Bon Kalindo Ndi Guru lake la Malawi first ayankhura izi pamene anapangitsa press conference lero

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 26. 08. 2024

Komentáře • 172

  • @user-mg5yy5hk9t
    @user-mg5yy5hk9t Před měsícem

    Anganga Alula malawi fist member all the way from mangochi mamatiyimilira mr big man keept up mangochi yosaopayo

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před měsícem +8

    Ndipo athu inuyo tchito mukuigwila mulungu azikusungani ndi moyo maka Mr boni kalindo simutopa mwamangidwa kambili mbili mukanakhala wina bwezi mutatisiya ife athu osauka sikuti ndinu Muthu ovutika ayi koma mumasiya pogona pabwino zakudya zabwino kukagona Malo onyasa chifukwa Cha ife aphawi kuzipeleka m,sembe pokhapo mulungu adzikudalitsani ❤❤

    • @RiyemaDomybusiness
      @RiyemaDomybusiness Před měsícem +1

      Exactly 💯💯 bon amatiyimirila ampwawi

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d Před měsícem

      @@RiyemaDomybusiness sure tidziwapephelela ndithu athu amenewa

  • @VungaQueen
    @VungaQueen Před měsícem +9

    Boni Kalindo munthu wotiyimilira 🔥🔥🔥

  • @Moses51
    @Moses51 Před měsícem +3

    The Dc bon kalindo keep up update 💪💪🇲🇼🇲🇼💯 osawopa

  • @user-ez8uk7py8n
    @user-ez8uk7py8n Před měsícem +3

    That is true it needs all Malawian to vote as long as he/ she is Malawian Mr president keep continue loving your poor people abd our country Malawi proud of you thanks

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Před měsícem +4

    I respect your Mr nkalindo together with Malawian fest and the cautrry everyone DC is so powerful as well and you are always welcome to our team of Malawi wholld my Allah bless you always about the what happened with Malawian

    • @esaMoha-dm4kj
      @esaMoha-dm4kj Před měsícem

      I am a Malawi but now I'm in the sauth Africa estan about working on

  • @WysonJalamu
    @WysonJalamu Před měsícem +8

    Big up the DC osatopa, osafowoka, osawopa malawi ndi wathu uyu, tili limodzi pa nsewu basi.

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g Před měsícem +9

    Please please ife TIKUFUNA ufulu wathu wovota a MCP asauchotse ponamizira ma id, aliyense akuyenera kukavota popanda id

    • @Franklifo2217
      @Franklifo2217 Před měsícem

      Nzelu mulibe enanu! Anthu omwe mumalephelesa malawi kutukuka🙌

    • @hudycorex1893
      @hudycorex1893 Před měsícem

      Inu amzeru kwambiri?​@@Franklifo2217

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c Před měsícem

      Anzeru ndinuyo? ​@@Franklifo2217

  • @MussaHassani-zg1hm
    @MussaHassani-zg1hm Před měsícem +1

    This is our president kalindo thanks so much for your help Malawias

  • @DavieBinzih
    @DavieBinzih Před měsícem +1

    More fire mr kalindo we proudly of you keept up we love you

  • @YousufMpunga
    @YousufMpunga Před měsícem +3

    Ndine Yusuf wakumangochi kmnso amalawi amene Ali kumaiko akunja apasidwe mwai wovota kuchokera kunja konko kumene ali

    • @patrickmacheso5062
      @patrickmacheso5062 Před měsícem

      That's true, we need to vote and choose the President that we want not this Manyaka Government, but the problem is Akazembe athu sathandiza or kuwapempha kuti atipatse mwayi ovota.

  • @WezzieChimuzi-ek7bk
    @WezzieChimuzi-ek7bk Před měsícem +1

    Good job my people Ambuye azikutetezelani ndi mwanzi wawo nthawi zonse ..

  • @user-uf4db7im7d
    @user-uf4db7im7d Před měsícem +1

    This government must go

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q Před měsícem +1

    yaa wa mcp ngati akunyasidwa ni boni karindo asavere khani zake ayi chonde ife anthu osauka tiyeni tizimuvera boni koma uzayime iwe boni tizakuvotere

  • @user-uf4db7im7d
    @user-uf4db7im7d Před měsícem

    Every malawian should be in a possession of ID, If the NRB is failing to reach all malawians for ID registration, you should expect Malawi to be on fire, because voting results will not be accepted, People have rights to vote for who they want not rigging.

