One of the best assuring speeches from the true servant leadership...mabodza a boma onse ali pa mbalambanda...boma lanji lodana ndi REFORMS...Apa a Malawi 🇲🇼 mwazimvera nokha utsogoleri wabwino after Bingu ndiye ndi APM basi...anatiphula mu cash gate apaso atha kutiombola mu 3 months only! Apapa ndayamba DPP 2024 camping 🏕 basi...
Pls Mr APM may God bless you all the time we're waiting for you to rescue us in aur loved Malawi country agaruwa atikwana ife tanchona mumaiko ano ayeni because of those people who call them self tonse alliance the don't know anything about running the country wht the know ndikuba basi in fact ndika group kamamafiya akuba komaso kwawo ndikupha
We are doomed, are these the choices we have. Who is less evil to the citizens. Come on dpp, you have a great Economist ,make him president for you party and let's get rid of the Nonsense not tonse , government
That's my vote ❤❤❤❤Yes indeed APM can change this Government only for 90 days very true, but Chakwera even titampatsa 20 years nothing can change only ana ake ndi mkazi wake plus azipongozi ake.
May almighty God continue to protecting you and gives you more yrs tinkaona ngat mukutisocheresa koma pano taziwa kut munalidi munthu wolungama mwa chimwenecho mutikhululikire pa zomwe amalawi tinkalankhula pa ulamuliro Lero alimi ife akumudzi tikusowa chichita tilibe ndalama zogulira fertilizer sitingakwanise kugula thumba limodzi 110 0000 mpamene mu nthawi yanu inali 17 to 18 Kulima ndiy tinalima koma mbewu tilibe ma ID athu Anatipasa koma mulibemo kalikonse anatinamiza kut muli mbeu komaso fertilizer komati bwana kukapangisa scan kupezeka kut ma ID aja ndiya Empty kotèro bwana ndi kugwada pamapazi anu bwana kutula nkhawa zathu monga ife akumudzi tikuvutika msima tikumadya ka wili pa week chifukwa chakapezedwe ka zakudya kakugisowa tikusowa mtengo wogwira pano bwana
Kunena chilungamo we were blinded pomuchotsa Peter pa mpando zilibwino chifukwa zafikapa ndipa usandiuze naneso ndunvutika 😢, eeetu 2025 Dpp ikalowa m'boma ikonza ma mistake ake akale aja poti adali wochepa osati izizi.
Pemphero la mtundu wanji ili? Ku malawi kulibe opposition. Boma lolephera nayonso Opposition mbola. Atolankhani athu mbola, amafunsa mafunso opusa ndi opanda phindu. Tinali ndi Eunice Chipangula pa dzana, ankadziwa kufunsa mafunso osati izizi, Kaya ma school ake anapita kuti. Mbola
i wonder who typed the name of president wrongly without fixing it . that is very bad . anyway i wish president Peter can be a minister of finance not a country leader neither LAZALO .
Zomvensa chisoni kwambili zipani 9 zoona kulephela kumanga chimodzi tikati dziko la Malawi mwina zithu tiona za chilendo koma mbuzi zeni zeni moni Steven maseya i hop uremember me I ❤ DPP A busa awa ngakuba Kwambili Pls tikupepha ma vote 2024 pls pls
Vuto lomwe ine ndimskhumudwa ndi dpp ndilakut kosuts amazimvetsa chison kwambir kom akamalamulir amakhal anth amwano limandinyasa zina kt An adhat lelo mul kosotsa zakuvutan
Everyone must vote for peter of course who else can Malawian vote for someone else except p.m , chakwela asazawone ndi vote imozi yomwe, pake wamubo lake iyaaa .😢 shameful on chakwela mufiti yomwe sakuva kulila kwa anthu
koma zoona zimene akunena a Bright Msaka? bwanji osauza a Malawi chilungamo. kodi mmatengera a Malawi kuntoso bwanji? you are just taking Malawians for granted. kodi chifukwa choti a Malawi ambiri ndiosazindikira? basi kufuna kuwazunza a Malawi ndi mitima yanu yongofuna kuzikundikira chuma basi? enafe tatopa nazo zamabodza zanuzo.
Inu tinakuonani kale nanu munalephera kale musatipusisepo boma lanu mumaliso ndi mavuto aakulu kwambiri. Bola tiyeseko ena amu dpp momwemo Koma usati inu madala ayi
Zidakukanikani kale chipani cha family ichi munadya kunakwana palibe chachilendo pa zomwe odalawa ayankhura ukamakalamba umakhala ndi makani...siyilani ena achiteko mbali Yao za inu zinatikwana..
