Aliyese ali ndi choice asiyeni anthu azimwa inu vuto lanu ndichani? Zausilu basi agalu inu mumaziwa mankhwala ndiinu nokha basi ? Osanena kuti business ilowa pansi bwanji machende anu nonse
Kodi a Chakwera adakhalapo nduna or mp asadakhale president? Its better Atupele coz anakhalapo muma unduna ambiri komanso he has had been served in different government parastetals. So he is eligible to serve the sit
@@Eric-gb9ms my brother send 2million this month from Israel ndipo taona kusitha kwa m bale wathu komaso sakakamiza mukhala ngati anakakamiza muthu bwanji
Kamwani gamora yooooo muchira akufuna kuti akhale ndi athu ambili azidwalabe HiV gorvinment likufuna kuti azidya Ndalama zochera kumayiko akunja ziti sizingawafikile athu odwara matenda waaaa ndikulimbikitsa kuti athu amwe akugulitsa mamkhwara wo kuti Azigulitsabe osawanvera athu achakwera woooooo 😮😮😮😮😮
Aliyese ali ndi choice asiyeni anthu azimwa inu vuto lanu ndichani? Zausilu basi agalu inu mumaziwa mankhwala ndiinu nokha basi ? Osanena kuti business ilowa pansi bwanji machende anu nonse
Aaaaa chakwera pa ulimi okhao ndiye mukunama fertilizer saoda ku butchery
Boma ioro
Mulungu chonde akanatipatsa uyu abale chonde kumwambakooo😊
Mankhwala amene akhodza kukhala ochidza koma,tsangavomele chifukwa amadyela momo.
Ena Ku MDF, Ndiku MCP Mupemphele Musaluze Zisankho 2025 Imfa Ya chilima Ija Ena Muzamangidwa,
Sindikukuopsezani ichi Ndilungamo ndithu
Yaaa zoona arv is powerful
In fact tose angoni tikanakhala pamoz mzimba ntcheu tiyeni tigwilane manja kumuzimbaso akanazisiya kaye tilimunyengo yolila
Ndani angavotele atupule,,olo atakhala opambana ku convention mwina Bambo wake ngati akulephela kuwina pawu mp kudela lakwawo adzawina u president????
Kodi a Chakwera adakhalapo nduna or mp asadakhale president? Its better Atupele coz anakhalapo muma unduna ambiri komanso he has had been served in different government parastetals.
So he is eligible to serve the sit
Mbuli munaivotela ija nde imaziwa chani?anthu kuyesa kukuuza kuti mbuli ziikuziwa chilichotse iyi koma inu kakaka laro ndi izi Malawi wasanduka Zimbabwe
Kupusa kwa chakwera kumatumiza anthu ku Israel kukalima pamene mukulephera kumawalimitsa kwao shame on you MCP
Ndiwe mbuli ndipo sukudziwa chomwe ukuchita iweyo kulima kumudzinkwanu akuletsa ndani ulesi wako usapake chakwera
Imagine to bring those mega farm in our country is better than to go work outside the country that's not good
@@kingsleyhopematchaya5184mbuli ndiwe you don't know nothing about economy
@@Eric-gb9ms my brother send 2million this month from Israel ndipo taona kusitha kwa m bale wathu komaso sakakamiza mukhala ngati anakakamiza muthu bwanji
Ayi mankhwala alipo a HIV