Am happy for Malawi. We need strong parties to compete inorder for the best to emerge at polls not having only one strong party in a nation of 20 million people it's unhealthy. Bravo DPP.
Am very glad to see you all attending a great NGC we have been waiting for a grace period of time and congratulations to you all in that wonderful room may God do wonderful things on behalf of your NGC services in order to come up with better results for the betterment of the candidates who will bring back Malawi's fruits to be fruitful to all Malawians,,,,,,,all the best guys.
Bravo to you newly appointed Dr clement Mwale indeed you know your description, you plead for these prodigal sons and daughters, you know that politics is game of numbers, this is not the time to loose anyone, when you are approaching convention, you need every member on endorsement, welcome nsonda,
Bravo my believed DPP this is the way to go,2025 tikuyiphula infact let me make it clear that nnali mmodzi Ochoka ndi chilima koma pano nnabwerera and I vow not to leave DPP again😂😂😂❤❤
This is what we have been wairing for", I like the way how He's Excellency shouted Mr Nsonda , Yes I agreed with He's Excellency for what ever he has said concerning Nsonda ..Mr Nsonda he is untrustworthy man n' he is hypocrisy. Much love to my Country watching from SOUTH CENTRAL L.A USA
Watching from south africa imeneyo ndiye dpp osati za a Nakhumwa ndi azawo anja a mcp ndipo sakufunika ku dpp achoke basi muthu kukhala leader of opposition Koma kumakanika kutsutsa ku parliament he is useless
Ineyo monga mr Raphael Katimba ndikungofuna kuwathokoza a president a chipani cha DPP ndipo zaonetselatu kuti a Peter Mutharika democracy yathu kuno ku Malawi amailemekezadi . and why i am saying this? Choyamba amudzudzula Nsonda poyela kuti iyeyu akakhala kumbali amawanyoza kwambili komanso Nsonda simembala wa DPP koma iyeyu anachita kubwela kuchokela ku chipani cha PP ndiye ayankhunso kuti Nsonda ali ndi ufulu kubwelera ku chipani chawo komanso ayankhula kuti iwowa monga president wa chipani sakukwiila wina aliyense ai. Komanso ayankhula kuti anthu onse amene amatengela chipanichi ku Court adziwe kuti aonongetsa ma million ambili ku chipanichi. ndanena dziko kuti mafiya ndichifukwa chake akuonda ndi mutu omwe. DPP oyeeee 2025 ikulowanso boma
I wish DPP gave the best Opposition than the nonsense have right now Otherwise Strong opposition results into good governance. Stop The nonsense disagreements
Mukuona ngati Peter muthalika angakonze mavuto a dziko lino. Izi zinayenera zichitike basi tili kumapeto adziko. Konzani moyo wanu lapani machimo, zonse mukuzionazi zikungosonyeza kuti wayandikila Yesu kubweranso
Am happy for Malawi. We need strong parties to compete inorder for the best to emerge at polls not having only one strong party in a nation of 20 million people it's unhealthy. Bravo DPP.
Am so proud ❤❤❤mwaitana onse koma...amene sanamvewo atengana kosayamba chake chipani monga gerezedar ndi mamuna wake nakhumwa andi owasatira awo budzi zonkha ...zonkha mene zikubebera izi zadongosolo azitulusa onkha namabodza pamenepo phati g
Kkkkkkk 🔥🔥
Watching from south Africa Pretoria and I am very excited for this NGC MEETING ❤❤❤
Am very glad to see you all attending a great NGC we have been waiting for a grace period of time and congratulations to you all in that wonderful room may God do wonderful things on behalf of your NGC services in order to come up with better results for the betterment of the candidates who will bring back Malawi's fruits to be fruitful to all Malawians,,,,,,,all the best guys.
Im very happy indeed we need adai to rescue Malawian facing more challenges in this country pple suffering now than before more fire
I can't wait to see you back in the government boss , you deserve to be the boss
Ine ndwakondwa kwambiri, mtima wanga wasangalala. Kuno ku Dedza anthu akuvutika kwambiri. Akugona ndinjala , ngakhale gaga akusowa , koma zimenezi kunalibe. Lero zakhala bwino anthu awone kusintha . God bless Malawi.
Bravo to you newly appointed Dr clement Mwale indeed you know your description, you plead for these prodigal sons and daughters, you know that politics is game of numbers, this is not the time to loose anyone, when you are approaching convention, you need every member on endorsement, welcome nsonda,
Iyi nde yakunganatu 💪💪💪💪
Bravo my believed DPP this is the way to go,2025 tikuyiphula infact let me make it clear that nnali mmodzi Ochoka ndi chilima koma pano nnabwerera and I vow not to leave DPP again😂😂😂❤❤
AM GOING TO GOVERN OUR NATION THE DAYS OF POLITICIANS ARE NUMBERED SO HELP ME GOD
Very colourful and fantastic. God Bless the DPP
Adad omwewo sizinazo ai yanga voti pa adad from Maputo Mozambique
My happiness has been restored 🔥🔥🔥🔥
What a relief , finally my beloved party showing a sign of life. Congratulations
The Father has Spoken and we love you So muchite Dad.
This is what we have been wairing for", I like the way how He's Excellency shouted Mr Nsonda , Yes I agreed with He's Excellency for what ever he has said concerning Nsonda ..Mr Nsonda he is untrustworthy man n' he is hypocrisy.
