![MALAWI WATHU](/img/default-banner.jpg)
- 121
- 603 201
MALAWI WATHU
United Kingdom
Registrace 27. 02. 2023
This a channel that we talk about anything to do with Malawi.Things that affect Malawi either positively or negatively.This ranges from politics, entertainment,economy to religion.So join us as we discuss these things.
UTM YATULUKA MU TONSE ALLIANCE...Zitha bwanji ndi a Michael Usi?
UTM,a Tonse Alliance partner with MCP has just announced that they are out of the alliance..watch the Press Announcement as it happens...
zhlédnutí: 253
Video
Osayiwara Kuti Zinayamba Bwanji?
zhlédnutí 3,5KPřed měsícem
We talk about the benefits of mines in Malawi and who are the beneficiaries?Does Malawi really benefit from them?
A PETER MUTHALIKA ASIMIKIZA KUTI AYIMASO || ZINTHU zakwera MITENGO chifukwa cha a CHAKWERA akutero?
zhlédnutí 531Před 2 měsíci
Following the Peter Muthalika Rally in Blantyre at Njamba Park
Mabungwe Omwe Siaboma AKWIYA Ndikuthesedwa kwa Mlandu wa Dr Saulosi Chilima...Mverani Nokha!!
zhlédnutí 1,3KPřed 2 měsíci
CSO Press Briefing..
Dr Saulosi Chilima Milandu YATHA||TSOPANO 2025 ULENDO UYAMBIKE!!
zhlédnutí 3,1KPřed 3 měsíci
Malawi Government has just discharged all corruption charges against the vice President Dr Saulosi Chlima...We say this when battle for the 2025 General Elections starts!!!
A Chakwera Akuti Mabvuto tili Nao Ku Malawi ndi atempolare....Njala,Katangale,Zinthu kudura?
zhlédnutí 1,1KPřed 3 měsíci
We talk about the benefits of mines in Malawi and who are the beneficiaries?Does Malawi really benefit from them?
KODI A VAISI PULESIDENTI AYAMBA KUTUMIDWA NDI A PULESIDENTI CHAKWERA PANO?
zhlédnutí 11KPřed 3 měsíci
We talk about the benefits of mines in Malawi and who are the beneficiaries?Does Malawi really benefit from them?
KODI AKUPINDULA NDI MIGODI KU MALAWI KUNO NDI NDANI?
zhlédnutí 388Před 3 měsíci
We talk about the benefits of mines in Malawi and who are the beneficiaries?Does Malawi really benefit from them?
Ambuye Mntengeni| Mowa Wachilendo Wagwedeza Mnzinda wa Blantyre|Anthu 8 Afa Kale...
zhlédnutí 1,2KPřed 3 měsíci
We are discussing the mysterious alcoholic drink which has caused 8 fatalities in Blantyre Malawi
Aphungu a DPP kukunthana mu Paliyamenti|Age Bill Yavuta!!!
zhlédnutí 2,7KPřed 4 měsíci
We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
Mwina Tinayiwala Mmene Zinaliri 2019 Kuti Enafe Tilowe M'Boma?Kotsutsa Kutatiphweteka !!
zhlédnutí 3,8KPřed 4 měsíci
Chilima press briefing 20219..
A John Kapito Akuti Katangale Wanyanya ndi Boma la Tonse Alliance?
zhlédnutí 7KPřed 4 měsíci
We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
Kamuzu Chibambo Kutsimikiza Kuti Tonse Alliance Sakudziwa chimene Akuchita|Amamangidwa Mmasamba
zhlédnutí 3,9KPřed 4 měsíci
We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
Mmene a Tonse Alliance Akuthawira Kulephera Kwao Posintha Malawi| Kuloza Chala Ogwira Ntchito m'boma
zhlédnutí 2,8KPřed 4 měsíci
We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
AKUSINTHA MALAMULO KU MCP CHIFUKWA CHAKULOWA KWA ULADI MUSSA M'CHIPANIMO?
zhlédnutí 2,6KPřed 4 měsíci
Peter Muthalika Press Briefing in Mangochi, Malawi,president of DPP
Peter Muthalika KUZUZURA President Chakwera kuti Wasokoneza Malawi...Amuchosa Chakwera 2025!!
zhlédnutí 3,2KPřed 4 měsíci
Peter Muthalika KUZUZURA President Chakwera kuti Wasokoneza Malawi...Amuchosa Chakwera 2025!!
