Jesus, son of living God ,protect Malawi and citizen, what ever planning for Malawi evil,,back to sender in Jesus mighty Name(Aisiah 54:17)(psalm 121:3)
Pamene Chakwerayo wapha Chilima pamodzi NDI wanthu ena bwanji sama ngidwa, wanthu wonse avotere Dpp, Chakwera NDI amzake a MCP amangidwe,mbuzi zimenezi za watola a Malawi
Guys ndili okhumudwa kuti tilimudziko lokonda social media mmalo mokonda wina ndinzake How come timakonda kujambula pamene anzathu akuthatha ndi imfa instead kupulumutsa myoyo ya nzathu?
Zoti ngozi zikuchitikazi zili ndi a supernatural cause n'zoduka mutu. Mayiko onsewa pa dziko lapansi satana, if at all he exists, azikalimbana ndi Malawi??? Khalani serious akuluakulu
iweyo amene wapeleka coment yot vuto ndi miseu iwe ukukana kut ku malawiko ngozi zimene zikuchitikazo ndiye kuti iweyo uli mumgulu la anzako asatanic wo iweyo. ndiye osa mapeleka ma coment opusa apa anthu akutha ndiy ife tiziti imeneyo si satanic munamuphelanji chilima
Tsoka mtunda ndi nyanja poti iopayo watsikira komweko.
Mulungu atsogolere dziko lamalawi komanso bushiri ndi chakwera amwalire ndithu.mulungu wachifundo chambiri wachisoni atichotsere anthu awiri amenewa
Jesus, son of living God ,protect Malawi and citizen, what ever planning for Malawi evil,,back to sender in Jesus mighty Name(Aisiah 54:17)(psalm 121:3)
Amen ❤ still speak
Min bus iyaka bwanji moti ikana yaka inali yama futayo satanic amafuna muli athu ambilimo yama futa kungo gundana ndiina thawi yomweyo imayaka
Bon kalindo ndi liwu la a Malawi.
Abale onse amene Amati ndi ma prophet ndi a satanic ziko la Malawi mwazaza a satanic kwambiri
Keep fire 🔥🔥🔥🔥 burning Mr kalindo
Bon kalindo amayakhula ngati wamisala koma there is a sense of truth in whatever he says, May the good Lord have mercy on Us
Anthu sakuziwa .vuto kumalawi kuno satana anatitseka kumaso
Hyv bro
Malawi Chikangawa Party ikugulitsa anthu ku satanic but remember God is watching
Fact
Izi ndie zoona zen-zentu achimwene, ndimaona ngati Inu simkudziwa. Kumalawi kuno zaka zamma mbuyom kunali anthu opemphera kwambiri, koma pano masatanc adziveka uprophet kumangonamiza anthu basi. Ndipo anthu ndfe zitsiru,tsiku nd tsiku anthu tikutha chifukwa cha zingoz zosaziwika bwino. Karelo izi kunalibe. Kungobwera maprophet awa ngoziso mbwe mbwe mbwe bwanji!!! Osazifusa amalawi bwa, zinaz zanyanya mmmmmm ai.
ndipo munasowadi love you Mr DC
Let us pray hard without cease! To shame the devil 😢
ndipo zinthu izi zinachitikapo ngati izi ndipo koyamba ndipo buchiri ndichakwera uyu kaya ambuye titsogororeni ndithu ambuye tikurira abare
Everything he speaks is 💯 true.... Amalawi kugona too much
Big up the DC
dziko lili mumanja mwa satana tizilipemphelera dziko lathu labwino la Malawi
Ziziwika zonse ndi thawi mulungu atiyang'anire plz
Ambuye atithandize atipulumutse kuzowawazi
koma anthu awa ngozi paripose anthu achipongwe kwambili kumpha anthu ngati nkhuku Mastanic ndipo yes ufiti uri ko mukunena zowona
Powerful speech from our beloved president, the Dddddd Cccccc!!!!❤❤❤
Ufiti uliko even ku azunguko ufiti ulikoso,
iweyo wa pasi pa nyanja amene ukupeleka ma coment ako auchitsiluwo chikumbu mtima chikugwire iwe wa mcp
The D C naked truth 🔥🔥🔥🔥🔥
Mafumu ndi anthu oipa kwambiri we need to get rid all of them
Wamisala anawona nkhondo zoona
Zoona DC tipephere kwambiri zoona ndithu
Mulungu tifungatilen ife ana Anu
The DC number one......
Ambuye atetedze dziko lathu tili pachiopsyezo
we need your mercy our father 🙏 🙏
Pamene Chakwerayo wapha Chilima pamodzi NDI wanthu ena bwanji sama ngidwa, wanthu wonse avotere Dpp, Chakwera NDI amzake a MCP amangidwe,mbuzi zimenezi za watola a Malawi
Osamasowa chonchi koma
Yes prayer is needed❤❤
Zoonadi Atsogoleri ambiriwa a dzikowa onse ndi afiti.ciffukwa amaipa mitima. Ndikumapha anthu.Mulungu yekha basi ndiye wa chikondi .saapha wosalakwa .ayi.Amfumu a kwathu..chief mwangata wa kuzomba t/ a Mulumbe .anandiuza kuti @ AZUNGU ONSE AKUNJA AJA NDI AFITI.NDIPO MAFUMU ONSÈNSO AMAKHALA AFITI CIFUKWA IWO AMAYANG'ANIRANSO AFITI ONSE; OSAUKA ONSE;AMISALA ONSE.OYERA MITIMA ONSE ;AKUBA ONSE.ETC.@NDIPONSO MABWANA ONSE AMMAOFESIWA NDI AFITINSO.SAMALANI NAWO NGANGA WATHU..INENSO PANO NDIINE MFITI MMUDZI MWANU MUNO.KOMA SINDIMAPHA ANTHU AYI.CIFUKWA KUKHALA MFUMU NDI KUKHALA NDI ANTHU MMUDZI ..EETU NGANGA WANGA ABITI CHAONA ANJAONA CHEMWALI.WANGU
Mulungu achitepo kanthu
The DC 🔥
Chilungamo ndi chipongwe
Mmmm osachulusa zambiri nayeso anali limozi kut tengera kumeneko koma pano iye akunena ngat simumozi mwaiwo zithu zikuvuta km titan sikut ndizose tingathandizidwe ndi president 17:44
Kuchikweza The Dccc
Ndp live ngoz zafka pawese mmm 😢😢
The DC mwana oopsa kwambiri President of the poor people ❤❤❤❤❤❤❤
Guys ndili okhumudwa kuti tilimudziko lokonda social media mmalo mokonda wina ndinzake
How come timakonda kujambula pamene anzathu akuthatha ndi imfa instead kupulumutsa myoyo ya nzathu?