Much love to my Country watching from SOUTH CENTRAL L.A USA
Imeneyo ndie NGC timadikila ifeyo,osati ya MCP ija ai!!!achina Dausi,,Nakhumwa zitsilu zawanthu
Muwasamale anthira kuwiri alimommowo, msonda and his friends, they're not for DPP party, they belong to mcp cruel party
Respect leaders, that's very true. All the best DPP NGC meeting
Koma chipililo penganjira ndi wa Zeru
Adandi kuwonda mwatha mukalowa boma mumadya bwino kwambiri kwabela amalawi mukufuna munenepeso sizitheka mungoyamba business yasomba kunyanjako bas akolo 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Am happy that chisare is out
Congratulations you guys appreciate you for that fantastic NGC meeting ❤❤❤
Nkhope zopanda mantha
Adadi is lukng gud
I am very very happy to the strong meeting l never see in my life
Peter is mature enough, about Ken Msonda and Nankhumwa shame
Ken Sonda ukutaniko kumeneko kape iweyo kwambiri
Adadi moto kuti buuu🎉🎉
Proud of you guys, 2025 DPP Bomaaaaa!!!!!
Ine ndamva kukoma kwambili ndi msonkhano umeneu ❤
Thanks APM that's the way to go
I'm from Northern living here in South Africa, to my side I love Dpp and I want to see the part untied
Nankhumwa galu wa chebe chabe usabvutike
Watching from south africa imeneyo ndiye dpp osati za a Nakhumwa ndi azawo anja a mcp ndipo sakufunika ku dpp achoke basi muthu kukhala leader of opposition Koma kumakanika kutsutsa ku parliament he is useless
bomaa iloo adady woyeeeeee dpp woyeeeeee ❤❤❤
Kha ngc siimeneyo aaaaaa🥳🥳🥳🥳🥳
I'm very happy with this NGC meeting osati zosokoneza zija
Iam very very happy with this meeting .....we are behind apm
NGC koma iyi osati ijayi ya zifwamba yachitika last week ya anyamata Malawi Young Pioneer ija!!!??
Very happy
Ayambaditu kale kunjenjemela kkkkkkkkkkk
Wow!!!45 Family member's DPP..thats very good numbers..God is Good
Apm 🔥🔥🔥🔥🔥
Am so proud of you guys keep it up
A dad ndi machine 2025 awina kle
Guys Msonda Akita akutaniko kumeneko yudasi
Timakunyadiraa kwambiri Mr apre
Aliyense Adad, Adad, Adad,,,,,our father APM 100%❤❤❤❤ 2025
Amalawi ataphunzira kuti nsanje simapindula chiyembekezo chao chili mwa inu adad koma osamuiwala atupere muluzi ndi mnyamata odekha
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤A P M 🔥
Watching from South Africa
Koma mbali ya ana ija akuva bwanjii
Nice
#viva DPP #viva....viva ADAD....Viva DPP Family..
This is most loved meeting
Live from Durban South Africa ❤❤❤❤
I'm glad to see DPP comes together again adady woyeeeeee ❤❤❤❤❤
Welcome back DPP🔥🔥🔥🔥
More fire Dpp
Adadi mumusamale mfiti nsondayo ndigalu kwambiri
❤❤❤❤
Tikudikira inu adad
Happy to hear this
Nice for Malawi 🇲🇼..........long live AMP
Zoona adad omwewo
Paline chazeru apa mumalo mopanga chimozi kutukula Malawi mulibbusy zaukape panyapano😊
Nankhumwa & grezerder shame, anthu osafunila dziko zabwino manyazi bwa?
That's what we were expecting ❤
Watching live from Paramaribo Suriname
🙏🙏🙏
Chisale pa ntchito yake
Mitu ya dpp nde imenei
Heavyweights All de best.
Chipani chongodzadza ndi nyambaro.....nanga achina big joe akutaniko kumeneko
Ineyo monga mr Raphael Katimba ndikungofuna kuwathokoza a president a chipani cha DPP ndipo zaonetselatu kuti a Peter Mutharika democracy yathu kuno ku Malawi amailemekezadi . and why i am saying this? Choyamba amudzudzula Nsonda poyela kuti iyeyu akakhala kumbali amawanyoza kwambili komanso Nsonda simembala wa DPP koma iyeyu anachita kubwela kuchokela ku chipani cha PP ndiye ayankhunso kuti Nsonda ali ndi ufulu kubwelera ku chipani chawo komanso ayankhula kuti iwowa monga president wa chipani sakukwiila wina aliyense ai. Komanso ayankhula kuti anthu onse amene amatengela chipanichi ku Court adziwe kuti aonongetsa ma million ambili ku chipanichi. ndanena dziko kuti mafiya ndichifukwa chake akuonda ndi mutu omwe. DPP oyeeee 2025 ikulowanso boma
Best ever ❤❤❤❤❤
But better kumayankhula zomanga kaya...choncho mugwirizana?
I love you Guys Viva DPP
APM ❤❤❤❤❤❤❤❤
A.P.M more fire
Chi combination cha ma....... 😂
This is what we call corrum
Boma ilo ana achepa🤣🤣🤣
❤dpp
tikudikira inuyo
Tsongolo la malawi 🇲🇼🎉
Viva Dpp viva apm
I wish DPP gave the best Opposition than the nonsense have right now Otherwise Strong opposition results into good governance. Stop The nonsense disagreements
Mwangisowa chonena Inu zinakusangalatsani ndizijazi zadzana
Make sure united you stand, no camp has any significant chances of success
Timadikilila mau Ngati amenewa apita Kodi mumachedwa Kuti ndimauwa nsonda ndiwoipa kuipa ndinkhope yomwe Mutu Ngati mbeza yowezela achule
Live from Sandton Gauteng
Koma nsonda ndi akamuna eeeeeee ayi ndithu
More fire❤❤❤❤❤❤❤
Zosagalatsa
A peter hoeeeeee❤❤🎉
I'm hearing only Tumbuka names here
Adad anafe timaikonda DPP chifukwa chainuyo adad osati anakhumwa magulu wachabe chabe