UTM sikumufuna Usi ngati mtsogoleri kutsatila imfa ya Chilima zili umu ndi Peter Jegwa

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 22. 06. 2024

Komentáře • 56

  • @MalawiTrendsTV
    @MalawiTrendsTV  Před 7 dny +4

    Oyankhula ndi Peter Jegwa

  • @shayrafernandeslatif9556

    Ndipoo olo kupeleka ulemu kwa SKC,ineso ndi nadabwa,kwa ine a Micheal Usi sanawoneke kukhudzidwa, ndi kuti aluza munthu wofunikila pawokha

  • @user-rk3gq7gd8f
    @user-rk3gq7gd8f Před 7 dny +8

    Zavuta basi bwerelani ku APM

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda Před 7 dny +3

    Nkhani nayipulika makola chomeni, suzgo la UTM, Uchisepuka, ngunandi,ntchindi zingawamo yayi, , Mulongozgi Chilima wanguwa wachali kusambizga wakumulondola wake,so ntchindi mulije mu UTM, and kuzenga mulije

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem Před 7 dny +4

    Manganya ndimfiti ndipo musaloredi

  • @irridessahmonterosa9943
    @irridessahmonterosa9943 Před 7 dny +3

    Micheal Usi is a traitor he joined MCP long ago so Chakwera should not lie that he has taken his vice from UTM.

  • @damianokachingwe3531
    @damianokachingwe3531 Před 6 dny +3

    Mmmmm amalawi muchedwa nazo nthawi zonse miseche basi walakwanji Michael usi

  • @stephancommercial580
    @stephancommercial580 Před 7 dny +1

    I'm following

  • @paundfeston
    @paundfeston Před 6 dny +2

    NDIPO MANGANYAYO NDI GALU NDIOMWE APHA CHILIMA ZIKHALE CHIMWENDO CHAKWERA NDI AFITI

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 Před 6 dny

    Live from south Africa cape town kuvesera mwachidwi

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah Před 7 dny +2

    We follow u

  • @BrightonKamwendo-db1ci
    @BrightonKamwendo-db1ci Před 7 dny +2

    Komaso anayenera kunkanila chakwera ngatidi anali wa UTM

  • @user-vn8zz1cw1t
    @user-vn8zz1cw1t Před 7 dny +3

    Anthu sakumfuna Manganya usi

  • @falliotphiri688
    @falliotphiri688 Před 7 dny +2

    You. Don't need to be liked by the people to be a leader... A leader will always have traitors against him

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Před 5 dny

    Anthu sangamupase wule usi chifukwa ndi udasi ndi amene anamupereka chilima

  • @DennmichSimb
    @DennmichSimb Před 6 dny

    It's too early to start fighting, Chilima chose Michael Usi as his deputy, let's give him a chance.Dyera some leaders in UTM.

  • @mayamikothomson
    @mayamikothomson Před 6 dny

    Dyera,dyera,dyera,miseche,miseche Yesu akukuonani

  • @Cathy-oc7vd
    @Cathy-oc7vd Před 6 dny

    Mmm... koma mwati tipita chitsogolo? Ija ndi ngozi tivomeleze

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Před 6 dny

    Usi ndi oipa uyu simunthu timuwona ngati alimbe iyeyo

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r Před 6 dny

    Choka apa naweso miseche amanena ziko rikunva ngakhare yesu zinthu zikarakwika amawa uza ophunzira ake ndiye ngat mukuti miseche kufuna kt zinthu zikarakwika anthu azingo penya nkawona chakwera akuku zunzani choncho chifukwa wawona nayeso kt ndinu anthu womango wombera mmanja bas kuthekera muribe ndemunya zeni zenitu simunat chifukwa nde akuchita kuwoneka kt sari mochezaso naye

  • @JabessKamatuwa
    @JabessKamatuwa Před 6 dny

    Sakumufuna bwanji munthu skc anamukhulupilira,njala nthenda sanjeeeee.

  • @paundfeston
    @paundfeston Před 6 dny +1

    ZOTI MANGANYA NDI WA U T M UZIWA NDIWE INE MULIBE

  • @kamphunguluhanga5716
    @kamphunguluhanga5716 Před 6 dny

    Constitution yimati president asankhe vp ngati vp wamwalira. Sono mugwirizano wa utm ndi Mcp unaliwoti bwanji. Kodi akanamwalira chilima Ali mboma kodi ndani akanakhala president????? Or zikambidwe muti bwanji Michael Usiyu ndi Automatic.

