Inuyo anthu a ku Mangochi ndinu adyera, mwagulisa vote yanu ndi ndalama. Ndipo olo mutati musazavoterenso DPP kapena UDF, Apm ndi Atupele sangavutike muzivutika nokha ndi nkhanza za MCP.
Kuwina wa mcp ku mangochi sizikutanthauza kut kumangochiko anthu ndi a mcp,,,kumeneko ndikwa DPP NDI UDF BASI, musamunyoze peter ndi atupele chifukwa cha chisankho cha counsellor,,MUSIILETU ZOMAMUNYOZA PETER KUTI WAKALAMBA,,IFE ACHINYAMATA ZIMATINYASA,,,APM MY VOTE 2025 ISHAALA
Komanso we have to learn a Malawi pazomwe tinachita poika m'boma mimbulu yomwe ikutiluma leloyi. Chakwera ankachita kusasa mau poyankhula asanalowe m'boma, koma now alind soft voice poyankhula. But I hope will not Rpt this anymore
Ayi sikut wadya koma ntima ukumuwawa kut anthuwa osakampangila bwanji kampeni mwanayi bwanji.zowawa palibe as dpp ndi as udf osakampanga support Bwanji?sanapange bwino iye sakufuna kut mcp isakhale ndi room ku southerner.koma akuipasa mpata akut aaah zaukhansalazi zopanda ntchito pomwe anzawo zomwezo ndipomwe akuziona zofunika kwambili.adzazindikila atagwa a dpp ndi udf 2025 chifukwa chonyozera zinthu zomwe zisali zosafunikila.so zomwe akutanthauza azikhala busy ndizilizonse a wiliwa.zaukhansala,za u mayor,mp ndi u prezident zomwe.mphwayi ndi tsoka ndipomwe aona izi mcp izilowa chonchi.
Sakunama ngati atopa apume basiii , a mcp akangowina vuto sikubela koma kuzikonda kwa MA oppositions leaders awo, palibe kutosya chala munthu, zikhalani mphwiiiiyo choncho kumadya MA sausage wo
Akunena zoona ameneyu ngakhale mukumutukwana....APM & Atupele were supposed to campaign for their candidates....chisankho chinali mkhonde mwawo why they didn't show up?
Zikugonadi kwambili mbuzi zimenez...anthu kuyeseera kuwakonda but they are too selfish....chilichose kumangoti ku page house,akufuna misonkhano azikapangila ku page house komweko.....yachita bwn mcp ndipo tiyivotera...awa even akazalowaso mboma kupepera kwake kudzakhala komweku...
Audio iyiyi ndiyowona anthuwa ifewo timawakonda koma za Ife saziwelengela popeza ndi anthu a ndalama zawo it's okay ifewo tifeyo tizivutika mene tililimu kaya azatiponya mu damu la ng'ona وا الله يعلم و احكم
Amayiiiineeeeee!!!! Palibe angati NYO-NYO-NYO pazimene mai ayankhulazi. Opposition you are very pan'yeroful. Simuyitha MCP mungovomeleza you are useless. Ife aMalawi obsauka ndiimene tikuvulala. You are stupid the Opposition,
Kodi kudula kwa zinthu akukuona ndi APM ndi ATUPELE Masa ndianthu njala, kusowa mankhwala, ana kulephela kupeza school fees, akuona ndiamene ukuwanenawo.muziganiza pofuna kulankhula,dyera anthu akumangochi.
Inuyo anthu a ku Mangochi ndinu adyera, mwagulisa vote yanu ndi ndalama. Ndipo olo mutati musazavoterenso DPP kapena UDF, Apm ndi Atupele sangavutike muzivutika nokha ndi nkhanza za MCP.
Ndiponso kwambili zitsilu za kumangochi akuona ngat anthu amene aja angavutik ovutik ndi omweo mahule
@@AngolanChinga Ndipo anthu ofooira zedi, ndalama alandira okha adyanso okha lero akulimbana ndi APM ndi Atupele.
