Video není dostupné.
Omlouváme se.

MCP yatengesedwa ndi nyamata wa ku Ntheu. Chakwera alibe mtendere wamtima

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 5. 09. 2024

Komentáře • 146

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana Před měsícem +18

    Zoona zake Zenizeni koma osadera nkhawa chaka chamawa kuvuta am from Ntcheu kwataine village koma mlungu adzatiyakha osaopa osafooka osatopa❤

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 Před měsícem

      @@GanizaniKamvazaana mukuenela osatopa kmaso osafooka nanga si moyo umaenda chifukwa cha vice president a chilima, moti ndimadandaula Kwambiri kut malova ngat inu tsopano muyamba kuba

    • @FrankSimfukwe-w1s
      @FrankSimfukwe-w1s Před měsícem

      Ndipo sitikuopa izisitikungokamba chabe km sitikuopa ife tikufuna chilima wathu chomuphela ndichani atiuze chomwe anawalakwila iwowo

  • @austenbushiri-cx1kh
    @austenbushiri-cx1kh Před měsícem +14

    Mawu! mawu! 🎉 big man

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Před měsícem +21

    Amalawi tonse timadziwa kut Chakwera anapha chilima mosogozedwa ndi Michael usi

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 Před měsícem +2

      @@Extratremendouszeus amalawi ake a ku nsipe komaso owelengeka palibe munthu ali ndi mphavu yakupha or yotembelera munthu mzake paja yesu anagonjetsa infa pokha-pokha mulungu akachivomeleza infa imabwela pamoyo wa munthu,

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Před měsícem

      @@yowasschitsosa5348 Izo ndizikhulipiliro za iwe
      Chikhulupiliro sagula
      Werenga ma verses awa ngat mumaopadi Mulungu
      Mark 14:48
      (Yesu sanamugwire )
      Mark 15:21
      (Akukamupachika munthu ochokera kumunda osati yesu wanuyo)
      Kms mwa amalawi 100 aliwonse 99 akudziwa kut Chakwera killed chilima together with usi.ndipo Bakili Muluzi tv ananeneratu kut usi salankhula kanthu chifukwa amulonjeza u vice...nde lero azikalankhula ...zopusa basi..dziko loyendetsedwa ndi a ma dramma lingakhle dziko kapena manyaka

    • @EdwinHowardmkandawire
      @EdwinHowardmkandawire Před měsícem

      Iweso kapolo ndege ija ankayendesa ndi chakwera?

    • @EdwinHowardmkandawire
      @EdwinHowardmkandawire Před měsícem

      ​@@yowasschitsosa5348kuswa zonene anthuwa

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Před měsícem

      @@EdwinHowardmkandawire sindilimbana ndi zifwamba za MCP...pano mwaluza mipando yonse ku Balaka,mangochi,Blantyre nd zomba..olo mmodzi owina....mesa anawatuma a Israel kuti akole ndege..pano report latulika koma sakunena,akukonza ulendonso opita kut German konko komwe kuli ofufuza...nde akukatani...iwe ndi chikangawa wakoyo are fools

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 Před měsícem +10

    Komanso kufatsakwina ndikopweteketsa ,
    Kufatsakwina ndikopusanako ,
    Amalawi ndife anthu ofatsa mopusa

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os Před měsícem

      Zoonadi a Malawi ambiri ndi ofatsa koma kufatsa kwake kopusa. Koma ena alipo ochenjera koma chifukwa choti opusa 97% ochenjera amakanizidwa ndi opusawo kuchitapo kanthu. Mantha too much.

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Před měsícem +4

    100%facts brother mcp ndi zigawenga mbiri safuta lero taziona yalembedwaso ina apa.

  • @PIYASSFKGCHIWAYA
    @PIYASSFKGCHIWAYA Před měsícem +11

    Ulemu wanu brother

  • @MeriaMasinga
    @MeriaMasinga Před měsícem +4

    Olo Monica akuziwa kt amunanga apha chilima

  • @AdamYas-ec9oc
    @AdamYas-ec9oc Před měsícem +9

    Mukunena dzona brather m c p kwake kuba ndi kupha

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu Před měsícem +8

    Mmmm man mwalankhura zoona ok

  • @bamusmajawa1619
    @bamusmajawa1619 Před měsícem +12

    Iye uja mpaka azafa akuzuzika

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 Před měsícem

      @@bamusmajawa1619 munamatu simulungu ameneo and palibe munthu ali ndi mphavu yotembelera mzake,

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj Před měsícem +6

    Bg ulemu wanuw mulungu adalise inuyyo nkwamasinku osse tiutseni soona sandege bg mn ashankwela angompedwa nawosso sikut wawaw kobas skc anashita nkumupha ndi ashankwela yemwyyo mfiti yyamundu😮😢

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Před měsícem +6

    Ndipo zowonadi zake. Ulemu umasowa.

