Kamuzu Chibambo Kutsimikiza Kuti Tonse Alliance Sakudziwa chimene Akuchita|Amamangidwa Mmasamba
Vložit
- čas přidán 17. 03. 2024
- We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
Mukutipsa nkhani zabwino komano zomaduladulazo ma discussion sizikuchita bwino ai
Mumene tayambira sizikuyenda sizikuyenda iye akukhuta osatenga action bwanji amalawi
Boss this si good BUT DONT INTERUOT THE DISCUSSION YOU ARE MAKING IT SO LOUSE, LOW, LOSE WAIT
Brian Banda ndi Kasakula amamutukwana kwambiri APM. Koma panopa they are regretting chifukwa mbuzi yayo Chakwela akulephela kuyendesa dziko momvesa chisoni.
Ndipo Brian banda ampepese EPM ananyoza koopsa
Kkkkkkk kodi munthu modzi nkuzunza amalawi ambiri mbiri malawi army osatenga boma bwa mupaka ti vote
amene aja ntchito imaziwa iwo ndikulanda makala basi
Amwene inuso mumaononga zabwino ndi ma comment anu upusawo bwanji osasiya program mene ilili bwanji
It is commentary... anyway ,thanks for your support
Martha chizu.ma started very well but it was blessing in disguise
Mumene tayambira sizikuyenda sizikuyenda iye akukhuta osatenga action bwanji amalawi