@@JonesChingaya-yf4gg mahule akumangochi ka mitu yao sigwila
Ayao ife sitimawawerengeratu kuti kuli anthu kumalawi kuno 😅
@@user-pe8uh6oq8qkkkkkkkkkkkkkkk Koma ndaseka🤭🤭🤭
Awa adya za MCP .
Kodi Atupele mmene anaigwilira ntchito yokopa anthu muja koma bwanji anthube tisankha MCP ?
Kodi APM ndi Atupele ngati satiuza kuti zinthu zavuta mdziko muko ndie kuti nafe sitingadziwe tokha kuti zinthu sizikuyenda mdzikoli ?
Ayawo ndiokonda ndalama kuyambila kale
Kuwina wa mcp ku mangochi sizikutanthauza kut kumangochiko anthu ndi a mcp,,,kumeneko ndikwa DPP NDI UDF BASI, musamunyoze peter ndi atupele chifukwa cha chisankho cha counsellor,,MUSIILETU ZOMAMUNYOZA PETER KUTI WAKALAMBA,,IFE ACHINYAMATA ZIMATINYASA,,,APM MY VOTE 2025 ISHAALA
Anthu mu kuposita zabodza izi, uyu wa mcp akuyakhulayu panyapako iwe
Nanyongo wake wamcp ameneyo
Choka apa iweyo chisiru palibe chomwe mungatiuze choka choka
Akudyesa banzi galu iwe
Koma a kumangochi ngati mukufuna kuti azikupasani ndalama a DPP ndi UDF simuzatukuka ndipo iweyo amene ukuyakhula ulibe nzeru ngati MCP umayikonda usamayakhule zopusa
Komanso we have to learn a Malawi pazomwe tinachita poika m'boma mimbulu yomwe ikutiluma leloyi. Chakwera ankachita kusasa mau poyankhula asanalowe m'boma, koma now alind soft voice poyankhula. But I hope will not Rpt this anymore
Ndagwilizana nanu amayi inu . A Chakwera anabwera kudzapanga kampeni ku Mangochi kumene kunali kumuthandiza kansala wawo pomwe APM and Atupele sanachite. Zotsatila anawina kansala wa MCP. China ndichakuti Mangochi ndi ya UDF and DPP muulamuliro wawo wonse sanasankheko nduna from Mangochi pomwe MCP inasankha nduna ku Mangochi (Ibrahim Matola). Chonde konzani khalidwe timakonda UDF komanso DPP kuno ku Mangochi. Zikomo
Sakunama munthuyu and Chakwera tidzamuvoteraso akapanda kusamala
Kavotele ndi ufulu wako
Mai mwalankhulatu, ayi ndizoona mukunenazo peter ndi atupele akugona,sanazukebe
Mayi uyu watumidwa ndi MCP iwe mangochi yake umakhala kut mdikukuziwa ine wakwagona ngati iwe
Nanyongo wake
Sakunama ayi Peter angoti phwiiii mnyumba kenako kumati i will win
Vuto rako ndi chani muzimayi iwe ngakhare murandire ndarama tose tipitiliza kuzuzika ndi MCP
Mwadya ndalama za mcp ndiye mudzitokota
Ayi sikut wadya koma ntima ukumuwawa kut anthuwa osakampangila bwanji kampeni mwanayi bwanji.zowawa palibe as dpp ndi as udf osakampanga support Bwanji?sanapange bwino iye sakufuna kut mcp isakhale ndi room ku southerner.koma akuipasa mpata akut aaah zaukhansalazi zopanda ntchito pomwe anzawo zomwezo ndipomwe akuziona zofunika kwambili.adzazindikila atagwa a dpp ndi udf 2025 chifukwa chonyozera zinthu zomwe zisali zosafunikila.so zomwe akutanthauza azikhala busy ndizilizonse a wiliwa.zaukhansala,za u mayor,mp ndi u prezident zomwe.mphwayi ndi tsoka ndipomwe aona izi mcp izilowa chonchi.
