ZOMWE ZACHITIKA KU ESCOM YAKU BLANTYRE🙌🙌🙌🔥

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 6. 09. 2024

Komentáře • 263

  • @ulemusopa965
    @ulemusopa965 Před měsícem +22

    The ESCOM guy knows his stuff, u can tell from the confidence and the content presentations,KEEP IT UP

  • @PeterKhumbilaZimba-ql9ue
    @PeterKhumbilaZimba-ql9ue Před měsícem +4

    If Usi can be in the office just for two years Malawi will change believe you me my fellow malawian's.

  • @user-xf6tf3mp7m
    @user-xf6tf3mp7m Před měsícem +7

    ❤❤❤ vp woyeeeeee ineso chimozimozi ndinalipira 2021,pakanapano sanandiyikile , gwilani ntchito bwana wanga mulungu azikuthandiza,

  • @harrykadango4871
    @harrykadango4871 Před měsícem +4

    The accountant is well knowledgeable. I like his confidence 🔥🔥🔥🔥

  • @user-lj8ug5lq8c
    @user-lj8ug5lq8c Před měsícem +7

    Mcp take care with this guy if you think u can use this guyz forget about that its a simple guy but taff in mind keep it up Bambo a Sikono

  • @yamikanimwanansi5067
    @yamikanimwanansi5067 Před měsícem +12

    Pena ndikumazimva ngat tidaluza zinthu, boma la chilima ndi abwanawa likadakhara labwino ndithu

  • @joelkachamba715
    @joelkachamba715 Před měsícem +1

    This man needs to become president don't look him down

  • @alickkachepa3801
    @alickkachepa3801 Před měsícem +4

    Keep it up Mr VP this is what we need

  • @chikaonekarh
    @chikaonekarh Před měsícem +1

    Dr Usi he deliver, whatever your political party is, but this guy is doing good work for Malawian keep it up Dr Usi

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Před měsícem +14

    Tikuferanji yabeba 2024😅😅😅😅

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Před měsícem +21

    Akusankha ma office ophweka, chomwe sakupitira ku immigration ndichani komwe anthu akuzuzika kwambiri?
    Akumuwopa ng'oma

    • @thomaschipinda6952
      @thomaschipinda6952 Před měsícem +1

      Because immigration woes are chakwera’s, his son and Mumba made so he knows

    • @dysonfysonchifundo2284
      @dysonfysonchifundo2284 Před měsícem

      Step by step 🪜 neer worry 😁 kk

    • @gibodynasty8201
      @gibodynasty8201 Před měsícem

      Munthu wangoyamba kumene, sangayambire zomwe mukuganiza, ali ndi work plan

    • @StainNkandawire
      @StainNkandawire Před měsícem +1

      Koma ine ndi kuona kuti kwanzeru nkumeneku amationjeza a escom

    • @brysonkambole8670
      @brysonkambole8670 Před měsícem

      You can't do everything once

  • @IsaacJoseph-x1h
    @IsaacJoseph-x1h Před měsícem +1

    that's greatest work in the country of malawi

  • @hourlyview4226
    @hourlyview4226 Před měsícem

    I have started liking this guy

  • @samiyatuimulani5274
    @samiyatuimulani5274 Před měsícem

    I love this guy I like this guy to be a leader of Malawi president I think Malawi.can be changed this guy looks like honest god open the way to him to read us god bless Malawi

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Před měsícem +3

    The way this guy looks at Manganya eeeh, ngati angomupatsa chi mbamaa.😅

  • @EsterNyirenda-y5k
    @EsterNyirenda-y5k Před měsícem +1

    Thumbs up the VP and don't end there gwedezani mose ngakhalenso ku ma office a ma civil servants gratuity mmene anawerengerera 2022 kufika lero ndi yomweyo ,,zofunikanso kukambirana

  • @JonathanMsiska
    @JonathanMsiska Před měsícem +7

    Anthu akufuna mupite Ku immigration mwachangu makamaka pa Mzuzu.

    • @PociahMack
      @PociahMack Před měsícem

      Anthu aku immigration akalakala kulowa pansi

  • @THOMASMCHOKOCHO
    @THOMASMCHOKOCHO Před měsícem +4

    mfanayo ntchito akugwira mwa chilungamo kkkkkk keep it up bro

  • @user-kw7wr4kq9w
    @user-kw7wr4kq9w Před měsícem

    Great work Mr president

  • @JohnThom-om5ke
    @JohnThom-om5ke Před měsícem +2

    I like what Mr vice president is doing. Eya agwedezedwe asamaiwale Kuti Ali apo chifukwa chaife.