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o Před měsícem

    The Dccccccc Booooooooon kalindo inu nde anthu oti mzika zamalawi tizikupemphererani kwambili 🙏

  • @NellieKabvina
    @NellieKabvina Před měsícem +1

    Pa ziphatsopo ndie zikudabwitsa zikupezeka kuti anthu ambiri akumadziwa tsiku lokuti akumaliza kupanga ma ID,,,sakulengeza tsiku loyamba anthu ambiri akudandaula

  • @harrisonlowheat6569
    @harrisonlowheat6569 Před měsícem +1

    My president

  • @RemaniNkhoma
    @RemaniNkhoma Před měsícem +1

    boni karindo tingopita mawa bwanji pa sewu kuti agaru awa tiwakhawurise

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 Před měsícem

    Lets presure dem evo!....aluta continua!

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e Před měsícem

    Good move Malawi First ❤

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Před měsícem +1

    I respect your nkalindo bisid ashankwela and everyone else has been in the path of mcp I don't respect anyone anymore because the people who keep and keeling Malawian people 2025 mashall Allah bless you nkalindo 😮😮😮

  • @ChristopherMadulira
    @ChristopherMadulira Před měsícem

    Congugulations Mr DC ntchito mukugwila anthu inu only God bless you ❤❤❤❤❤

  • @AnussaAlli
    @AnussaAlli Před měsícem

    Big up the DC Bon kalindo continue timakunyadlan❤❤❤❤❤❤🎉🎉

  • @jogechawa6192
    @jogechawa6192 Před měsícem +2

    Bon Kalindo and malawi first our hope basi

  • @dawsonwaya4722
    @dawsonwaya4722 Před měsícem

    Za ziiiiiiiii munthu unalephera kuimirira constituency ndiye ukati amalawi osauka aaaa zangokuvutani Moya, .

  • @OdettaLowrence
    @OdettaLowrence Před měsícem

    Ulemu wanu Mr Born 🙏🙏🙏🙏

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z Před měsícem +1

    Boni karido ndikatundu

  • @SamKaposa-i5c
    @SamKaposa-i5c Před měsícem

    Viva malawi first Richard mphepo umadziwa kuyankhula more fire dc

  • @Okalekale
    @Okalekale Před 25 dny

    Tikufuna tidziwe kuti ndi ndani amapanga sponsor gulu lanuli Mr.Kalindo?.The nation should know if you claim to advocate for transparence.

  • @BacklinebwanaliBwanali
    @BacklinebwanaliBwanali Před měsícem +2

    Akupatsen moyo was utali

  • @user-dq9oe8sp8k
    @user-dq9oe8sp8k Před měsícem

    Ifetu though tilibe ma ID kma tikazavota
    Angoona kuzinamidza agwapewa
    Fireeee the DC❤

  • @KeftonChimaliro
    @KeftonChimaliro Před měsícem

    Iyayi zonsezitu akupangazi akufuna ndalama mtambo samachitaso chocho anango kuwapatsa zochita ndikungokhala duuu osayakhulaso amalawi anthuwo ndi amodzi Lucia's. Anayimba kale

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer Před měsícem +5

    Wa mcp ngt born kalindo amakunyasa usamaver nkhan Zak iwey ndy opanda zelu ife tikufuna dziko libwerer ngt kal osat mukumakambo shem on you 😢😢😢😢

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Před měsícem

    Well done guys kpt up

  • @YohaneChitapini
    @YohaneChitapini Před měsícem +1

    Mumakwana ndipo ndinu nokha boss ndagwada ndikumvesela

  • @MikeKoloko
    @MikeKoloko Před měsícem

    Mumatiimilira, big up

  • @usherjamson174
    @usherjamson174 Před měsícem

    Mulungu azikhala namu guy's 💪💪

  • @MercyJohnsonkanchure
    @MercyJohnsonkanchure Před měsícem

    Mr Kalindo Mulungu azikupansani zeru zakuya ngati Solomon ❤

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo Před měsícem

    Never give up guys let's see what happens

  • @ShariffAbdul-m9t
    @ShariffAbdul-m9t Před měsícem

    I salute you

  • @TiyamikeMakande
    @TiyamikeMakande Před 28 dny

    Mumatiuankhulira ndinu bwana ,mutiyankhulireso za ndrama za masiye ku Capital hill Chaka chino nchachitatu ndrama sakutipatsa tikuvutika ndi ana