What do you mean
The DC bon kalindo 🎉
Amen ambuye timenyereni nkhondo
🤗🤗🤗 ALIYESE PA MALO AKE 😅😅😅
Speech yako tinaisowa Dc
Mulungu alowelelepo😢
Bon kalindoooo
Pitilizani kung'alula mmativetsa kukoma,🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Yes apitilize amene amadana ndzoonaz mdziwe nchito zake ndzomwezo moto kt buuu umupeza wa MLUNGU patsogoropa
Munasowa Mr dc
Koma mkulu uyuyu amayankhulatu
Abushiri ndi achakwera ndi asataniki anthu akupha
Zonse mwakambazi ndizoona tikupezeleledwa cause voice yathu siipita patali andalewa sakutimva
Powerful msg mr
Zoti ngozi zikuchitikazi zili ndi a supernatural cause n'zoduka mutu.
Mayiko onsewa pa dziko lapansi satana, if at all he exists, azikalimbana ndi Malawi??? Khalani serious akuluakulu
❤❤❤
Amen 🙏
You are saying truth
iweyo amene wapeleka coment yot vuto ndi miseu iwe ukukana kut ku malawiko ngozi zimene zikuchitikazo ndiye kuti iweyo uli mumgulu la anzako asatanic wo iweyo. ndiye osa mapeleka ma coment opusa apa anthu akutha ndiy ife tiziti imeneyo si satanic munamuphelanji chilima
Fuso ndrakut Kodi kumbuyoku miseu yoipa kunalibeko yaipa lero!!?
@@TimothyMwandila-r9p eti amwene miseu yaipa lero
@@TimothyMwandila-r9pkoma ndipo.
Zoonad big
The people's first!
❤
Kodi ma audio amenewa akalindo muli pa payroll?
Dziko lilipamoto tiyeni tipephere molimba amalawi
Big op the DC stanic iliku Goshen city
Aliyese payekha azipemphelera malawi ,zochitika masiku otsili(2timoteyo 2vs3))
Yiponde fada 😅 munthu umatopa basi kung'alura
Ooo ambuye tetezelan malawi
Amezing
The DC number one
Amen mau achimbikitso ndizoonadi amalawi tipephere akhalitse bonikalindo amatiyakhulila
Kom mu2yo wanena chilungamo akubweza sembe
Makamaka tsoka liyenda chakwela mulungu amukathe ndithu ndichifukwa Chake akati ndikapanda kuwina ndisakhetsa mwazi wanga
Mr presdent❤❤
Legend
Khaniyi A DC akunena zoona
Km nyoo akunena zoona❤❤
Amen 🙏❤❤
Zoonad km
Ambuye atithandize please
Ngozi yimene ija ndya satanic ndthu oasakayikaso ayi
Abale sizikuyenda Mulungu atichitile chifundo
11:48 Ambuye atichitire chifundo
Zona zake the DC
11:48 Ambuye atichitire chifundo 12:23
🔥🔥🔥
The DC ulemu wanu
Focus pray
More fair mumatiyimila
❤❤❤❤lovekarido
Mulungu atitetenzere....choipa chibwerere kowochipanga...DC mumatimvetsa kukoma
Nkhani ndimisewu yoipa si satanic osalozana zala umenewu ndi umbuli, dziko lilonse kumachitika ngozi
Ndiwe Mbuzi omvesa chisoni kwambili, ndipo ulibe nzimu wachiziwitso. Akazakuphera abale ako moaned uziwe Kuti Chakwera ndiwa sanic. He is evil than devil himself.
Ndipo zowona mulungu amuthandize azake akulila ataya moyo wabare awo iye kumarakhura atankhuta deyayo osangopita kumakanyera bwanji
Vuto lake sinu anthu otseguka mmaso. They hide it in the plain sight and you still can’t see it
Zinu izo,
aboni kalundo anatha akalindo anali kale
Inu kale lanu mwapanga chani?
Kaya tamufuse bare wake wachakwerayo
The DC
chilungamot chimenecho
Live DC
Exodus 14vs14😢😢😢
Pita ukawathandize iweyo umakonda kulalata deyile chisilu
Chitsiru ndiweo moti iweo suva chisoni mene zililimu garu wamkulu mbuzi ya munthu mutuluka m boma dikira
Iwe ndiyed ndi galud wamva!!! Moti kufa kwa anthu ena ukumakondwa eeet???
Iwe usatipalamulitse ndye mmodzi mwa afitiwo et??
Iwe mutu wawukuluwo wava ? Ulibe zelu et
Bushiri Chakwera promised mwazi 2019 pa compaign