  • @aubreyvisuals2416
    @aubreyvisuals2416 Před měsícem

    Uyu Michael Usiyu amafunika adzigwira ntchito ndi boma lilironse lingalowe coz this is stunning

  • @user-hx8rr1mq7u
    @user-hx8rr1mq7u Před měsícem +3

    Bwana ntchito mukugwira keep it up

  • @MansonNyamwela-g5r
    @MansonNyamwela-g5r Před měsícem

    Wow that's fantastic, keep it up don't fear any body you are there for the benefits of Malawian and you make me feel better

  • @MadalitsoChimbalanga-eu6fj
    @MadalitsoChimbalanga-eu6fj Před měsícem +1

    Manganya keep up good work do the same to forest,and water sources

  • @user-ub1mw7ce5p
    @user-ub1mw7ce5p Před měsícem

    We are appreciating your work our VP, that's what we need. Thank you.

  • @glorychakhala2059
    @glorychakhala2059 Před měsícem +1

    Keep it up tsiku Lina mukasuzumireko ku NRB uko kuliso vuto

  • @JohnChikopa-b6s
    @JohnChikopa-b6s Před měsícem +1

    Inu escom ndimanyaga ine ndinalipila magedzi 2021 paka pano koma anthu akumanga nyumba mwezi umodzi kuwalumikizila magedzi

  • @Iqradiss
    @Iqradiss Před měsícem +1

    Nice work vp

  • @PatrickNyirenda-i2s
    @PatrickNyirenda-i2s Před měsícem +1

    Dr michel mumatha tavutika kwatha ndinu mayankho anthu

  • @JaneMwanyongo
    @JaneMwanyongo Před měsícem

    Bwana muzafikeso ku mzuzu Escom ndinalipira 2019 mpaka pano sanayikile magetsi

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 Před měsícem

    Vice State Presedent Dr.Usi, keep it up. Malawi is in a rut professionally.

  • @LumbaniMthala
    @LumbaniMthala Před měsícem +1

    Izi zokha nduzikonda izi Vp mukugwira mtchito keep it up

  • @phillimonmaila4269
    @phillimonmaila4269 Před měsícem +1

    Keep it up Usi

  • @hourlyview4226
    @hourlyview4226 Před 2 dny

    Manganya is sturbon, you can't interfere and influence in the decision making of someones office, the issue here, he is acting on the information which the people are feeding him, koma that is totally wrong, he was supposed to seat on the visitors seat not there, again, he is trying to put pressure on that accountant, I believe he is aware that this man is a professional si mbuli and he is holding a high office so respect is needed asaiwale so kti this guy is a permanent employee and him, his job will end next year

  • @IreenChilingulo
    @IreenChilingulo Před měsícem +1

    Mukanauuza kuti aliyese amene analipila magesi kale kale ayikilidwe magesi pasanathe mwedzi

  • @user-jg6hm3hm6l
    @user-jg6hm3hm6l Před měsícem

    Vp good development and I like it 👍🔥🔥🔥🔥

  • @WelosPhillimone
    @WelosPhillimone Před měsícem +1

    Mupitenso ku immigration Mr VP

  • @austinjailosizuze
    @austinjailosizuze Před měsícem

    Good development bwana,I really like you.

  • @AbdullahaziziAmoswalala
    @AbdullahaziziAmoswalala Před měsícem

    ❤good job mr vp izizi zomwe amphawife tikufuna chifukwa anthuwa amatailira kwambir

  • @lydiabanda3796
    @lydiabanda3796 Před měsícem

    VP mukamatelo anthu aziopa kuchita zinyengo, so Malawi akhuza kusintha kathawi kochepa, well done 👏