  • @RanaQari-py4bd
    @RanaQari-py4bd Před měsícem

    Mumakwana guys we love you all the time 🙏🙏🙏🔥🔥🔥🔥

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Před měsícem

    Malawi first all the best u are representing poor people. To be honest Malawi is the poorest country in the world our leaders are selfish we are going backwards.

  • @AlidWidon
    @AlidWidon Před měsícem

    Wosawopa bon kalindo tili limodxi 💪💪💪🔥🔥🔥👆👆

  • @AndrewNyondo-ut3gk
    @AndrewNyondo-ut3gk Před měsícem

    King David bon kalindo the DC❤

  • @lastonkandiyado4526
    @lastonkandiyado4526 Před měsícem

    Respect 🎉🎉🎉

  • @HarrisonMangani
    @HarrisonMangani Před měsícem

    They need to address those issues other wise Mmmmm panunkha mphira

  • @nelsonmhango7515
    @nelsonmhango7515 Před měsícem

    Inu ndi king

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Před měsícem +3

    Pick up guys chilungamo ndimwano

    • @patrickmacheso5062
      @patrickmacheso5062 Před měsícem

      Ndimayesa ngati mukhala kumbuyo kwa a name anu kkkkkkkk let's fight together, this country is belongs to all Malawians not MCP only.

  • @RanaQari-py4bd
    @RanaQari-py4bd Před měsícem

    🙏🙏🙏🙏🙏 Thnx good work

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 Před měsícem

    The DC ❤

  • @KhalidwePentani-c6q
    @KhalidwePentani-c6q Před měsícem

    Zopanda ntchito izo akalindo mumangofuna udindo ngat mungakwanitse kutumikila dziko aaaa zawumbuli

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo Před měsícem

    Congratulations mr DC

  • @GodisoneNoel
    @GodisoneNoel Před měsícem

    Asirikali achirendo muzikorathu zichepe mr DC

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf Před měsícem

    Only GOd Bless you DC

  • @MuhammedNtaba
    @MuhammedNtaba Před měsícem +1

    ❤❤❤ The DC

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Před měsícem +2

    Akumangeni ngati mwaphwanya malamulo dala mbuli

    • @kenmasta
      @kenmasta Před měsícem

      Ndiye mmene akumamumangamo ndiye akumamupeza ndi milandu yanji,,,,..ndaletu zisakusokonezeni mchimwene andale amabwera amapita koma Malawi adzakhala yemweyu ndiye let's love Malawi.

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Před měsícem

      @@kenmasta mwanena nokha awa asiyeni koma akanalankhula zinthu zambili ndi za against popeza ine ndinapanga nawo compain ndiye sanandipatse udindo awona, zimenezo ndi zabodza,chikuwawe sichimanga dziko amwe awa ndi a ndale musokonekera sayamika ndi ankhwidzi amafuna zawo ziwayendere kalindo akudya makobidi inu mukudya nawo 🤗🤗 ayi so bola yesu

  • @user-dy5bj9ck5e
    @user-dy5bj9ck5e Před měsícem +3

    The DCCC

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli Před měsícem

    Good move bafethu salute you

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 Před měsícem

    Point of correction not guru lake koma Born kalindo ndi guru la Malawi 🇲🇼 first

  • @YohaneChitapini
    @YohaneChitapini Před měsícem +1

    Guys inu musazafe mulungu azikudalisani

  • @PempheroMoleni
    @PempheroMoleni Před měsícem

    Firr the DC

  • @EliasMcray
    @EliasMcray Před měsícem

    Go go ahead

  • @AnockyDavidd
    @AnockyDavidd Před měsícem

    Congratulations to all

  • @gracetjomane-jj3ib
    @gracetjomane-jj3ib Před měsícem

    Kutundu uyu the DC❤❤❤❤❤❤

  • @SueWahna
    @SueWahna Před měsícem

    Big up Malawi first 💪💪

  • @Fridayasani
    @Fridayasani Před měsícem

    Osawopha Bon kalindo tikukupembela kwamulungu Kuti anzikala nawe kwina kulikonse komwe udziyenda

