![Ndine Mkatolika](/img/default-banner.jpg)
- 125
- 274 113
Ndine Mkatolika
United States
Registrace 15. 08. 2014
Za Chikatolika
Fr. Nthalika: Nanenso Ndalipeza Buku la Malamulo lija mu Nyumba ya Chauta.
Mutu wa Ulaliki: Nanenso Ndalipeza Buku la Malamulo lija mu Nyumba ya Chauta.
Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
zhlédnutí: 7 457
Video
Fr. Elizeo Nthalika: Something is Rotten in the State of Denmark.
zhlédnutí 3,5KPřed 28 dny
Mutu wa Ulaliki: Something is Rotten in the State of Denmark. Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr Elizeo Nthalika: Kulikonse komwe aliko, Mulungu ali komweko, ife lathu ndi Pemphero.
zhlédnutí 12KPřed měsícem
Mutu wa Ulaliki: Kulikonse komwe aliko, Mulungu ali komweko, ife lathu ndi Pemphero. Wolarika: Fr Elizeo Nthalika.
Fr. Elizeo Nthalika: Ukaristia, Pangano Langa ndi Mulungu Wanga.
zhlédnutí 679Před měsícem
Mutu wa Ulaliki: Ukaristia, Pangano Langa ndi Mulungu Wanga. Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr Elizeo Nthalika: Nzeru za Anthu Wamba.
zhlédnutí 2,5KPřed měsícem
Mutu wa Ulaliki: Nzeru za Anthu Wamba. Wolalika: Fr Elizeo Nthalika.
Fr. Nthalika: Ngati mutiazimpatsa Mulungu Ntchito yanu, Ntchito ya Umulungu ati ayigwire nndani?
zhlédnutí 842Před 2 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Ngati mutiazimpatsa Mulungu Ntchito yanu, Ntchito ya Umulungu ati ayigwire nndani? Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr. Elizeo Nthalika: Kupha Maloto a Makolo.
zhlédnutí 1,2KPřed 2 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Kupha Maloto a Makolo. Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr. Elizeo Nthalika: Nthenda ya Lizunzo, chida cha Dyabulosi.
zhlédnutí 864Před 2 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Nthenda ya Lizunzo, chida cha Dyabulosi. Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr. Elizeo Nthalika: Yesu wanu ndinthano, Nkutheka Yesu wanu ndi Chipikichuwale.
zhlédnutí 749Před 3 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Yesu wanu ndinthano, Nkutheka Yesu wanu ndi Chipikichuwale. Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr. Elizeo Nthalika: Sichisoni chokha Chifundo, Koma Mwai ndi Mayankho.
zhlédnutí 904Před 3 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Sichisoni chokha Chifundo, Koma Mwai ndi Mayankho. Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr. Elizeo Nthalika: Wokonda kulengezetsa Umphawi wake, Amazikodolera Satana.
zhlédnutí 927Před 3 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Wokonda kulengezetsa Umphawi wake, Amazikodolera Satana. Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr. Elizeo Nthalika: Chifukwa chani zabwino zambiri zimachitikira Anthu Ochepa?
zhlédnutí 1,1KPřed 3 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Chifukwa chani zabwino zambiri zimachitikira Anthu Ochepa? Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr. Nthalika: Nanenso tele ndufuna ubale Watsopano ndi Wosatha (Lachinayi Loyera)
zhlédnutí 864Před 3 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Nanenso tele ndufuna ubale Watsopano ndi Wosatha. Wolalika: Fr. Nthalika. LACHINAYI LOYERA
Fr. Elizeo Nthalika: Ine mwini ndiye Supporter wanga Number 1.
zhlédnutí 925Před 3 měsíci
Mutu wa Ulaliki: Ine mwini ndiye Supporter wanga Number 1. Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika.
Fr. Elizeo Nthalika: Kodi Nzotheka Kumukonda opanda kumugona?
zhlédnutí 1,2KPřed 4 měsíci
Chaka cha Yosefe Woyera. Mutu Wa Ulaliki: Kodi Nzotheka Kumukonda opanda kumugona? Wolalika: Fr. Elizeo Nthalika: Kodi Nzotheka Kumukonda opanda kumugona?
Fr. Elizeo Nthalika: Ndindani Azauchitire Umboni Ukaristia?
zhlédnutí 927Před 4 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Ndindani Azauchitire Umboni Ukaristia?
Fr. Elizeo Nthalika: Amayesa Akapanga zimenezo Ndiye kuti Akupemphera.
zhlédnutí 1,3KPřed 4 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Amayesa Akapanga zimenezo Ndiye kuti Akupemphera.
Fr. Elizeo Nthalika: Nkhani za Mumtima Zikusakaza.
zhlédnutí 1,6KPřed 4 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Nkhani za Mumtima Zikusakaza.
Fr. Carel Ernest Kafunsa: Tiyang'ane ku Mtanda wa Yesu.
zhlédnutí 376Před 4 měsíci
Fr. Carel Ernest Kafunsa: Tiyang'ane ku Mtanda wa Yesu.
Fr. Elizeo Nthalika: Tsoka Malawi kudalira anthu, Kufulatira Mulungu.
zhlédnutí 7KPřed 4 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Tsoka Malawi kudalira anthu, Kufulatira Mulungu.
Fr. Nthalika: Tingaimbe Bwanji Nyimbo ya Chauta ku Bagamoyo, Gombe lapatsidya la Nyanja ya M'chere?
zhlédnutí 19KPřed 4 měsíci
Fr. Nthalika: Tingaimbe Bwanji Nyimbo ya Chauta ku Bagamoyo, Gombe lapatsidya la Nyanja ya M'chere?
