BON KALINDO LERO PA 11 JULY 2024 |

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 9. 07. 2024

Komentáře • 117

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 Před 20 dny +15

    Bon Kalindo,Kamlepu Kaluwa,Comrade Ntanyiwa,Wanda Msiska and his friend,Brian Banda and others you are really philanthropic and patriotic. May God bless you abundantly.Religious,political, traditional and social leaders here in Malawi are all ordained to the mentality of cupidity hence very unable to transform Malawi philanthropically and patriotically.

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 20 dny +4

    The DC mwana wayankhulira m Malawi mommuno osati mpakana kukabisala ku Zambia ayi chi Bon Kalindo chinatha mantha ndipo sichiopa Unyolo anta more 🔥🔥 Mr president waife anthu osauka😅😅😅😅

  • @BlessingsMbawa
    @BlessingsMbawa Před 19 dny

    Bon kalindo iweyo umatha kulankhula bwino. Chifukwa kulankhula kwako umanena zoona zokhazokha kumvera chisoni amalawi munyengo zowawa zomwe tikudusamo kamba ka utsogoleri olephera wa chakwera. Osafooka , osatopa mpakana satana ameneyi tithana naye 2025 ino. Keep it up wakulu ndimakunyadirani kwambiri

  • @ChrissySalimu
    @ChrissySalimu Před 19 dny +1

    Sikusinja imweyo kkkkkk taimbaso Mr DC aifeeee❤❤❤

  • @ishmaelcassim806
    @ishmaelcassim806 Před 20 dny +1

    Mr bon kalindo you are number one. More fire Mr dc❤

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 Před 19 dny +1

    🤣🤣🤣🤣🤣 ngati Malawi ndiwandani Mr DC

  • @ThompsonMakwakwa
    @ThompsonMakwakwa Před 20 dny +2

    Aaaaaaaaaaaaaa@ koma nde zafikapotu mpaka muchenga machende awo ndithu

  • @user-gm3cx2xn9o
    @user-gm3cx2xn9o Před 19 dny +1

    Ife si osauka ndipo sitisilira kukhala ndi president osauka😂😂😂😂😂

  • @JibuzahDrag
    @JibuzahDrag Před 20 dny +1

    Fire Mr president mumayakhula zilungamo zokha zokha

  • @AfricanKingdom-uv1qb
    @AfricanKingdom-uv1qb Před 19 dny +1

    God protect mr DC

  • @ChristinaSinoyakapawo
    @ChristinaSinoyakapawo Před 19 dny +1

    Ndabwereza kawili nyimbo yoooo anaphaa mubale wake gwenembe chifwukwa cha udido

  • @hajrazuwaja4993
    @hajrazuwaja4993 Před 19 dny +1

    😂😂😂amangidwaso uyu ndithu sikusinja ndi gwenembe koma Mr the DC kkkkkkkk

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje Před 19 dny +1

    We love you the DC

  • @richardkumbambe-tg9qi
    @richardkumbambe-tg9qi Před 20 dny +2

    Great indeed. Let's all rise ip.

