PHALOMBE BIG BOY LERO 26JUNE,,,,2024 TSIKU LINA WINA AZALIRA.....A MALAWI TIYENI TICHOTSE MANTHA

Sdílet
Vložit

Komentáře • 165

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya Před 3 dny +4

    Inu assemblies tabwerani muliwuze zoona dziko, kodi uyu mwati analidi m'busa? 😭😭😭😭😭😭😭😭Malawi waliratu

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 Před 2 dny +1

    Basi mr bon kalindo ankhale president wa ziko ndipo ndizomwe ndikuona aaaaa❤❤❤❤

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa Před 3 dny +4

    Apapa mene mcp yafikapa ofunika tonse tidzuke tikaduduze chakwela ku state house kumweko azipita kwawo kukasiya mbuzi imeneyi isatitenge ngati ife a Malawi ndife anthu opusa ai

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu Před 3 dny +4

    Palibeso zoendetsa bwino kuno , achoke basi awa palibe chilimo awa

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope Před 3 dny +3

    Kuyankhula zanzeru aise ndipo chakwala sindikuonela kukondwa ndipo ufe ndithu pasana pamako

  • @Alliechamolie
    @Alliechamolie Před 3 dny +2

    Watiphela chilima pano ma radio angokhala chete kuwopa ikukamba zowona ndi social media basi museke ma radio anuwo😊

  • @AubreymjBanda
    @AubreymjBanda Před 3 dny +2

    Tell them my brother listen from Zambia

  • @princedetbozsmallboy1749

    Well spoken my brother amene akukhalilabe kumbuyo chakwera ndi boma lakeli ndimfiti yothelathu

  • @user-yg2oi5ln7h
    @user-yg2oi5ln7h Před 3 dny +3

    Tatopa ndithu ndachakwera achoke

  • @DaudJulius-hz8uy
    @DaudJulius-hz8uy Před 3 dny +3

    Amwene nthawi yomulangiza chakwera inali kale pano anytime is teatime osakhalanso za tsikulina mapeto ake atiphatonse galu amaneu akuenera kuchoka lero olo m'mawa pano

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em Před 3 dny +2

    Enough is Enough we're tired, on 10 July something is going to happen , Malawi viva let's unite together

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 Před 3 hodinami

    If only we can deliberate over our national teasers philanthropically and patrioticallly other than provocative demonstrations,Malawi will achieve her blissful vision and missions for prosperity

  • @OweniMalokooweni-es9qx
    @OweniMalokooweni-es9qx Před hodinou

    🎉🎉🎉🎉 ndipo kwambili zikwanje pa 10 komo ku pramet

  • @JamesDaud-jz7uq
    @JamesDaud-jz7uq Před 2 dny

    Big up phalombe boy, dziko la Malawi is for every one, Chakwera akutidzolowera heavy,akuona Ngati Ali Ku church what he knows is stealing and killing

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Před 3 dny +1

    Azakhumudwa tsiku Lina chakwera Born Kalindo Ali President Tidzabwedza

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 Před 2 dny

    Go malawi Goo!!achoke and analowela mademo mbavazi anaoipa chakwela

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Před 3 dny +1

    Apolisi opusa samalani. Musiya ana Anu chifukwa chofuna tuteteza chigawenga komanso mbava yanuyo.
    Muli busy asilikali komanso apolisi kuteteza mbavazi.
    10 July ndilo tsiku mulisunge apolisi komanso asilikali.
    Palibe zopempha chilolezo

  • @user-qu5cv9ex4j
    @user-qu5cv9ex4j Před 3 dny +3

    Go konko pa 10 pano tikaonesana konko

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před 3 dny +2

    Koma MCP nyasi zachipani agalu kwabasi

  • @user-ui4ux5kc8d
    @user-ui4ux5kc8d Před 3 dny +1

    Kodii inuu ma big boy pa 10 sipanatalike pa 29 bwanji oloo pa 30 tikhozatu oloo lero lomwe tatopa nazo ifee

  • @Alliechamolie
    @Alliechamolie Před 3 dny +1

    Kalu ameneyu analibe chilicose koma amalawi matha kukondamoyo tatiyeni tichangamuke ngat pa Mozambique

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před 3 dny +1

    Ndipo masoohenya abwino boni kalindo adzakhale plesdent wazuzika kwambili ndipo chakwela tikukhala ngati ku Malawi si kwathu njenje mulungu atithandize 😢😢