Fr. Elizeo Nthalika: Mulungu Kumamuyesa, Nthawi zina azizichitira Yekha Umboni.
zhlédnutí 966Před 5 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Mulungu Kumamuyesa, Nthawi zina azizichitira Yekha Umboni.
Fr. Elizeo Nthalika: Yesu akati wadya bwino, kodi ankadya chani?
zhlédnutí 1,5KPřed 5 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Yesu akati wadya bwino, kodi ankadya chani?
Fr Elizeo Nthalika: Nafenso ndife Anthu achipangano, tiyeni tichenjere manja ndipo tidya nawo.
zhlédnutí 520Před 5 měsíci
Fr Elizeo Nthalika: Nafenso ndife Anthu achipangano, tiyeni tichenjere manja ndipo tidya nawo.
Fr Elizeo Nthalika: Mtima wanga ukukondwa mkati mwanga…
zhlédnutí 553Před 5 měsíci
Fr Elizeo Nthalika: Mtima wanga ukukondwa mkati mwanga…
Fr. Elizeo Nthalika: Umunthu ubwezeretsedwe M'malamulo athu komanso M'mitima ya onse Amaudindo.
zhlédnutí 1,1KPřed 5 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Umunthu ubwezeretsedwe M'malamulo athu komanso M'mitima ya onse Amaudindo.
Fr. Elizeo Nthalika: Pangani Ubale ndi Mulungu.
zhlédnutí 770Před 5 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Pangani Ubale ndi Mulungu.
Fr. Elizeo Nthalika: Zosilira zanu ndizo zizamange Moyo Wanu.
zhlédnutí 683Před 5 měsíci
Fr. Elizeo Nthalika: Zosilira zanu ndizo zizamange Moyo Wanu.
Fr. Ernest Kafunsa: Kodi Ineyo Ndimamudziwa Ambuye?
zhlédnutí 301Před 5 měsíci
Fr. Ernest Kafunsa: Kodi Ineyo Ndimamudziwa Ambuye?
Fr Elizeo Nthalika: Zabwino zisakubalalitseni, koma inu dziwani chimene munabwelera.
zhlédnutí 591Před 5 měsíci
Fr Elizeo Nthalika: Zabwino zisakubalalitseni, koma inu dziwani chimene munabwelera.
Amen fr
I love FR Mthalika me my late brother Jackson Mapira.
Amen
Anthu anga akuonongeka chifukwa cha kusadziwa. Abale anga mwa Ambuye kukamva mawu muzikhala ngati ophunzira aku beleya omwe amati akalalikidwa ndi paulo amapita kukawerenganso malemba kuti zomwe amaphunzitsa zija ndi zoona? Read your bible then come back to me, bible mulibe mawu oti chauta pa ma verse omwe amawerengawo komanso si buku la malamulo koma chilamulo ndi zosiyana nde osamangothamangira kunena amen mukunamizidwa you have to be very careful bible is a word of God not a magazine.
Powerful massage
Amen Fr Nthalika
Amen Father
Fr Amen Amen
Ichi chimandiwaza heavy
Amen 🙏
Amen and Amen
Absolutely true Father I like it
My favorite lesson. Apa nde mwalakatula. Nafe anthu wambafe tili ndi nzelu.
Kkkkkkkk akuti muntu ameneyi anali mbusa .....kuba kokhako
Woitanidwa mchoonad Samasowq
Amen
Amen🙏🙏🙏🙏🙏🙏
😭😭😭 Ambuye bwerani mwachangu mutonthoze dziko la Malawi 😭😭Kam Lord do not delay 😭 Ambuye musakhale chete tikumira
Nanenso ndilinawo umboni mumati sisimusa bambo ntalika
Amen father 🙏🙏🙏
Amen
Munthu wamulungu ambuye azikudalitsani
Amen Amen Amen
Amen fr,wakumva amve ndithu
Amen
Amen brother
Powerful
Amen
Kutumikira Ambuye muchoonadi nkokoma.Ambuye azikutetezani nthawi zonnse
Kumeneko ndye.ku.bwera
Ameen munthu wamulungu poima pa chilungamo
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
Ameen
Amen
Amen
Amen uku ndiye kuima pa choonad ambuye akhale nanu thaw zose
inuyo mulungudi anakusankhani kuti mutumukure osati ansembe enawa akulandila ndalama ndalama kunyumba yachifumu kubisa chilungamo mulungu akuze malire Anu father
Powerful
Amen fr
Mau amphanvu ndithu ndipo tatolapo kanthu zikomo ambuye akudalitseni
Amen
Mulungu akudalitse a ntalika
Amen father, ndikhulupilira azibusa ambiri ankanakhala ngati wansembeyu bwezi chilungamo sichikuvuta kuchipeza, koma ambiri mantha ndi dyera, Mulungu apitilire kukutezan fr Ntalika mpakana chilungamo chitaziwika.
Mukulankhula ngati mkwiyowo utabwera mungapulumuketu anthu oyipa a catholic, palibe chimene mungalankhule cha nzeru
Keep on hitting the nail on the Head. Poti ndi satana, sakumva. Keep it up from.
Amen Fr
GOD bless you keep on preaching Hard Amen:
Inde fada,
Zoonadi atisinthira Mtsogoleri.
MCPigs ndi ufiti