  • @ernestchabwerah4144
    @ernestchabwerah4144 Před měsícem +4

    I like the guy wogwira ntchito_yo, anali pa easy ..... Nice

  • @jamesmulangalimatemba5351
    @jamesmulangalimatemba5351 Před měsícem +1

    This is what we need

  • @lydiabanda3796
    @lydiabanda3796 Před měsícem

    Go head 💪💪💪💪💪💪

  • @AbrahamSimfukwe-u2j
    @AbrahamSimfukwe-u2j Před měsícem

    The guys has a magufuli's character

  • @user-dd4pn6uw7c
    @user-dd4pn6uw7c Před měsícem

    😂manganya is learning how to capture the data kkkkkkk

  • @alinafekekentandika7320
    @alinafekekentandika7320 Před měsícem

    Better than the president

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Před měsícem

    Chief accountant 🔥. Big man

  • @felixtembo9602
    @felixtembo9602 Před měsícem

    Keep it up bwana vc.please don't stop this business maybe Malawi can change for the beta

  • @gavinklenzmajawa-nr3jt
    @gavinklenzmajawa-nr3jt Před měsícem

    My vice president.....
    Time is not in his side he just trying to make alot of allowances by creating visits ongowononga ndalama koma sathandiza kalikonse Ku dziko lino iyayi ndi nthawi yanu.masiku tikuchosera away.tikuthothani ndi voti

  • @alinanemaster3549
    @alinanemaster3549 Před měsícem

    Keep the fire burning Mr vp🔥🔥🔥

  • @Mickeykasambula265
    @Mickeykasambula265 Před měsícem +2

    Izizi zikanayamba 2020 ija malawi bwenzi ali pena

    • @pettersen2717
      @pettersen2717 Před měsícem

      Boma linayamba kugwila nchito. Kwathu kuno zachibwana zedi🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @Christopher-xc2ey
    @Christopher-xc2ey Před měsícem

    Ine ndinalipira mchaka cha 2020 mpaka pano sakudzandimangira.escom ndilibe nayo mawu

  • @ayaanchaudhry9370
    @ayaanchaudhry9370 Před měsícem

    Fighting for poor malawians , keep it up chief ,

  • @thomvin9121
    @thomvin9121 Před měsícem

    My fellow accountant ... shaaaa wabvatu

  • @marthachapepa2692
    @marthachapepa2692 Před měsícem

    I hope this supervision, will lead to the good management of the company.

  • @LindeHotel
    @LindeHotel Před měsícem

    Mbambande Mr vp......amationjeza ma guys mma ofesimu...amatitenga ife a Malawi ngat opepera....gwirani ntchito bwana

  • @alinafekekentandika7320
    @alinafekekentandika7320 Před měsícem

    Zinazo addressing the wrong office

  • @elsa1973
    @elsa1973 Před měsícem +4

    Vp is cleaning Malawi wow what a nice job

  • @PetroKachingwe-jf7dh
    @PetroKachingwe-jf7dh Před měsícem

    Keep it up Dr Usi
    Nice job

  • @PeterPatrick-c2r
    @PeterPatrick-c2r Před měsícem

    eish mawa bs ndikupita ku escom kukapanga apply ichichi chitithandiza di amalawi💪

  • @LuchenjeriMnessa2-xx7cg
    @LuchenjeriMnessa2-xx7cg Před měsícem

    Honestly Michael usi ndamufila heavy,mukuitha bigy

  • @BerthaMisanjo
    @BerthaMisanjo Před měsícem

    Great job a Vice President

  • @LimbaniNsipu-g8l
    @LimbaniNsipu-g8l Před měsícem

    The follow up is a good idea some
    civil servants are lazy people.

  • @MarkoKaunga-l1n
    @MarkoKaunga-l1n Před měsícem

    Good job mr pitilizani

  • @user-lf7de5jf5b
    @user-lf7de5jf5b Před měsícem

    Ntchito ilipo muzingo konzeka m'ma office, good job !😂😅

  • @kinggasperagain
    @kinggasperagain Před měsícem +2

    Muzabwereko kuno ku mzimba enafe nalipira kale sinzikutheka sakutiyikila ma gesi

  • @AllanChaviriwa-n6c
    @AllanChaviriwa-n6c Před měsícem

    The confidence is just too much bro

  • @MartinKayola
    @MartinKayola Před měsícem

    3 million yanga mpaka pano magesi ndilibe

  • @Amoslibuda3rdson
    @Amoslibuda3rdson Před měsícem

    Good development VP

  • @BeynoMike
    @BeynoMike Před měsícem +1

    Guys ndimaona ngati manganya ndi kape koma pano ndasimikiza kuti ndi dolo

  • @LucyMsimuko-m3p
    @LucyMsimuko-m3p Před měsícem

    Mumaona ngati Chakwera opusa kusankha Dr Usi aka Manganya.
    Wina alakalaka kuthawa ntchito