Kalanga Ife,Tithawira kuti?Akuti Namondwe Filipo Akuphikidwa pa Nyanja ya Indian Ocean Kubwera ku MW
zhlédnutí 2,3KPřed 4 měsíci
Kalanga Ife,Tithawira kuti?Akuti Namondwe Filipo Akuphikidwa pa Nyanja ya Indian Ocean Kubwera ku MW
Zayamba KUULULIKA ZAMALIFOMU ANAPELEKA CHILIMA kwa a PULESIDENTI
zhlédnutí 33KPřed 5 měsíci
Zayamba KUULULIKA ZAMALIFOMU ANAPELEKA CHILIMA kwa a PULESIDENTI
Mneneri Wakale wa MCP Wazomeleza kuti A CHAKWERA AKANIKA KUKWANILITSA ZIMENE ANAWAUZA A MALAWI?
zhlédnutí 9KPřed 5 měsíci
Mneneri Wakale wa MCP Wazomeleza kuti A CHAKWERA AKANIKA KUKWANILITSA ZIMENE ANAWAUZA A MALAWI?
MaBishop Akuti Utsogoleri Wa Masomphenya Kulibe ku Malawi|Akufuna Kutsintha 50%+1 Zikumveka Ngati?
zhlédnutí 14KPřed 5 měsíci
MaBishop Akuti Utsogoleri Wa Masomphenya Kulibe ku Malawi|Akufuna Kutsintha 50% 1 Zikumveka Ngati?
Kodi Aphungu Athu Amatiyimiladi Ife a Malawi kapena Zipani Zao?
zhlédnutí 1,3KPřed 5 měsíci
Kodi Aphungu Athu Amatiyimiladi Ife a Malawi kapena Zipani Zao?
Mmene Anthu awa Otchedwa 'OMENYERA UFULU' Amatipusisira a Malawi?
zhlédnutí 7KPřed 5 měsíci
Mmene Anthu awa Otchedwa 'OMENYERA UFULU' Amatipusisira a Malawi?
Mmene ANASAUKIRA a MIKE CHILEWE chifukwa cha Anthu Asanje ndi Andale!!
zhlédnutí 4,6KPřed 5 měsíci
Mmene ANASAUKIRA a MIKE CHILEWE chifukwa cha Anthu Asanje ndi Andale!!
Mmene John Tembo Anaphera Tsogolo La Kinnah Phiri Losewela Mpira Kunja !!!
zhlédnutí 5KPřed 5 měsíci
Mmene John Tembo Anaphera Tsogolo La Kinnah Phiri Losewela Mpira Kunja !!!
Mary Navitcha a DPP Kuyanka Zimene Anayankhula a Pulesidenti mu Parliament...Kusambwaza SONA !!
zhlédnutí 1,1KPřed 5 měsíci
Mary Navitcha a DPP Kuyanka Zimene Anayankhula a Pulesidenti mu Parliament...Kusambwaza SONA !!
A Malawi Ambiri Akuti a Chakwera Amangodziwa Kuyankhula Osati Kugwira Nchitoyo...Mvelani Nokha!!
zhlédnutí 4,2KPřed 5 měsíci
A Malawi Ambiri Akuti a Chakwera Amangodziwa Kuyankhula Osati Kugwira Nchitoyo...Mvelani Nokha!!
BREAKING NEWS!!! a ACB SANAUDZIDWE KUTI NDALAMA ZAPELEKEDWA KWA SATTAR?
zhlédnutí 2,4KPřed 5 měsíci
BREAKING NEWS!!! a ACB SANAUDZIDWE KUTI NDALAMA ZAPELEKEDWA KWA SATTAR?
Kodi a Nyuzipepala Apepesa Zokhuzana ndi Sattar ndi Boma kuti Contract Palibepo Yanyuwani?
zhlédnutí 885Před 5 měsíci
Kodi a Nyuzipepala Apepesa Zokhuzana ndi Sattar ndi Boma kuti Contract Palibepo Yanyuwani?
TILIDZIWE KHALIDWE la Uladi Mussa|Kodi angathandize a Malawi?
zhlédnutí 7KPřed 6 měsíci
TILIDZIWE KHALIDWE la Uladi Mussa|Kodi angathandize a Malawi?
Mneneri wa ACB KUTHAWA MAFUNSO a Brian Banda Okhuzana ndikuchuluka kwa Ziphuphu ku Malawi!!
zhlédnutí 14KPřed 6 měsíci
Mneneri wa ACB KUTHAWA MAFUNSO a Brian Banda Okhuzana ndikuchuluka kwa Ziphuphu ku Malawi!!
