Před měsícem

    Welcome to UTM Mr

  • @ChifundoChiwanda-ru3pg
    @ChifundoChiwanda-ru3pg Před měsícem

    Ngati akufuna kupita ku UTM apite koma tione kaye performance yake Ali ku reserve bank and also ku DPP. sometimes timakhala ndi anthu oti atha kugwila ntchito bwino dziko ndikutukuka koma amalephera chifukwa sapatsidwa mpaka bwinobwino or kuwagwiritsa ntchito mosiyana ndi mbali yomwe iwowo amayiziwa and atha kupanga deliver mosavutikira if they given the necessary resources. So I believe ngati anagwirako ntchito ngati nkulu wa reserve bank nzeru zilimo, he can be useful ku dziko lathu

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před měsícem

    Wayiwonera patali sangamake pa Apm

    • @isaihmagani5697
      @isaihmagani5697 Před měsícem

      Osapusisika inu uyu ndi Cousin wa APM pachi bale chawo

  • @PatrickMtira
    @PatrickMtira Před měsícem

    Mwapusa mr mukanangokhara komweko bwezi trem inayo akanakupatsani kuti mudzaimire km apa palibe mwachita

  • @robertkalima874
    @robertkalima874 Před měsícem

    wachita bwino kusiya chipani cha kubanja

  • @JasonMailos
    @JasonMailos Před měsícem

    Muuzeni akalowe Ku MCP asati nyatsa

  • @AbdulrahimoMassamba
    @AbdulrahimoMassamba Před měsícem

    A UTM musanyadire,woteroyo ngwa dyera

  • @user-vx5kv8dz3d
    @user-vx5kv8dz3d Před měsícem

    Wachita bwino akalowe UTM . Vote yanga azaipeza

  • @user-ru1mm7bf4p
    @user-ru1mm7bf4p Před měsícem

    Wadabwitsa ndani munthu olo chipani alibe

  • @BrianJoe-z7u
    @BrianJoe-z7u Před měsícem

    Aaaaakabambe kabambe

  • @user-jj1zv2rs7f
    @user-jj1zv2rs7f Před měsícem

    Munalibe impact iliyonse mwainu yen Danish bwino

  • @user-kq6rp6hn7y
    @user-kq6rp6hn7y Před měsícem

    Welcome to UTM

  • @user-jj1zv2rs7f
    @user-jj1zv2rs7f Před měsícem

    Go well

  • @AndreaSignala-hk2yg
    @AndreaSignala-hk2yg Před měsícem

    DPP 2025 boma muzakumbuka

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Před měsícem

    Kabambe akuthawa chani ku DPP? Kapena Biden wa Malawi?

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Před měsícem

    Zakhara bwino chipan cha banja ichi

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve Před měsícem

    Pitani ku aford basi

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Před měsícem

    Ku Dpp usogoleri kulibeko koma dyela kukakamila udindo gogo imeneija osapasako mpata achinyamata

    • @DalitsoMatope
      @DalitsoMatope Před měsícem

      Achinyamata ngati inu alepheratu

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga Před měsícem

      Chakwera wapasa ndani mpata?? Mesa nae wakakamira 😅

    • @DalitsoMatope
      @DalitsoMatope Před měsícem

      @@MzadziWangaakufuna amalizitse kudya misokho ya malawi

    • @SaidiMbawa-st6bj
      @SaidiMbawa-st6bj Před měsícem

      @@DalitsoMatope zikugwilizana bwanji usogoleri ukufunika kwa Ana chakwela so ndi wachikulire bola awa not gogo ngati Peter kabambe kuti achoke kuli vuto kumeneko uzavomereza mochedwa

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana Před měsícem

    Ali ndi tsoka ameneyo

  • @hamischikalimba6626
    @hamischikalimba6626 Před měsícem

    Peter Mutharika sangasiye mpando once voted into power unless death takes him. So l salute that decision Kabambe has made

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

      Ndipo zoona Peter Munthalika sangasiye mpando wa chipani cha achimwene ake zoona

  • @user-nw6ie3xx8b
    @user-nw6ie3xx8b Před měsícem

    Prophet liyabunya analankhula za utm Zana kuti ayigula, liyabunya is not just a prophet like others no he is Elijah of our generation, love u prophet, bless me my name is Paul kheche mvuma

  • @WilisonWada
    @WilisonWada Před měsícem

    😂😂😂😂

  • @LaitoneJefitala
    @LaitoneJefitala Před měsícem

    Wachita bwino alowe chipani chapamaloponse ngati catolica

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Před měsícem

      Catholic zoonadi ndi church ya pamalo pose koma mulibemo choonadi, like praying for the dead, Christmas, forgiving sins like God himself,kubatiza ana,ubatizonso wabodza,kuletsa kukwatila,kumafuna kupanga control boma pomwe church and state siziyenera kuphatikizana, kusintha sabata from surtuday to sunday,tsiku kumayamba usiku kuthanso usiku mmalo moti tsiku liziyamba kulowa kwa dzuwa kuthanso kulowa kwadzuwa ndi zina zambili bible likuti turukanimo mmenemo anthu anga babulo wagwa wagwa amayi wa a chigololo wa zonyasitsa za dziko ndipo mpingo umenewu uli ndi ana ake omwe amaitsatira zochita zakezo monga sunday keeping and all things that are out side the bible these practices are from pagan the chief of all paganism is the enemy of God called satan thanks for understanding ❤❤❤❤