Look at statistics from 90s kwacha imapanga gain only time ya tobacco tikamafika these months get affected and mind you tobacco selling seasons imafika November koma pano by August msika watha where do you expect it to gain?
That's why Kabambe you had the audacity to grant your colleague loan ya 187 years eti ? Mumaononga chuma ndinudi you have come out in open kuti muli mu boma you were the ones enjoying
Mutalika akuwoneka bwino kwambiri timangomunyoza akadali ndi nzeru
One of the best assuring speeches from the true servant leadership...mabodza a boma onse ali pa mbalambanda...boma lanji lodana ndi REFORMS...Apa a Malawi 🇲🇼 mwazimvera nokha utsogoleri wabwino after Bingu ndiye ndi APM basi...anatiphula mu cash gate apaso atha kutiombola mu 3 months only! Apapa ndayamba DPP 2024 camping 🏕 basi...
Politics is a profession where people venture in to sustain their families.
Respected to you thanks for coming and to talk Tu your people thanks
I'm gonna fasting for you to win in 2025
May almighty God continue to grant you knowledge ❤mr.
President
Too far. This year we want change.Amen
Kukhala Chete sikupusa DPP is greatest democracy in Malawi God bless DR president Mthalika Mthalika
Chakwela ndiwe bb ndipo kungonva kuti wafa tsiku la Christmas lisitha kuzakumbukira dzana la chilombo iwe! Ndizako Chilima munve kut anthu akupephera kut bola miyoyo yanu isakhalepo kt anthu 17 million apulumuke. God munve kulira kwathu😢😢
Kabambeyu ndiyemwe ine ndimamuona kuti ndi solution ya malawi
Only chilima wud change our country.Chilima has my vote
I love this speech may the good Lord keep blessing Mr munthalika
Ilove dpp
Pls Mr APM may God bless you all the time we're waiting for you to rescue us in aur loved Malawi country agaruwa atikwana ife tanchona mumaiko ano ayeni because of those people who call them self tonse alliance the don't know anything about running the country wht the know ndikuba basi in fact ndika group kamamafiya akuba komaso kwawo ndikupha
Madala team, zinthu zimayenda ndi nthawi, kukwera mtengo wa zinthu ndi nthawi basi, osamnamiza anthu
Adad....Boma iro❤❤Ife tili pa Mbuyo panu.....osaopa ...more fr🔥🔥🔥
Bright Msaka you are very bright
We are doomed, are these the choices we have. Who is less evil to the citizens. Come on dpp, you have a great Economist ,make him president for you party and let's get rid of the Nonsense not tonse , government
Tabwezani matayi mwazimanga kwambiri mukulempela kuyankhula maka amsaka 😂😂😂😂😂😂
That's my vote ❤❤❤❤Yes indeed APM can change this Government only for 90 days very true, but Chakwera even titampatsa 20 years nothing can change only ana ake ndi mkazi wake plus azipongozi ake.
We need you back, sorry kusamva kwa2 pano tkulra nako
This is wat we call a leadership ❤
Yes there is need for muthalika to come in and dialogue the chakwera
May almighty God continue to protecting you and gives you more yrs tinkaona ngat mukutisocheresa koma pano taziwa kut munalidi munthu wolungama mwa chimwenecho mutikhululikire pa zomwe amalawi tinkalankhula pa ulamuliro
Lero alimi ife akumudzi tikusowa chichita tilibe ndalama zogulira fertilizer sitingakwanise kugula thumba limodzi 110 0000 mpamene mu nthawi yanu inali 17 to 18
Kulima ndiy tinalima koma mbewu tilibe ma ID athu Anatipasa koma mulibemo kalikonse anatinamiza kut muli mbeu komaso fertilizer komati bwana kukapangisa scan kupezeka kut ma ID aja ndiya Empty kotèro bwana ndi kugwada pamapazi anu bwana kutula nkhawa zathu monga ife akumudzi tikuvutika msima tikumadya ka wili pa week chifukwa chakapezedwe ka zakudya kakugisowa tikusowa mtengo wogwira pano bwana
Kunena chilungamo we were blinded pomuchotsa Peter pa mpando zilibwino chifukwa zafikapa ndipa usandiuze naneso ndunvutika 😢, eeetu 2025 Dpp ikalowa m'boma ikonza ma mistake ake akale aja poti adali wochepa osati izizi.
