Saiwalika,timangodzirimbikitsa to try to live again without them in our lives. Koma saiwalika maka ngati munkakondana. They will ever be part of our lives
@@alfreddannyulemuchinombo6068 The Original is this one, was done by Precious Fazili ft Evance Meleka but could not make it to have a fair airplay so Evance Meleka did the Remik of the song after a year.
watch the original HD Video here czcams.com/video/E4b1K0M88T0/video.html
2024 and we are here, this song always touch my heart
This song I can play again & again they is big message 😭😭😭😭😭 we need to be serious pamaso pa mulungu ndithu
This song 😭😭
Saiwalika,timangodzirimbikitsa to try to live again without them in our lives. Koma saiwalika maka ngati munkakondana. They will ever be part of our lives
Saiwalika, no matter how you choose to move on with life. Sangaiwalike
Always in tears while listening to this song😭😭LORD HAVE MERCY
Such a wonderful and meaningful piece of music......May the good Lord help us so that our names should be found in the book of life......
Ndipo ndimalira ndikamanvera nyimbo iyi imandililitsa kukumbukira zomwe bambo anga akhala akuchitira anthu ali moyo koma pano zonse anaiwala ai zikomo
Sorry dear😢
Almost in tears...it will be painful to see our names missing in the book of life...let's pray had and repent
This is true and i love this song let's just pray
Ndipo zoonad timakoma tilimoyo chonchi koma tikafa ndendende mitengo youma guys 😢😢😢😢
Nyimbo yolilitsa muli uthenga umu Like that man Mereka...CHIKONDI Cha padziko lapansi mmmmm God help us....
The song makes me wonderful day to think about life all about
Kuyamika mn unthuyu amayiba
Very clear message. Let us continue praising God
indeed they will all forget you 😭
I'm humbled with this song glory be to the almighty for the very important message in the song
Very strong touching mesage.this world is not our no matter how they pretend to love u
I like the message from this song boladi kupephela eishhh
Eeee kma nyimbo iyiyi imandifikisa kutali😭😭😭
Spiritual songs, nyimbo za umulungu, nyimbo za chi Malawi
Exactly guys we as we human we don't have evalasting life. Let's born again.
This song lremember my dad what happens on his funeral indeed munthu amakoma ali moyo zoona
Am impressed with the message
This song give me hope to God and remember my late John chimbalanga who lost his life 2hrs from 12 noon to 1pm due to BP
Sorry hope he is resting well in Gods hand
Sure pano ababa mkhope yanu inatithawa mmaso mwathu ,munapita ngati bodza,chikondi cha dziko lapansi chimathera mmanda😢😢 rest in piece mr B G J MAGWIRA ,many many years muli mmanda taisowa mkhope yanu ababa😭😭
My favorite, reality hits differently
nyimbo ni nzuri na tujifunze kutokana na wosia huu.
Mulungu atithandize mmoyowu 😢
Lord 🙏🙏🙏 have mercy on me 😢😢😢😭😭😭
Lord have mercy on us this is true and it happens
😭😭😭😭😭Rest in piece father
It's a fact in life,we need to plan because whether we like it or not one day we will be no more
But this song,eeeeesh😉😢😢
Well composed
Powerful message
Powerful message 😊
I started listening to evace meleka in 90s but what talented man the voice your just blessed much love in cape town Tonga boy
Powerful message 🔥
Powerful song
This is so powerful
RIP my Boss Chilima 😢
Nyimbo yimakhala pa repeat
Is a big message esh life
You are the best ones
Za dziko zachabe chabe ndalimbisika bro meleka
😢😢😢😢true song
Waisokoneza nyimboyi mwiniwake siimaveka like ikuvekeramu imaveka bwino kwambiri mwa nthetenya
Ndipodi inu
Who did the original song?
@@alfreddannyulemuchinombo6068 The Original is this one, was done by Precious Fazili ft Evance Meleka but could not make it to have a fair airplay so Evance Meleka did the Remik of the song after a year.
Sindikumvapo kanthu, please tayankhulani timve bwinobwino
What a song 😢
Hard Hitting Reality
Gospel truth
Big massage 😢
Abwana ameleka mumaitha ambuye akudaliseni chifukwa cha nyimbo zanu
😢 song of the moment😢
Powerful song keep it up
For sure
Nice song
Powerful message in the song
life is harsh anything can change in a matter of seconds
Amen
Eish this song
The message is strong
I know most of his songs 🎉but gospel wooo I was shocked defenetly gospel is in your blood
This song is like ulaliki
Some times ndimafuna osadzakwatira coz of this song
Why bro...would you want your partner to be sad for life?
Am so proud of this song MY the almighty be with you all the time
The world of pain let's stick to God
Timakoma tili moyo anthufe koma kungofa basi zonse zatha Evance umaimba bwino Ambuye akulitse masiku amoyo wako kuti mupitirize kudalitsa
hey im from Zambia,im looking for the song called tiri pa depoti,tili paulendo
Good song
💔😭 dziko lapasi ili aaaa
muito triste mexe muito com migo 😢
Adzandiyiwaladi😭😭😭
Nice songs
Spirtual song God bless u
Nyimbo iyi imandisundithira Kwa Mulungu
Powerful .
I love De song n de msg in t
Message
Koma poyimbapo misonzi sunkatuluka?
Uthenga wamphamvu
Mmmmmmmm meleka nyimbo mwapasaso ndani kodi? Pa audio inkaveka bwino kwambiri nangaso izi ndi ziti???????
Kodi this song anaimba ndani kwenikweni??
Ndizoonadi timakondana tilimoyo anthufe
I fell guilty but only God knows
Kumapephela ndithu
So help me God
Reality based
Rest well Dr Chilima 💔😭
Umatha
Mulungu atithandize mmoyo uno wowawitsa
That's is true but if you loose the first one all comes is player
Comédia chitoto
Thanks 😢
😢😢
😭😭😭😭😭😭
Even I iam worried about.
Exactly
Painful time
But this song
Nyimbo inkaveka bwino kwambili Mp3 ime idayimbidwa ndi mwini wake. nanga uyu wawononga nyimboyu wachokelaso kuti????
Zimukunama bare anyasisa nyimbo yabwino nanga izi Ndye ziti ziti Kkkkkk
Kuyimbaku zikuoneka kuti si mbali yanu
Tamakalimani tchomoliya basi amwene
@@hopelitta2267 kkkkkk ndaseka
This is the original song, Precious Fazili featured Evance Meleka in Choruses....that of Evance Meleka is just a cover of this one
Nyimbo aimba bwino zedi n adhawa ndioyimbanso abwino zedi anaswa
Koma mwati voice imeneyi ndiimene iii mu mp3
Anangoononganso voice yi
Awesome thanks Mr meleka
Sinimagona ngati sinavele iyi nyimbo,nimagona na mahedset mmatu kuvela cabe nyimbo yanu ameleka from Lusaka Zambia
Iyi voice ndiyaku Nigeria seru
😭🙏
Your number 🥺