  • @GShaba-wm9uk
    @GShaba-wm9uk Před 3 dny +1

    Amade...Amade...yakukenya ichitike kumalawi kwathu kuno phaka chakwera anyere kaya kuzipha aziphe tilimbe naye tchinto azaluza kwaoko

  • @ChristopherUmari
    @ChristopherUmari Před 2 dny

    Amalawi tiyeni tisaope apolice nawotso apolice wo sizikuwasangalatsa tiyeni tipange ngati kenya

  • @user-oq5rg5mz7q
    @user-oq5rg5mz7q Před 3 dny +1

    Mitimayathu ili Mwamba asiyeni pamene titachile mademopo opolisi tizaphana, kunkuyu zikhale ng'oma tizathana naye

  • @user-ti8yq4sj5o
    @user-ti8yq4sj5o Před 2 dny

    I support u to put someone who is suffering now to be our future President like bon kalindo

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve Před 3 dny +1

    Ukuneneska razarus must fall , Ine Kuno nanozgeka pa 10 July ,Lazarus gwenembe achoke

  • @user-nw3yq5xb4i
    @user-nw3yq5xb4i Před 3 dny +1

    Ndipo mwalakhula moveka bwino president ndiomwe akuononga maiko ndithuditu tikuvuti kusauka chifukwa chama president wa

  • @KittyNdazi-bm1lh
    @KittyNdazi-bm1lh Před 3 dny +1

    Zamveka we are tired I miss chilima for good analakwa chani?

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Před 3 dny +2

    Akutamika kumanga anzawo nthawi yawo ikubwera nawonso amagidwa kuba kupha agalu

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Před 3 dny

    Mau mau audzeni Big boy ndipo ndakodwa Nanu kwambiri tiyeni tipange zomwedzo Indeeeee opusa anaimba Ng'oma ochenjera navina azaziona ndithu Bola kuotcha nyumba yawo akuona ngati Malawi ndi amao ndi achagogo awo Big boy Moto kuti Buuuuuu🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 Před dnem

    Guys let stand for the truth ,chakwela must step down before 10 if not fire every timaoffce topusa ta mcp anthu amagazi mumanja nfiti kumampha anthu ofunilila anthu zambino

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn

    Zamaphunzirozi ndiku Malawi konkuno maiko ena amasankha munthu ngakhale osapita ku sukulu chifukwa utsogoleri si maphunziro ayi koma luntha kuchokera kwa Yehova. Za maphunziro izi ndi dyera komanso kuponderedza anthu anzeru za chilengedwe

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r Před 2 dny

    Muwoneseni kenya kenya bas kkkkkkk anzanutu anaikidwa ku mzuzu ku zorozoro uko nthawi ya bingu marawi itakungana mpaka masiku atatu asirikari nkat kuchoka nthawi imene ija sindina woneposo mademo anzeru

  • @user-rv8pq8yg4s
    @user-rv8pq8yg4s Před 3 dny +1

    Chakwera achoke walephera, tili kusewu koko more fire

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d Před 3 dny +1

    Guys chakwela timuonese mwaziona ruto chimodzimodzi ndi chakwela akuziona ndi madolo chimunthu banda usamale

  • @EdwardSamuel-xj8qq
    @EdwardSamuel-xj8qq Před 3 dny +1

    Wopha chilima aphedwesonaye,busa Wang,nombeyo

  • @user-gx5ht9gm3z
    @user-gx5ht9gm3z Před 3 dny +1

    NO PAIN NO GAIN AWUZE BIG BOY BON KALINDO ONE DAY ITS ONE DAY AZAKALA PHULUMUS INSHA ALLAH

  • @user-um6yo6nc3e
    @user-um6yo6nc3e Před 3 dny +1

    Tilikonko ku ma demo ko anthu amenewa atilowa Mchala kwabasi

  • @adamusaidih8570
    @adamusaidih8570 Před 3 dny +1

    Amenewo ndiye mau chakwela ndimbuzi yamuthu

  • @HusseinMoffatt-mi1fl
    @HusseinMoffatt-mi1fl Před 3 dny +1

    Zoonadi chakwela waonjeza akupanga zamanyi ngati akuzuza buys a mkaziwake

  • @feliciajohn6041
    @feliciajohn6041 Před 2 dny

    Pa 10 gokoko more fire

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před 3 dny +1

    Gwenembe anapha m, bale wake Chilima zachisoni ndithu😭😭😭

    • @LeendaDeborah2005
      @LeendaDeborah2005 Před 2 dny

      Sikusinja ndi yemwe adapha gwenembe. Komabe nzachisoni kuti Chilima azitchedwa kuti malemu 😢😢😢

