Yes ndizoona ,koma chikufunika ndichoti mukhulupirire kuti Yesu khristu ndiye Mulungu wolenga dzonse, maina Ena monga yehova,allah, Yahweh,ndimafano .koma dzina la Mulungu ndi Yesu khristu Basi. Then lapani ndikubatizidwa Mudzina la Yesu
We are nearing to the end of this world. Zizindikiro zikuonetsa kuti Yesu ali pafupi kudza. Ambuye Atithandize. We are nearing home. Jesus is coming soon.
Yes that's where part of the fallen angels were arrested and locked underneath and the book of Revelation affirms it that the holy one of Israel AHAYAH GOD ALMIGHTY will release the arrested fallen angels to kill the whole 3rd of the world. In that dreadful day of the Lord, Malachi chapter 4 verse 6 as well as the book of Revelation chapter 17.
Exactly apa tizingoyang'anila kumwamba bass coz zizindikilo ndi ndiye zikuonekad thank you for your update bg
Yes ndizoona ,koma chikufunika ndichoti mukhulupirire kuti Yesu khristu ndiye Mulungu wolenga dzonse, maina Ena monga yehova,allah, Yahweh,ndimafano .koma dzina la Mulungu ndi Yesu khristu Basi. Then lapani ndikubatizidwa Mudzina la Yesu
BMTV ndiyotsogola ndipo timakodwa tikamalandila ma uthenga ambili zose zosayiwala. Timakhala tikudikila mosalekeza chifukwa. Muli chiphuzitso komaso kuzindikilitsa. God bless you
Mmm ndili ndimatha chifukwa ndikuganiza zomanga nyumba komaso komabe basi kumangopephera kuti mulungu andichitile chifundo.komaso dzikoli lisathe chifukwa zovuta ndizambili zokomaso zilipo mmm koma big man timakunyadilani tizindikilitseniso zina.amen
Tonse anthu aku Malawi palibe zomwe tikuziwa kupotsa inu big 👏
Great one
thanks so much achimwene inu mamakwana keep doing good work.
Thanks for the information bro , mumatitha
THANKS FOR REMINDING US
May God bless you
Thanks for the reminder
Ndinu president wa history, keep up bro, more respect from me here in Capetown
Obrigado pela informação.
u are number one my brother. timakunyadira .am mr Banda ackim from Zambia lsk .Apollo camp
You are super bro...keep it up
Exactly 💯 nthawi yathadi
Ulemu wanu bm tv🙏🙏🙏
Thanks for your advice ❤️
Thank you for your tips of the Bible keep up the good work mumakwana🙏🙏🙏
Tizingopempherera
Amwene mumayitha bible olo chakwela sangakuthe inuyo, more grace Big Man
Thank you bro
Thanks Bm
Thanks bro
Ndizoona
You are emazing man where do you take all this things
Mumakwanira inuyo brox ngakhale sitinakuwonenipo bg up
Thanks BG
Inuyo ndinu dolo bg man thanks
Much love
I believe you brother mumaitha kwambili
AMEN M'PINGO AND FOLLOWING.......
Ndizoona izi mapeto aziko ngati mukukomedwa zikomedwani chocho 🤣🤣
My boss 🤝🏼❤️
Thanks for uploading much love here in KUWAIT
Inu mmazitenga kuti? Respect ❤
Ulemu wanu Big 👍👍👍🤝🤝
BIG 👍
Mumaitha a bro, keep up good work, timadziwa zambiri kudzera mu program yanuyi.
We are nearing to the end of this world. Zizindikiro zikuonetsa kuti Yesu ali pafupi kudza. Ambuye Atithandize. We are nearing home. Jesus is coming soon.
Ai big unuyo ambuye akukugwilisani chito pitilizani ndimakukondani
Ndipo koopsa mmmm amatha zedi
Big up my boss
Bravo bg mn mmakwana
Big up big mumatha zedi koopsa❤❤❤❤❤
Mumakwana bigy potidziwitsa 🔥🔥🔥🔥🔥
Salute
Bingo bingo😊
Apaatu mkulu malemba akukwanitsidwa ndithuuuuu!
