Sizachilendo Nduna Kuona Nduna Ikupeleka Ndalama Kwa Delegate Kuti Awine Convention - Billy Malata

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 29. 08. 2024
  • On Nyasa VoiceBox Billy Malata says it is perfectly ok for a Cabinet minister to spend money on party delegates in order to win a seat at the party's convention. Being a minister and competing in a party convention is not a reason to subject the individual to smear campaign.
    Pa Nyasa VoiceBox Billy Malata wati sizachilendo kuti nduna ya boma iwononge ndalama kukopa nthumwi za chipanichi kuti apexe mpando kumsonkhano wa chipanichi. Kukhala nudna ndikupikisana nawo pa msonkhano wa chipani si chifukwa chomuyipitsira munthu mbiri pa kampeni.
    #malawi

Komentáře • 33

  • @GiftChitsulo
    @GiftChitsulo Před měsícem +3

    Amalata simungakambe za MCP zokha osanenako za dpp chifukwa mukuoneka kuti mukulimbananaotu dpp chifukwa khani imene mukunenazo ndi za MCP koma inu mukukamba za dpp zikuoneka kuti mukuiopa dpp

  • @patassonelucaszovuta3431
    @patassonelucaszovuta3431 Před měsícem +2

    Muphana sumunati nzimu wa chilima wakwiya

  • @SurprisedDrumKit-ql7rj
    @SurprisedDrumKit-ql7rj Před měsícem +1

    Abilly malata meafunsidwa za mcp osati za dop ndie zoyankha mopepelazi achitsilu inu pa

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Před měsícem +1

    Amenewotu akuwululana ifeyo amalawi tikusangalala kuti akuwululana

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Před měsícem +1

    Komatu nkhani ndi komwe akutenga ndalama.chifukwa ngt kuli chimbava choipa kut mcp nde ndie chithyola...ngt anafika pogula magalimoto 30 amwana wake yekha,nanga akazake ,nanga iye mwini...nde izi nzopusa

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 Před měsícem +1

    This how you politicians play with taxes??? You are backing each other then by taking it as normal? Why not also rebuking misusing that money??

  • @LuciusKazembe
    @LuciusKazembe Před měsícem +1

    Akupasa dzingat pano wasiya yogulisa masache

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 Před měsícem

    Mr malata anapengapo kodi?

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy Před měsícem

    Komano ndalamazo sanamugwire nazo 😂😂😂

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Před měsícem

    Iwe ndimbudz kwambiri kdmata ndindan?

  • @ChristopherMatemba-m4g
    @ChristopherMatemba-m4g Před měsícem

    Atamungwila ndimatumba andalam pa airport..

  • @AdmoreSingini
    @AdmoreSingini Před měsícem

    Koma kugawa ndalama for campaign ndi mulandu azanthu a ACB akuti bwanji,.?

  • @SamuelMthengo
    @SamuelMthengo Před měsícem

    Onongoni ndalamazo pakuti nthawi yanu yatha.

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 Před měsícem

    Wasowa zokamba iwe osangonena zaku mcp zakozo bwanji a DPP chikuwakhuza ndi chiyani mbwaaaa iwe

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před měsícem

    Mwasowa chokamba inu, inu nde zithumwazo mulibe? Musalimbane ndi Dpp siyinayambepo yagawa ndlama zimenezi tikuwonera kwa mcp

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Před měsícem

    Amalata mukatelo mwadyapo zoyakhulula achitchola koma zilipo koma osalimbana ndi DPP akupanga zawo Nanu pangani zanu tangoyamika kuti mukuwululana nokhanokha komande mphanatu munadya olakwika SKC

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy Před měsícem

    Try to do your own things dont mention Dpp kuulurana mukuulurana nokha a MCP ife tilibeko

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo Před měsícem

    Iwe uzikamba za mcp osati DPP ayi iwe ndi ngalu kwambiri et

  • @user-cv3zw9ic6d
    @user-cv3zw9ic6d Před měsícem

    Akugula iwe galu bweletsa masache kuno tisesere kuchimbudzi

  • @user-iw6cz5ft2l
    @user-iw6cz5ft2l Před měsícem

    Amalata mwatani kd?

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa Před měsícem

    Nthawi yanu dyeranitu

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před měsícem

    Galu wa MCP utu munawonapo nduna ya dzachuma kele kaja ikumwadza ma milion ngati mene mukupangila inu a MCP nde muwone KWACHA INATHA KALE KALE PANO CHIDZUDE CHA NDALAMA CHIFUKWA CHA UCHISILU WA CHAKWELA NDI MCP YAKOYO INU AGALU KWABASI

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před měsícem

    Machende ako iwe wagwa nayo

  • @user-bk4sm4jn9y
    @user-bk4sm4jn9y Před měsícem

    Ken panyapako galu wachabe chabe

  • @OswinDzama
    @OswinDzama Před měsícem

    Ifemusatisokosereinu muona kutsogoloku

  • @WillamLawson-gk1lw
    @WillamLawson-gk1lw Před měsícem

    Choka iweee zaziiiiiiiiiiii

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa Před měsícem

    Chitsiru iwe mbuzi ya munthu maphwala ako wakudyesa ndalama simplex chithyola Banda

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d Před měsícem

    Malata mbuzi

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před měsícem

    Mbuzi iwe malata

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc Před měsícem

    Galu wachabe chabe

  • @SymonNamalomba-sh3fu
    @SymonNamalomba-sh3fu Před měsícem

    A Richard chimwendo Banda akuphatu aise