    • @mayomayo-uf9hu
      @mayomayo-uf9hu Před 2 dny

      ndipo mzoopsa guys

  • @SteveSamson-t9d
    @SteveSamson-t9d Před 2 dny

    nsitingapange chifukwa manda kwambili tiyegalasi kuyamba kuthawa

  • @OssmanAbubaker-st7pu
    @OssmanAbubaker-st7pu Před 2 dny

    Tatopa tatopa chakwera out ndi gululanu muchoke

  • @MAFUNSOMOLESI
    @MAFUNSOMOLESI Před 3 dny

    Go ahead my boss I love you so much

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Před 3 dny +1

    Ine sindikupanga comment
    Koma boma likadzasintha,ngat anyani amenenewa simudzawamanga...tidzapanganso mademo kutanthauza kut it is a must kumanga aliyense anene akutizunza lero.....

  • @ReginaNyilenda-ug1lf
    @ReginaNyilenda-ug1lf Před 2 dny

    We coming from deference country we are ready to do!!!!!! Mr chakwela please step down we are tried with u!!!!!!!

  • @Alliechamolie
    @Alliechamolie Před 3 dny +1

    Kodi titakhala five million angatikwanise

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Před 3 dny +1

    Uku ndiye kuswa kwenikweni😂😂

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Před 3 dny

    Tili konko tipange zomwe zachitika ku Kenya a malawi tisapuse anthuwa atitola!!

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 Před 3 dny

    Chakwera walephela komaso kupha kwa Chilima anapanga zolakwika and I hurt Chakwera with passion because of the death of Chilima.

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk Před 3 dny

    Powerful speech Big Boy

  • @user-yu4np2wq4s
    @user-yu4np2wq4s Před 3 dny +1

    Kutelokotu chilungamo chimapweteka akuyendela iweso akumange 😂😂😂😂😂

    • @ceciliakayira7891
      @ceciliakayira7891 Před 3 dny

      Tikuona ndi maso athu zonse zomwe zikuchitika. Kuteroko akutitseka pakamwa by kumangana

  • @ceciliakayira7891
    @ceciliakayira7891 Před 3 dny

    Kenya yayambitsa kutiphunzitsa kulimba mtima

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Před 2 dny

    Malawi ndikumuziwa ine sangapange mademo ngat a ku Kenya

  • @user-qu5cv9ex4j
    @user-qu5cv9ex4j Před 3 dny +1

    Awuzeni zowona Antalya again amenewa

  • @innocentnjoka7014
    @innocentnjoka7014 Před 3 dny +1

    Truth have spoken

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Před 3 dny

    RAZARO wadzilonda tamuuzeni watizolowera kwambiri tiyeni ku nseu basi

  • @nmbongeni27955
    @nmbongeni27955 Před 3 dny +1

    Yes🤞🤞🤞🇿🇦💪🏾💪🏾💪🏾💪🏾

  • @user-il8cn7ko9m
    @user-il8cn7ko9m Před 2 dny

    😂😂😂 siku lina pa mpando wa u presedent pa zakhala muthu wamisa ,,,

  • @WatsonNtchito
    @WatsonNtchito Před 3 dny +1

    This is only the action!

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Před 3 dny

    Malawi muno mukukhala ngati tilibe zipani zotsusa angokhala phwiiiii kudikira kuti Born kalindo aziwamenyera campain thats not true this is time for you to rise takumbukirani momwe ankachitira a mcp ma demo amapanga daily.

  • @StellahMsodoka
    @StellahMsodoka Před 2 dny

    Iwe u president ungakukhale tayimilani tikuvotereni

  • @evansjohn7766
    @evansjohn7766 Před 2 dny

    5:43 mantha to much a Malawi,kkkkkkk......simukwanisa anzanu amachita mademo mowirikisa inuyo mungathe?aaaaaa......koma pakamwa basi

  • @joekamphulusa4767
    @joekamphulusa4767 Před 3 dny +1

    Makape a mcp 🚮🚮🚮

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda Před 2 dny

    Chakusuzga ntchivichi iwe ?