  • @ambeweburton
    @ambeweburton Před měsícem

    Timenyeleni nkhondo please mulungu imvani kulira kwathu

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e Před měsícem +1

    ❤❤❤❤ guys

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Před měsícem

    Amarawig fct muri nbi mfunbo zabwini timakuyamikirani

  • @InnocentKavalo
    @InnocentKavalo Před měsícem +1

    Zoona big umakwana dc

  • @Malambia
    @Malambia Před měsícem +1

    Mr kalindo ulemu wanu

  • @ritchardchakuma5725
    @ritchardchakuma5725 Před měsícem +1

    Apomwayikwanisa maiko enasaziwa Chichewa pakufunika ayaluke mbavazi 💯🔥🔥🔥🔥🔥

  • @kurhikhoza8298
    @kurhikhoza8298 Před měsícem

    Tipiya pa sewu akapanda kuyakha

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z Před měsícem

    Zikomo boni karindo umatiyimilila big Kom amalawi sitimayamika

  • @user-dy4gc2hr5e
    @user-dy4gc2hr5e Před měsícem +1

    Good move

  • @AgnessChiwalo
    @AgnessChiwalo Před měsícem

    Your good man bon

  • @LukaJaulanchirwa
    @LukaJaulanchirwa Před měsícem +1

    You people you thinking harder that is good Diction thank chakwera is not thinking

  • @chikoko-uj2tt
    @chikoko-uj2tt Před měsícem

    Salute 🫡 The DC

  • @ntandokazindzwana3083
    @ntandokazindzwana3083 Před měsícem

    Fire fire tili pa mbuso pa malawi oyambirira

  • @JafaliAjusa-zg2xi
    @JafaliAjusa-zg2xi Před měsícem

    Respect Mr

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm Před měsícem

    The DC'S mwana woooopsa kwambiri chilungamo chiyende ngat madzi.

  • @AgnessChiwalo
    @AgnessChiwalo Před měsícem

    ❤❤❤ good news

  • @shephardlonex3371
    @shephardlonex3371 Před měsícem

    Booooooooni kalindo

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo Před měsícem

    Go konko bwana DC❤

  • @HajaSande
    @HajaSande Před měsícem +1

    Zikomo kwambiri umawona patali

  • @PreciousKARINGANIZA
    @PreciousKARINGANIZA Před měsícem

    Tilikomweko

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj Před měsícem

    Following with all my chidwi

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 Před měsícem

    I'm sure, the government you will grant our request

  • @MaryNgola
    @MaryNgola Před měsícem +2

    Mmene wafikira Malawi alipodi amene akumamuona uyu kt akupanga zolakwika? Iweyotu wa MCP nkana akukubowa

  • @shephardlonex3371
    @shephardlonex3371 Před měsícem

    Munene kuti ife ngati A Dpp

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Před měsícem

    ❤❤❤💯💯🔥🔥🔥

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Před měsícem

    Auzen anthu adyerawo amve ndithu

  • @JoshuaNyirongo
    @JoshuaNyirongo Před měsícem

    Go konko..

  • @user-hr6dj4xc8l
    @user-hr6dj4xc8l Před měsícem

    Koma mukuvutikatu kwambiri, munayambilira muja

  • @user-ru6fc3qy5n
    @user-ru6fc3qy5n Před měsícem

    Zilibwino kwambili osaopa

  • @kashmirmohakashmirmoha8659
    @kashmirmohakashmirmoha8659 Před měsícem

    Ulemu wanu DC😊😊

  • @ShadreckChimaimba-l9y
    @ShadreckChimaimba-l9y Před měsícem

    Kunoso kwachitika zodabwitsa kunkhoma

  • @ShadreckChimaimba-l9y
    @ShadreckChimaimba-l9y Před měsícem

    Osatopa big