Velikost videa: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Zobrazit ovladače přehrávání
Automatické přehrávání
Přehrát
Ine chiyambire kumvera gwedegwede pg imenei ndyomwe mwandyankhulira zakukhosi kwanga❤❤❤❤❤.Ma ministers chilichose chopangiridwa mix salary pwapwapwa.
Ndipo mulingo umenewo chakwera azanyera pogona asakufuna ndipo apolisi zitsilu zeni zeni bwanji zikungolora zinthu zaziiii
Kodi anthu oyankula chilungamo mudakalipobe may the good Lord bless you ❤❤
Muli bho guys ..Mr chikangawau kapena Kuti chifungau NDI a police Ake nkhumba Za anthu kusaphuzira kuseku kuzolowela nyau
Mr Banda keep up the good work,kumeneko ndiye kulankhula
Mwati munthu ameneyo anali Busadi ka pena anagobisalirapo I think fisi koma chikopa cha nkhosa
Chikondi tilibe a Malawi, tikadzayamba kukondana Malawi adzasintha koma ndimene zilipanopamu even tizisintha maboma nothing can change
Bambo Banda mulungu azikudalitsani ndi moyo wautali ndiwa thadzi mumati imilila
Rule one: don't be friends with a criminal party Rule two: obey Rule one
😂😂😂😂. Zilipati kod zama mega kkkkkkkkkkk😅😅
Dziko la Malawi likuyendetsedwa ndi munthu osadziwa chochita
Adzitenga madzi akumwa akutinyasa
Malo mozilemekeza achakwera angotukwanidwa ndi ana omwe zoona izii kungochoka komvina zinyawu kukhala sogolere wa ziko yooooo
Chakwela wanyanya guys, waonjezakwambili
Makamaka wachitrauza ngati parachute uja,ndimasuit ake ngati Apollo ii, kuipa nkhope ndi mtima ngati Bermuda triangle
😂😂😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Tipangano za ku kenya soon
Apolice ambili ndi mbuli ma loya ndophuzila kwambili, Apolice ambili ali certificate ya standard 8 to MSCE. Mabuzi Anu Apolice Nonse
Dzikomuno kulibe president dziko lili pa Auto pilot ili aaa
Chinese Bus or cars parts are very expensive..
Well spoken guys
Eti 2minamina sugar wakwera mafuta forsake
Kutereku chilungamo chayakhulidwa apachi wina zamuwawa
Mukunena zoonatu kwambili
Zowonadi bwana
Apa mwalankhula nkhani zamisonkho zimenezi zingafike bwanji kwa adindo?
Timanena kuti ifa ya biyeni muyaluka nazo izi mkungomanga anthu without real reason
Mumatha guys
Boma ili yalephera basi
Achakwera awauze anthu awo oipawo amene awazungulira kut zisankho zikubwera ndipo anthu amenewa adzakhaula ndithu
Woyipa ndi Chakwela yo, iye akusekelera zopusazo bwanji? Inuyo ndi anzanga mukuziwa kuti ndine wakuba komano muli nane phatiii opepela ndi ndani?
Ine chiyambire kumvera gwedegwede pg imenei ndyomwe mwandyankhulira zakukhosi kwanga❤❤❤❤❤.Ma ministers chilichose chopangiridwa mix salary pwapwapwa.
Ndipo mulingo umenewo chakwera azanyera pogona asakufuna ndipo apolisi zitsilu zeni zeni bwanji zikungolora zinthu zaziiii
Kodi anthu oyankula chilungamo mudakalipobe may the good Lord bless you ❤❤
Muli bho guys ..Mr chikangawau kapena Kuti chifungau NDI a police Ake nkhumba Za anthu kusaphuzira kuseku kuzolowela nyau
Mr Banda keep up the good work,kumeneko ndiye kulankhula
Mwati munthu ameneyo anali Busadi ka pena anagobisalirapo I think fisi koma chikopa cha nkhosa
Chikondi tilibe a Malawi, tikadzayamba kukondana Malawi adzasintha koma ndimene zilipanopamu even tizisintha maboma nothing can change
Bambo Banda mulungu azikudalitsani ndi moyo wautali ndiwa thadzi mumati imilila
Rule one: don't be friends with a criminal party
Rule two: obey Rule one
😂😂😂😂. Zilipati kod zama mega kkkkkkkkkkk😅😅
Dziko la Malawi likuyendetsedwa ndi munthu osadziwa chochita
Adzitenga madzi akumwa akutinyasa
Malo mozilemekeza achakwera angotukwanidwa ndi ana omwe zoona izii kungochoka komvina zinyawu kukhala sogolere wa ziko yooooo
Chakwela wanyanya guys, waonjezakwambili
Makamaka wachitrauza ngati parachute uja,ndimasuit ake ngati Apollo ii, kuipa nkhope ndi mtima ngati Bermuda triangle
😂😂😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Tipangano za ku kenya soon
Apolice ambili ndi mbuli ma loya ndophuzila kwambili, Apolice ambili ali certificate ya standard 8 to MSCE.
Mabuzi Anu Apolice Nonse
Dzikomuno kulibe president dziko lili pa Auto pilot ili aaa
Chinese Bus or cars parts are very expensive..
Well spoken guys
Eti 2minamina sugar wakwera mafuta forsake
Kutereku chilungamo chayakhulidwa apachi wina zamuwawa
Mukunena zoonatu kwambili
Zowonadi bwana
Apa mwalankhula nkhani zamisonkho zimenezi zingafike bwanji kwa adindo?
Timanena kuti ifa ya biyeni muyaluka nazo izi mkungomanga anthu without real reason
Mumatha guys
Boma ili yalephera basi
Achakwera awauze anthu awo oipawo amene awazungulira kut zisankho zikubwera ndipo anthu amenewa adzakhaula ndithu
Woyipa ndi Chakwela yo, iye akusekelera zopusazo bwanji? Inuyo ndi anzanga mukuziwa kuti ndine wakuba komano muli nane phatiii opepela ndi ndani?
Chakwela wanyanya guys, waonjezakwambili