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona Před měsícem +4

    Ndithu iwe wa ku ntcheu ukunena zoona inenso ndine wa ku ntcheu ndithu MCP ndiyakupha kuyambira kale mtima umatiwawa koma mulungu akudziwa zonse ndithu patenge nthawi bwanji koma adzatiyankha amalawi

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 Před měsícem +1

    Brother More Fire 🔥....Auza Amenewo....Nthawi zonse chilungamo chimamphweteka muona mufa nd ma BP. MCP yakumpha

  • @user-yv3jp3it2t
    @user-yv3jp3it2t Před měsícem +4

    Osaopa man chakwela anapha chilima sibodzatso ayi

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před měsícem +6

    Mau amenewo mulungu akudalisa mcp ndi yakupha auzeni ndi mbusi za anthu awa

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Před měsícem +2

    Komaso kuyakhula chilungamo MCP sikanawina kapanda chilima olo akamayakhula mwamatama akhala dzaka zingati osawina

  • @RafiqueChibwana
    @RafiqueChibwana Před měsícem +5

    Inuyo mwalankhuladiii boss ulemu wanu

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 Před měsícem +1

    Zoona auzeni Amalawi wokomedwa Chiliungamo chimawawa A words without aparch mau Mau Mau Mau, anthu ena akumayakhula choncho chifukwa anatisiyawo sa abale awo.

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo Před měsícem

    Osatopa osafooka osawopa 💪💪💪 chakwera machende Ako aise

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e Před měsícem +3

    Kuyakhula kwachilungamo chakwera anapha chilima

  • @StevoZimba
    @StevoZimba Před měsícem +1

    Wa Bakili Muluzi VT amanena zoona😊

  • @WilliamLimwalwo
    @WilliamLimwalwo Před měsícem +3

    Zoonadi dzake, more fire,the truth will prevail 😂😂😂😂😂😂.

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji Před měsícem +2

    Ndi chipani chakupha chimenecho Cha MCP ndikukuba ndiye chitukuko chawo cha MCP basi

  • @Lingstone-r3z
    @Lingstone-r3z Před měsícem

    To stand on the bright side with truth and faith for all Malawian ❤

  • @peterlowole7841
    @peterlowole7841 Před měsícem +4

    Malawi ife ndife amantha ausilu , big mwalankhula ngamo Amen

  • @KaungaYawaka
    @KaungaYawaka Před měsícem +3

    Chakwera ndiwakupha vuto anzathu achewa kuberekana nde chimene chikumlimbisani mtima mumadya naye

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz Před měsícem +2

    mcp tidakwilira limodzi ndi chilima zimu uwakwatha Wina ayelekeze kuyimila ku ntcheu mcp timpha timuyatsira nyumba osatiseweletsa😢

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 Před měsícem +2

    Zoona mcpbinapha chilima zoona chakwera akuziwa ndipo ife ku mwera tizailowerela amaona ngati amalawi ndiopusa

  • @ChisomoMsiska-oi2vg
    @ChisomoMsiska-oi2vg Před měsícem +2

    Koma nkulu uyu wayankhula za nzeru kwambiri

  • @user-cn3gi2vf5n
    @user-cn3gi2vf5n Před měsícem +1

    Catholic bishops are very sharp amaima pa chilungamo Mcp ndi yokupha

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Před měsícem +3

    Auze aise,

  • @ElphinaChirwa-qk3cy
    @ElphinaChirwa-qk3cy Před měsícem

    Straight talk eeeee anthu munatipweteka kwabasi imfa iyiyiyi
    Ndipo mabala akupweteka