Sakunama ngati atopa apume basiii , a mcp akangowina vuto sikubela koma kuzikonda kwa MA oppositions leaders awo, palibe kutosya chala munthu, zikhalani mphwiiiiyo choncho kumadya MA sausage wo
Kodi ndindani namachende ameneyu... ??? Walandila zingat Ku MCP??
Nanyongotu uyu
Ayao ufulu wawo samauziwa. Koma ndalama basi. Peter ndiwachikulire, anakapedza wina oimira Dpp. Tupere ndiozikonda, uzimva ndalama
Muluzi ndiworakwa anatenga arendo chipani cha UDF kusogoza arendo rero mwawonatu
Akunena zoona ameneyu ngakhale mukumutukwana....APM & Atupele were supposed to campaign for their candidates....chisankho chinali mkhonde mwawo why they didn't show up?
Koma 3 kwacha inampelekaadi yesu 😂😂 Awatu zilipo alandila
Ndipo kwambiri tu mmm
😂😂😂😂😂😂😂
Nanyongo wako Uona chomwe chidameta nkhanga mpala siudya bwino ka 2kwacha akupatsako anzakoo akuba zochuluka tikulira limodzi ndiiwe wemwe nanyongo wako
Kalindo anayamba kale akukutakatani koma inu dyooooooo ngati akukumetani
Akutuma iwe, olo president akanabwera ndiye akadavotera councillor? Inu ndi ofoila
Wachita kuinekelatu kuti akutuma
Mwadya zingati bwana
Ndiye osangovotela MCP yo bwanji chosokosela ndichani
I'm a gree with this guy cuz chiyembekezo cha a Malawi nd Dpp koma kuiyonaso Dpp yakeyo siyoifela ayi anthu akulila koma iwo szikuwakhuzaso ayi
Iwe usalire.zimthu zili bwino.ngati umachikonda chipani cha DPP dziwa zilibwino.
Inenso mjomba zandinyasatu kwambiri.Mwambi uwu upite kwacha dpp ndi dug
Chete chete sausa nyama komatu hoi hoi.uyoo uyoo.kapena kuti ndakuona ndakuona
Chilungamo icho mzowonadi ineso ndakwiya nazo ,kumangochi Pana mcp Aaaaaaaaaaaaa chitaponi khanthu mabwana a DPP komaso mcp please please, zikomo.
Kunena chilungamo munthuyu akukamba zoona Amuthalika ndi Atupele mukupanga zithu zauchisilu kwambiri ndalama muli nazo koma kuumila ndi kusathandiza kupanga Campaign basi
That's why analandidwa boma....kupepera too much....mmene imachedwera milandu kut akagamule kuma courtko akufuna azizapitisa nkhani ya ma I'd mu august chaka chamawa, kulemphera kuwaunikila komabe sakuonapo vuto...ndaikonda mcp kwambili
Don't trust who's talking this nonsense
Ndipotu muzawina inuyo mwadya chim'basi cha mcp or mwanyoze bwanji a opposition inuyo nde adyerawo
Tiye uko kape tizingodyani zimene akupasa zo chikwela
Kugulitsa vote chifukwa cha ya singachite
Zoooonaaa auzeniiii afasa mopusa kwambiri
Mukufuna mumuphenso chifukwa chaukhansala udikire ukuona September ino iwe khala ndi chakwerayo,,
Akutumani mwina
Sanatubwe koma akunena zoona kwambili akuluwatu
Ukufuna upusise ndani badyerera paja anakupangirani sadakatu inu---- kukonda kusheta
Kulakhula kwambili mwalakhula bwino kwambili muthu wamkulu otsutsa boma palibepo akupanga athu akungodikila kuti akhale president akhala bwanji ngati makhasala akuluza chamba basi
Olo ikhazikike MCP ndiye mumpuza ndani
Achituma ichi😂😂😂😂 adad okalambawo 2025 akudzakulamula pusi iwe
Et
Palibe chomwe ulankhula chakwera agula mavoti koma come 2025 sadzakwanitsa Malawi onse. Iwe galu anthu safuna afuna ulamuliro okomela onse
Akutumani ndi ayaniso inu musatinyasepo? Ingopephani inu,,iwe usatinyasepo wamva ifeyo tili kuno kulilongwe komwe kuli azako a MCP ukunenawo,,wadya zambiri za MCP anakupezawo.