  • @user-qc5lh3xw2h
    @user-qc5lh3xw2h Před 20 dny +1

    Powerful Mr president ❤

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd Před 19 dny +1

    Mwana wowopya kwambiri!!!!!!!!!❤❤❤❤❤❤

  • @user-cg5ml7ym4v
    @user-cg5ml7ym4v Před 20 dny +2

    Tili pa mbuyo panu DC ❤❤

  • @AbdulsEdsan
    @AbdulsEdsan Před 19 dny +1

    Mr Kalindo great soldier

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba Před 20 dny +1

    😂😂😂😂😂 malawi ndife makape timaopa muthu ot tamuvotela tokha

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah Před 19 dny

    Bon kalindo dddccccc❤

  • @julietmussa5103
    @julietmussa5103 Před 19 dny +1

    Sikusinja ndi Gwenembe yemweyo....ana amphunzile

  • @Moses51
    @Moses51 Před 19 dny +1

    The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉🎉

  • @user-ln5hw7dn9g
    @user-ln5hw7dn9g Před 20 dny +1

    Ndakhalira kuseka😂😂😂😂😂😂 iweyo ndi wani

  • @fatsanibanda5213
    @fatsanibanda5213 Před 20 dny +1

    Yes iweeee ing'alure basi😂😂

  • @chrisneySwanepoel-yu5vd
    @chrisneySwanepoel-yu5vd Před 20 dny +2

    God protect mr kalindo

  • @bamusmajawa1619
    @bamusmajawa1619 Před 20 dny +1

    Mr Bon Kalindo on fire 🔥🔥💪

  • @JosephPindani
    @JosephPindani Před 20 dny +1

    Km chakwela watopa m'chenga mpaka nd wa boma kkkkkk😅😅😅😅😅

  • @AubreyBamus
    @AubreyBamus Před 16 dny

    My vote bn

  • @PeterMoosa
    @PeterMoosa Před 20 dny +1

    More fire mr winiko

  • @user-mi3fw1zg8b
    @user-mi3fw1zg8b Před 19 dny +1

    😂😂😂😂 Mr DC

  • @shamimmahomed6709
    @shamimmahomed6709 Před 20 dny +1

    Bon kalindo yemweyo kuti wawawa!!!

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Před 20 dny +1

    😂😂😂 koma ndaseka DC ayi taa sikusinja Kodi

  • @JuvenileDebwe-bv8ow
    @JuvenileDebwe-bv8ow Před 20 dny +1

    kkkk koma chimwana chakwa njedza kkk

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Před 20 dny +1

    Kkkkkk wapolice samwa ambuye nditengeni

  • @user-sp4kn8rh2j
    @user-sp4kn8rh2j Před 19 dny

    Hahaha kwachema 🔥

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 20 dny +1

    Make mbuuu mwana mbuuuu 😅😅😅

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m Před 20 dny +1

    The Dc ❤❤❤❤

  • @thandothando6556
    @thandothando6556 Před 19 dny

    Super super😂😂

  • @AdiniKhama
    @AdiniKhama Před 20 dny +1

    Mr DC osafowoka

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3z Před 19 dny

    ❤❤❤❤smdc

  • @user-mx5cx3gl4h
    @user-mx5cx3gl4h Před 19 dny

    Osafowoka bon kalindo

  • @user-fd7wj3mg2i
    @user-fd7wj3mg2i Před 19 dny

    Mulungu azikutetezera nkhondo mukuimenya

  • @AlexNkhata-c8n
    @AlexNkhata-c8n Před 19 dny

    Zoona akunena B kalindo

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d Před 19 dny

    The DC!!!!!!!!!!!!!!!

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 20 dny

    Tang'alulani the DC kuti atongwe-tongwe a MCP amve bwino lomwe. This Boniiii Kalindo the DC, mlowa mmalo mwa Solobala amene ananyongedwa pa makako nda agalu MCP ya Kamuzu ndi John Tembo

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt Před 20 dny

    Bwana apolice atraffic akuonjeza bwerani mnseu wa Bunda every 200m atraffic ndie a area 3 amabwera 3koloko am kuyimba pa mnseu mmmmmmm Malawi

  • @user-tm6wl5tt3u
    @user-tm6wl5tt3u Před 17 dny

    Umakwana iweyo

  • @RabsonSabit-nc5ds
    @RabsonSabit-nc5ds Před 19 dny

    Uyu ndi nyoooo

  • @JasperKaleni-dx6nn
    @JasperKaleni-dx6nn Před 19 dny

    😂😂the dc

  • @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un

    Bon kalindo tili limodzi

  • @PachaloShaba-pf5vw
    @PachaloShaba-pf5vw Před 19 dny

    Good boy

  • @van-wykchilapondwa6981

    Great 👍

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu Před 20 dny

    Kkkkkkkkk koma a Kalindo agogo anu ankakuuzani nthano ya sikusinja mukupita ku nzuzu , ndiye mwati ankakuwerengeranu mu chikangawa? Komanso mwati anaphana chifukwa cha udindo? Ndipaseni page ndiwerenge nawo basi . U are number 1

  • @MemoryKamanga-jv4jh
    @MemoryKamanga-jv4jh Před 20 dny

    You are welcome Mr dc

  • @irenioeugeniosumila6647

    Ulemu wano A Kalendo

  • @frankdonovanntambira
    @frankdonovanntambira Před 20 dny

    Ndipo Boma Lamanyi ngati ili ine sindinalionepo Aaash!!