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v Před měsícem

    Chilungamo aise Chakwera ndiyemwe anapha Chilima chifukwa cha udindo

  • @MrBone-zj1wq
    @MrBone-zj1wq Před měsícem +2

    Zitsiru zimenezo zimene zikuti zalowawa ndale,mbole zawo kwambiri

  • @corretabanda7685
    @corretabanda7685 Před měsícem +2

    Walankhula bwino brother

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s Před měsícem +1

    Kwambliii Mr your talking the truethhh

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v Před měsícem +2

    Zoona chakwera anamupha chilima

  • @marthansaliwa7732
    @marthansaliwa7732 Před měsícem +3

    Zoona zokhazoka ndithu. Mulungu Ali pampando

  • @JumaJuma-i9t
    @JumaJuma-i9t Před měsícem +3

    Ndipo kumeneko ndiye kuyankhula

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před měsícem

    Chakwela Tu wapanga chitukuko tisaname Ayi Koma chitukuko chake ndi cha kumaliseche Kwa azikazi ayeni osati chitukuko cha amalawi Ayi mu andiloko chakwela pamodzi ndi uyu wakuzimbabweyu usi

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f Před měsícem +1

    Chakwera wakupha tonse tikuzwa

  • @lysonkaselema7321
    @lysonkaselema7321 Před měsícem +1

    Ntcheu ndimaiziwa ndiimeneyi

  • @SandlessWakhuluma-ns1io
    @SandlessWakhuluma-ns1io Před měsícem +1

    Mau ndiwo mweo ayakhula munthu.

  • @LouisAndrew-jr1yj
    @LouisAndrew-jr1yj Před měsícem

    Ukavomereza kuti Yesu ndi Ambuye, udzapulumuka🙏🙏

  • @user-my4gr1pv8h
    @user-my4gr1pv8h Před měsícem +4

    Tizamusinja amweneo big ngamo

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Před měsícem

    Chakwela achoke and ngati Pali munthu woti akuyenela kumangidwa ndi chakwela ndi nduna zake

  • @user-gr5zt6kw3s
    @user-gr5zt6kw3s Před měsícem

    Well said bro

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před měsícem +3

    Chakwera Mutu Ngati machende amkango

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu Před měsícem

    Zoona bro,ndipo anthu awawa ndi oyipa ndiposo ineyo amandinyasa heavy ndipo moyo wanga sindifuna kumawona,ndimava kuphweteka ndipo ineyo ndikanakha nfiti tikanaphweteka ndithu

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon Před měsícem

    😂😂😂😂 amati wina ludo kkkkkkk😅😅😅😅

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm Před měsícem +2

    Mau amphavu bro MCP ndiyakupha idapha anthu ambiri

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q Před měsícem

    Mawu oveka chakwela dzelu alive mamuna ndi wabakili muluzi tv ameneuja amaganiza hsve

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE Před měsícem +1

    Kunoso ku mzimba ndife okwiya kwambiri

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa Před měsícem +1

    Sindinu nokha akuntchewu ai even boma lakhotakota ndife okwita big pafupi ziko lose nyani chakwela mbuzi akupha

  • @misoMoyo
    @misoMoyo Před měsícem

    Sindikuona chifukwa chopangidwira remove nkhani aliense akuona yekha Mene zinaendera Kodi chilungamo mukufuna chotani kuchita kuoneka zokha kuti anamupha mukufunanso chani Chakwera ngoipa anatiphera mngoni wathu Rip skc

  • @Patricklichakala
    @Patricklichakala Před měsícem +3

    Thanksyou big

  • @MarcosDjussa
    @MarcosDjussa Před měsícem

    Zoonad brother umakwana

  • @JosephChikabadwa
    @JosephChikabadwa Před měsícem +1

    Ngakhale Mulungu Kumwambako akuwona Lingatalike bwanji Tsiku Lina Oyipayo Adzagonja Ndithu Mulungu Wathu Ndiwam'kulu Ali ndi NTHAWI YAKEEE AYANKHA M'mapemphero Athu

  • @LinesiKanzota-fw7sj
    @LinesiKanzota-fw7sj Před měsícem +1

    Zowonadi ndi zowawadi chakwera ndi Muthu oyipa

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 Před měsícem

    Well spoken my brother ❤❤❤

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb Před měsícem +1

    Chilungamo chimawawa

  • @ElizabethMajiga
    @ElizabethMajiga Před měsícem

    Ndimwana yemwe akuziwa kuti chakwela anampha VP wake basi

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v Před měsícem

    Zoona big palibenso munthu oganiza bwino angazavotere Chikangawa mcp anthu panopa ndiokwiya

  • @EdwinHowardmkandawire
    @EdwinHowardmkandawire Před měsícem

    Inuyo chikhala mmaziwa kusaka ndege munkalekelanji kupita kusaka ndege a kapolo a anthu

  • @kondwamlungu8384
    @kondwamlungu8384 Před měsícem +1

    Ukuteta yayi àuze zowona

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Před měsícem +1

    Ndipo live zoona zake tikuziwa bwino lomwe

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa Před měsícem +1

    Zowona sikunama ai mcp ndi akupha anthu zisiru za mcp mafiti

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 Před měsícem +1

    Usawope muphwanga chilungamo chake nchakuti chilima anachita kupha a mcp ndichakwera

  • @EdwinHowardmkandawire
    @EdwinHowardmkandawire Před měsícem

    Fotseki chikwera sangasowe ntendele ndipo mutaya nthawi

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Před měsícem

    Tiphe zinyau zinayi kuti tibwenze zomwe chipani cha nyau chimachita.