Kod mcp kumwaza ndalama zosez akufunabe kuyimila ziko kumachita kut amalawi sakwafuna bas kufuna azingokubabe
Nanyongo wako mai iwe ...oipa anthu akumangochi dyela ....akalamba amako
DPP inapita ndimwini wache Bingu...
Inuso nanu mukulankhula zopanda nzeru mukuona ngati mukulankhula zanzeru
Uko ndiyekuyankhula anthu awa sakudziwa zomwe akupanga amangofuna azilemela okha
Zoonadi atsongoleli apngeni athunu saport
Zikugonadi kwambili mbuzi zimenez...anthu kuyeseera kuwakonda but they are too selfish....chilichose kumangoti ku page house,akufuna misonkhano azikapangila ku page house komweko.....yachita bwn mcp ndipo tiyivotera...awa even akazalowaso mboma kupepera kwake kudzakhala komweku...
Awa sakuliziwa boma lolamula kodi saziwa kut boma lolamula limakhala ndikuthekera kowina mmene akufunira
Audio iyiyi ndiyowona anthuwa ifewo timawakonda koma za Ife saziwelengela popeza ndi anthu a ndalama zawo it's okay ifewo tifeyo tizivutika mene tililimu kaya azatiponya mu damu la ng'ona وا الله يعلم و احكم
Peter wakalamba , chifukwa chache chisale azingomudyera mkazi wakeyo
Akutumani a mcp kuti muyankhule izi.
Moti khansala ameneyo alamulira mpaka 2030? Nde mmene mwavotera mcp kudela limenero katundu watsika ntengo kumeneko?
Manyaka amzimayi osavinidwa iwe.
Mwapaga nonkja dyera chifukwa Cha ufa ndi 5000 yochokera kugulu la chikagawa anthuwatu malamulo akuwadziwa musayelekeze ndi buli yachikagawayo akayayendaso tiyamba kunena kuti mwalawira kuyamba ka mpeni tinkhala tikulubwa zabili ndiye siku zipanizi sizikudziwa lamulo komano opupwa ndamalawi aku magochiwo komaso zoberazo
Mpaka kupanika kukhosi, 😂😂 bwanji osangonena kut mwamva kukoma chifukwa chot khansala wa MCP wawina, za ziii
Choka iwe usapusise anthu. Ndiwe wa mcp. Pasanapakoso
Nsalu zikutandizani chani moti muzimuuza chakwera wanuyo kuti asise zinthu bwanji
Simukunama mjomba ichi NDI chilungamo
Ndiiwe chitsiru aise. Ulibe nzeru
Fada iponde
Amazipasa udindo
Every time same leader the mtalika
And the muluzi boring
Kkkk ayi mvuto ndinu anthu akumangochi nokha sikudziwa kuyipa komvotela mcp mene wawonenfila chakwela paka kupasa khasala nde mumafuna a dpp ndi udf akuwuni kuyipa kwa mcp aaa pena anthu akumangochi mumawoneka ngati ochenjela kuma ayi tulo basi mafumu dzisilu nde mumati udf olo dpp adzikuwudzani dzochita kkkk khasalayo wachitawo wangalusa apa kulusati aku paka mcp amangochi kukodze nyumba ayu dyela kwambili nde mcp akusangalala ndi uchisilu wanu achiyawo dzikani dzukani
Galu wamunthu wadya ndalama Za amcp
Basi tiyeni tizingovotera mcp iyo tizivutika tose tizifa tose chocho
DPP ikugonadi kalindo amayankhula kale
Machende anu mwadya za mcp ayao wophusa adyela
Mbuzi yamuthu palibe nzelu kd ndimamuna nkaz sindikumvesa
Peter mutharika is too old we have said. this several times
Wayankhulayu akundinyasa ngati manyi ake
Opepera ndinu ayao akugulitsani fertilizer k110 000
Inu ndi zisiru izi zakalamba sizikufuna tikungozikakamila tizijowa zikungotimanisa zabwino palibe zoti atibela tulo takale ndiye akundinyasa pomwe ndikuwaonapo
Galubwako😊
Zoona peter ndi atupele atilakwira komanso atikhumudwitsa 2025 atisamalenso tikonza kugulitsa mavote athu.ku MCP komweko anthu amenewo angokhala duuuuuuuu
You're alright my friend
Nde nchawadi, kulalata choncho, wakwiya.