Go on dpp we need to change
zeru mumakhla nazo when you are out of government. mukalowa ubongo ose umathawiria kuchinena.
Dpp chipani chosamalira anthu osauka
Dr Kabambe muli masomphenya😮
Bravo my president.you deserve another chance
kodi mulibe office? Basi anthu akulu akulu peya peya kunyumba ya munthu?
Munali muboma munalephera inu kozani kaye mavuto akuchipani then mutiuze solutio ya dziko
That's great
I Like how blind we are as Malawians 😅😅😅😅 timayiwala mmmmmmmm
kkkkkkkkkkkkk ameneyo nde mMalawi
Peter yemweyo 2025 bas mbanva zichoke chakwela ndi chilima chokani mwaulemu
Sitikufunaso mzukwa uwu wa ku Thyolo udzatilamuleso.
I love u fadah God may bless u ❤❤❤❤
Achakwera tangosanzikani mwaulemu pitani kunyumba mukalele zizukulu asiyeni ena apitilize mutengane nda chilima chonde ndichokereni mwaulemu
Amai awa 120000 feteleza shop itiyo a navicha kupanga rent minda musaiwale kwanu kulibe minda ili mmanja mwa ma estate tisanyozeke kuti mukupanga rent minda kwathu kuno uzani a Malawi chilungamo
Aaa Aaa Aaa ndie chani
Yes Malawi is in bad shape but dpp is not a solution,too much tribalism
Pemphero la mtundu wanji ili? Ku malawi kulibe opposition.
Boma lolephera nayonso Opposition mbola.
Atolankhani athu mbola, amafunsa mafunso opusa ndi opanda phindu.
Tinali ndi Eunice Chipangula pa dzana, ankadziwa kufunsa mafunso osati izizi, Kaya ma school ake anapita kuti. Mbola
Zimayi walankhula kokwanila mfundo zenizeni
Did you accept defeat Mr APM?
Kuvomeleza nkofunika kenaka mupepese kuti mutapasidwa mpata nanunso dziko munaliononga
IS THERE ANY CHANCE TO SPEAK WITH PRESIDENT PETER ? I HAVE SOTHIN G TO TELL HIM BUT IN PERSON .
Zazii, Mandala Team, yopanda ndi mtchere.
i wonder who typed the name of president wrongly without fixing it . that is very bad . anyway i wish president Peter can be a minister of finance not a country leader neither LAZALO .
Chipani chot chalamulapo never my vote
Za ziii zokhazokha izi, mungokangana nokha nokha dyela,boma mukaliwinila kuti inuyo
Mmmm Ona macoment inuyo zuyekuyenderani vuto kondwani ndi azake angofuna udindo not masomphenya
Agogo mukukhalira nthawi yanzanu, kapumeni kumanda tioneko zina ife.
Dad kutengeka kwathu pano tikulika# my vote 2025
❤❤❤❤
Tiyeninazo please mutitandise ife kuno tikufa 🇲🇼😭😭😭
Boma iloo❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉
One love adad
Inu zimenezi musatiwuze ife zimenezi mukamuwuze chakwela kuseliko ife palibe chomwe tingapange anthu okula mtima inu musangatithandize nonse ndi mbamva
Zomvensa chisoni kwambili zipani 9 zoona kulephela kumanga chimodzi tikati dziko la Malawi mwina zithu tiona za chilendo koma mbuzi zeni zeni moni Steven maseya i hop uremember me I ❤ DPP
A busa awa ngakuba Kwambili
Pls tikupepha ma vote 2024 pls pls
5 advisors.... who do nothing. you had 5 of them.
Vuto lomwe ine ndimskhumudwa ndi dpp ndilakut kosuts amazimvetsa chison kwambir kom akamalamulir amakhal anth amwano limandinyasa zina kt An adhat lelo mul kosotsa zakuvutan
Ndiye mungayelekeze ndi manyaka apanowa
Zizii mbavaa inu dpp
Eyetu nde udolowo nyumba izinkhala ndi office
Wa nyau party ukumva bwanji ku dambweko 😊😊
Everyone must vote for peter of course who else can Malawian vote for someone else except p.m , chakwela asazawone ndi vote imozi yomwe, pake wamubo lake iyaaa .😢 shameful on chakwela mufiti yomwe sakuva kulila kwa anthu
Moto kuti buuu
koma zoona zimene akunena a Bright Msaka? bwanji osauza a Malawi chilungamo. kodi mmatengera a Malawi kuntoso bwanji? you are just taking Malawians for granted. kodi chifukwa choti a Malawi ambiri ndiosazindikira? basi kufuna kuwazunza a Malawi ndi mitima yanu yongofuna kuzikundikira chuma basi? enafe tatopa nazo zamabodza zanuzo.