Akomaamakana ndipotimawanyadila
Akamunaamenewo amativesakukoma jo
Is this comedy 😅😅😅😅
Gwaradi sakufunika kumupasa ndarama ayi kuthandiza kwake kuimirire ndi munthu wina azimupangira kaya ndi nyumba iyeyo akapeze yomanga kare ndikumuikamo mmmm zokhudza bwanji kuntchuka koseku 🤔
Jumping Jack !
Zopanda ntchito izi, anthu akuvutika kwambiri kumudzi, okalamba, aumphawi, olumala, amasiye, odwala, osamalankhula mwachibwana kut Mulungu Ali mbari yanu yet zinthu sizili bwino, kulankhula ngati anthu opanda mzeru, palibe chanzeru chomwe mukuchita chopindulira Malawi kuposa kumangomanga wanthu ndi kusintha maina azipatala zoti simudamange ndinu, 4 years just for nothing, shame on you guys, mzipatala mankhwala mulibe, chitetezo taaa, ma school Nde mwakweza ma fees, anthu akumudzi omwe alibiletu chiyembekezo ndipo alibe chilichose akwanitsa bwanji kulipilira Ana awo ma school, chakudya Nde kulibiletu, chomwe mukuganiza mkuti tidzadzitsa bwanji matumba wathu kuti tidzabele zisankho, AGALATIYA opusa, oyamba ndi zabwino kutsiliza ndi zoipa, When I said amalawi akuvutika I mean it, mukamadya bwino kumitundako musamati aliyese a kudya, go to the villages and see how life is, you will cry, anthu a kugona ndi njala and you are expecting those people to go and vote for you this coming 2025 nonsense, MAY The Soul of SKC continue to Rest well and hope he is watching you all,
Ufiti
amapanga sewero
Kuyankhula koputsa kwambili,Kodi moyo ndi wanu??? Inu anthu omvetsa chisoni kwambili
It is supposed to happen.. MCP is a big party sangalore kuberekedwa
Chakwera ndi mbudzi yamunthu
Koma malawi kodi mukhalabwamji? monga azomba ndi azisuzo mumamwalila apanda kanthu kalikose.
Mwagwanayo UTM yakutulukani forever Chakwela kwamai ako
chisankho chabwino koma osanyoza adzanu ayi
Chakwera ndi munthu olephela ....mkazi olanda amavuta
Anamangindwa chifukwa chani
Ayi ndth anthu matha kuvina eeeee😄
Osayiwala chipande ndipowomola
Tso pali chimene wapanga chakwera success! Agalu achabe chabe.
Za ziiiiiiii! Chakwera ndi MCP yake akagwere uko
Zakuvutani bas
2025 president wanu chakwela? Is so sad for Chilima 😢 rest well
Ubwino simuvota nokha
Anthu akuba akugawana ndalama za boma
Mbudzi ya mdzimayi mulungu dzikusunga ndi moyo wawutali pomzunza anthu
Oloko akupaseni ndalama koma dziko lilingati galimoto ngati siiwe dilaiva sungakwanise kuyendesa achakwela alephela
Mcp we no need it again yatizuza mokwana
Chakwela Galu wohipaa
2025votiyo yakuba chani musayi namize fiti yanuyo bozaa Galu lwe
Agalu lnumuzaziona mungotiphe ndinyani wanuyo agalu lnu
Mbuzi iweeeeee meeeee 😂
Ameneyo ndi neneli wakale nanga watsopano watipo chani
Kuzinamiza pamenrpo😢😢😢
Fack you all you taken advantage our country fack you all amcp
Ohhhhh amenewo nde ma results aifa yachirima inuyo Malawian okuzidwa?
Pamsana pako iwe, koma ukuliona dziko, chamba et kuyankhulila kumaliseche kt pant adzimva kapena pakamwa
Oooooh yes, chakwera emweyo mukudya naye bwino
Wandevu ameneyi sanasochere Wakuda angapezeke kwao
Ndi chimene chinamupha chilima
Kuyankhula komaliza mawu anuwo sumuzayankhulaso 2025 mukugwa
Kd mcp ndichan pamalawi
Emusipi idziwe kuti kunja kuno kuli Mulungu ndipo Mulungu sangalole Kuti Amalawi tipitirize kuvutika
Chakwela ndiye chani
Fundo sinakhazikike amtolakhaniwa
good story scripting i like this
Very Sad Story 😔😔😔😔😔
Nice
Tembo
From Tz,nanenso ndinamva kuti anamwalila,ndadabwa kuona alimoyo
Program yabwino