Video není dostupné.
Omlouváme se.
Další v pořadí
Automatické přehrávání
Fredo's speech - Final Candle for SKC at Zingwangwa Youth CentreFredokiss
zhlédnutí 34K
BON KALINDO LERO PA 13 AUGUST 2024 |DZIWE TV
zhlédnutí 20K
Koupím Barče Cokoliv Co Trefí Šipkou!DodoCZ
zhlédnutí 74K
Survival Skills: Steam Distiller for Dirty Water in Extreme Conditions. #survival #campingSergio Outdoors
zhlédnutí 17M
Ženu pronásleduje vrah #horrorshorts #shorthorrorstory #shorthorrorstoriesPrézovy noční můry
zhlédnutí 194K
Symmetrical face⁉️🤔 #beautySwasti Ji
zhlédnutí 14M
UTHENGA OCHOKERA KWA SAMEER SULEMANI |DZIWE TV
zhlédnutí 655
President Mnangagwa officiates at the Defence Forces Day Celebrations at Rufaro Stadium 2024Rory Studios News
zhlédnutí 360
ZA MAPASPORT ZAVUTA BOMA LAPATSIDWA MASIKU OCHEPA KUTI LIYANKHE |DZIWE TV
zhlédnutí 3,5K
FDLR, M23, WAZALENDO,...MENYA ICHIHISHE INYUMA Y'INTAMBARA IHORA MU BURASIRAZUBA BWA DRCNonaha Media
zhlédnutí 707
Latest On Changing SADC Venue, South Africa Ready To Mediate Talks Between Chamisa And MnangagwaZim Confessions And Deep Secrets
zhlédnutí 1,2K
Do u want the result? 🤔 Elsa and Nevada #elsarca #tiktokElsa Arca
zhlédnutí 17M
Jak rozebírat tyhle skleněné mlýnky na sůl, pepř a další koření? 🤔Vojta Dalekorej #WRTECH
zhlédnutí 334K
WHO CAN RUN FASTER?Zhong
zhlédnutí 15M
Lifehack on how to make a salt bath bomb.Mamasoboliha
zhlédnutí 10M
Comfortable 🤣 #comedy #funnyMicky Makeover
zhlédnutí 15M
What is going on? 😂 (via haechii_br/IG) #shortsSportsNation
zhlédnutí 15M
Sad To Announce I Did Not Qualify For Mens 2024 Olympic Gymnastics TeamThe Rock
zhlédnutí 11M
It is very very difficult for the UTM to make an alliance again with the MCP and the reason it's not only that they've killed Saulosi Chilima but even before Chilima died the alliance was already broken and Chakwera openly said that he'll stand for the MCP as a presidential candidate in 2025
Umenewu ungakhale mgwirizano wabwino kwambiri.
Yes in politics there is no permanent enemy,UDF ,DPP, UTM can upset the tables.
APM is not alone for campaigns
MCP ndi chakwera akuchoka kale, palibeso kuwina apa, a Malawi akuzunzika kunjaku.
Who cares, pathako pamako
@@robsontyg3928inunso ndia chitsiru bwanji...kulalata zomwezi
@@fanie6913 mahule, chomwe umadziwa nding'andula kumatako kwako kununkhako
Ndizofunikira km chilima ndiye ai ndiokula mtima.
Udf ,dpp, musalole chilima ai.
Good Message
Chilima ndi okula mtima we he must stay there in Tonse Alliance!!!
Kuli zinthu 2025
Yes
Mukuti Chilima ndi mistake munampatsako mpata kuti alamule kapena ndi zomwe mumalota
Akulu akuluti posankha msogoleri amayang'ana khalidwe,satenga aliyetse chifukwa ndi wandevu za waiti ayi, ndiye ziwani kt APM anamuona kt alibe zomuyenereza kukhala msogoleri. Ndiye vuto ndilokuti ziko lathu lazaza ndi anthu mbuli zophudzira.