  • @WelosPhillimone
    @WelosPhillimone Před měsícem

    Bwana VP mukapitiliza kuyendera ma department osiyanasiyana,,i hope mu dziko muno katangale akhonza kutha

  • @KhumbatiraGift-iu4sv
    @KhumbatiraGift-iu4sv Před měsícem

    Zantchito Machine Katundu Madzi

  • @SaisonMwenda
    @SaisonMwenda Před měsícem

    Go dipper Mr vice president anthuwa akutikwana kwabasi specia nkhatabay nayoso yanyanya kwabasi zisathele kumwela kokha ayi kumapitaso ku mpoto

  • @MonacyThera
    @MonacyThera Před měsícem

    Athu amenewo mmmh bola mwawayakhula eeshiii kulipila magesi koma nkukhalaso kapolo wowayendera amakonda chinyengo too much

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb Před měsícem

    We to support the vice president he doing we.goverment workers are not helping to develop the country it must stop.Mr Usi can you go and sort out immigration officers as as possible.

  • @user-dl9hv8un5i
    @user-dl9hv8un5i Před měsícem

    Keep it up bwana

  • @user-wq3cg9nc6b
    @user-wq3cg9nc6b Před měsícem

    Good work chief

  • @JuliusChazinga
    @JuliusChazinga Před měsícem +2

    Kukoza dziko ND komweku uku

  • @BEATRICEMEDSON-bt6ir
    @BEATRICEMEDSON-bt6ir Před měsícem

    Good leader ship Bwana Usi

  • @RuthStambuli
    @RuthStambuli Před měsícem

    Please, visit more institutions. They do delay payments of suppliers.

  • @JohnThomas-m3y
    @JohnThomas-m3y Před měsícem

    Ali ndi nzeru mkuluyu keep it up mwina ma service ena atha kusinthako

  • @edsonphangula5817
    @edsonphangula5817 Před měsícem

    Good job keeping up

  • @LuciaJeremiah-sd6tk
    @LuciaJeremiah-sd6tk Před měsícem

    Your doing great job mr vp

  • @user-kw1wo2cr3p
    @user-kw1wo2cr3p Před měsícem

    Pitilizani aUsi zaonjeza chilipilireni kale kale mpaka pano akuwalumikizila wolipira kumene

  • @JulioPaul-dt2pt
    @JulioPaul-dt2pt Před měsícem

    More to fire ,there taking long to give us magesi

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Před měsícem

    Uyu chief accountant akuyiziwa ntchito ,no pressure poyankha

  • @chisomobanda8067
    @chisomobanda8067 Před měsícem

    Well done Mr VP

  • @berthamigodi6529
    @berthamigodi6529 Před měsícem

    We need vp like ussi 4ever

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Před měsícem

    Lero manganya sindimunena naga nkhani ya Escom eeee 🙌🙌🙌🙌achita bwino kupitako anthu awa akutinzunza kwambiri Kaye akati magetse azima eeee mavuto samakuthandiza nsanga 😊

  • @yohanebenard7300
    @yohanebenard7300 Před měsícem

    That's why I will never trust any politician you do come like God Saint,deep down your heart you hv different plans

  • @GipaMusic
    @GipaMusic Před měsícem

    Ntchito yabwino boss man

  • @LfBajomusicBajo
    @LfBajomusicBajo Před měsícem

    Koma izi xinalikuti thawi yonse

  • @Christopher-xc2ey
    @Christopher-xc2ey Před měsícem

    Keep it up Mr usi😅

  • @MacfelsonMunthali
    @MacfelsonMunthali Před měsícem +1

    Odya zake no mlandu

  • @KennedyPhiri-c7g
    @KennedyPhiri-c7g Před měsícem +1

    Pitaniso Ku migration Kuma passport uko ziyemde bwana anthu asagone Ku Lilongwe

  • @batistakamizola659
    @batistakamizola659 Před měsícem

    Bravo Mr Michael Usi

  • @NumbDee
    @NumbDee Před měsícem

    Uyuyu tikuferanji tisiye uko antha kusitha malawi

  • @EnoEno-h4g
    @EnoEno-h4g Před měsícem

    Umayitha ayaruke 😂😂

  • @yohachimwaye5859
    @yohachimwaye5859 Před měsícem

    zeru zokha zokha❤