  • @IssahAluba
    @IssahAluba Před 20 dny

    aaaaa zayambika liti tchega omwewu gati mwatopa nawo phandowo apatseni ena MCP is very nonsense iyaaa

  • @griviniakanjaula4456
    @griviniakanjaula4456 Před 19 dny

    More fire mbuyanga alomwe alomwe nophiya

  • @user-ng4ic8jo8b
    @user-ng4ic8jo8b Před 19 dny

    Koma iwe ndigalu kwambili

  • @RichmanNkhoma
    @RichmanNkhoma Před 20 dny

    Mbambande me. Kalindo

  • @user-vq6zr4tn8v
    @user-vq6zr4tn8v Před 19 dny

    Muma tiimila osatopa

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Před 20 dny

    A opposition zochita zamwo ndi zimodzimodzi

  • @JohnZyambo-q8h
    @JohnZyambo-q8h Před 19 dny

    ❤❤

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Před 20 dny

    Kulephera kuja ndi kumeneku, anthu ndi okwiya kale , atopa ndi boma ili

  • @Chipilirodaniel1989
    @Chipilirodaniel1989 Před 19 dny

  • @JohnZyambo-q8h
    @JohnZyambo-q8h Před 19 dny

    🎉

  • @scoltenroma6240
    @scoltenroma6240 Před 20 dny +1

    Kuswa kuswa😂😂 akavote ndiamawo Oh yes 🔥🔥

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu Před 20 dny +1

    Koma ndiye mwafikapo mpaka kulesa anthu kuti asamavuule mchenga really? Nyumba zanuzo munamangila mchenga munakawoda ku America? Silly people

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt Před 20 dny

    Atsala atigulitsa mphweyaa kwatsala

  • @TapiwaKhwisula
    @TapiwaKhwisula Před 20 dny

    Mo faya mr dc

  • @SilenceChepiano
    @SilenceChepiano Před 20 dny

    DC ndimava kukoma mukatiyimilira

  • @charitykalua8507
    @charitykalua8507 Před 19 dny

    The DC😂

  • @JamilahChitulu
    @JamilahChitulu Před 20 dny

    😂😂❤

  • @MecyMalothi
    @MecyMalothi Před 20 dny

    The D C!!!!

  • @Aisha-db6ds
    @Aisha-db6ds Před 20 dny

    Eeeee koma ationjezadi apa ndiye yalakwa,,
    Tipindilana ndenvu mkamwa ulendo wake ndi umeneu

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no Před 20 dny

    Anapha zake chifukwa chaudindo

  • @stevejizaremu3396
    @stevejizaremu3396 Před 20 dny

    The DC

  • @StanleyChirwa-d6b
    @StanleyChirwa-d6b Před 20 dny

    Koma Chaka chamawa tikhapana ndithu

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar7468 Před 20 dny

    Koma why sakuyamkhulapo za manganya ku mcp palibe audio olo imoz inakambapo za Mr usi

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr Před 19 dny

    Ipondeni Fadah

  • @SolomonShaibuh
    @SolomonShaibuh Před 20 dny

    Ndkhulupilira kut a Malawi mistake iyiyi sitizachitanso

  • @FrancisChimwaza-t7d
    @FrancisChimwaza-t7d Před 20 dny

    Iswani ndithu man wamkulu ndi mulungu basi

  • @phillgatoma4857
    @phillgatoma4857 Před 20 dny

    😢😢😢😢😢😢

  • @KennethMchenga-j9c
    @KennethMchenga-j9c Před 20 dny +1

    Pliz a DPP tadzukani kodi mukunafuna amalawi atani

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 Před 20 dny +1

      Ndipo zomwe akupanga a Dpp akumabowa kwambiri anthu akuzunzika ndi boma Koma aliphee ngati akumetedwa

    • @IbrahimYusufu-z9d
      @IbrahimYusufu-z9d Před 20 dny

      Akufuna tidziwe kut tidapanga mistake.. ankatiuzatu paja

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 Před 20 dny

      @@IbrahimYusufu-z9d ndiye bola akazaluzanso asazalile chifukwa agalu a MCP akuwatakatu osusawa

  • @lawrenceblacktealyson8015

    I don't want to be Malawian anymore

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Před 20 dny

    Km inuyo mumakwana kkkkkkkk the Dc

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Před 20 dny

    Mitu singwiradi.anthu onse anafa aja mwanzi wawo sukhara chete.

    • @JeanKambala-gm1zr
      @JeanKambala-gm1zr Před 20 dny

      Mwazi unja wakuchingawa ukuwayenda Mitu anthu amenewa mchenga wobwela ndibvula 😅😅😅😅

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Před 20 dny

    Kodi achakwerawa mchiyani makamaka zikuyenda koma??