Malawi intelligence
Yes that's where part of the fallen angels were arrested and locked underneath and the book of Revelation affirms it that the holy one of Israel AHAYAH GOD ALMIGHTY will release the arrested fallen angels to kill the whole 3rd of the world. In that dreadful day of the Lord, Malachi chapter 4 verse 6 as well as the book of Revelation chapter 17.
Ulemu wanu broo
Ine mumandisangalasa zedi keep up.
❤❤
Eeeeeeee uyu ndi mtunda wina😂
Oh Allah
Tikuyenera tiziwerenga bible ndipo tilape azibale Anga ndikumachita zabwino nthawi zonse
Zoona tizikozeka
Mumakwana big
Inuyo ndi one
❤❤❤❤❤
Thix bg koma tipangeniso update Ukraine War
Brother mukuti bwanj za Dzikoli ??
Lithe ndye zolapa titan ?
Komanso enafe takwatira kumene kaya
Kkkkk
Unamuva ndindani kut dzikoli lidzatha ena atadzakwala kalekale?
Oh my God!!
Koma abambo inuyo ndulodala bele munayamwalo ❤ ulemu wanu
amen
Following mwachidwi
Kodi pakati pa chigumula chanowa ndi m'tsinje umeneu chinayamba ndichani???????????????
Tafikadi mapeto anthawi ya pansi pano 🤔🤔🤔,
Ambuye atichitre chifundo
Apopo ngati baibulo likutiuza kuti musinjewu ukazangoyamba kumphwela ndiye kuti ufumu wakumwamba wayandikila tikuyenela tisatile nanga tisuse ngati ayi
Cholemekezeka kuti Yehova anapatsa mphatso yolengeza zisisi za Yehova, pempho langa ndi ili Mulungu akuthandizeni pa nkhani zanu.
Keep it up we are together
Rispect
Eya, malemba akukwanilitsidwa. Zikomo
We need more information from ukrain and Russian war tikuona kuti kukuchitika chipwilikiti kwambili than u sir
inu simunalakwe kunena izi anthu angouzana kuti ndikuona mukulemela malo monena kuti lapani Mulungu akubwela.
Inuyo bg ai chanel mupanga nacho dola
Persian Gulf ndi nyanja kod et??
Ayi tikapumad kumwamba
Umakwana fada
Zosayenda 😹😹
Iweyo sukulu unapita aise
Zoonad big hadith imanenanso choncho kut msinje umenewu uzaphwela ndipo pazatuluka golide ndipo anthu azayamba kilimbrana golide ndipo anthu azaphana
Aaah is very dangerous
Munthu uyu amakamba zoona zokhazokha ndipo Mulungu azimusunga
Hadith inakambadi kuti Euphrates akangophwela mmmmm chabwino palibe
Mulungu atithandize NDIPO atikomele mtima, popeza lonjezo lake silipita pachabe
Tikuphuzi zinthu ZOFUNIKA pililizan
Malemba adakwalisidwa chalako ndi nthawi basi🙉🙉
Koma bro mmawelenga staff
Basi ife tizingokhala zosezo akuziwa ndi Mulungu wekha baai
Ndipo osakayikila izi ndi zizindikilo zamapeo aquamarine bas Zoopla zikubwela ngakhale tikumatha one kut pano machimo sakuopedwa
Mumafatsa pochita zinthu boss
Sankiyu, Tingolapa basi kuti yesuyo akamabwera azatitenge akamazabwerera kumwamba
Ndizoonadi mbiriyi ndimomwemo ndithu
Ee ndikufufuza bwino ee abuye wamoyo akuchititsa kutekha kwama prophes oonse achitike anthu aonongane okha okha Athamandike Yehovah.
Ulemu wanu Big
Munabweraa bigy mumakwanaaa
Ulemu wanu
Mumakwana bwana
mufuna tisamange nyumba?
Injury time,
Umakwana iweyo