Ndye angakhale president ndani of coz there is no permanent udani in politics
good news that's we want thank u
APM ,UDF , UTM apange zomwezo( chakwera watinyasa matongo yake
😂😂
Ndipo kwambiri
😂😂😂😅 yoooo
Amenewo ndi mantha
Awona nyenkhwe sanati akang'wing'wiwo
Joker waife tampanga kale withdraw❤ chilima
Okay ziomo 🔥🔥🔥🔥👍👍
Ndipo musazikonde kapena kuzengereza pangani zomwezo
Dpp iyende yokha ngt amalawi akufuna zinthu zisinthe
Kuti anthu azizaba bwino pitala akugona. Pa mpando
Kuno Dpp ndiye yapita apa mwawonaso waboma apa 2025 muwonaso
😂mabodza ku Malawi 😅.. muzitorere
More 🔥
Chilima adzatsogolere adzawina coz chilima Ali ndi value pa ndale
Nkhani ndiyomweyo, koma pa nkhani ya president sangakulilane mitima?
Zipani zigwirizane kuyendera limodzi kuti mcp isaone mpata
Yes ndizoona zizacitikadi mukunenazi
Ndizoona zomwe akuyakhulazo Kuti MCP igonjele UTM zithu zikatelo zikhala bwino app AI awasiye apange zawo
Migwirizano imeneyi are not for development
Hehehe DPP president wake ndani? Pitala hu za 80+ana ake anayi😂😂😂😂😂
Dpp ukulowa m,boma awa alephela basi ayenela kuvomeleza
Mugwilidzano ukhodza kukhalapo,,,,,funso!!! Kodi pa athu atatuwa president a khala ndani??????
Kod mwat gogo wathu apm pano ali ndizaka zingat 😂😂😂😂 koma azakwanisa kuyenda from Nsanje to Kalonga Nkhotakota to Mchinj
Amwene umburi inu eee mukura Kuti?
Utm ikagwele pulesident wa utm ndi wosapanganika inuyo ngati mukujiya ya utm mwagwa nayo amalawi salola
Olo DPP ithayima payokha izawina chifukwa chakut ndi mene ilili panopa Malawi 🇲🇼 Sali bwino Malawi 🇲🇼 wathu tikulila ndimene akutipangila Amene akulamulia Lero lino
OK
I'll never trust any alliance , onsewa ndimbava zeni zeni ndipo alibeso phindu
NO PAIN NO GAIN TIMANDIKIL ZIMENEZ VIVA UDF VIVA APM VIVA UTM
Any Government involving chilima mistake
But alliances have already failed
Zikhala bwino zagwilizano
Ndizoona mcp ikapanda kugonjerana ndi utm chawopalibe a mcp azamva nkhwangwa ili m'mutu😂
Zikumveka ndthu bro ndpo izi ndizotheka even a Malawi ambiri adzalikonda ganizo limeneri fog sure
Maganizo abwino tipange zoti mcp isalamulirenso mmalawi muno
Nice alliance
Atsitse katundu ngati satelo achoka ndipo Malawi tikati no is no.
Wapenga matumbiyu akufunako ndalam😅😅😅
Udf ndi Dpp zilibwino ,koma Utm aaaaa no idea sir
UDF AND DPP THAT'S WOLL WILL BE BETTER WE DON'T WANT MCP ANYMORE IN MALAWI .
Mgwilizano wa DPP, UDF and UTM ukadzangiwina mu 2025 mkuyamba kulamulila mmmmmmmmmmmm Chakwela ndi nduna zake tidzambwandila ngati nkhuku wa ku prison because aononga misonkho ya a Malawi ndie tidzafinya banja lonse la Chakwela,,,,,,adzabweze zathu
80yrs wakalamba mdalayu
UTM ikhale komko kwa a Satana aliko.Ife DPP+UDF+Aford we can agree.
UTM not good guys
Gwirizano ukharepo basi chakwera watikwana
Tinned momveka pano popanda migwilizano palibe chipani chingapambabe 50+1 ilipoyi.