  • @FrankiePangan
    @FrankiePangan Před 19 dny

    😢😢😢😢

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt Před 20 dny

    Bwana ine office kuno ku Lilongwe tikupita kokayang'anira mayeso koma no allowances 😅

    • @PeterChilombo-ou2cd
      @PeterChilombo-ou2cd Před 20 dny

      kkk iwe usandiseketse no what?aa. wabodzaiwe

    • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
      @ChikumbutsoJohn-rs4tt Před 19 dny

      @@PeterChilombo-ou2cd ok u can not believe it,maybe your side, koma kuno tili sanatipasebe za Theory subjects

  • @muneeladan8580
    @muneeladan8580 Před 20 dny

    Mafia

  • @RidsonChafulumirah-r2y

    DC

  • @isaacchiwaula731
    @isaacchiwaula731 Před 20 dny

    Ubwino wake a Chakwera omwe mukuwanenawo sakuyankhani nkomwe, mumangobwebwetuka zaziii ngat ufulu omwe mumamenyera anthu osaukawo umathandizapo kalikonse, tikungogonabe ndinjala ngat mumati mukayankhula apa mumatipatsa ndalama, phindu lanu ndichani, ine ndiye nsaname zimandinyasa izizi, palibe chomwe munthu wanzeru angayamikire pazomwe mumayankhulazi, coz maboma onsewa zochitika ndizimodzi palibeso wabwino apa, n zonse izizi zilibe nzeru, nanga mpunga souseg zimenezo zikankhale zoyankhulira anthu osauka kapena zangolowa zidani zanu?? Zopusa

    • @StanleyChirwa-d6b
      @StanleyChirwa-d6b Před 20 dny

      Samayankhatu mosathepo mau ap😅😅😅

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon Před 20 dny

      IWEYO ndi opusa kwambiri ndi chakwera wakoyo ngati akutuma cadet mbuzi, ngati iwe ukidya ndi mcp usawanyase AMALAWI AKUVUTIKA , ndiye uzikayankhula mbwerera zako zankutuzo , ngati sizikusangalatsa amakutuma kuti uzimvera ndi ndani ulibe manyazi ? Cadet supit

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 Před 20 dny

      @@HalisonSolomon ukufuna ndikuyankhe? Born kalindo umamudziwa? Zomwe akumayankhula amayankhulira iweyo, it's wat u think? Ok kavotere amene ukumufunayo n uzandiuze kut zinthu tsopano zilibwino pamoyo wako. Kalindo sankatukwana DPP ndi Peter munthalika? Lero mwaiwala

    • @StanleyChirwa-d6b
      @StanleyChirwa-d6b Před 20 dny

      @@isaacchiwaula731 inu musokosa mungosiya kuverako bas sizokakamiza izi boss

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon Před 20 dny

      @@isaacchiwaula731 iwe sungamakhale KUMBUYO kwa mcp ngati sukuona momwe dziko lavundira ndiye kuduka mutu kumeneko , usiyamitse mene chakwera amatenga boma linali motani ndiye pano zilimotani ? Ndiye timusiye chakera alamuleso lidzakhala dziko? Anthu adzakhala ngati ndani, tiyeni tiganizire ana omwe taberekawa tisakhale ngati a police ndi asilikali amene asankha kigwira ntchito ndi chipano malo moteteza malamulo adziko,

  • @BudaEarth
    @BudaEarth Před 18 dny

    U na problematic

  • @chadreckchibwithala1493

    DC PANTCHITO IFE WOZIWA ZINTHU WE KNOW KUTI ABONI KALINDO ALIPO PA NTCHITO YOSUTSA CHILICHOTSE NDE MUWONE ALOMWE AVEKERE EEE OOOO UUUU KUKUWA AGALU ACHILOMWE MKUNYA MCP IS GOING NO WAY 2030 WOOOOO CHAKWERA.

    • @JeanKambala-gm1zr
      @JeanKambala-gm1zr Před 20 dny

      Zosantheka Brazil ndipo idzankhala yazikwanje zomwe² mwaphela saulosinever again MCP achimwene

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon Před 20 dny

      2030 mcp ikakhala mnyumba mwa kwanu zopusa anthu opanda nzeru ngati akukudyetsani ndiye muphe anthu chifukwa choti mukudya ndi mcp yakuphayo yankhanza zachibwana

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Před 20 dny

    The DC