Worthy watching osati zina zija
Boma iloo 🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤❤❤❤❤
Chaponda ekhayu kuyankhula ndiye kumamuvutilapo pan'gono
Sorry Mr APM,you are in the shadows of incompetence. Your government did nothing to the development of Malawi. Today is not tomorrow.
Me kumastand following
Adad omwewo 2025
Koma Maseya pa prayer NDE mwaiphatu
He just said that the. Depreciation is man made
Nthawi ya peter timadya kanayi osat uyu wa nyawuyu angoyendayenda munthu nkulukulu
Massive prayer. Amen❤
Ati kaya munalodzedwa😸
Adadi 🔥🔥🔥
Koma Amayi mwarankhula bwino... Ambuye Akudalitseni
Adad 2025 boma❤
Inu tinakuonani kale nanu munalephera kale musatipusisepo boma lanu mumaliso ndi mavuto aakulu kwambiri. Bola tiyeseko ena amu dpp momwemo Koma usati inu madala ayi
Zopanda ntchito izi inuso musakhale ngati abwino zinakuvutani kale izi ndi zizindikiloza masiku otsiliza mukawelenge bible muzinamiza anthu osazindikila omweo
Was Dausi present?
Munthu mukumuzuziranji akudwala??? Komatu inu a dpp munthuyu mulibe naye chifundo
True leadership
Ineso nikuwona sogolo mwakabambe nakhumwayo ayi nakhumwa zikumulephera kulidaopuzishoni muchenjele posankha ameneanga zasamale chipani cha dpp nakhumwa akhoza sithachipani mukhalemaso
Munapha achalubino inu adpp
❤❤❤❤❤❤ APM
Apm ndi machine including their executive 💪
Machine ogona mpaka tpin izigwilitsidwa ntchito ndi bodyguard memories still fresh
Olembedwa ntchito mosaoneka bwino apose aku mombera University?
Boma ili latipha koma adad adatiuza koma kusamba anthufe
Ndiiiithu munthuyu mukadamuvera chisoni osabweretsa kabambe or nankhumwa adzalankhule bwanji???? Mukumulakwira mutharikayu
Akuluakulu ndi dambo mozimila moto a bro....even judges put on white hats meaning to say there's is wisdom in grey hairs
Mukunamiza ana anu makadeti
Zidakukanikani kale chipani cha family ichi munadya kunakwana palibe chachilendo pa zomwe odalawa ayankhura ukamakalamba umakhala ndi makani...siyilani ena achiteko mbali Yao za inu zinatikwana..
I thought is my phone me too no sound, dpp is my trust.
APM mbambande
True why devaluation comes when people are expected to buy agriculture inputs why why chakwera knows nothing
Look at statistics from 90s kwacha imapanga gain only time ya tobacco tikamafika these months get affected and mind you tobacco selling seasons imafika November koma pano by August msika watha where do you expect it to gain?
That's why Kabambe you had the audacity to grant your colleague loan ya 187 years eti ? Mumaononga chuma ndinudi you have come out in open kuti muli mu boma you were the ones enjoying
Cholinga musagule fertilizer njala ipitilire
We love u papa
NOSENS AKUBA NDIA SANKHO INU
Mcp nde panja penipeni mumalo moti akanaliphula ziko pamoto nde iwomso kuliteleka ndi nkhuni zikulu zikulu
😂😂😂😂😅
Kkkkkkkkk
😂😂😂😂😂😂🎉
Panja Bola km ku toilet
Zikuoneka ngati a DPP sakuziwa chomwe akulankhula akalankhula za kusowa kwa mankhwala zipatala ulamuliro wawo Ku chipatala sikumapezeka mankhwala,,, komaso ndi anthu ozikonda kwambiri,, ongoona zao zokha osati za antnu,,, lero muli busy kunamizatso amalawi ndizambiri zomwe munakanika
You malawian why saying 2025 it's 5 years that's 2024 voting constitution ya dziko la malawi imatelo osati 6 years malawi wake uti?
Chokani apa
Kkkkkkkkkk koma ndizoonadi chitsotso chimaoneka mchamzakodi tiyenazoni
100%❤