Komaso iwalani kuti utm ingapange alayansi ndi dpp. Zinazi mukungoganiza
Chilima adapangidwa addicted wa mgwilizano
1:32 Mcp ndi UTM akuyenela Kuykendala be limozi asaiyane
Koma zoona chilima mukumufunaso ine ayi
Ndipo akapanga chibwana chilima alamulazikol
Ndiye atapanga mgwilizano PPP UTM. UDF president adzakhala ndani poti chilima watopa kukhala wachiwili. Komaso Gogo muthalika akufunaso kukhala president. awo ndimaloto achumba sizingatheke
Kkkkkkkk azakhala chilima president Peter sakufunatu kuimila koma akumukakamiza
Mcp kusamva akuonangat ndalama zingagule vote
Yes,ziyenela kudzakhaladi choncho kuti mcp idzamve kupweteka
Ngati UTM , udf achite alliance ndi dpp ziribwino coz ndinthwi ya chilima ndi atupele kukhala atsogoleri chifukwa muthalika wakula ndiye kuti anyamata awiriwa azatenga upresident mmodzi mwa awiriwa
Nkhaniyo ndiyoonadi
Here we go ❤
MCP sitikuifuna lokoitatheratu
Zosezi ndi udyera mwala oyendayenda suyanga ndere
Pangani zomwezo basi mesa chilima anamukana awa nanuso pangani mugwirizano basi😂
MCP NDIYAMPHAMVU KOMASO NGATI UTM INGAPITESO KU DPP TIITCHULA KUTI NDIYOYENDAYENDA NGATI MPHEPO ILIBE KUKHAZIKIKA PAMOZI AKANAKHALA KAZI TIKANATI NDIHULE WAKULU KOMA ZONYOZA AZAWO AYI
MCP sikuwinanso or mutasakanikilana ndi UTM
What ever allayance bola chilima atsogole apo ayi zivuta
Chilungamo chimawawa SKC ndikatundu ameneyu
50+1adzapangitsa kt alliance ichitike chifukwa Pali be adzapeze 50+1% koma chakwera ndi khuluku
Phatikizanani tizakunyeyeni dziwani dziko Lamawi a landlord anatenga
Chilima ndye ai sitikumufuna nd khuluku olo APM sangalole zmenezo
Zitatelo DPP utm plus udf can help to rescue malawi
Ndipake DPP ndi UDF kupanga ngwirizano zikhonza kuthandiza ziko lamalawi akazalowa m boma koma azaonese chisanzo cha bwino
Apa zikuyendera KUt chilima abwerere zachitika manyazi kuziko izi
Aaaaa zimenezo tilibenazo ntchito aphatikizanebava zokhazokha mbuli zidzawavotela Koma ozindikira sangapange apa asowa kolowera asiye ndare azipanga zina
Dpp woyeeeeeeeeee with UDF. + UTM. 2025 mcp inya manyi.
Mwakhwana akalindo munthu wamkulu
Bola apange zomwezo
Compaign ya ulendo unoo nde kuli zinthuuu🤣🤣🤣🤣
Kkkkkkkk palibe chomwe mungapage
Ndipo akapanda kumusalamala Chilima apita nao DPp
Atrue news
Not UTM chifukwa Chikima has no direction
Gwilizano wa UDF ndi DPP ndiwakalekale Musachite kukaikaso ali limodzi paka 2030 woo
Zoona bhola zisakare ntchotcho
Chakwera aonesa ubusa wakedi kutidi anali woona,komanso apange mipingo kugomezeka kapena ayi kutengela iyeyo.
Km chilima vuto ma joke amamuchulukila komaso mmene wapangila zinthu zake aaaaa kukhululupilira kukuvuta tsopano😊
Chilima ndi chipani chale musyireni akhale nacho payekha
Chilima ndiokanika ndipo ndiopsya mmaganizo
Atha kupanga ubale koma DPP ikazalowa mmboma mumuona azagalukilanso mmutu mwa Chilima simumayenda bwino
Ndip kwambiri ayiwala kale kt chilima ndioyipa mtima
Utm ikhalebe komwe iliko Chllima not a trusted young guy.
Pangani zomwezo guys ife chakwera watikwana sitikumufunaso talira mokwana koma mulungu ayakha popano pasara pang'ono chabe
MCP siyingawine
That's gud
Dpp udf komanso afford ine utm toto ndakana,
Thanks very much appreciate
Ndipo tingompempha Chihana kuti nayenso azajoine mgwilizano umenewu enawa owone nyekhwe
Chihan akanabwera ku dpp
Kodi guys mzungu ndiwosaloledwa kuyimila zikolathuli pazisakho
That's only solutions mzungu bola
Apo niboma kale mcp ili mmadzi
Zonse zomwe mukunezi mzanzelu koma kumadziwa Kati dpp inaluza ililimodzi apamukatengela kudzikonda malawi akhalabe pamavuto
Add Aford and PDP
Akuyenela Kuykendala limodzi kuti akwanilitse maso phenya awo 2063