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i Před měsícem +4

    Mwakhwana brother uko ndiko kukamba

  • @LilianMbaisa
    @LilianMbaisa Před měsícem +1

    Ndipo asabweredi

  • @TimexKaufa
    @TimexKaufa Před 27 dny

    Chilima adakwera mundenge ndi dzigawenga ndi chifukwa a mcp adakana kukweranao

  • @FrankSimfukwe-w1s
    @FrankSimfukwe-w1s Před měsícem

    Ife tikudziwa bwino kt anapha chilima

  • @FrankAdonis-zl6qc
    @FrankAdonis-zl6qc Před měsícem +1

    Ndukugwirizana nazo mbale zoonadi zimenezo mcp chipani chongokhalira kupha

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi Před měsícem +2

    Fire

  • @user-ld8gb9xm7v
    @user-ld8gb9xm7v Před měsícem +1

    Thanks brother

  • @MaritaBanda-p4z
    @MaritaBanda-p4z Před měsícem

    amenewa akufunika azasinjidwe kumene komas kunena zona palibe wa mcp angapite ku ntcheu azikalakhula mbwelera

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe Před měsícem +1

    Palibe zandale apa Koma choonadi

  • @isaaczuze
    @isaaczuze Před měsícem

    Chakwera ndi munthu yemwe anapha chilima ....kuyipa mtima

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt Před měsícem

    Ulemu waanu brother. Osawanyengelela a MCP ndi makape opanda ntchito.

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j Před měsícem +1

    Lero mutenthedwa ndi message yoti inaperekedwa kale kale mukanakhala ozindikila a MCP bwenzi siku lomwe uthengawu inaperekedwa mutaumva

  • @patassonelucaszovuta3431
    @patassonelucaszovuta3431 Před měsícem

    Koma olo zitalowa ndale palibe vuto chifukwa anthu adafawa ndi andale ndie sindikuona vuto

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Před měsícem

    Komanso ndege inagwera poyeratu eehh

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Před měsícem

    Zaphabvu brother

  • @Marymahendra
    @Marymahendra Před měsícem

    That’s true chakwara killed Chilima for president and is everywhere in world know that Mcp party is not good people and l love Chilima behaviour than chakwara is to man .

  • @chipiesato-ut7hx
    @chipiesato-ut7hx Před měsícem

    Osaopa osatopa osafooka mcp yakupha ndizoona

  • @user-ec4jo9cu4d
    @user-ec4jo9cu4d Před měsícem +1

    Izi nde zoona ine okhara mchewa km imfa iyi yokha idandipweteka😭😭😭😭💔💔💔

    • @spargomw
      @spargomw Před měsícem

      😭😭😭😭😭😭😭

  • @user-ww9rj2wx8d
    @user-ww9rj2wx8d Před měsícem +1

    Zowonadi brother

  • @AndrewMagombo
    @AndrewMagombo Před měsícem +1

    Zoona anthu a mcp okumpha

  • @AlexPhiri-in1re
    @AlexPhiri-in1re Před měsícem

    Zoona bro

  • @moseskapelekeza8849
    @moseskapelekeza8849 Před měsícem +2

    Kodi muli joz

  • @ELLENKANJERE
    @ELLENKANJERE Před měsícem

    Zimawawa kwambiri ighowa ngati anali amai ake or achimwene mhu akhoza kumva motani akaona muthu akangwa pamseu anthu mosachendwa akufika pamalo ngati anali pafupi koma mmmm za chisoni

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko Před měsícem

    Mudzayese ngat inuso elazi mudzayipomde

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 Před měsícem

    This is the truth

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před měsícem

    Auzeni chilungamo afitiwo

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e Před měsícem +1

    Asakuopyeze mchimwene auzeni chilungamo

  • @CorneliusSande
    @CorneliusSande Před měsícem

    Eeeee koma Mulungu yekha adzamenya nkhondo

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem

    Chizaone chipande powomola