  • @TressLuka
    @TressLuka Před 3 dny +2

    Game on 😢😢😢😢

  • @RegistermoseskashonKashon

    Iwe galubwako mpaka pampando born kalindoyo chitsilu iwe wava

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt Před 2 dny

    Tiyeni nafe tilionese bomali amalawi maiko anzanthu zinthu zikumasitha chifukwa satsekelera boma boma liziopa anthu not anthu aziopa boma ndichifukwa chake amatizuza

  • @CiprianoBindissone
    @CiprianoBindissone Před 2 dny

    Akulu akulu ndidziko lonse Izi dzikoli lingotha

  • @MarciaNetonMagulinho-dq3fi

    Koma nde anthu mwatopadi tsopano ndakuwonan ee koma zinthu sizili bwino mkomwe ayi kkkkk😂😂😂😂😂

  • @HassanJameskananjie
    @HassanJameskananjie Před 3 dny

    What are we waiting for here let's go guys

  • @user-il8cn7ko9m
    @user-il8cn7ko9m Před 2 dny

    Mwa chakwera mulibemo usongoleli ,kupha ,kuba ,

  • @user-lb5gt4uv3s
    @user-lb5gt4uv3s Před 3 dny +1

    Tikwapulanamo mmenemo soon

  • @MasterJailos-kv5sd
    @MasterJailos-kv5sd Před 2 dny

    Muzikapangira kupariyametiko

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Před 3 dny

    Komaso wamisarayodi ankhaledi mpampando aramuliledi

  • @user-lw9su5om5z
    @user-lw9su5om5z Před 3 dny

    Tiyen Tiyen tonse bas ulemu watha!!!!..

  • @PhillipNyaugwe
    @PhillipNyaugwe Před 3 dny

    Thyolo mulaje phalombe zomba chikwawa sanje blatantly chilazulo usakapagiseko sokhano chakwela uziwezimenezo uzafa uli ndi achitetezo tili pano ku school timaliza pomwepano

  • @AlickJam
    @AlickJam Před 2 dny

    My malawi

  • @PharrohmagawaZimba230
    @PharrohmagawaZimba230 Před 3 dny +1

    Anthu mumafika potopa kkkkkkkkkkkkkkkkk

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em Před 3 dny

    Enough is Enough we're tired

  • @MelvinVanRooyen
    @MelvinVanRooyen Před 3 dny

    Chakwela fiti went weni achoke bac watibela mokwana

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Před 3 dny

    😅😅😅😅😅😂😂😂🎉yomweyo galu iwe Gwenembe out go go go go

  • @user-pl8kw3dc9d
    @user-pl8kw3dc9d Před 2 dny

    Chakwera ndiwakupha kutumbu kwake

  • @AgnessKavalo
    @AgnessKavalo Před 3 dny

    Yomweyo galu iwe😂😂😂😂😂😂

  • @MasterJacqueline-cp3bu

    ✌✌

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Před 3 dny

    💪💪💪💪💪

  • @LameckBanda-ph2nh
    @LameckBanda-ph2nh Před 3 dny

    Facts

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i Před 3 dny

    Zoona brother

  • @shepherdkingston
    @shepherdkingston Před 3 dny

    💪💪💪

  • @ChristopherNikola
    @ChristopherNikola Před 3 dny

    Komadi tikugonadi bwanji tiyeni tidzuke guyz

  • @PreciousElias-lx2pz
    @PreciousElias-lx2pz Před 3 dny

    Ndilibe loya ine

  • @AubreyThipa-zc6vs
    @AubreyThipa-zc6vs Před 3 dny

    Boma lathapo kale ili president angokhala chifukwa cha mphavu ya constitution uyu, pa 10 Pano timuyendera

    • @user-qq1uj7ct6n
      @user-qq1uj7ct6n Před 2 dny

      Amalawi tiyen tizuke pamene Kenya yatizindikilisa kupanga zinthu nkulimba mtima. freedom is coming ... Koma mmaso mwanga ndikuona nkhondo kumalawi. 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @FunnyKalimwayi
    @FunnyKalimwayi Před 3 dny

    ndili pambuyopo tiyeni

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Před 2 dny

    Chitsiru chen Chen za zii tikuziwa ndiwe ntumiki wa dpp koma enafe sitilola zautsiru uzipangira kwako komweko ku lomwe belt

  • @ChimzyGwadira
    @ChimzyGwadira Před 3 dny

    Khani koma imeneyo tili limozii inu

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember Před 3 dny

    Enough is enough now we don't want shit

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Před 3 dny

    Ulendo ulikodi konko.
    Komanso aonadi

  • @MariaDaud-cv6xr
    @MariaDaud-cv6xr Před 3 dny

    Auzen ❤