  • @ErickTym-u2m
    @ErickTym-u2m Před 6 dny

    Manganyayo ajudziwapo Kanthu ndi mfiti manyi ake mkolo wako pa make ndi chikwelaniyo mbobo yake ya Monica nkholo wake mfikti wamake

  • @EmanuelMuotcha
    @EmanuelMuotcha Před 5 dny

    Zoona uyuyu siwa utm ayi samalani inu UTM mutheka chipululu ngati simusamala mangadya akutengelani ku bagamoyo njoka saweta mcp ikukhazulani

  • @trustDaud-gu6ke
    @trustDaud-gu6ke Před 6 dny

    Micheal utsi sakukwanila the late chilima was number one

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před 6 dny

    Mthamangiseni galu ameneyo ndi mfiti

  • @jonathanmbewe4246
    @jonathanmbewe4246 Před 7 dny +1

    Eish

  • @user-mv4us2yx1o
    @user-mv4us2yx1o Před 6 dny

    Poti mwaziwa kuti manganya ndamene anapha nawo achilima,timaona ngati simukuziwatu mfiti iyi

  • @felixsaidi6715
    @felixsaidi6715 Před 6 dny

    Ine ndikuwona ngati Usi Alibwino. Koma chakwerayo amuyipitsira mbiri yake .

  • @MerryWayson
    @MerryWayson Před 6 dny

    Usi Sitikuyenera kumuwelengera kut amapanga za Chilima cos infa ya Chilima Usi ndili Shure kut amadziwa zachiwembuzi amadziwapo khanthu

  • @JabessKamatuwa
    @JabessKamatuwa Před 6 dny

    Sakumufuna bwanji yet munthu anali VP ku utm.

  • @heavyt70
    @heavyt70 Před 4 dny

    Akutumani eti usi wakhala liti akupanga za utm? Usi ndi vise president wa mcp

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Před 6 dny

    MANGANYA NDI WA MCP KOMA ANAKAJOINA UTM MOTUMIDWA NDI CHAKWERA POFUNAFUNA NJIRA YOPEREKERA CHIRIMA UYU NDI GALU

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Před 6 dny

    Ndipo nkhope yake inali yowuma Gwaaa ngati yachakwela

  • @user-vf3jy9li3d
    @user-vf3jy9li3d Před 6 dny

    Ndipo amkachita kunyokodola kukamwa kuonesa kuti zomwe amalankhula anzawo kwaiwo zinali zopanda pake chilipo chomwe amadziwa.....

  • @AlfonsoTheka
    @AlfonsoTheka Před 6 dny

    Komano inuyo mmafuna vice president akhale ndani poti vice President anatisiya otsatila wa vice president anali micle usi mukuwona kuti adakasankha ndani ? Kuti akhale vice President za imfa ya a chilima i think tiyeni tinsiye mulungu akhale mulungu okupha ndilupanga nayenso adzaphedwa chimodzimodzi kulibe wambewu kudziko lapansi

  • @LINLYLUNGALUNGA
    @LINLYLUNGALUNGA Před 6 dny

    Mkunena zoona

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 Před 6 dny

    Manganya ndi m'thira kuwiri moti zonse zachitika zija akuyenera kuyankhulapo kanthu.

  • @EsterKapungwa
    @EsterKapungwa Před 4 dny

    Wadya zake alibe mulandu kkkk

  • @PatsonZimba-nv9mc
    @PatsonZimba-nv9mc Před 4 dny

    Vautesi,,,

  • @ForsterThawan
    @ForsterThawan Před 6 dny

    Uyuyu wadya za chakwela galu uyu

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm

    Manganya ndi mfiti uyu galu wachabe chabe

  • @falliotphiri688
    @falliotphiri688 Před 7 dny +1

    Kudelera basi

  • @mayamikothomson
    @mayamikothomson Před 6 dny

    Karma will know their addresses ,time is coming.

  • @ephraimkadamika
    @ephraimkadamika Před 6 dny

    Utsi is betrayer we don't need him in utm

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc Před 6 dny

    Apodi zoona ndithu,mau amenewo

  • @SamuLameck
    @SamuLameck Před 5 dny

    Jelasi basi mukanakha inu mukanakana

  • @jacquelineboya9529
    @jacquelineboya9529 Před 7 dny

    Zilibe umboni kuti utm yamkana usi dikirani osalubwalubwa apa awo ndimaganizo anu

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Před 6 dny +1

      Zoona anthu akungoyankhula timve okha osati anthu aaaa

  • @charleskaleso536
    @charleskaleso536 Před 6 dny +1

    Complete nonsense, akanakana nthawi yomweija Chilima alipo coz eniake amkavana and anayendetsera limodzi chipani from the grassroots. Izi zitayeni. Touch real things not this trash

    • @AbouzaidahSayeed
      @AbouzaidahSayeed Před 6 dny

      AKulankhula ma nonsense paliponse kumangofuna kuipitsa munthu

  • @MasausoMsiska-rz3id

    Traitor