Zamwanyazi kwambiri, umbombo zipani izi, akati tiyeni tikamwe tea ku page house eee amayenda chothamanga
Mumadana ndichilungamo
Tiyeniko inu akutumani inu munganene chani choti mungafokese anthu za ziiiiii.wakula chani
Aaa mayi inu mwadya zambili mufuna mumupheso
Iweyo ukunenawe akutuma Iweyo udali kuti?
Mbuzi iwe wadya ndalama za mcp
Vote ili mumtima hiyaaaaaa
Zopusa basi zangondionongela bandle
Komatu atupeletu samakakamiratu izi komanso kuyankhula koteroko mbali ina siukuyankhula bwino wadyera ndiwe anthu samapanga ndalama ndicholinga Choti azikupatsani zaulele ayi nawo alindimavuto awo komanso kuyankhula kopusa ukuayi anzanu amafuna kuona kuti kubera kwao kuzayambapati ndiye paoneka iweyo ngati wapatsidwa ndalama galu iwe uona kuti anakutumawo akuonedi
Amayiiiineeeeee!!!!
Palibe angati NYO-NYO-NYO pazimene mai ayankhulazi. Opposition you are very pan'yeroful. Simuyitha MCP mungovomeleza you are useless. Ife aMalawi obsauka ndiimene tikuvulala. You are stupid the Opposition,
Wasowa zochita zandalama funsa chakwara hule tsek
Chakwera anakupatsan ufa watha apa mwayamba kuliraso chokan agalu inu mukusokosa mesa mwavota kale pasana pako
Izo ndizoona agalu awa ndiokwana ine nde anandibhowa kale
Kodi kudula kwa zinthu akukuona ndi APM ndi ATUPELE Masa ndianthu njala, kusowa mankhwala, ana kulephela kupeza school fees, akuona ndiamene ukuwanenawo.muziganiza pofuna kulankhula,dyera anthu akumangochi.
Chomwe akuyankhula sakuziwa Chakwera adaononga almost 5million kuhonga wanthu koma MCP no more 2025
Vuto ndinu Anthu Akumangachi osavotela Adadi bwanji uligalu kwabasi inu simumaziwa kuti mukuvotela MCP dyela mangochi
Umphawi wamukwana uyu zisiyeni inu azelunu bapangani kampeniyo
Inu kuvutika ukuku mkofuna kuteroko adad akusekan paja mumkat mukufuna kusitha pitilizan kusithako atifinyadi ana osamva inu
Koma. Munthuyu akuyankhula chilungamo
Chiticho
kusonyeza kuti nonkha simukuwona mumafuna akupangileni kapeni
Ndiye vuto la zipani za pamtundu kkkkkk
Alakwa ndinuyo achina kinka makoloni